Ndichifukwa chake Yesu Khristu atabwela sanalimbane ndi ufumu wa Dziko la pansi iye anangobwela kuzapulumutsa chotaikacho bas...He k ew kut ufumu wa Dziko la pansi ngwa oipayo
Muzithako kupanga zanu komaso kuvomeleza zinthu zikachitika aliyese azamwalila nde musapake ena imfa ya munthu azamwalila nthawi inakwana bas iyi ndinthawi ya Usi mufune musafune
Chifukwa chani chirima anamunkhulupirila manganya nanga ndichifukwa chani manganya sanachosedwe unduna maulendo onse omwe ankhala akusintha maunduna manganya hi was a trusted person to chirima
Dr. Chilima had no intentions to quit the alliance? Chilima spent more time in courts with powerless position.... Malawians, learn to use your heads properly in reaction to everything which enters into your heads. God shouldn't be mentioned everywhere brethren because a day is coming. Stay blessed.
Za dyera basi olo inu mukuyankha pasi pasi muganiza ngati gwilizano amauthesa mwini wake malemu koma a malawi muzachangamuka liti ndindale akufuna kukakamila gwilizano cholinga simukudziwa shame
Thawi yonseyi bwanji simunkavala uniform ya utm even mwini wakeyo Ali moyo aaahhh we can't trust you bwanj wakakamila ku mcp relo mwayamba kuvala uniform ya utm chifukwa mu kuziwa kuti joka akufelani alimanja aahhh
Manganya akufuna kuononga chipani cha utm. Anthu amene alipo si a utm wose koma ena ndima khwangwala. Manganya ndi sweet talk. Ndichifukwa chani manganya akukakamira ku mcp pamene chilima anafa ifa yovesa chisoni. Manganya aononga utm ngati pamene nankhumwa anaonongera dpp. Manganya amalawi asakupusiseni akukuyikani mukamwa mwamukango.Akufunako chani ku mcp? Mcp yo ndiyimene yinachedwesa kufufuza ifa ya chilima. Mtsogoleri basi palipose ngongole ngongole pamene pali bungwe limene likuyendesa zangongole koma pule ndi vp busy kuyakhula ngongole munthu opusa zeru ndi amene akusangala ndingongole koma wazeru amazisakira yekha chuma ndipo akachipeza chimakhala changeiro pamaso a Mulungu.Manganya ngati ukufuna khala ku mcp ko ndi ufulu wako koma asiyire azako apange za utm
Usi sakuwelenga bible. Munthu wazeru satumikira mabwana awiri nthawi yimozi. Ngati utm ukuyifuna tuluka ku mcp ngati sikuifuna utm khala ku mcp ko ukuganiza kuti marry chilima akusangalala nazo chimene ukuchita. Ifa ya chilima ikutipweteka amalawi munthu inde amakhala ndizifika koma kufa kwa chilima ndi azake cabinet yose yinapanga rigsin ndi president yomwe koma potimanyazi mulibe and amalawi tikuseketera zithu zoduka mutu.
May God give you more wisdom Manganya our Vice president, Dont be shaken lots of people are pharisees
Iyi inali apayi ndi Group la odyazake alibe mulandu,,palibe wa utm apa.
Ndichifukwa chake Yesu Khristu atabwela sanalimbane ndi ufumu wa Dziko la pansi iye anangobwela kuzapulumutsa chotaikacho bas...He k ew kut ufumu wa Dziko la pansi ngwa oipayo
Utsogoleri wabwino ulimo umu ,, bwana VP, you got it✊✊✊✊✊✌️✌️✌️✌️
The guy is so wise. Now I know why even President Chakwera did not hesitate appointing him
Muzithako kupanga zanu komaso kuvomeleza zinthu zikachitika aliyese azamwalila nde musapake ena imfa ya munthu azamwalila nthawi inakwana bas iyi ndinthawi ya Usi mufune musafune
Osadabwa kuti all this time he never wore UTM uniform….. all of a sudden wakayipeza. Shupiti zako Manganya
Manganya the best man. Keep the vibe
1.kusayankha ma diss it's fearing kut abwera ambiri
2. Ati nthawi yoyankha alibe koma aziganiza ngongole, kodi akuona ngati wafikapo eti. Apanga mpaka liti?
5. Lero ndie anaganiza zovala party cloth? Ndie wu betrayer umenewo
Suka kamunthu kakupha aka...kamwana ka chikangawa aka😮😮
Don't let enermy scatter us. Viva UTM
Wagwa nayo Usi dziko lakutulukira kale kuti ndiwe wa mcp osokoneza iwe ukuganiza ukawina ku convention
Tikuferanji at the best level, za drama zenizeni, nanunso oyimba ng'oma kumavina apa mumavinirapo zichani?
Chifukwa chani chirima anamunkhulupirila manganya nanga ndichifukwa chani manganya sanachosedwe unduna maulendo onse omwe ankhala akusintha maunduna manganya hi was a trusted person to chirima
Kodi mukamati chakwera akumakukumbutsa kuti chilima ankati tipangechani kkkkkk seriously manganya bwanji sankamugwilitsa ntchito ngati mmene akupangila iwemo 😢😢😢😢 manganya sudachenjele bwino
Eti eti chilima amangonyozedwa lero zatani manganya bzy bzy chonch chadza ndiyani
Thank you Mr vice
VP ndi more fireeee
Image moto Boma ilo
ndikufuna chisot ndi maglass ndipitilize kupanga masewelo ndi nyimbo ya winiko umandisewelesa
Dr. Chilima had no intentions to quit the alliance? Chilima spent more time in courts with powerless position.... Malawians, learn to use your heads properly in reaction to everything which enters into your heads. God shouldn't be mentioned everywhere brethren because a day is coming. Stay blessed.
Palibeso zoti tingakambilane nanu athu okupha inu ngati mukulephela kupeleka ma information yangozi ndiye mukuganiza kuti tingakusekeleleni afiti osekelela 😢😢😢😢😢😢
More fire mr vp l love u more , hel
Zopanda nzeru zomwe akulankhula awa, ngongole kodi aliyese angalandile ? Azimayi mumangoziwa kuyimbira zilizonse ndizopusa zomwe.
Kupusa amalawi eeeeesh 😢😢😢
akutukanani eya mwaonjeza inu aaaaa
Yaaaaa coma vice president uyuuu anakonzaa zowonaa
michael USI ALIBE MFUNDO...NDIPO NDIMA DRAMA ENIENI...PALIBE UTSOGOLERI APA
Utm pitani ku conversion zosezo zitha 😢
Thats true Mkumano wa UTM uzathesa zonsezo.
You are. right
Manganya ndi khuluku. Posachedwapa mulungu si James. Zomwe Iye amafuna zachitika. Betrayer
Anthu ongoyankhula zopanda umboni.Personal opinion kumaipanga present ngati fact
Chisiru ichi chopanda mfundo akukakamira ku MCP coz Cha u vice president ukuonangati a MCP akukuonera kukondwa?
Malemu Chilima anatuluka mu Alliance asanamwalire paja?
Ku off camera anagawa ma bwa?😅
Mukhale pa nthuzi mulandire kanganyanse
Only azimayiii km abale tiziona
Bwana Vp chimwalireni Sck munakumanapo ndi Nec yanu ya Utm ngati mtsogoleri,,,muyenda bwanji ndi alliance kutengera kuti amene anasaina wamwalira?
Mutifusileko kut Kodi iwowo ngt mtsogoleli wa UTM anayitanitsa ana awo ngt akambilane nawo? Zakutulukako nanga ndizoti UTM ndiyomwe idzakhale patsogolo mu 2025 ngt mwagwilizano wawo?
Tinalodzedwa ndithu,VP kukhala manganya ,munthu waku Zimbabwe😮😮😮😮😮
Come to mcp my friend
Lero nde mwavala za SKC?😅
Nose muli kumeneko ndi bambo asikono Mr yudasi tiye uko osakamba za madam mery akulira mwamuna wawo fisi lwe ndi chikangawa anthu okupha analakwachani skc 😢😢😢 manganya lweyo
Komatu
Chikuwalimbikitsa nchiyani kulimbana ndi ngongole mmalo mongogawa ndalamazo akufuna kuwabelanso amphawi
Bwanji zomwe ukupanga Bwanji sakamulora chilima kumatero ndi chifukwa utm yeniyeni ukukwiya nawe
The VP is wise 🎉
Awaaa koma? Azimai kutengeka😮
Ngati alidi mtsogoleri wa utm bwanji sakupanga push za report ya ngozi ya ndege kuchikangawa kuja ???????????
Mzimayi ndiwoyimitsa mutu kwabasi amangoyimbila m'manja zilizotse
Good speach ndale Zapa internet no good zipani Zina kulemba anthu Kuti aziwapatsa malipilo nchito yake kutukwana mulunga sangakuwiniseni muluzaso
Kamthila kuwiri aka kamunthu kowumila aka kayambise Chipani chake kazafa ngati galu aka
Wamfupiyu mzeru alibe uyu ndiye bambo asikono galu kumtumbo kwako
Only fools can trust this short man
Kambelembele uyu
Mwasoketsa kit ya UTM,,,, KKKKKKK,,, HEEEEDEEEEEE😂😂,,, OCTOBER IS NEAR,,,
Akufuse ngati ndani? Just wait for convention
think carefully about this I dont think Saulosi would still be in MCP by this day today
Dr Manga palibe cha nzeru mukunena apa
Micheal Usi is a unifying leader regardless of political divide.
Kodi Dr manganya Inu ngat msogoleri wachipani Cha Utm mwachitapo Chani kut athu azigwirizana kuchipani Chanu, chifukwa zikuoneka kut mukuyenda nokhatu kuchipaniko akuluakulu onse akukukayikilani mutani,kut athu ayanjane komanso chipani Cha Utm chikhale chaphavu
UYUTU MBOLIYA MAKE AKUPUSITSAI GALU YU
Aaaaaaaa....iwe sungatputsitse ase......apa pokha wanama bacccccc....Awa wangoveka za UTM...aaaaaaaa ahaaaa!!!!
thiko wa mapoto awir utm and MCP unapha chilima nthiko
Kkkkkkkk
Ndikamamvera awa ndumasowa chonena zumangondiseketsa
Awa si a utm,awa ndi a group yake ijayi amati odyazake alimbe milandu lija 😅
Za dyera basi olo inu mukuyankha pasi pasi muganiza ngati gwilizano amauthesa mwini wake malemu koma a malawi muzachangamuka liti ndindale akufuna kukakamila gwilizano cholinga simukudziwa shame
Choka okupha munamupha Zanu kut mutenge mpando wake Ausi Muli ndimulandu ndimulungu sure
Uli ndi umboni iweyo?
Maumboni alipo bro
Mukuyankhula zonsezo chifukwa inuyo zanu zikuyenda, mukuwauza anthu kut tonse ndi amodzi. Funso ngat tili amodzi ndichifukwa chiyani a President akungolemba ntchito abale awo komanso azinzawo??? Kodi umenewo ndi umodzi? Bwanji simudzuzula kusankhana kumeneko.
Akulu awa akufuna agulise chipani cha UTM.chakwela msamale nayo.or iweyo usi usamale akutafuna
Why today?
Mayi Chilima,,,, tiziwapemphelela chifukwa munawaphela amunao
So many plane crushes in the world achimwene sizinayambe kumalawi
Oro utani naweso uzafa waphesa chilima iwe mwachidule ndiwe yudasi iskariot ndipo pa exclusive unanena kut umapita kwa achakwera komaso kwa chilima zomwe zikuonesa kuti ndiwe waphesa chilima
Wa chisokoneza chipani cha UTM
Uyu ali ndi fundo zogwira mtima
This shortman cant be trusted....
Wisdom defeats knowledge
Thawi yonseyi bwanji simunkavala uniform ya utm even mwini wakeyo Ali moyo aaahhh we can't trust you bwanj wakakamila ku mcp relo mwayamba kuvala uniform ya utm chifukwa mu kuziwa kuti joka akufelani alimanja aahhh
Wayaluka pano angobwebweta
Manganya akufuna kuononga chipani cha utm. Anthu amene alipo si a utm wose koma ena ndima khwangwala. Manganya ndi sweet talk. Ndichifukwa chani manganya akukakamira ku mcp pamene chilima anafa ifa yovesa chisoni. Manganya aononga utm ngati pamene nankhumwa anaonongera dpp. Manganya amalawi asakupusiseni akukuyikani mukamwa mwamukango.Akufunako chani ku mcp? Mcp yo ndiyimene yinachedwesa kufufuza ifa ya chilima. Mtsogoleri basi palipose ngongole ngongole pamene pali bungwe limene likuyendesa zangongole koma pule ndi vp busy kuyakhula ngongole munthu opusa zeru ndi amene akusangala ndingongole koma wazeru amazisakira yekha chuma ndipo akachipeza chimakhala changeiro pamaso a Mulungu.Manganya ngati ukufuna khala ku mcp ko ndi ufulu wako koma asiyire azako apange za utm
Anthu ali apawa palibe wa utm angovala ngati a utm
Manganya amatha
I like manganya but I smell something fishy in him
Azimayi muzatiphetsa
Mesa umati suyankha nde ya nthikoyo ukuikambiranji aaaaaa iwe galu wakumpha
Panga chako chipani , achilima anachoka pa vice president ku dpp alimboma ndikupanga Chao chipani
I can't trust this guy now
Aaaa kamthira kuwiri ako shupit kopereka nzake
usi akuti chani kodi???UTM kufika chaka chamawa yikhala ma katani okhaokha😂😂😂😂😂
Iwe manganya usagawinitse anthu autm koma ndalama ndi satana udamupha chilima
Michael Usi usaganidze kuti an'thu ife ndiwopusa ayi , We know the all strategy that you are Playing .. Iweyo muntima mo ukudziwa kuti UTM Unatuluka chilima ali moyo , Makaka a UTM Wayamba kuvala pomwe CHILIMA wamwalirapa , Iweyo olo utapanga timapulani takoto " Koma a Malawi tikudziwa kuti Imfa yachilima iweyo unatenga nawo gawo ,Even Chilima atati Mulungu amudzutse lerolini " , Iweyo ndimunthu woyamba yemwe ungakhale m'dani wa CHILIMA . Anthu womwe alipamenepowo " We know very well kuti ndi anthu a chipani chako cha MCP , Koma apa wangowaveka makaka a UTM kuti anthufe tidziti" Ukutsatilidwa ndi anthu a UTM , Iweyo palibepo chomwe ungamatiwuze a Malawi ife ' Then nkuyiwala zachipongwe chomwe munamuchita CHILIMA ku chikangawa kuja , Chilima munamupha imfa yowawa kwambiri . Ndipo iweyo siwukuyeneranso kumakamba chilichonse chokhudza CHILIMA , MUNTHU WOYIPA , WOPANDA CHISONI , WOPANDA MANYAZI
Ngat alliance ilipo a pule abwere poyera kut ati akaime pa ballot paper nd ndan ulendo uno?
Ng'oma sound yake ndi mcp
Palibe chanzeru apa
Zikuwoneka kuti mungakhale tsogolo umu
Uyu ndie satana bas
kkkkk lero tavala makaka achipani koma zilko, drama sizithu. tisapusepo apa ndi ngongole, tiyeni tilembetseni zimenezo ndi ndalama zathu.
Rip SKC only God knows😢😢😢😢😢
Watenga a mcp okha okha apa manganya
Politics. Its something one will never understand. 😂
Usi sakuwelenga bible. Munthu wazeru satumikira mabwana awiri nthawi yimozi. Ngati utm ukuyifuna tuluka ku mcp ngati sikuifuna utm khala ku mcp ko ukuganiza kuti marry chilima akusangalala nazo chimene ukuchita. Ifa ya chilima ikutipweteka amalawi munthu inde amakhala ndizifika koma kufa kwa chilima ndi azake cabinet yose yinapanga rigsin ndi president yomwe koma potimanyazi mulibe and amalawi tikuseketera zithu zoduka mutu.
Lero wati avaleko makaka a UTM
Otukwanawa ndi adpp
lero bola mwavalako makaka a UTM
Lero mpaka kuvala za utm mmm koma dzikoli
Utm sichipan inu ,,vote Dad
Kwanu konko
@@AngelinaMzowa napangani zoti Lero mudye bwwnj
Yudasi anapheleka chilima 🤔🤔
Mwayamba liti kumvala za UTM a manganya
Mwana wa Chikangawa
Mwanadi wa chikangawa
Akuziwapo kanthu awa pa imfa yachilima
Power full