A MICHAEL USI AYANKHULA ZAMBIRI 🙌🙌🔥🔥LERO PA 4 August 2024

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 8 сен 2024

Комментарии • 154

  • @TrynessChirwa-qj5td
    @TrynessChirwa-qj5td Месяц назад +8

    Ufumu WA Mulungu uwonekere. Mau ogwira mtima. To God be the Glory and Honour

  • @user-yb3su3hi9f
    @user-yb3su3hi9f Месяц назад +6

    Osamalankhula kwambiri.muzikumbukiraso kut Palibe amene anakuvoterani

  • @RitaKainga
    @RitaKainga Месяц назад +1

    Suppoter #1 wa Chikangawa

  • @yusufbreak905
    @yusufbreak905 Месяц назад +6

    Iwe usamatchule dzina lachakwela pls ife sitikufuna

  • @VanPaul-sv9yx
    @VanPaul-sv9yx Месяц назад +10

    Waboma analenga dziko za nziiiii dziko ndila Mulungu ili

  • @WisikiBlack-gj4gu
    @WisikiBlack-gj4gu Месяц назад +3

    Usi zautsilu ife ayi wamva, wayamba ndale kumene , ndalama yoseyi ikubedwa bomamu uzitiuza zakovidi ife ndiza kolela ife manganya ngati ulibe zokamba uzingosiya osamalakhula wamva usatinyasetu ifeeee

  • @joyahmedjoma4615
    @joyahmedjoma4615 Месяц назад +3

    Ukurakwisa kumachura mr chikangawa please chonde inu simuntha kuyankhura

    • @kenmvula2123
      @kenmvula2123 Месяц назад

      Inu mukanika kupanga type Chichewa yet you are criticising the VP. Shut up and listen.

  • @giftkamwiyo9175
    @giftkamwiyo9175 Месяц назад +5

    Mbuzi yamunthu

  • @SimonJesimani
    @SimonJesimani Месяц назад +2

    Kudyera mwazi wa SkC.

  • @user-fd1tu6ku1r
    @user-fd1tu6ku1r Месяц назад +7

    Mfundo zake zosagwira Mtima

  • @SaidiMbawa-st6bj
    @SaidiMbawa-st6bj Месяц назад +2

    Kodi kungokhala osapanga comment ngati zithu zakunyasani bwanji koma kutukwana chingakupindulireni ndi chani chifukwa izi sikuti iwo amava zawo zikuyenda ntchito akugwila

    • @MpogoroMwikoko
      @MpogoroMwikoko Месяц назад

      Vito MALAWi sanje ndi kaduka musiyeni maiko usi naye akhale vp AAA MALAWi zosiyirana izi AAA

  • @JereEdwardMaxine
    @JereEdwardMaxine 3 дня назад

    Mwalankhula mokwana Bwana

  • @ChifundoZimba-jh7dh
    @ChifundoZimba-jh7dh Месяц назад +1

    Koma zeru sizimenezi Big up VP

  • @RowlandChimzimu
    @RowlandChimzimu Месяц назад +3

    Palibe chazelu chimene walankhula uyo

  • @mikegobede3830
    @mikegobede3830 Месяц назад +3

    Zaziiii

  • @emmanuelchavula7144
    @emmanuelchavula7144 Месяц назад

    Dear SKC wherever you are the guy you trusted is no longer value what you planned for young and old generations 💔💔 our hero continue resting well😢💔💔 if it means to take us to promise land through him then God forgive us 💔 you departed un-expectedly ndife athu nditha kukakhula or kuganiza zambiri 💔💔💔 komwe muliko SKC control us spiritually through God intervention. 🙏🙏 we missed you so much at least mukanasiya mau or umboni winawake kuzera mwa ena ake or mulungu oneserani mphamvu yanu potitengera kuchoona 🙏💔❤️🙏

  • @lastonekaponya7675
    @lastonekaponya7675 Месяц назад

    Ameneyu asatinyase ndi WA Congress

  • @user-hd7wq2yc6m
    @user-hd7wq2yc6m Месяц назад +4

    Koma Utsi kunena zoona u vp sakukwana, zoona vp anganene kuti dzikoli eniache ndi ama church ndi boma uyudi bolaa drama aja amapanga koma za u vp ndiye panja angochitadi kumukokerapo

  • @RodgersMhango-ff2nu
    @RodgersMhango-ff2nu Месяц назад +1

    Zawuchisiru Basi, iwe Micheal usi sungandipange convince kuti ndikamuvotere chikangawa.

  • @chirwaellace1093
    @chirwaellace1093 Месяц назад

    Zazii nawo awa akafula

  • @Aisha-db6ds
    @Aisha-db6ds Месяц назад +2

    Inu ndiye aiso

  • @user-pt8wb4vw6r
    @user-pt8wb4vw6r Месяц назад

    Amen dr usi

  • @hazibatizoni9366
    @hazibatizoni9366 Месяц назад

    Zanzi...palibepo chanzeru apa

  • @TrynessChirwa-qj5td
    @TrynessChirwa-qj5td Месяц назад +3

    Mau okoma,a VP Mulungu alandire ulemu ndi Matamando ukulu wanu Mulungu uwonekere ...mu Dzina la Yesu Khristu

  • @GoodluckVithumbiko
    @GoodluckVithumbiko Месяц назад

    ndipo mzimu wachirima ukugwira nthito mitu yabararika anthu awa tisaname sukuyenda vote yanu kuribe

  • @MasterMapira
    @MasterMapira Месяц назад

    That's ZEC My Church.... Very Beautiful ❤️... More fire 🔥🔥 Hot 265

  • @GoodluckVithumbiko
    @GoodluckVithumbiko Месяц назад

    akufuna chakwera azimuyamikira uzavota wekha uyo

  • @KennedyPhiri-h9h
    @KennedyPhiri-h9h Месяц назад +6

    Uyu alibe mzelu mbuzi ya munthu uyu mwamudziwa lero yohova galu wacheba cheba

  • @ChifundoZimba-jh7dh
    @ChifundoZimba-jh7dh Месяц назад

    Chakwera My vote

  • @limbanikamanga7514
    @limbanikamanga7514 Месяц назад

    Chipembezo will remain a potent weapon mu toolbox ya wa ndale wa mu Africa. No wonder, wandale and wamkachisi/wamumzikiti are always pachinzake. Akangosemphana, systems fall.

  • @Kamwachale
    @Kamwachale Месяц назад +2

    Funso komwe akufunsa amalawi kuseriku nlakuti Kodi anthu omwe akukukondani inu a Michael Usi azapereke Mavuto Anu Ku UTM kapena Ku MCP yankho liri lonse lomwe mungapereke perekani zifukwa zake

    • @anthonynkhoma4265
      @anthonynkhoma4265 Месяц назад +1

      Munthu samadedwa ndi anthu onse. Inu mutha kumadana naye Usi pazifukwa zodziwa inu. Anthu ena asadane naye chifukwa chakuti inu mukudana naye. That's life.

  • @SaidSamuden
    @SaidSamuden Месяц назад

    Kod amanganya palipose chakwela mukutchule simungayakhule osanenapo za chakwela

  • @user-nf5go5ic9x
    @user-nf5go5ic9x Месяц назад

    Abale ndale mpaka mu church mupta nazo kut izi, Jesus Christ is the president of presidents, Judge of Judges, please, please 🙏🙏🙏. Muzwakonzera masku apadera anthu awa osamaphatikiza ndzaumulungu please let God be God

  • @Shys-t7e
    @Shys-t7e Месяц назад

    Iyenso anagwilitsidwa ntchito ndi satana pomupeleka nzache chilima, ukuona ngt anthu sakudziwa, mbuzi ya munthu iwe

  • @user-kb9kk9pb9l
    @user-kb9kk9pb9l Месяц назад +1

    Uzilalikira za kuchikangawa

  • @Martinmkapangakapanga
    @Martinmkapangakapanga Месяц назад +1

    anachimwa ndi chakwela anatenga boma mwakuba mulungu anakwiya

  • @GoodluckVithumbiko
    @GoodluckVithumbiko Месяц назад

    komaso ndi mbuzi yotherathu ndaramazo koma kunkhata ndarama kubomako abare

  • @giftmasenti5732
    @giftmasenti5732 Месяц назад

    Ma glass munagula nokha kapena munatenga Kwa malemu? Ngati munagula nokha munagula aakulu kaguleni size yanu😂😂😂

  • @TiwongeChikhoza
    @TiwongeChikhoza Месяц назад

    Kugoyakhula za nonense basi amalawi ukutipangitsa ndi uphawi ndithu ,coz palibepo chanzeru ayakhulapo apa

  • @josuasitima
    @josuasitima Месяц назад

    chikangawa ,kuvala chikopa cha khosa km ili mimbulu yoopsa

  • @paulmanyamba5437
    @paulmanyamba5437 Месяц назад

    Ndichifukwa mulibe manyazi kuti chilima anakupangilani chani komatu 2025 ili kubwela brother

  • @user-lj7si9qy6w
    @user-lj7si9qy6w Месяц назад

    Manganya ponyankhula fundo zake zonse ndi drama poyankhula

  • @AliceChipeta-pc3nb
    @AliceChipeta-pc3nb Месяц назад

    Inu zaboma ndi church zikungwifizana pati

  • @MosesSolomoni
    @MosesSolomoni Месяц назад

    Mukaitanidwa kuma Church osamakamba za boma kapena za chakwela ai

  • @INNOCENTMOFOLO-io8tg
    @INNOCENTMOFOLO-io8tg Месяц назад

    amanganya kampeni ndikutchalitchi komwe 😂😂😂 komatu inu muzindikila zomwe mukulankhulazo mutasowa nazo mayankho usi ulibe chikondi ndipo anthu akutukwanadi sunati

  • @user-pt8wb4vw6r
    @user-pt8wb4vw6r Месяц назад

    Lamulo lalikulu pamalamulo 10 uzikonda mzako monga uzikondela ameeen ausi

  • @HaliJana
    @HaliJana Месяц назад

    KOMA USI MACHENDE WAKO WAVA IWEYO UKUMACHULA DZINA LA MULUNGU BWANJI MZIMU WA CHILIMA UKUZUZIKA IWE

  • @user-sw6rz4tz3z
    @user-sw6rz4tz3z Месяц назад

    Ndamuvetsesa Michael Usi kuti ndiwa MCP ati campaign kwa Chakwera, misala yake

  • @user-sm2qw9ii4y
    @user-sm2qw9ii4y Месяц назад

    He is a good guy only that his senior is the problem

  • @LouisNgowera
    @LouisNgowera Месяц назад

    Koma zoti winawake anadzeetsa mavuto akuthawira Ku Nenevi mu sitima ukuzidziwa?Phepo NDI mafundo zidatha atamuponyera madzi kumezedwa NDI nsomba ukudziwa iwe Manganya

  • @ChifundoZimba-jh7dh
    @ChifundoZimba-jh7dh Месяц назад

    Michael usi amakwana

  • @GoodluckVithumbiko
    @GoodluckVithumbiko Месяц назад

    wabararikatu uyo vp chikangawa akusekerera kutcharitchi akumenyaso kapeni wabararika usi wamphetsa wathu imwekazitape

  • @Alinafe-o1u
    @Alinafe-o1u Месяц назад

    That's why I like this man

  • @LindaNkwazi
    @LindaNkwazi Месяц назад

    Don't forget Chikangawa iwe

  • @frezarphiri3480
    @frezarphiri3480 Месяц назад

    Kodi uyu aziyenda mu BT mokha?? Or ngongoleyo azipeleka ku anthu aku BT okha ndiwo A Malawi??

  • @HurmlysLangwan
    @HurmlysLangwan Месяц назад

    Anachimwa chakwerayo

  • @KHUMBOH
    @KHUMBOH Месяц назад

    Just the right person for the job in such times

  • @INNOCENTMOFOLO-io8tg
    @INNOCENTMOFOLO-io8tg Месяц назад

    mukungogawa ndalama 😂😂 koma guys

  • @MarthaMbewe-uk5nn
    @MarthaMbewe-uk5nn Месяц назад +4

    Manganya siyani ndale mukapitilize zisunzo chonde kuti mukalowe bwino ufumu wakumwamba please

  • @AlexMwambayiGriffin
    @AlexMwambayiGriffin Месяц назад

    Inu lakhulan zogwira mtimat,sanje zokha zokha bas

  • @user-pc6ds2xv8i
    @user-pc6ds2xv8i Месяц назад

    Vp u r really true 👍

  • @gracemkandawire8769
    @gracemkandawire8769 Месяц назад +1

    Kodi ndikumapemphero,,osanenako zolimbikitsa anthu bwa,,mwapeza nyumba yaulere,,galimoto komanso ndalama,,mungakumbukenso komwe mwachoka

    • @user-sh6gi5uq3l
      @user-sh6gi5uq3l Месяц назад

      Mulekeni micheal usi agwire ntchito yake musamupepuse umphawi amauziwa mkuluyu

    • @user-sh6gi5uq3l
      @user-sh6gi5uq3l Месяц назад

      Zotukwananazo enafe zatikwana ndipo sizingakonze zithu olo kumanga ziko kodi mukufuna chilichonse chiziyenda momwe mukuganizira inu mmmmm ai ziko sasenza limakuphinja

    • @estherkambewa7791
      @estherkambewa7791 Месяц назад

      Tili masiku otsiliza, oipayo sagona tulo, kufunafuna oti amulikhwire

  • @dondamissonchdziwe3958
    @dondamissonchdziwe3958 Месяц назад

    Woipa amabisala nchurch,usamànene za MCP NDI chakwera m'busa wonyenga wakupha.chilima,ndiwe amene chitsiruu Satanayo ndiwe galu.uku tenga za zisuzo kupita nazo ku church, mpamene uku mango imba nyimbo za kuthezo pa msonkhano mbuli mbuzi ya Munthu Iwetu si president adaku sankhula ndani?mbava inzako chakwera mu ulure amene adapha Chilima,ankhandwe Inu,mu charichi simo ya nkhula za m'boma Wanthu aSatana Inu,mu ulure za imfa Ku Chikangawa mbuzi inu

  • @user-co3wr3rn4h
    @user-co3wr3rn4h Месяц назад

    Mwapha chilima skc kuti mutole ufumu munya muwona zaboza basi

  • @user-nu3dq5hi7q
    @user-nu3dq5hi7q Месяц назад

    Kuyesesa kuzikokelera koma sizikuthekabe😂😂😂. Kodi unali ulaliki, kapena Nthawi ya zolankhula-lankhula?

  • @JimmyIsaac-xd4ef
    @JimmyIsaac-xd4ef Месяц назад

    Kodi amapitila ulaliki kapena ndale

  • @samanthamuller7643
    @samanthamuller7643 Месяц назад +4

    Ndichisiru manganya chome wachabe chabe palibe chomwe ukunena apa iwe galu kwabasi

  • @ErnestChansa
    @ErnestChansa Месяц назад

    Tisamatukwane bwanji Kwa anthu afiti oipa mtima omwe anapha mzimu ya anthu osalakwa akuzuza anthu amoyo Iwo mabanja awo akusangalala pomwe ena akufa ndinjala ponyelela pa president chakwela mumuwuze

  • @JamesIngeni-ku3qj
    @JamesIngeni-ku3qj Месяц назад +1

    Chikangawa 2

  • @user-ty1vq9lq6w
    @user-ty1vq9lq6w Месяц назад

    Awa ndie ayiso

  • @BlessingsNyaude-t6n
    @BlessingsNyaude-t6n Месяц назад

    😊manganese usatipusise

  • @HashoAlfred
    @HashoAlfred Месяц назад

    Kod akuti chani ameneyu?

  • @tamalangoma2765
    @tamalangoma2765 Месяц назад

    Zoonadi ,nsiyeni mulungu akhaledi mulungu, nasty politics won't help Malawian. Our VP said it all.

  • @PaulineKamwana
    @PaulineKamwana Месяц назад

    Uyu ndie ndi panja peni peni cx munthu sangamalankhule zopeperazi m church .anachimwa ndi chikangawayo posiya kutumikira Mulungu nkusankha ndale

  • @HalisonSolomon
    @HalisonSolomon Месяц назад

    AKUONA NGATI KUPEZEKA KU CHURCH MULUNGU AKUKHULULUKIRANI MUTAPHA CHILIMA AGALU INU MANGANYA NDALE SIMBALIYAKO PITA KU TIKUFERANJI MFITI YACHABE CHABE IWE PETRO OMPEREKA YESU

  • @user-pl8kw3dc9d
    @user-pl8kw3dc9d Месяц назад +1

    Iweyo sukarowa ndi chikangawa

  • @user-bk4sm4jn9y
    @user-bk4sm4jn9y Месяц назад

    Ochimwa ndi chakwera yemweyo coz anasiya ntchito yake ya ubusa kukayamba ndale, nde mulungu wakwiya naye ndipo akufuna awonese ukulu wake pa chakwerayo. Iyeyo si mulungu ayi, komaso amalawi si ochimwa, mr chikangawa nde ochimwa

  • @tamandanimaliro7519
    @tamandanimaliro7519 Месяц назад +1

    muzigulako magalas asayiz anu bwana

  • @zondanitzulumusicfly.5202
    @zondanitzulumusicfly.5202 Месяц назад

    The speech of supporting evil.

  • @user-un6qv6sj3h
    @user-un6qv6sj3h Месяц назад

    Kkkkkk Mr 1 and 1 chakwerayo ndi ndani achitsilu awanso paliponse ine ndi chakwera 1 and 1 meaning

  • @MariamJohn-dg4em
    @MariamJohn-dg4em Месяц назад +1

    Analytical inu, chilima ali kuti ? Tikufuna report ife, sitidzasoya kudandaulakfikira ukulu wa mulungu zaoneke

  • @edsonphangula5817
    @edsonphangula5817 Месяц назад

    Wonderful speach akunena zoona

  • @bysongeorge3243
    @bysongeorge3243 Месяц назад

    A VP pitaninso ku Lilongwe mukayenderenso ma Church ndi Misika after that mupitenso mukayendere anthu ku Mpoto....kkkk

  • @INNOCENTMOFOLO-io8tg
    @INNOCENTMOFOLO-io8tg Месяц назад

    ndikuona anthuwo akuyankha kut anachimwa ndichakwera pomuthawa mulungu simunati ndipo nzeru zikuchokani

  • @user-qx6sr3ww8n
    @user-qx6sr3ww8n Месяц назад

    Usi mapaxiako

  • @ManMen-kp2ze
    @ManMen-kp2ze Месяц назад

    Koma ziliko , chaka chinoo, kodi ndi campaign kapena ulaliki, kapena drama?

  • @OwenNandewe
    @OwenNandewe Месяц назад

    Mulungu ndi amene akudziwa

  • @LindaNkwazi
    @LindaNkwazi Месяц назад

    Bwinotu bwino

  • @user-kq6rp6hn7y
    @user-kq6rp6hn7y Месяц назад

    Ok! Chifukwa Cha chikondi ndiye ife tizikuyimnirani mmanja mukulephera kukwaniritsa zomwe mudalonjeza? Maganizo opepera ochokera Kwa vice president. Worry not one year remaining

  • @MpogoroMwikoko
    @MpogoroMwikoko Месяц назад

    A dpp chilima amamunyoza kwambiri wamwalira ayamba kumuyamikira zichani zimenezo. Mukuwona ngati achina kabambe ndi a utm aja ndima supporter's a dpp kuyambira kale kale mumupase u president muwone mugulisa chipani

  • @SamuelMthengo
    @SamuelMthengo Месяц назад

    Siza social media,muja achakwera ankati 2025 ndiyimanso chilima alipompo muja inali social media?iwe usatipusitse wamva!

  • @Kenmoney-xp7tz
    @Kenmoney-xp7tz Месяц назад

    Chitsiru uyu okondedwa amakubela? Kodi galu ise ndalama zakuba zakupengetsa eti

  • @user-ti9yk4eg2l
    @user-ti9yk4eg2l Месяц назад

    Ndale ku church mmmmmm mwaonjeza

  • @SildaKatundu
    @SildaKatundu Месяц назад

    Bwanji sanamukonde Chilima chakwerayo ?

  • @user-ro1nm1jj2r
    @user-ro1nm1jj2r Месяц назад

    Amen

  • @SueWahna
    @SueWahna Месяц назад

    Kod mazenerawo amakhwepa😅😅😅

  • @user-lr5bz7qk2d
    @user-lr5bz7qk2d Месяц назад

    Nthawi yonse Unali kuti wakutuma chikangawa galu

  • @MabvutoMichaelPanagona
    @MabvutoMichaelPanagona Месяц назад

    Wabodza Michael usi ukupanga kampeni

  • @wanangwamwafulirwa8839
    @wanangwamwafulirwa8839 Месяц назад

    VP sakuziwa chomwe akufuna kunena.....fuduless, kumpeleka zake kut azanjoye ndiye pampandopo. Chiuta yekha abakwapulengi

  • @EmilyBanjachikwatula
    @EmilyBanjachikwatula Месяц назад

    Ochimwa ndi amalawi pomuvotela DR chikangawa