Amalawi mulungu atikhululukire chifukwa sitimadziwa comwe tikuchita chakwera anatiseka maso ndi mphavu zake wakumidima kt tisamaone ubwino wa peter mutharika koma kunena zoona chakwera alibe masophenya utsogoleri mwa iye mulibe koma mutharika abwererenso 2025 dpp woyeeeeeere chikangawa alongedze adzipita
Comrade palibe cha mzeru chilichonse wachitapo chikangawa ndi amene akufunika mademo a dziko lonse lapansi,peter ndi mtunda 2025 akubwerera osati manyakawa, dzisilu dza MCP ana a satanic
Manganya si munthu ndpo zintchito zake zikuoneka kakuchita kusangalala ndikungolubwalubwa ngati gwape, osamva chison ndi ifa ya mnzako, ine ndee kamandinyasa kwabasi😮😮😮
Ulemu wanu Comrade Ntanyiwa. Kodi Chakwera chomwe akufuna ndichani anapha SKC lero akulimbana ndi chipani UTM. Munthu akupitilizabe kudana naye munthu alikumanda.Manganya ndi Yudasi ndipo a mcp amachitadi kulakhura SKC alipommwepo. Mulungu atimenyere nkhondo ndithu.
Amene anayera kwapangira mademo ndi chakwerayo mumakwena mtanyiwa mafuso a bwino
Mangadya ndi mfiti akusokoneza chipani chikangawa palibe wachita ana ngo bwela kudzaba kuononga ndi kupha Satana weni weni
Palibe chifukwa chomulolera manganya ku covetion
Akamawapatsa nsalu za UTM anthu a MCP ndi cholinga choti aziwoneka ngati a UTM alipo ochuluka omwe ali pambuyo pa MCP, akuzinamiza wokha. Akuzipanga okha chinyengo, ndipo posachedwapa ndikutha kuwona Manganya akusowa kolowera
Borani muthalika kusiyana ndi mfitiyi
Ndipo kwambiri tu mmm
Ndipo Chakwera ndi mbuzi ya munthu
Mulungu salakwitsa kalikose adziwa pomuyika aliyese wokhudxiwa ndi ifa ya chilima
Limpopo fm with comrade ntanyiwa machine bambo
Watumidwa usi ndi mbuzi ya munthu koma utm singathe ayi
Apano ndigone chifukwa nkhanga zomwe ndimadikira zafika 🎉🎉🎉🎉
Chakwela wapha chilima, ndi chakwela
Kodi conversion siyingakapangikire ku tcheu
Ndipo live
Michael usi ndigalu akathera ku convention ya UTM
Chilima mmmmh 😢😢 kufa imfa yosadziwika bwino, chipani chake nkumachilondanso akufuna chani kwenikweni a MCP wa?????
Wicked world, satana ndi olephera
Chikangawa ndiwoyenera mademo😢😢😮
manganya ndimunthu oipa tikuonerani patsogolo uzazindikila
Ntanyiwa sadzatheka pa Limpopo fm
Waiting for the chikangawa report
Palibe chobisika pansi pa thambo
Sindife wokhutira ,ataaa pang,ono
Voti ili mu mtima osati mu chovala cha chipani, SKC and 8 others mhsrip 😭😭😭
Tafika kale Mr ntanyiwa lreland
Ndikutha kuona magazi ku UTM
Onse amayenera kumangiridwa ma demo sakukhonsa onse vuto anthu timayiwala zakumbuyo timakumbukila zanthawi yomweyo yangolakwa ndi infa tima funa kuyeza utm awiriwa alephera
amalawi tinazitemberera tokha kumuchotsa Peter Mutharika ndikumuyika satana pampando lero akutipha taonani amalawi anzanga
koma ndikuona ngat kukhuta komwe timkakhuta ndi apeter Mutharika muja
Paja amkati akufuna asitha ndiye asithaditu
Peter was good
Ndikuupempha Mzimu wa S K chilima ukuvutitse manganya. Asagone tulo mtenderenso asaupeze mpaka imfa yake
Tinazimbidwa ndikukhuta nthawi ya Peter ija lero ndizimenezi kkk
Yofunika apo ndi step down achakwera atule pasi
Oyenera ma dem ndi chakwera
Amtanyiwa mudzapatsidwa u minister mu m,boma LA dpp
Chakwera ndiye afunika ma demo
Athetsa chipani chake cha odya zake alibe mlandu UTM singathe akunama kwambiri kafula ameneyu ndipo zimuonekera asowa kolowera amenewa
MCP ndi makape tithana nawo manganya akudziwapodi kanthu.Mai kaliyati pachilomwe timati chonsamva anachiphikila muliponda musapite kulilongwe
Amalawi mulungu atikhululukire chifukwa sitimadziwa comwe tikuchita chakwera anatiseka maso ndi mphavu zake wakumidima kt tisamaone ubwino wa peter mutharika koma kunena zoona chakwera alibe masophenya utsogoleri mwa iye mulibe koma mutharika abwererenso 2025 dpp woyeeeeeere chikangawa alongedze adzipita
Chakwera ndi APM onse ndi olephera, dziko la malawi likufunika new blood.
Manganya usatilakwitse chonde yendelani zanu.
Chakwera ndiye akufuna ma demo
Tazindikula amalawi kuti manganya siwa UTM 😂😂😂😂
N kape akulamulirai APM tinamulakwira
Mukuchedwa palibenso zama demo boma ndilomweli la Dr Lazarus maccarthy chakwera,simunganene zoti mademo muwayamba lero,mademo mwakhala mukupanga kale inu a dpp zaka 4 zonse boma la MCP likulamulira kuzera kwa Boni kalindo,koma Amalawi ndi anthu wozindikira kuti akumatumidwa ndi dpp,mukungovutika Mcp ikutengaso boma oloko chisankho chitachitika lero.
Manganya ndi wasataneki,mzeru zake zikufanana ndi kufupika kwa msinkhu wake
Manganya. Usamale. Nthawi. Yako. Yatha. Unanpeleka. Chilima. Usamale. Kwambiri. Usadzitame
Zonsezi God is the judge, don't worry
Manganya galu chitsiru. Unafupika ndi nzeru zomwe.
The answer is we don't want lomwe people to rule us anthu ozikonda kwambiri
Ine ndimaona ngati manganya ndi Munthu wabwino koma uli Dyabulosi weniweni mwana wa Satan 😢
that's the fact black or white without manganya chilima ndi Raphael sadakafa, munthu oyipa kuposa hetra 😢
Chakwela mbuzi yamuthu chikangawa alibe zelu zaku yendesa boma mbuzii
Ka michel usi ko nkachitsiru kwambiri
Antanyiwa mukumuyelekeza president muthalika ndi mbuzi iyi yilipoyi?muthalika ndakatundu osayelekeza ndi thelele lilipoli
Comrade mmmmmmm ulind bodza 😂😂😂😂😂😂 mpaka nkhan ya degree yafika kumeneko
Apa ndiye panja peni peni
Ayi. Ife. Sitikukhutira. Uyu. Ndi. Oyipa. Kwambiri. Chakwerayu.
Mr president mtanyiwwa ulemu wanuw km munkushedwa ndilipoti llandege bwanji
Ndi lerotu😂😂🎉
@@Yoxym we've been 200 in ons to withng the nganga sawona lipopo from yesterday antill now on please mtanyiwwa ☝️🙏
Vuto nonse amene mumakhala ngat a utm si ndinu ,ndinu a dpp
Chidule antanyiwa tipangira chakwera mademo
Mr chikangawa ndiyemwe akuyenela kupangilidwa mademo eeee uyu watizuzatu
Amane amayenera mademo amphamvu ndi chakwera
Ausi akufuna kufa naye
Amenenyu wachikangawayu ndiye akufunika mademo chikangawa
Manganya unaphesa chilima nyini yamako😢😢😢
Yeni yeni😢😢😢😢😢
Ndipo machende ake ozendewera pansi manganyayo ndi chikangawa party
Vuto a malawi munaika chitsilu pa mpando, munthu kumtola chipiku mpaka pulezidenti?a malawi sitinali serious ngati dziko
Wonse palibe wabwino wonse wali ndi mavuto ofanana.
umakwana comred auzeni anthuwo
Ngati akub madigili anthu ena mosiyeni naye afa ngati chilima tili popano ndithu
Tiuze zoona MTANYIWA
Comrade palibe cha mzeru chilichonse wachitapo chikangawa ndi amene akufunika mademo a dziko lonse lapansi,peter ndi mtunda 2025 akubwerera osati manyakawa, dzisilu dza MCP ana a satanic
Tinataya nthawi.2020 .kupanga.masankho
Mayiko usi mutu mwake mulibe dzelu mumayenda mazi okhaokha
Kma chikangawa sunzatheka iweo👉👉
Lusiyasi ujaso ana chita kumupha kuti ti iwale ifa ya chilima Abanda ana chila
True he knows how Chilima killed manganya Utsi he failed to go n visit n see where Chilima n 8 others killed shame
Alomwe mwayamba liti kumukonda chilima anthu oyipa inu
Manganya ndi mbuzi ndikufupika kwake Kuja galu amene uja
Akazafa chakwela ndi manganya ndizasangarala
Chifwamba ndi usi
Peter muthalika ndiyamen tingamenyele khond
APM Sadayenele kuchitsedwa pa mpando pano tikuvutika Zedi.
Ndipo zomvesa chisoni kwambiri
Sizinakhare bwino
Palibe cha nzeru chachitika katundu wakwera mitengo ma business tinaduka
Can't wait kumva report Mr mtanyiwa.
Tingakondwele ndi munthu opha anthu chingawa ife ayi
Oyenera ndi chikangawa Peter inali nsanje chabe
Ndipo zinari za against esh
APM tinamulakwira mfumu
Waiting for report ku fm ntanyiwa🔥🔥🔥
Chikangawa watikwana kwambiri
Basi busy kuipitsa mbiri ya anthu mupindulanji
Kodi ndani asakuziwa kuti UTM inachoka mumgwirizano,
Ndichifukwa chiyani akugwilisa nsalu za UTM
Michael Usi usamalise ndi unthira kuwiri wakowo, omweo ukudya nawo iwe mkumasangalala adzakupha.
Devil at work 👹⚒️🔨⛏️⚒️👹
Chikangawa achoke
Mcp chipani chokumpha 2025 pack and goo with you manganya
Ndipo sangawine awa straight tu
Chikangawa
Usi ndi wa MCP, Chakwera achoke APM pachiongolero APM boma
Micheal Usi akuziwapo kanthu pa imfa ya Chilima polonjezedwa kuti apasidwa u vice president
Chidanti malunga ndi galunso
Kumalawi anthu ndi atulo kwambiri akanakhala maiko ena chikangawa ndi NDUNA zake atathamangitsidwa kale pampando
Usi ndi wa mcp osati utm asatiputsitse ife palibe chimene anapanga kumwalira kwa chilima
Manganya si munthu ndpo zintchito zake zikuoneka kakuchita kusangalala ndikungolubwalubwa ngati gwape, osamva chison ndi ifa ya mnzako, ine ndee kamandinyasa kwabasi😮😮😮
Sizitheka Manganyayo akatenge amake ndi azilongo Ake akawasiye Kuchikangawa kwakeko