Bon Kalindo lero pa 11 July kufotokoza mopanda kuopa aliyense - “MUNDIMVA NDIPO SINATI”

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 19 окт 2024

Комментарии • 81

  • @ReginaKaingana
    @ReginaKaingana 3 месяца назад +5

    More fire mukutiimilira bwana! Ife timasowa mpata oyankhura zakukhosi kwathu. God bless you and protect you. Amalawi tikuvutika

  • @EversDman
    @EversDman 3 месяца назад

    Bon kalindo wathu wathu 🔥🔥🔥💯

  • @LuyoloTlhapane
    @LuyoloTlhapane 3 месяца назад

    A pule athu ❤❤❤god protect your mr born mmatiimilila

  • @CARLOSKAMANGA
    @CARLOSKAMANGA 3 месяца назад

    Ulemu wanu big❤❤❤❤❤

  • @PeterKasiya
    @PeterKasiya 3 месяца назад

    Boniiiiiiiii kalindoooooooooo Mwana owopswa kwambili

  • @MomeryPhiri
    @MomeryPhiri 3 месяца назад

    ❤❤❤❤❤❤❤ love it

  • @FlorryVugy
    @FlorryVugy 3 месяца назад

    A president Bon mumatiyimilira😂😂😂😂😂 Sikusinja ndi gwenembe😂😂😂😂

  • @DauglassNkhoma-dj9lp
    @DauglassNkhoma-dj9lp 3 месяца назад

    😂😂Boni kalindo wangadula kkkkk boooo towopa kubwelako kumalawi

  • @JowasiMasina-fy8ji
    @JowasiMasina-fy8ji 3 месяца назад +1

    Mukazava kuti boma lawanyera ndi zimenezo anavako kuti Koma Malawi ayi ndithu komaso kamuzu samapaga zimenezo ayi amati zithu zikamakwela iyeyo amakambolana ndi anuwake kamphani kuti atsitseko anthu ake alibe ndalama ndiye inu mukuzitega bwanji zimenezo kodi dziko la Malawi mwalitani tamakumbukirani komwe munali azanufeso tikuva kuwawa ngati munkhavera inu muja kuli mulungu kumwamba zonse mukupagazo akuziwona ndithu tsiku lina lidzakwana la 40👏👏

  • @ZayileMkhala
    @ZayileMkhala 3 месяца назад

    Zoona amwene

  • @neemahkapatamoyo9563
    @neemahkapatamoyo9563 3 месяца назад

    Kkkk koma abare zowona mchenga omwewo omwe analenga Mulungu mwini nthaka zowona mpaka kumagulitsa ayi zikomo dziko ili 🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌

  • @LoganKulupando
    @LoganKulupando 3 месяца назад +1

    bon kalindo sukunama luchenza. Lijoni ikupanga khazakwambili longopackngi 1ooooo u lube amakumanga kuselo

  • @AlgentChilanga
    @AlgentChilanga 3 месяца назад

    Ndipangeso replay pakanyimboko kandisangalasa bwanji kkkk koma uyu ndi pangolin 😂😂😂😂😂😂

  • @JoeMatiya
    @JoeMatiya 3 месяца назад

    Inu ndinu Muthu wankulu kalindo Bon mumakwana

  • @FarookRaphael
    @FarookRaphael 3 месяца назад

    More fire komanso mukuyankhula ngat chinyanja service channel Africa

  • @nicholasmutano6017
    @nicholasmutano6017 3 месяца назад

    Uyuyu ndi mandrax sichamba, akufuna titani tilowele kuti si misala iyi?

  • @AlgentChilanga
    @AlgentChilanga 3 месяца назад

    Awa ndi machine poyankhula the DC mwana wowopsya kwambiri 😂😂😂

  • @AffickChaona
    @AffickChaona 3 месяца назад

    ❤❤❤❤❤

  • @PeterMaulana-qk5uq
    @PeterMaulana-qk5uq 3 месяца назад

    Ooh...ambuye dalisani anthu amene akumenyela ufulu m'malawi chonde musalore kt mbava za mcp zilamulire dziko lathuli AMen!!

  • @PrinceBlessings-bv5bs
    @PrinceBlessings-bv5bs 3 месяца назад

    😂😂😂😂😂 lero wayaka moto kalindo❤❤❤❤❤ a opposition please chitanipo kanthu awawa aikanika dziko olo manyazi alibe

  • @SydneyMwale-u9w
    @SydneyMwale-u9w 3 месяца назад

    Aaaaa yai awawa akufuna kuti tiyiwale kunlankhula za chilima.
    Agalu a anthu ndithu

  • @ShupikaiBelloh-z7l
    @ShupikaiBelloh-z7l 3 месяца назад

    Awa ndie mawu

  • @RhodaKalumbi
    @RhodaKalumbi 3 месяца назад +1

    Kkkkkkkkkk ana ofewa odya mipungu nthawi ya mayeso apolice akungosilira

  • @BernadettaTengula
    @BernadettaTengula 3 месяца назад

    Koma ine uyu ndimasowa pomuyika ,,ati chifukwa cha udindo😂😂😂

  • @NdawaPhillipfortunePhakatie
    @NdawaPhillipfortunePhakatie 3 месяца назад

    Motor 💥 kalindoooo

  • @EllinaBitto
    @EllinaBitto 3 месяца назад

    Bulaza wathu❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤

  • @FrankMilias-og3js
    @FrankMilias-og3js 3 месяца назад

    Kulankhula mosaopa nyooo sss winiko

  • @UthmanKapungu
    @UthmanKapungu 3 месяца назад

    Fire!!!!!!!!!! Bon kalindo nazoni tatopa ife

  • @BlessingsKalonga
    @BlessingsKalonga 3 месяца назад

    Aliyese ndi wakuba koma kusagwidwa Judgement day tidikire oweruza

  • @ThokoJanuary
    @ThokoJanuary 3 месяца назад

    Ai zikomo 🥱

  • @SmartMoles
    @SmartMoles 3 месяца назад

    Zofunikila kulangura mwayangure kumene

  • @JoyceChitsulo-mw7wg
    @JoyceChitsulo-mw7wg 3 месяца назад +1

    Makosana apa nde mwapita

  • @RamseyWasi
    @RamseyWasi 3 месяца назад

    Blasa,
    Malawi saadzatheka mpaka kale kale. This is my second SMS to you mr Dangerous Child (DC)
    My opinion:
    Kungosiiya utsogoleri wa anthu osawukawu.chfkwa or titatan,kusawukaako sikudzaatha.

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 3 месяца назад

    Mpakana tizigulisana mchenga wamudziko lathu zoona?, kusavukatu uku sopano aati!?, chaza ndiyan choti tizikhala ndi linces yovuwulila mchenga ?, ndepoti amalawi mumkafuna kusintha zinthu , zimene mumkafuna kwa abusa zija mzimenezi😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂❤❤ , mo 🔥🔥🔥🔥🔥🔥 mcp kkkkkk

  • @directorkfuture118
    @directorkfuture118 3 месяца назад

    Ameneyo asamwe mowa 😂😂😂

  • @TshepoModise-xs4qu
    @TshepoModise-xs4qu 3 месяца назад

    Koma nkhaza zake mpaka licence ya mnchenga Mmmm zovuta bwanji eeee

  • @BlessingsKalonga
    @BlessingsKalonga 3 месяца назад

    Ubwino wake ukuzimenyera wekha khondo uzalemera wekha

  • @VincentMalika-w7x
    @VincentMalika-w7x 3 месяца назад +1

    Ndipo eeeeee tikudziwona kuno tikulemba mayeso apolici ache akupemphaso dzokudza zakudya zath

  • @gerrardgladstone2473
    @gerrardgladstone2473 3 месяца назад

    Akuti kufuna kumangidwaaaaa 🤣🤣🤣

  • @PeterGrant-ih1sr
    @PeterGrant-ih1sr 3 месяца назад

    Athuawa atakhala alipo okwana 4 ziko muno athuwa atasitha ndithu😂😂😂😂

  • @FwasanMwenefumbo-zq7sg
    @FwasanMwenefumbo-zq7sg 3 месяца назад

    The DC 🔥

  • @GiftMvula-u7t
    @GiftMvula-u7t 3 месяца назад

    😂😂😂😂 mpaka muchenga license

  • @DaudiAbdullah-o5l
    @DaudiAbdullah-o5l 3 месяца назад

    Mumatiyimilila

  • @ikmusic-s9f
    @ikmusic-s9f 3 месяца назад

    koma nde eeee mpaka licence mchenga

  • @D.RJALLI-qo6yd
    @D.RJALLI-qo6yd 3 месяца назад

    Ine ndikudana ndi ma opposition akumalawi ndi agalu kobasi makamaka dpp ikungoyang'anila wosalangula khatu kumbonà lamasuso ngati ili ndiye boma adzalipesa bwanji dpp tadzukani ife tampudzilapo ndipo talapa mamisiteki athu bwelani nditu mutiwombole kwa agalu awa

  • @EdwardMukholi
    @EdwardMukholi 3 месяца назад

    Kkkkkkkkkk koma chakwera ndiye ndiye zikuchoka kuti zimenezi

  • @ChrispinEdward
    @ChrispinEdward 3 месяца назад

    Bwanawe pafika boma umuthu walimbe akungo funa kumupanikiza Muthu osawuka kut azikhala ndima strees bas komano azidikile kut Pali mwambi waphala lakaka ukaza fika pomva kukoma limakhakut lathamo mupoto

  • @HelenamoisésLisboaMoisésLisboa
    @HelenamoisésLisboaMoisésLisboa 3 месяца назад

    Ambuye akudalitsen

  • @MathpeterLemon-ls1ns
    @MathpeterLemon-ls1ns 3 месяца назад

    Ati kutitola kapena chani

  • @ChisomoamitoniSauzandeamiton
    @ChisomoamitoniSauzandeamiton 3 месяца назад

    bwana ng'alurani ndithu tili nanu nanu

  • @PearsonSalima
    @PearsonSalima 3 месяца назад

    Dc

  • @South2023-x2o
    @South2023-x2o 3 месяца назад

  • @GraceChilunga
    @GraceChilunga 3 месяца назад

    Koma amalawi tinalakwanji kt tizunzike,,,galu uyu wazunza miyoyo ya anthu osalakwa,,chitsiru cha m'busa munthu opanda conscious

  • @Shelifibraheem
    @Shelifibraheem 3 месяца назад

    Big up bro

  • @pempheroraynnoxmpesi8713
    @pempheroraynnoxmpesi8713 3 месяца назад

    😂😂😂😂msusi olo nthuli amatayapotu a dpp

  • @sir-wanton-2001
    @sir-wanton-2001 3 месяца назад

    Kkkkk Kkkkk uyu akazankhala president azamujaje nda uyu ndi dolo

  • @ericlarks8165
    @ericlarks8165 3 месяца назад

    ,🔥🔥🔥🔥

  • @HendersonDziwa
    @HendersonDziwa 3 месяца назад

    Dzelu zachepa kkkk

  • @CarolineSululu
    @CarolineSululu 3 месяца назад

    Koma uyu inu kkkk ati apolice osilila mpunga wa nyama 😂😂😂😂 ayi zikomo

  • @YonaMartin-kb3do
    @YonaMartin-kb3do 3 месяца назад

    😂😂😂😂 akavoterana ndi amawo yemweyo kupuma palibe

  • @maxwellcaptain3937
    @maxwellcaptain3937 3 месяца назад

    Kalindo samaopa😂😂

  • @CaptainNyenga
    @CaptainNyenga 3 месяца назад

    😂😂😂😂😂 koma DC

  • @lytonmaseko4534
    @lytonmaseko4534 3 месяца назад

    😂😂 kung'alulatu

  • @AaronLitete
    @AaronLitete 3 месяца назад

    Kkkkk boma lopusa

  • @benjulius6070
    @benjulius6070 3 месяца назад +2

    😂😂😂😂😂😂

  • @JuliusMunthali-z7j
    @JuliusMunthali-z7j 3 месяца назад

    Awuzeni

  • @wangachindeya8577
    @wangachindeya8577 3 месяца назад

    Bigiliman naweni

  • @AnthoniohMazengera
    @AnthoniohMazengera 3 месяца назад

    Hahahahahahahahahaha😂😂😂

  • @GiftKulture
    @GiftKulture 3 месяца назад

    🤣🤣🤣🤣 mipunga

  • @Aluwenkareem-ev3ro
    @Aluwenkareem-ev3ro 3 месяца назад

    😂🤣😂🤣

  • @PhillipMtonga-g7o
    @PhillipMtonga-g7o 3 месяца назад

    🤣🤣🤣🤣🤣🤣 zamanyazi kuntonse alliance

  • @BenjaminKayembe-j7j
    @BenjaminKayembe-j7j 3 месяца назад +1

    km eeee awawa ndsbwsna gayz mmmmmm amakwana km

  • @CollenChapenda
    @CollenChapenda 3 месяца назад

    K.K😂

  • @YohaneMbewe-u4k
    @YohaneMbewe-u4k 3 месяца назад

    😂😂😂😂

  • @ReubenDshaba
    @ReubenDshaba 3 месяца назад

    😅😅😅😅

  • @Kachelephiri
    @Kachelephiri 3 месяца назад

    Awa.akulila.ayesetse.2025.azawinekwawo.ump.kwawo.kma.ngatiakukanakwawo.ndiakanene.jilose.tingamuvele.galu.wachabechabe.

    • @ChristopherKawilam
      @ChristopherKawilam 3 месяца назад

      Uku nyoza bon kalindo,, zeru ulibe iwe uku Kanika kulemba kumene galu iwe

    • @ChristopherKawilam
      @ChristopherKawilam 3 месяца назад

      Yamba wapita Kaye Ku school ya mkaka uziwe kulemba...... galu iwe

  • @myheartforkids2876
    @myheartforkids2876 3 месяца назад

    😂😂😂😂😂

  • @ZioneNyirenda
    @ZioneNyirenda 3 месяца назад +1

    😂😂😂😂😂😂

    • @Em-Dazo
      @Em-Dazo 3 месяца назад +1

      😂😂😂😂😂😂😂😂