I greed with you True spoken Misewu sitingadye Olo atamanga ngati kwa america simungawine Anthu akufuna chimanga ndi fertilizer,zipangizo za kumunda ndiye munkhoza kuwina
Komano inuyo a John kunena zoona munthu uyu wanyoza kapena wangonena zomwe zikuchitika? Wakamba mopanda mbali ngakhale DPP waikamba umunthu wanu udachoka eti tiziti kwanuko anthu akunjoya ndimmene zinthu zilili you must be ashamed of yourself
Ife DPP yi ikutipatsa maganizo a àMalawife tonse..tatopa nazo izi .APM anaphunzira nkhanza ku India chifukwa mkazi wake woyamba amene anabereka naye ana awiri aakazi.aja ..Peter ÿo anaphunzira nkhamza za Asilamu .muhamadan Holy Jihad.crueties .in Africa historically
Ife a UTM tivotera dpp.
mcp ndichipani cholephela kuchokela kale mcp isazinamize ife tonse tivotela dpp dpp dpp basi nothing else
I greed with you
True spoken
Misewu sitingadye
Olo atamanga ngati kwa america simungawine
Anthu akufuna chimanga ndi fertilizer,zipangizo za kumunda ndiye munkhoza kuwina
Wayakhula zanzeru bro
inu dpp sugar 500 kwacha fertilizer 18.000 nchele unali otchipa chimanga chinali chotchipa ife amalawi tonse tivotela dpp kufuna osafuna ife bolani dpp
Am agree with you
Kodi inu, ena nanu or mukuti ndi a chakwera mukunena zoona dziko li likuyenda bwino, tamawopa Mulungu inu, chakwera ndi munthu wolephera kwambiri, kuba, kupha, kumanga anthu, osalakwa, a comrade inu Mulungu wathu, akudalitsen powawuza chilungamo. awa, anthu osavawa, anthu sakuwafuna, awa, God bless bro
Amen brother
Very true much respect
Ulibe zelu mbale wanga
Koma mwayankhula mau ogwira mtima zikomo kwambiri
Awuuuze amvesese
Tavulala A Malawi kwambila kuba to much Mcp
Komatu chakwera ndi bale wanu, m'chimwene wanu weniweni. Musavere manong'onong'o. Asatana. Ameneyo ndidani wanu owonekera. Muzilankhura moganizirana
Powerful speech auze brother
Komatu munthu uyuyu, akuyankhula chilungamo akuluakulu.Mutatenga malangizo awawa Zitha kukuthandizani achina Kunkuyu
Umakwana bg man zoona zake osamubisa chikangawa
Voice
Anthu wozungulira mutu kuti boma ndilomweli 😅
Akamuna chilungumo chimamasula awuzeni.
Mau amenewo pa ground sipali bwino
Boma ili kuba ndi kupha basi ndi chomwe akuziwa
Ausilu ameyo sakusiwa chimene akupanga
Ndipo uyu awona saona vote oloko imodzi
Uthenga wabwino kwambiri
Anthu akumudzi pali pamavuto kwambiri
Awa akunama kwambili amalawi akumaona
Akunamiza ndi Chimwendoyo
chakwera and mcp adeliver machende pantumbo
Tangopereka # ya mpamba or Airtel Dollars.warankhura zibambo uyu guys
Ukumva kupweteka ndi iweyo uchedwa ndi mzere wadawe,Boma ndilomweli
Komano inuyo a John kunena zoona munthu uyu wanyoza kapena wangonena zomwe zikuchitika? Wakamba mopanda mbali ngakhale DPP waikamba umunthu wanu udachoka eti tiziti kwanuko anthu akunjoya ndimmene zinthu zilili you must be ashamed of yourself
Mulungu akudarisen uthenga wabwino kwambili mulungu azisalilani amwene
Zoona n boma ili likuononga dollar kugula anthu ,kuba Malo mopanga fix mavuto ochuluka mdziko lathu
😂😂😂😂😂😂 awuzeni
Mtima wakuphweteka .UDF is a party with peolple.
Ndipo live mawu abwino awa
Manganya ndi wa chipani chake chimanchedwa kuti wodya zake alibe mulandu ndie chipani chake Manganya
Awuzeni sakuziwa amenewo
Chakwela simunthu
Kodi APM.akalowa m'boma sadzayambiranso nkhanza zakezo zija ankapanga zija **ngqti akupanga Holy Jihad"?
Palibe wabwino padziko pano sure
Ife DPP yi ikutipatsa maganizo a àMalawife tonse..tatopa nazo izi .APM anaphunzira nkhanza ku India chifukwa mkazi wake woyamba amene anabereka naye ana awiri aakazi.aja ..Peter ÿo anaphunzira nkhamza za Asilamu .muhamadan Holy Jihad.crueties .in Africa historically
Mmmm ndiye kuti chani?? Zopanda nzeru basi.
Inu kumayangula bwino mn nkhasa sachakwela olo satana akuchepa paka kupha chilima yemwe anakanga kuti alowe m boma
Nanu mwalemba ma comment awiri koma opanda nzeru. Kutenga thelere kuthira mu Thobwa. Lembes sms imodzi yoti tive
Osapanga chako chipani udzapange utsiru wakowo azako alipa ground iwe basi unyani awine asawine vuto ndilako alemera kaya Kadett moyo kuwawa ndiye tikuti bomaaa ndilomweli ndipo sitikusintha secure our brothers alubino
Enafe ndi a chakwela ndipo muva ukweche chaka chino
Crocodile ndi muthu Oyipa kwambili ngati idya amin
Sakufunikaso kuyendesa dziko basi angoba ndi kupha basi zimenezo ndizimene amaziwa crocodile
Komaso miseu akumanga ndi achima urereso basi
Mmmm inu Chakwela akukupatsani chani?tikuvutikila limodzi apa akukugailani ndalamazo dololo
Mbunzi yamunthu imeneyo ikumvutikaso kwambiri namapwala ameneyo
Zoona n boma ili likuononga dollar kugula anthu ,kuba Malo mopanga fix mavuto ochuluka mdziko lathu