Zifukwa Zomwe Zingapangitse MCP Kuchoka M'Boma - Concerned Citizen

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 14 окт 2024
  • On Nyasa VoiceBox, A Concerned Citizen, outlines the reason why MCP will not win the Next Election.
    Pa Nyasa VoiceBox, Mzika Yokhudzidwa, ikufotokoza zifukwa zomwe MCP sichidzapambana pachisankho Chotsatira.
    #malawi

Комментарии • 42

  • @MathewKalinkhu
    @MathewKalinkhu 3 месяца назад +1

    Ndipo achmwene inu mumasanthula bwino kwambiri, zomwe mwanena zoona zokha zokha. 100%.

  • @ProspaMitumba
    @ProspaMitumba 3 месяца назад

    I agree with you Mr😍😍

  • @PrinceBlessings-bv5bs
    @PrinceBlessings-bv5bs 3 месяца назад +1

    Koma ndizoona ndithu... Azitolankhan panopa akuopa kwambir, sakuyankhura tchutchu ai... Bodza anthuwatu amayenera achoke mdzina la mulungu please 🙏

  • @JonathanMtambo-w6e
    @JonathanMtambo-w6e 3 месяца назад

    You are 100 percent right

  • @Spaw-BTheGogoBoy
    @Spaw-BTheGogoBoy 3 месяца назад +2

    MCP ku moto 🔥🥵 izikakukuta mano

  • @Homeofpeace321
    @Homeofpeace321 3 месяца назад +4

    Komatu Iwe Chakwela Mmene Unapha Chilima Muja Usazitenge Opambana Iyayi. Udindo Uliwo Pangafupike Pangatalike Umatha, Iyi Si one Party System.
    Chitsiru

  • @SolomonNjolomole
    @SolomonNjolomole 3 месяца назад +5

    Zoonadi chidule akuluwa ndi kupha apambuyo pawo chomcho sibwino ntchito za satana kumaoneka ngati abusa.

  • @marryphili5419
    @marryphili5419 3 месяца назад +2

    Mukunena zoona abro kupanga mugwirizano ndi MCP zikungofanana kuti wuli pa wubwezi ndi mkango mukangosemphana pang' ono basi iwe ndi wulendo

    • @UTHMAN-WAYA
      @UTHMAN-WAYA 3 месяца назад

      Hahaha izo ndezoona yhoo👀

  • @JunaKananji
    @JunaKananji 3 месяца назад +1

    ❤❤❤❤❤❤waganisa bho Love you ❤❤

  • @lyiemax
    @lyiemax 3 месяца назад

    I salute you big man ❤❤❤

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda8711 3 месяца назад +4

    Dzowona anthu akudziwa chilungamo pano

  • @HendrickBanda
    @HendrickBanda 3 месяца назад

    That's facts bro

  • @dondamissonchdziwe3958
    @dondamissonchdziwe3958 3 месяца назад +1

    Bakili Muluzi mu 1994, Ndi kamenya kwaya Ana imba nyimbo nthawi imeneyo ndiri kalasi 7.Anati MCP,eeeee, MCP,Anthu aja Ndi akuphààaaà,Abale MCP,eeeee, MCP Anthu aja Ndi A kubaaaa, MCP wakupha Chakwera woyeeeee wakupha aaaaa,aku Phani Nonse kumeneko oooo,thamangisani mimbulu yoooo

  • @GoodsonLindani-gf8pn
    @GoodsonLindani-gf8pn 3 месяца назад +2

    Zoonadi big chakwela akumamvera anthu oipa awa,chimwendo banda, h mkaka, z ng'oma, mkukuyu, gotani hara, ndianthu okupha, oyambisa kusankhana mitundu ndi zonse zonyasaamenewa ndiagalu.

  • @dontreybanda278
    @dontreybanda278 3 месяца назад

    Good massage boss

  • @LilianKachala-yz2xf
    @LilianKachala-yz2xf 3 месяца назад +1

    Good Speach

  • @joykhonje
    @joykhonje 3 месяца назад

    U T M please pangani mgwilizano ndi zipanizina

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of 3 месяца назад

    Mbuzi yamunthu mbuli yosapita ku school

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of 3 месяца назад

    Uchitsilu ukabvota wekha ndi tiyana tako ndiwe mbuzi yamunthu

  • @tuzijachaba-zl6pm
    @tuzijachaba-zl6pm 3 месяца назад

    Mwanena mfundo za phindu zokha zokha ifenso tikuwona choncho palibe kuwina

  • @tuzijachaba-zl6pm
    @tuzijachaba-zl6pm 3 месяца назад

    Muli ndi mfundo zabo!

  • @FrancisNyayi
    @FrancisNyayi 3 месяца назад

    18 to 35achinyamata awa

  • @JoshuaJumbo-mp3ze
    @JoshuaJumbo-mp3ze 3 месяца назад

    😅😅😅😅

  • @ChimwemweKondowe-nj4lx
    @ChimwemweKondowe-nj4lx 3 месяца назад

    Kumeneko nde kukamba tchutchutchu

  • @OmegaChingamuka
    @OmegaChingamuka 3 месяца назад

    Manganya ndi chipani chake chija odya zake alibe mulandu ndi amene atapange ngwilizano ndi MCP

  • @eliasmpita3916
    @eliasmpita3916 3 месяца назад

    Ndikuvomereza kwambiri zinthu zadula. Mafuta ophikila, mafuta agalimoto, fetereza, zopindulira anthu.

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of 3 месяца назад

    Sukudziwa chomwe ukunena and zikuoneka kuti iweyo mcp sukuidziwa dikila 2025 ndipamene mcp udzidiwe galu wachabe chabe

  • @HalisonSolomon
    @HalisonSolomon 3 месяца назад

    Iweyo nkulu umadziwa kuyankhula mbambande inuyo

  • @MosesTangwe
    @MosesTangwe 3 месяца назад

    Ndipo or kumudziko munthu amene Sali pa You tube kumufunsa angoti bola Pete yemweuja chimanga chimkapezeka mu admark. soap timkakwanitsa kugula😢

  • @RCFAKI-mx4dv
    @RCFAKI-mx4dv 3 месяца назад

    Hello

  • @HalisonSolomon
    @HalisonSolomon 3 месяца назад

    Nayenso chakwera ndi oipanso osati omuzungulira okha akanakhalakuti si oipa sibwenzi akumvera zopusa achoke basi

    • @VeronicaChirwa-ct4os
      @VeronicaChirwa-ct4os 3 месяца назад

      Indeeeee Chakwera ndi chimunthu choyipa kwambiri ku ubusa kuja amangobisalirako chabe basi. Anthu tikudziwa kuti ndi munthu oyipa kwambiri.

  • @PhillspicJere
    @PhillspicJere 3 месяца назад

    Koma mukuvutika ndi RUclips pamene ovotera MCP sali pa RUclips ndipo alibe nthawi yokuyankhani

    • @LamieTiger
      @LamieTiger 3 месяца назад

      Palibe amakonda MCP asadzakunamizen bwana athu angodyanawo tindalamato athu kuvotera tonse ija anavotera kwen kwen chifukwa cha mfundo dza chilima mu tonse muja mukanakhala opanda chilima akanaluza and ikanakhala one on one amene akanavotera MCP anali akubanja kwachakwera ndiiweyo ndiathu amuchipaniwo bas coz ngakhale azigogo athu amaziwa Kut MCP ndikaleromwe inali yokupha yokuba yoononga

    • @PhillspicJere
      @PhillspicJere 3 месяца назад

      @@LamieTiger wabadwa mochedwa iwe palibe chomwe ukudziwa ukungoona kuyankhira nkhani za akulu akulu,

    • @CHIWIKAJUNIORNYAMBOSE
      @CHIWIKAJUNIORNYAMBOSE 3 месяца назад

      😅😅😅 akulu akulu zigawenga😢

    • @SheenahMwalabu-iz3pr
      @SheenahMwalabu-iz3pr 3 месяца назад

      ​@@LamieTigerndizoona anthu ammidzimu samveradi Koma ndizomwe zachitika panozi adana nayo mcp ndizokaikitsa kuwina munchoonadi. Adzaberatu awa,, Ine ndechokavotanso ndizandichoka cz palibe yemwe nkumuona okamuvotelanso apart from malemu Chilima 😢

    • @Lee-lee-w1r
      @Lee-lee-w1r 3 месяца назад

      Nde ngati samakhala pa RUclips why did they arrest Bon Kalindo over the RUclips audios?? Musavutike a MCP wo amakhalapo pa RUclips