Ya mwalankhula bwino kwambiri koma chimodzi mwaiwala ndikuoona ngatiso A DDP amphunzile kulemekeza NDi kutopa anthu omwe amawasankha chifukwaso amakhala NDi kusimbwa kwambiri kunenna zoona NDi amene anayamba kuliponya dziko la Malawi pamoto
Nannuso adpp mwatengela inuyo mmene mnalandila boma ku udf basi mkuonaso ngat mcp alanda boma kwa inu daily alomwe zokamba kamba si ufumu ayi ili ndi dziko
Ndipo times radio ndiyomwe so amathandizaso kumenya campaign lero it's your turn walakwa Jim Brian musiyeni nthawi ya Dpp anali ndi kasakula kusambwadza Dpp a atseka radio ndindani asiye matola nkhani osamwopseza ayi
Tathokoza chifukwa chachilimbikitso chanu kwa chipani cha DPP pamodzi ndi a Malawi onse. Komanso mwayankhula mosonyeza kulikonda dziko lanu . Kuwalilira a Malawi pamaso pa Mulungu Namalenga
True Son of Malawi, MCP has captured even judiciary just as Zuneth satter did with Malawi Government. How can a court injuction be greater than constution.?!
mavuto aku chipani chanu asatikhudze. a Malawi mwawafuna lero, muli m'boma munkava za munthu? si aja mumagula zikwanje kuwapatsa anyamata aziwopsyeza otsutsa boma?
So touched, MCP ndi ma coward awa boma anachita chooanda ili Kuba komwe sitinawonepo kuwononga dzikoli kodi alamuli 10yrs basi dziko latha po sure.. Anthu awa a choke before it's 2 late anthu kusamva mwaziona tsopano zipatso🙌🙌🙌
So so so very true sir God Bless you for this revelation. Chomwe munthu amadzala ndi chomwe amakolola. There's no forever money, richness, and flavored life. Time will tell. They think they are in Heaven with poor peoples money but they living in hell.. Yes time will indeed tell. Busy pleasing lucifer but lucifer has his own time. People are having sleepless nights praying. We are praying every poor person is praying. Mulungu amakhala chete. Very soon they will see. God will rise for us. MCP ndiyodzadza ndi mbava, akhupha ndi afiti.
Olo apasidwe ndalamazo sangawinebe .DPP ikakanidwa mojority sizavota. Mcp izazivotela yokha
Koma inuyo mmene mukuwonela ndichipani kapena munthu uti amene angakoze dziko lamalawi kuti tisavutike chifukwa dpp idatizunza lelo mcp.ikutizunzaso.
Ya mwalankhula bwino kwambiri koma chimodzi mwaiwala ndikuoona ngatiso A DDP amphunzile kulemekeza NDi kutopa anthu omwe amawasankha chifukwaso amakhala NDi kusimbwa kwambiri kunenna zoona NDi amene anayamba kuliponya dziko la Malawi pamoto
Aaah iwe be serious
Powerful talking that's real, keep it up thank you so much Biggy 🔥🔥🔥🔥
Nannuso adpp mwatengela inuyo mmene mnalandila boma ku udf basi mkuonaso ngat mcp alanda boma kwa inu daily alomwe zokamba kamba si ufumu ayi ili ndi dziko
Ndine oyamba akulu mukunena zoona thawi ya piter anthu ambili amabwebwetuka amabungwe amipingo koma lelo kùli zii Ali ndi mbali yawo
Akuona Ngati akhala muyaya pampandopo
Indee
Ndipo times radio ndiyomwe so amathandizaso kumenya campaign lero it's your turn walakwa Jim Brian musiyeni nthawi ya Dpp anali ndi kasakula kusambwadza Dpp a atseka radio ndindani asiye matola nkhani osamwopseza ayi
And all departments have captured including some judges
Tathokoza chifukwa chachilimbikitso chanu kwa chipani cha DPP pamodzi ndi a Malawi onse. Komanso mwayankhula mosonyeza kulikonda dziko lanu . Kuwalilira a Malawi pamaso pa Mulungu Namalenga
Mwalankhula chilungamo chokha_ chokha ndipo Ambuye atipulumutse , atichotsele boma lankhaza limeneli
Ndipo zovetsa chisoni kwambili kutengela ndimene dzikoli athu ife tikuvutikila 😢😢 ndipo mulungu akuona adzalipila misozi yose mmm chosadziwa ndipo tikanadziwa sitikanavotela m,busa chakwela
Allah ndye yakho, sachedwa en safulumira.
In sha Allah
True Son of Malawi, MCP has captured even judiciary just as Zuneth satter did with Malawi Government. How can a court injuction be greater than constution.?!
Aaaa kutemberera mupita ndinu kumasano
mavuto aku chipani chanu asatikhudze. a Malawi mwawafuna lero, muli m'boma munkava za munthu? si aja mumagula zikwanje kuwapatsa anyamata aziwopsyeza otsutsa boma?
Dzikoli ligulitsidwe tigawanepo ndalama aliyense aziona kwake kolowela, Atsogoli azipani ambili mitu mwawo muli manyi.
MCP ndiyankhaza kwambili
Big mukuyankhula momveka pitilizani kutiimilira akusowa ofotokoza chilungamo ngati inu
Komatu mukuliladi akulu. Dpp inatizuzatu inu munali kuti. Lero inuyo ndi anzeru kkkkkkkkk. Zomwe mwalankhulazi ndi zofuna za mtima wanu ndipo muchedwa nazo.
CHISIYENI CHILUNGAMO CHIYENDE NGATI IMFA COZ IMFA IKAFUNA KUTENGA MUMTHU SIIONA KUTI PALI ADOTOLO ,ASIN'GANGA,WA CHITETEZO WAMFUTI AYI IYO IMAYENDERA LAMULO LA AKALIMAUTI
Kulankhula kwanzeru kosonyezq kt munthu alindi unongo
Ndiye ukulankhulazi ukufuna ife titanii ingopita ku Parliament ukalankhule kumeneko
Koma nthawi nkachutsiludi. DPP kulira Lero?
Ndpo malemla uja Mene amavutila kupaliament eeeeee Koma lazalo. Watienjeza asaaa Maka chinankhumwa
just like the way people stoped tuning to mbc, zodiak they will also stop tuning to times
Apm ndi boma liti inu ndinu a bolzano eti dpp its a family
Party kulibe democracy kuja
Ndi a mcp amenewo si adpp akanakhala adpp akanatulukanawoso zimene ndi mbuzi za mcp
Eishhh may the good LORD Bless you Brother, Mulungu amenye yekha nkhondoyi anthu akuzunzika kwambiri
Koma afumu mumatha kulankhula ndinu Number one
Ndikupemphe mbale wanga kuti upitilze osamva akhale choncho ambuye azikudalisa you are very strong i support you
Uko nkulila kwa cadet
Mwana wazeru iwe God bless you
May God bless you my brother
Koma nkulu uyu ndiye walatsa ntchende garutu, zonse zomwe wanyakhula apapa sananyike ayi mbari zonse zonse
So touched, MCP ndi ma coward awa boma anachita chooanda ili Kuba komwe sitinawonepo kuwononga dzikoli kodi alamuli 10yrs basi dziko latha po sure.. Anthu awa a choke before it's 2 late anthu kusamva mwaziona tsopano zipatso🙌🙌🙌
Brian banda should just open his own Radio. A chunga kaya enawo nanga zimene akukapamba ndizomveka..
Kulibe chanzelu chomwe ukunena iwe zinayamba lelo zimenezo ungofuna ndalama galu iwe khala chete Malawi niotembeleledwa bwasi
Amalawi nthawi zose timakoza zinthu zitafika posauzana ndipodi ndipo mulungu akupenyelera zosezi kubuula kwanthu ndikunkhulupira kukuveka kwa mulungu ndipo anthandizana nafe
Komatu a chakwera inuyo mukudziwa anthu akulira misozi yamagazi kamba kainu? Ndithu mulungu womoyo akukathe Amen
So so so very true sir God Bless you for this revelation. Chomwe munthu amadzala ndi chomwe amakolola. There's no forever money, richness, and flavored life. Time will tell. They think they are in Heaven with poor peoples money but they living in hell.. Yes time will indeed tell. Busy pleasing lucifer but lucifer has his own time. People are having sleepless nights praying. We are praying every poor person is praying. Mulungu amakhala chete. Very soon they will see. God will rise for us. MCP ndiyodzadza ndi mbava, akhupha ndi afiti.
Man mwayankhula monveka bwino ndithu I hope kuti Time radio yanva ndithu
Very useless Malawi
Ulibe fundo
Following bro ,
Mawu amphamvu
Sir ,Mulungu akutsogolereni this is a very good speech .
True talk
Glory to God,His time is coming when He shall rescue malawians
Eishiiiiiiii brother keep it up well explained eeeeeeeeeeeee ndipo auzedi zenizeni ❤❤❤❤❤❤❤❤❤
Amcp akuopa mutharika ndi mlona akusokonedza ku dpp
Mwalankhula bwino Ambuye Akdalitssni
Ambuye timenyereni nkhondo mdziko la Malawi
Ndizoonad bwana wanthu akulira ndimavuto 😢😢😢
Kuyankhura mwamphamvu komanso mwanzeru ❤🎉
Kuyakhula kwabino❤
Eeeee koma lelo ndiye mwalatsadi abwana
You are taking my Brother Very true
Mwanena momveka bwino achimwene
Hara akuchitidwa control
God bless you sir, great revelation.
Very Brave, big up Brother
Zonazale mukulankhulà zoona
Indee mukunenazi zoona ndithu
Mau abwino kwambiri ❤❤❤❤❤
Brian Banda amatitsegula m'maso musamupinge pinge
❤❤❤❤❤
❤❤❤❤❤
Mau a mphamvu comrade
Adzayamkhadi sure
Powerful words bro
Dpp my vote
Kulira kwathu mulungu akumve
kumene mulungu akuona
Atani atani APM ndi bomaaaaaa basi boss umatha kunena Chilungamo zedi❤❤❤❤
Thanks for your powerful revelation Sir, 🙏
Lucius banda lero akumanandi ndithu mulungu
True man of GOD