Dr Mtumbuka is the best kutsogolera chipanichi, Kaliati akhalebe SG azichepetse ndipo pa SG Palibe angapikisane ndi Kaliati, Usi is not fit for any mpando anaonetsa kuti ndiwosakhazikika.
Mery Chilima should come upon and lead the Party and stand for the Presidency, she's the only person who's going to destroy MCP and Lazuro chakwera with his goons.
Kaliati ayimire basi atumikira ndi malemu mosawazembera mwachilungamo .komanso achigwira chipani cha utm.koma a usi chipanichi chikhala cha mcp a usi akatenga ndipo adzachisintha zina siyizakhalanso utm .koma odya zake alibe mulandu plus chikangawa party
I wish she could kuti angopitiliza kutitsogolera than anthu adyerawa, omwe amadikira a chilima apite Nde adzidzalowa chipani bwino, Ngati Yehova angawafulumizitse kutero, atero it can be hard koma yehova amapanga zose ndi cholinga, anthu atakhala ngati Mai kaliati chipani cha utm chidzalimba mpaka kale
😂😂😂. Paja chikangawa party mukusapota usi cholinga atenge chipani kupitaso ku MCP, nde bola atapita komwe anachokera than ku MCP azingophedwak ngt mmene mwaphera chilima 😢
No leadership qualities in Patricia kaliati,UTM please open your eyes, Incase you partner with DPP in 2025 with KABAMBE ,just know that the end of UTM , DPP should also mindful of APM leaving the power to KABAMBE due to age , which also will mark the downfall of DPP ,SO both UTM &DPP should open their eyes
Dr Mtumbuka is the best kutsogolera chipanichi, Kaliati akhalebe SG azichepetse ndipo pa SG Palibe angapikisane ndi Kaliati, Usi is not fit for any mpando anaonetsa kuti ndiwosakhazikika.
Mery Chilima should come upon and lead the Party and stand for the Presidency, she's the only person who's going to destroy MCP and Lazuro chakwera with his goons.
Ayi Akaliyati ndiwomwe angavale nsapato ya achirima ndipo akuwonesa kusapendekeka ayi koma ena onsewo musakopekenawo abwera ndimpeni kumphasa
Apeseni mwai mai kaliati nawo aimed nawo tiyeseko azimai pa u presdent
Mai Kaliati my vote, enawo ayimire zinazo
Osazamuvotera Micheal Usi simunthu wabwino chipani achigulisa ku MCP Chikangawa party
Kaliati ayimire basi atumikira ndi malemu mosawazembera mwachilungamo .komanso achigwira chipani cha utm.koma a usi chipanichi chikhala cha mcp a usi akatenga ndipo adzachisintha zina siyizakhalanso utm .koma odya zake alibe mulandu plus chikangawa party
I think Mary chilima and Brian Banda would be a breath of new air
Merry Chilima My Vote
I see merry chilima coming up wait and see
I wish she could kuti angopitiliza kutitsogolera than anthu adyerawa, omwe amadikira a chilima apite Nde adzidzalowa chipani bwino, Ngati Yehova angawafulumizitse kutero, atero it can be hard koma yehova amapanga zose ndi cholinga, anthu atakhala ngati Mai kaliati chipani cha utm chidzalimba mpaka kale
Mary Chilima be strong.we need you come on
Sizose zonyezimira zili Gold, UTM ikhale maso pa utsogoleri wa president chifukwa kulipo kugulitsa munda wawo kenako mkumadzapangaso ganyu mmunda mwawo momwe, vuto la a usi samadziwika kuti Ali mbari iti chifukwa samakhala open pamikumano ya utm ndi zochitika zose amadzipatula muzambiri, anthu onse omwe alowa chipani chilima atamwalira sakufunika kuwakhulupilira mwachangu chifukwa mitima mwawo akungofuna mipando, we will regret sure, anthu 5 akalimbilane mpando umodzi afuna chani kwenikweni, apa Pali dyera osangoti matipate, nuona ngati kutsogolo kwa utm kuli kasavana ,
Mayi kaliati my vote
MANGANHA anapha chilima
Mary Chilima tikumufuna ife
Michael usi wakomedwa ndi Mcp so akhonza kuchigulitsa chipanichi bola akaliyati or Kabambe
@@ChimmsRichardOrden apa tipitire kaliat.zopatsa alendozi ayiii
@@henryphiri6100am with you
mery is only one who have more flo utm open your eyers
Ife anuwake a UTM tikudziwa president wanthu
Iwe wa MCP izo ukufunazo singachitike
Dr usi akuyenera kuyimira u president ku UTM
Ndinu a mcp ndipo mumutengatu ameneyo
@@billymhoni9527 manganya ndikape
Usi ndiwa chikangawa😂😂😂😂
Utsi ayi wa chikangawa
Mfiti ya munthu kufuna kudzamaliza mtundu eti
Mwawi uli ndi awiriwa Utsi ndi Kaliati.
Utsi akawina chipani chilimba monga mmene Chilima adasankhila. Sadasankhe kulalata ayi..
Atakatenga Kaliati, chipani chikhala under DPP ndi kutha ngati makatani
😂😂😂. Paja chikangawa party mukusapota usi cholinga atenge chipani kupitaso ku MCP, nde bola atapita komwe anachokera than ku MCP azingophedwak ngt mmene mwaphera chilima 😢
Khani ilipan ndi ya utm not MCP kodi walowera pat iwe
Ndinu a mcp
Ndiwe oipa using wake utiyo
Utsi amuchose nga mcp awo
Manganya si wa UTM.
Okuphayo musayelekeze mutha nonseeeeee
Usi azawine Ali ndi usogoleri chilima anasiyilanji kuwasankha inawo bwanji
Kopanda Usi Ku UTM singawine kozi akupanga kamupeni ndi Boma Popano anthu akumuziwa
Usi ndi wa MCP mapeto ake UTM itha koma ena okay apikisane tikudziwa kt enao akupikisana cholinga a usi achoke pa mpando
Dr manganya usi ayimile
Ndi amene anasakhidwa ndi chilima komanso amaye ndesela limodzi munthawi yawo sanga gulise chipani ndi munthu wina ayi
Why do you hurt running of Chilima, honestly Chilima was not stupid to choose Usi. Kaliati ndinu chitsiru 0:00
Usi ali ndi chipani chake ndi gulu lachina masangwi.dikirani munva kuti odya zake wabweranso ndipo ali ndi boma mgwirizano
Dr Usi akuyenela kutenga enawo amuthandize MAI mkulu ulemu wao ku SG chair
Manganya Siwa Utm iyeyu ndiwa Odya Zake alibe mulandu
Ine isupport usi koma achoke aliko plzzz for malawi to ❤ him basi
Manganyao ndikatundu mpatseni mwayi
Wayamba lit dale
Mpaseni ku mcp konko
Manganya anapha chilima
Mmmm utsi Nd wa chikangawa party
No leadership qualities in Patricia kaliati,UTM please open your eyes, Incase you partner with DPP in 2025 with KABAMBE ,just know that the end of UTM , DPP should also mindful of APM leaving the power to KABAMBE due to age , which also will mark the downfall of DPP ,SO both UTM &DPP should open their eyes
Nkhani ndi Mary Chilima muona Ena onse athawamo
Ausi atha kukhala upule not kaliyat kulalata sangasogolele
Obera kutsogolera utm: usi...
Manganya is a president of UTM ,, don't give female
Usatipangile zochita
@@AlinafeKanyikakoma ndiponso hahahahah
Usi basi anamsankha yekha malemu. anasiyilanji kusankha enawo ndipo potsankha usi anawonamo mwini wake
Manganya akungofuna kugulisa chipani
Kaliati ❤❤
Kaliati boma
Uyo maiko usi ndi wa kongeresi mm paka achigulisa Ku MCP simuthu wabwin
Kaliyati vuto alibe ulemu ndi anthu
Manganya chipani chache cha NTHIKO nchimozimozi ndi MCP NG'ONA PARTY, dzimbalangondo
Vuto la usi si wa utm coz akipanga zimezizo coz adzagulitse athu ku mcp zomwe sizili zoyenera
Imeneyo ndiye democracy
Usi ndi wa mcp kumpasa mpando ndiye kuti chipani chathapo basi nonse mukhala a Congress party utm be careful
Kaliati ai pau presedent iwe ndi SG basi
Usi ndi galu kwabasi
Manganya ndiwa chikangawa part
Kodi angamvotere usi ndi ndani yudasi ameneyu koma ine musatiyese mwamva
Kukanakhala kobvuta kuti ausi azionesere kwambiri kuti akusapota utm pamene akugwira ntchito ku boma zambiri zimaoneka kampeni ikayambika panopa ndikobvuta kuti ausi anganene zolakwika aboma akweni akapusa aluza mbali zonse akayerekeza kuimilira uprezident
Manga samakhala serious ku chipani cha utm komanso ndale adziwika momwe asakhidwa u vice
Usi ndi galu
Kodi amanganya alikuti mesa paja Yao sinatuluke
Manganya ayi mapeto ake apitisa chipanichi ku Mcp
Mpakana kaliati kufuna u president? Aaaah koma Malawi Malawi ai ndithu
Kaliati kukhala mtsogoleri wa chipani, are you serious 🤔
Akufuna usi woo ndi a mcp
Hi
Osaopa usi agulisa chipani
Forget a bout utm
Maiko usi ayi ndi wamcp
Inu usi ndi wa mcp bwanji mumasokoneza zinthu
katunthu ndikaliyat maiko usi agulisa ku ng'ona kaliyati chilimba
Us basi
Dr usi akuyenera kuyimira u president ku UTM