Times chichitikileni malilo achilima chinachake pakatipani chachitika ma program anu sakukoma mukuyeneya muzikonze mukuonesa mbali muzochitika zanu Kanakonda ndalamazo mulandile ndipo mudye koma muzima pachilungamo ndipo muzitiuza zoona😔😔
I am waiting 2025 all Malawian tikazavota amene azawineyo ndikukhala president boma limenero ndi lomwe lizachete kafukufuku wa ifa ya anthu amenewa amene anamwalira pa ngozi ya ndege mizimu ya abalewa iunse mumtendere osatha 😭😭😭😭
Ndege yagwera kutali ndi midzi ya anthu yeti it's not far from villegers ndiye iyeyu sanadziwe kuti amanama zosezi ngati alibe choyankhula akhale chete komanso zonsezo zikanati ndi zabwino zokhuza za zosatira za kuchipatala ko bwedzi abanja sanabwere poyera why delay yeti aziti angonenapo izi zokha zinazo azanenabe, presdent wanuyi has something to do ndi imfa ya chilima period
Well come dont forget kuti every accident has acause,car ,motor bike,an aeroplane lets just calm we wiil have good answers dont talk things without umboni because its acrime
Kodi amene akupanga defend chakwelayi amupasa zingati akuona ngati akunamizatu mwana wakwaotu cz zokhuza ngozi zija msagwilise njira yowaseka pakamwa anthu kuti alankhule, komanso funso ndiloti kodi zomwe amapanga a silikali wo zoti tiyeni tikasake ndege uku osati kwinako amawalangiza ndi ndani komanso potumidza anthu nine akasake ndege zimenedzo ukudziona kuti ndi zazeru komanso kusiisidwa kwa kufufuza ndege basi nkhani zonsezo iweyo ndi ukadaulo wakowo sungaone kuti something was off here, let malawian explain there views malingana ndi momwe a presdent anuwo anapelekera uthenga wao unali osagwira.
Taziyayakhurani zanzeruuu ngati ma citizens amalawi bax bzy talking foolish thing yr stupt you tow gys mukuwona ngati mwawinaaa time yovata ikubwerah muzarirah ng,weee😂😂😂😂
Ndipo mukanangosiya osatiuzanso chifukwa chilungamo chili pa Limpopo fm, Bakili tv n Booooon Kalindoooo bas ena nonse mbuzi za anthu zopusa sitikufuna ife
Chilima sangaphedwe chonchija!!🙆🙆🏽🤦.....we have nothing to lose....we are coming
Agalu abodza ife chilungamu tachidziwa muzinamiza ana osati ife amalawi, mwapha anthu afiti inu
Times chichitikileni malilo achilima chinachake pakatipani chachitika ma program anu sakukoma mukuyeneya muzikonze mukuonesa mbali muzochitika zanu
Kanakonda ndalamazo mulandile ndipo mudye koma muzima pachilungamo ndipo muzitiuza zoona😔😔
Report lachani umboni ife tilinawo jacket anamumvula ndani?? Nsapato anamumvula ndani?? Osawopa chakwela wapha chilima umboni ife tilinawo
Kumadziwatu kuti Chilima wachita ku phedwa ndi a MCP,paja mwalandira ndalama a wonder
Ine wonder amandionekera wa mcp aaa
Atolankhani achinyengo awa tonse tikudziwa kuti ndalama za magazi zilizonse ponse
Kachilungamo aka ena sakondwa nako kuzolowela kunamizidwa times mwapamba kugwila tchito yeniyeni thanks
thank you for teaching us guys i agree with we must use our brains
Kodi ndege ndiyomweso inamvula chilima dzovala ?chilingamo mukufuna inuso ndiye chiti chionadi mukuchidziwa
Musavutike umboni tinaupeza kale black box ilikuti nanga maphone alikuti anthu wonse anali ndimaphone ndichifukwa chiyani anali wovulidwa zovala
Andevu zamwayi zanu munadya kale simunganene zoipa za Mcp ayi
Ine zikundidabwitsa Kuti mchifukwa chani akubanja akuti satulutsa report lonse,akubisa chani????? Apatu zangoonetseratu Kuti zomwe anthu ambiri akulankhula Kuti a Chilima anachita kuphedwa,zomwe akupanga a boma kumamanga anthu chifukwa choti akulankhula molira komaso kufusa mafuso pazodabwitsa zomwe zinachitikaso kutsatira ngozi imeneyi
Odziiwa salankhula zambiri amangoti Insha Allah kutanthauza kuti zonse akudziwa ndi mulungu ndipo ndi mwini zonse
Zoona mbale moti anthu wose adakaganiza choncho zikanakhala bwino
Chakwera anapha chilima musatinyase munachita kuwakhapa
Nkhan ndyakut chakwera anamupha chilima ndi anzake mcp ndiyakupha kd chakwera chiyambire kulamura kumalawi ndi ngozi zingat,nanga anamuvura zovara chilima ndan samalani mulungu akukanthan nonse muli pambuyo pa chakwera
Zoona zeni zeni tizaziziwa MCP ikazachoka pampando ndipo sikale.
MUBISE MUNENE IFE TIKUDZIWA KUTI CHAKWERA,ANACHITA PLAN YOPHA CHILIMA MUKUCHWDWA NAWO UMBONI WANU NDIPO CHAKWERA UFA OSANYELA IWE UWONASO
Abusa akudziwawonkha kuti kugwa ndzanja la Yehova ndikowopsa akonda chinyengo asiyeni adzaziwona chimwemwe chawo adyelatu.
I am waiting 2025 all Malawian tikazavota amene azawineyo ndikukhala president boma limenero ndi lomwe lizachete kafukufuku wa ifa ya anthu amenewa amene anamwalira pa ngozi ya ndege mizimu ya abalewa iunse mumtendere osatha 😭😭😭😭
Awanda amzanu munalinawo pa program wa sanati waze asadzabwereso mwamva?
Ife sitikupanga nawo zinamizanani nokha nokha munamaliza amcp ndi kukhapa
Wander ukungonena chakwela mwina kt alindimamina mumutu
Tidzingo koment zachina JB zachina ntanyiwa bakili muluzi TV ndi ena akunjawo bas ife sitidzilemba km ma koment kwaolemba akunjawo bas
Koma osayiwala Kuti mphekesera ili pawiri;
Kukhala yoona
Kapena...
Kukhala bodza😢😢
Mboni yayikulu ndi Mulungu amene anali ku chikangawa amene amawona zonse,la 40 likadzakwana zizaulirika
And mukazilowetsa ndale mukulakwisa because muona ngati lamulo ndi loyipa
Ndege yagwera kutali ndi midzi ya anthu yeti it's not far from villegers ndiye iyeyu sanadziwe kuti amanama zosezi ngati alibe choyankhula akhale chete komanso zonsezo zikanati ndi zabwino zokhuza za zosatira za kuchipatala ko bwedzi abanja sanabwere poyera why delay yeti aziti angonenapo izi zokha zinazo azanenabe, presdent wanuyi has something to do ndi imfa ya chilima period
Anthu kumalawi kuno amasangalala ndimabodza gwelo LA zonsezi ndiumbuli basi
Ndipo ine uyuu wandebvuyi amandiyelamo kobs amazimva nzeru kom ndimbuli yothelatu
mafuso ndiye ambiri choti muziwe vuto mphanvu tilibe bs mthaw yanu
Achitsilu chamunthu a ndevu zatsoka mulungu akulangani inu agalu
Zawusilutu zoti tidzinamizana 😮😮
mabodza ayamba osanena moopa ayi anafa ndi mabala ayi
Azanena akazakhumudwisana 😢😢zitapanga xpire😢😢😢😢
Chachikulu akubanja afotokoza okha zilibwino ndiye makape ena azitengela za ndale chilungamo akubanja achiziwa
Abanja awophyedwa ndi Boma. Zoona zidzadziwika boma likadza sintha.
@@stevezulu2108 naweso ofoyilatu mene adaliri chilima uja anthu akwawo angaope boma ali ndi masapota ambili adafotokoza chilungamo palibe amene angachite naye matha chilungamo ndichimenecho Mulungu akuziwa chilichose
Well come dont forget kuti every accident has acause,car ,motor bike,an aeroplane lets just calm we wiil have good answers dont talk things without umboni because its acrime
Anthu aku ena I inu so kuti mwadya buns ya mcp
Ineso pang'ono ndayambaso kudanwa nazo mmmmm ndalamatu inapha yesu tisaiwale. Athuwa ...........????????
Nde akubitsa chifukwa chani! Or asaneneso zilibe tchito so abitsa bwanji kunena uthenga wenweni 😡😡😡
Etii angotipwetekatsa mtima
Kodi amene akupanga defend chakwelayi amupasa zingati akuona ngati akunamizatu mwana wakwaotu cz zokhuza ngozi zija msagwilise njira yowaseka pakamwa anthu kuti alankhule, komanso funso ndiloti kodi zomwe amapanga a silikali wo zoti tiyeni tikasake ndege uku osati kwinako amawalangiza ndi ndani komanso potumidza anthu nine akasake ndege zimenedzo ukudziona kuti ndi zazeru komanso kusiisidwa kwa kufufuza ndege basi nkhani zonsezo iweyo ndi ukadaulo wakowo sungaone kuti something was off here, let malawian explain there views malingana ndi momwe a presdent anuwo anapelekera uthenga wao unali osagwira.
Olo ingo zisiyani.
Mukundisokosera mukanena zotsatira za kuchipatala mmalo monena zakugwa kwa ndege?!!
Chilungamo chizaziwika basi
Yaaaaa
Mcp yakumpha
Mwapha Munthu
Akubanja anena chilungamo ndipo tadziwa basi otukwanawa ndimowa ndifodya
Ndichifukwa chani akumanga wina aliyense woyankhura fir the whyy
Later kumafufuza
Palibe chotukwana koma akubanja ndi anzeru siopusa koma wanzeeu sangamasure pano kumbukirani pa bingu anafotokoza chinapha bingu???? anthu amzeru amatero kuti mlungu awamenyere nkhondo popeza zachitika kale
Komaso apolisi naonso akuyenera kuphunzitsidwa mokwanira,akuyenera kuti lamulo limeneli alimvetse,asangotumidwa ai
Koma mwina achita bwino kusanena iwowo akubanja ndimtaya makoko .
All of you one day you will pay one by one for what you did to Chilima and others
Chakwera anampha chilima ndemukukamba chani nkunkuyu zikhare ngoma nose muzaziona analakwanji chilima
Agalu inu ngati simukuziwa chimene mukupanga kuli bwino mungokhala sibwino kuyiyimira MCP chipani chamagazi
Inu achina wander dyani ndalamazo ndi chakwera zisiru lnu times palibe chazeru pano
Pa... Pako
Guys Malawi wathapo basi tivomeleze, mpaka wonder kumayankhula moduka mutu
chonchi! Ndiye amene angatiimile ndindani?
Dziko silinathe vuto lilipo ndilakut mumakonda ma negative
Akuyankhula apapa panya pawo ndithu
Uyunso wadya ndalama zaboma
Zoona zidzadziwika MCP ikadza choka Mboma.
Zao izo or cent sidadyepo nde worries what bisani
NDALAMA MDANI WA CHILUNGAMO
Zitsiru Inu mwadya ndarama zochuruka thus why mukuyakhurah zopusaaa
Paja madolowatu adya za MCP sizodabwisa
Izizi nde ndizopoila kuti tizinamizana
Kodi anthu Inu atakhara mbale kapena mwana wanu mukhoza kuyankhula zokhuta choncho
Tizakumana pakachele bola chilungamo tuchidziwa
Umbuli ndikufa nanga kumafika pomagenda m'mdipiti wa galimoto zonyamula maliro pali umunthu pamenepo .
Imeneyoo timayintcha aggressive ndizinthu zopusa mafunaaa tizisekererah inunso umbuli mulinawo cozi mukufusa funso lopusa kwambiri
Chakwela wamupha chilima zasala zosatila Zach
Munagulidwa Ndi mcp agalu inu
Chinyengo ichi agalu inu
Zitsiru izi zinadya ndalama
koma eee msova a dpp
Pano akutiuza zina kusongolokuso azatiuza zina akubanjayoo
Man akubanjawo apasidwa chiseka pakamwa apapa zaoneselatu chifukwa palibe chobisila choona choti chimasule amalawi tathandiza kulila lelo akatibisile alibe chisoni nafe ata ine basi ndazituluka akubanjawo mwina alandila ma banzi
Eee
Taziyayakhurani zanzeruuu ngati ma citizens amalawi bax bzy talking foolish thing yr stupt you tow gys mukuwona ngati mwawinaaa time yovata ikubwerah muzarirah ng,weee😂😂😂😂
Mwaononga kawailesi kanu takasika
Indeeee awonongadi Wailesi yawo pano sitikumvetseranso tasiya kuwadalira
Define assassination
Zopusa chakwera ndiwakupha basi olo Mbiri yake ndinyasa wapha Mia, busa wake reason kufuna mpando
Don't post this .who a u.
Chibanzi😂😂😂😂😂😂
MCP ndi yakupha
leave chakwera alone put the matter in the hand of God
Zachamba ngozi lmavura zovara lnuso madya mabanzi
Anapha ndi chakwera
Zitsiru inu mwadya zakukuyu eti,anthu Ali kunja akulankhula chilungamo ndiye mukuti abwere kumalawi mufuna president wanu wazawaphe kumalawi kuli ufulu panopa pathako panu achina wonder
Kkkkk km anthu muli ndi nkwiyo
Ndipo mukanangosiya osatiuzanso chifukwa chilungamo chili pa Limpopo fm, Bakili tv n Booooon Kalindoooo bas ena nonse mbuzi za anthu zopusa sitikufuna ife
Anthu akakhara ogudwa sasowa kulira kwathu ngati amalawi misonzi yathu ikhare pamutu panu