LERO PA 19 BON KALINDO WABWELA NDI KUTOKOTELA BUNGWE LA MEC NDI CHIPANI CHA MCP ~ AKUTI AZABELA
HTML-код
- Опубликовано: 18 окт 2024
- LERO PA 19 BON KALINDO WABWELA NDI KUTOKOTELA BUNGWE LA MEC NDI CHIPANI CHA MCP ~ AKUTI AZABELA
Welcome to our channel, where we dive deep into the intricate and evolving world of Malawi’s politics. From the rise of powerful political parties like the Democratic Progressive Party (DPP) and Malawi Congress Party (MCP) to the powerful impact of the UTM Party and other parties like UDF, AFORD, PP, MMD, and PETRA, we bring you insightful analysis on the key players shaping the nation. Explore the journeys of leaders like Lazarus Chakwera, Saulos Chilima, and the influential activist Bon Kalindo as they navigate the challenges of governance, power struggles, and the quest for a better future.
Our channel is dedicated to unraveling the complexities of Malawi’s political landscape, offering you detailed breakdowns of alliances, rivalries, and the significant events that continue to define the country’s destiny. Whether you're interested in historical perspectives or current political dynamics, we provide in-depth coverage and engaging content that keeps you informed and inspired.
Subscribe to stay updated on the latest developments, and join us as we explore the fascinating stories that shape Malawi’s political narrative.
NOTE : We try to be as neutral as possible when giving you news from all parties. Maybe sometimes we may seem to offer or insult a certain party, kindly forgive us and above all, tell us in the comment section.
#MalawiPolitics #PoliticalAnalysis #DPP #MCP #UTM #LazarusChakwera #SaulosChilima #BonKalindo #AfricaPolitics #PoliticalActivism #petermutharika
Zoona abooooon anthuwa ndimamafia
a DPP muzimva zonena zamasapota anu, anthu akamakusapotani sikuti ndizitsiru ayi koma amakhara kuti they have put their hope in you.
This government has pushed us into an inconsolable state due to policy of Chakwera, now a Malawi analawako utsogoleri wa DPP ndiye akutha kusiyanisa kuti bola DPP. Musamangoyankhula tamatengani ACTION ine ndikanakhara oziwika ku DPP nditaika giya yoopsa
Mbudzi iwe bon kalindo mbambande
Mbuzi ndi amako
Achewa nawosondianthu akuyda gaga owawa kulilongwe kokuno kuli mavuto kuno achewa azanga tiyeni tivotele dpp otsati agaluwa ayi
Iwe ukunyoza bon kalindo pa nyini pa mako
He is a true fighter only that amalawife timava khwangwa ili mumutu
Osutsawa ndizitsilu agalamuka panopa ife pamene sitinalandile kuno ku zomba
Ku Machingaso sadalandile Ma ID
Iwetu bon umanena zoonadi komano ungoalimbikitsa otsutsao kuti asago enso ayi
Ndi zoona
Kalindo machende ako palibe zazelu zomwe unganene iwe umafuna akhale wa dpp
Macende abambo ako
Iweyo,,machende ako kwanu nonse
mmm bodza lenileni motivsalima hospital yawonongeka lero kapena nthawi ya Peter
Smartmatics😂😂😂😂😂
Samalan bomali lifuna kupweteka Ku mwela pa ziphAso
Nyanyu wa misomali
Koma zomwe akunenazi boniyu akukamba zoona aopposition akugonadi tikapanga zamasewera chakwera adzalowanso mmboma tichitepo kanthu abale ikutipha mcp
Ndipo katundu akakwera tonse amalawi tikuvutikila limodzi tonse mtendere tilibe, tisanamizanepo apa
Chomwe ukufuna iwe anthu aziba ndalamazo. Choti muziwe ntchiti ngat boma sili ngathe kutulusa ndalamazo kukagula zinthu monga chimanga nde kut palibe amene angalandile chimanga izi zimatengela usogoleli umene ulipowo nde mfundo yot misonkho yanthu si mfundo ayi
From Cape Town. Town centre Mitchell's Plain. God ahead u my brother
Iwe usatinamize ife tili konko ngati kumudzi kwathu njala kulibe amene ukunenawo ndi ana a ma sikini
Iwe pa kholo pa mako ndithu,,otsewa akuvutika ndinjala ndi amasikini patumbo pako galu,, ine wa kumachinga
@@SliviaJosephy maka kumeneko kuzolowera zolandila mukhaula muzilima osadikila kuti anthu ena akulimileni Inu muzingochindana
Ndpo kwambili
Vuto asilikali athu ndi ogona kwambili akanakhala maiko ena bwezi bomali atalanda koma vuto satana awalavulila mmaso ndichifukwa kuli ziiii sakutenga bali koma mudziwe kut mulungu wakwiya nanu mot awachose anthu
Bon kalindo kuyipa nkhope ndi ntima womwe sindinawonepo boza ngat ili kut mtalimanja akuyenda msonkhano ndi chakwera
Iwe ndi galu kwambili ndi mcp yakoyo ungamanyodze bon kalindo iwe ndi okongora?
Iweyo ukunama ndiwe mwana wotembereredwa
Iwe ndiwe....... kape mphwanga ndikukuziwatu bwinobwino
Iweyo ponyelelapamaamako ndipomwepalipotembeleledwa mapwalaakonso nkhumbaiwe nyiniyamakono plaiz wako