Bwana twaibu, ndakupezani mochedwa pa nkhani iyi ya chinyamata, ndaphunzira zambiiri, koma Izi Za menstruation, ine ine, zandichitikira Kwa Zaka zambiiiri pa umoyo wanga, Moti zanditengera mu mabvuto ambiiiri, mu zigololo zomwe ndachita mu Zaka zambiiiri, Kwa Zaka 50 Moti ma bizinezi anga asweka , Moyo wanga Uli chose kamba ka dzigololo dzosatha , ndachita dzigololo ndi akazi ambiiiri, chinthu Ichi ndikufunitsitsa chitandichoka, zonse mwachezezera ndi anyamatawa, ndazinva, Ndipo ndimakutsatirani mu ma Audio Anu onse, Ndipo NdadzIWA mochedwa, Ndipo ndikuoneka ngati watsoka. Ndipo ndanvetsa kwambiiiri, Mdikudzinvera chisoni Kwambiiiri. Ndine Gerald Dilla, Ku Lirangwe
Fuso langa tsiku la lero nari. Kodi visible church ija munkanena titha umakumana bwanji, poti ndikaona ku 7 mitundu ya athu iri momo, ccap iri momo, ndingoti mipingo yambili mitundu ya athu yadzadza nditani kuti ndipezeke pa visible church? Monga atumwi adakhara oyera ntima nayenda mu mzimu umodzi, please please help me. Ntima wanga usautsika kuno ku kasungu west kamboni tc
May our living God continue blessing and keeping you healthy for us in jesus name Amen 🙏
Amen
From Moçambique beira amen
Pastor twaibu you are doing a very good job you have transformed my spiritual life
True massage Mr twaibu go ahead
Amen ndithu brother mm tadutsamo m'menemo ngakhale mkazi amapanso zozigona yekhazo Mulungu atikhululukire
Appreciate you thanks for your ministry.
Kalanda Dorothy South Africa 🇿🇦 ♥️
😊
Zomwe akulankhulazi inenso ndikudusamo😭😭😭😭
Ineyo mulungu andikhuze chifukwa uthenga mwatengawo ndayendamo ndipo masiku akusaziwa muli ifa yamuyaya chifukwa muli uchimo
Uthenga wabwino ambuye akudalitsen 🙏
Ambuye alemekezeke tadziwa kmanso taphunzilaa ambuye akudaliseni munthu wa mulungu
True man of God
Abusa chonde gvm nambala komeleni mtima
Amen
Ndimatsatila ma uthengawa koma ulilakiwu kuchokera kuno ku South Africa
Twaibu I'm from Zambia 🇿🇲 was TB Joshua part of you guys 😢
Nimayamikila kwambiri kuno ku Zambia
From Mozambique Maputo ❤❤❤
❤
❤❤❤
Thank you so much
Fusa pazakulela , timati kulela ndi oipa ndee tigwiliskenge tchito vichi .. to avoid preg..
Bwana twaibu, ndakupezani mochedwa pa nkhani iyi ya chinyamata, ndaphunzira zambiiri, koma Izi Za menstruation, ine ine, zandichitikira Kwa Zaka zambiiiri pa umoyo wanga, Moti zanditengera mu mabvuto ambiiiri, mu zigololo zomwe ndachita mu Zaka zambiiiri, Kwa Zaka 50 Moti ma bizinezi anga asweka , Moyo wanga Uli chose kamba ka dzigololo dzosatha , ndachita dzigololo ndi akazi ambiiiri, chinthu Ichi ndikufunitsitsa chitandichoka, zonse mwachezezera ndi anyamatawa, ndazinva, Ndipo ndimakutsatirani mu ma Audio Anu onse, Ndipo NdadzIWA mochedwa, Ndipo ndikuoneka ngati watsoka. Ndipo ndanvetsa kwambiiiri, Mdikudzinvera chisoni Kwambiiiri. Ndine Gerald Dilla, Ku Lirangwe
Mumanditsitsimutsa kwambiri
Nanga anthu oti ali moyenda ngati maiko akunja koma mpata oti angaotche pad kuti atetezeke angamatani ???
Fuso langa tsiku la lero nari.
Kodi visible church ija munkanena titha umakumana bwanji, poti ndikaona ku 7 mitundu ya athu iri momo, ccap iri momo, ndingoti mipingo yambili mitundu ya athu yadzadza nditani kuti ndipezeke pa visible church?
Monga atumwi adakhara oyera ntima nayenda mu mzimu umodzi, please please help me.
Ntima wanga usautsika kuno ku kasungu west kamboni tc
Ndili ndi fuso ....what if munthu walota kuti mnyamata yemwe ukundeta nayo wamulota katatu kuti siwako ndiye upange bwanji....umusiye kapena utani? Please please help