Bon Kalindo lero pa 11 July kufotokoza mopanda kuopa aliyense - “MUNDIMVA NDIPO SINATI”

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 8 сен 2024

Комментарии • 81

  • @user-ix2ux5ss1b
    @user-ix2ux5ss1b Месяц назад +5

    More fire mukutiimilira bwana! Ife timasowa mpata oyankhura zakukhosi kwathu. God bless you and protect you. Amalawi tikuvutika

  • @EversDman
    @EversDman Месяц назад

    Bon kalindo wathu wathu 🔥🔥🔥💯

  • @PeterKasiya
    @PeterKasiya Месяц назад

    Boniiiiiiiii kalindoooooooooo Mwana owopswa kwambili

  • @MomeryPhiri
    @MomeryPhiri Месяц назад

    ❤❤❤❤❤❤❤ love it

  • @LuyoloTlhapane
    @LuyoloTlhapane Месяц назад

    A pule athu ❤❤❤god protect your mr born mmatiimilila

  • @user-xm5cq1fb8g
    @user-xm5cq1fb8g Месяц назад

    Ulemu wanu big❤❤❤❤❤

  • @JowasiMasina-fy8ji
    @JowasiMasina-fy8ji Месяц назад +1

    Mukazava kuti boma lawanyera ndi zimenezo anavako kuti Koma Malawi ayi ndithu komaso kamuzu samapaga zimenezo ayi amati zithu zikamakwela iyeyo amakambolana ndi anuwake kamphani kuti atsitseko anthu ake alibe ndalama ndiye inu mukuzitega bwanji zimenezo kodi dziko la Malawi mwalitani tamakumbukirani komwe munali azanufeso tikuva kuwawa ngati munkhavera inu muja kuli mulungu kumwamba zonse mukupagazo akuziwona ndithu tsiku lina lidzakwana la 40👏👏

  • @DauglassNkhoma-dj9lp
    @DauglassNkhoma-dj9lp Месяц назад

    😂😂Boni kalindo wangadula kkkkk boooo towopa kubwelako kumalawi

  • @user-kk4uj8ko8k
    @user-kk4uj8ko8k Месяц назад +1

    bon kalindo sukunama luchenza. Lijoni ikupanga khazakwambili longopackngi 1ooooo u lube amakumanga kuselo

  • @neemahkapatamoyo9563
    @neemahkapatamoyo9563 Месяц назад

    Kkkk koma abare zowona mchenga omwewo omwe analenga Mulungu mwini nthaka zowona mpaka kumagulitsa ayi zikomo dziko ili 🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌

  • @user-zt3gv7md6x
    @user-zt3gv7md6x Месяц назад

    Zoona amwene

  • @user-be5fc3ed1i
    @user-be5fc3ed1i Месяц назад

    Ndipangeso replay pakanyimboko kandisangalasa bwanji kkkk koma uyu ndi pangolin 😂😂😂😂😂😂

  • @user-hx6jl2jq9j
    @user-hx6jl2jq9j Месяц назад

    Aaaaa yai awawa akufuna kuti tiyiwale kunlankhula za chilima.
    Agalu a anthu ndithu

  • @FlorryVugy
    @FlorryVugy Месяц назад

    A president Bon mumatiyimilira😂😂😂😂😂 Sikusinja ndi gwenembe😂😂😂😂

  • @FarookRaphael
    @FarookRaphael Месяц назад

    More fire komanso mukuyankhula ngat chinyanja service channel Africa

  • @user-dj6rc3lc4t
    @user-dj6rc3lc4t Месяц назад

    Inu ndinu Muthu wankulu kalindo Bon mumakwana

  • @AffickChaona
    @AffickChaona Месяц назад

    ❤❤❤❤❤

  • @user-hq8fw5hz2l
    @user-hq8fw5hz2l Месяц назад

    Awa ndie mawu

  • @PeterMaulana-qk5uq
    @PeterMaulana-qk5uq Месяц назад

    Ooh...ambuye dalisani anthu amene akumenyela ufulu m'malawi chonde musalore kt mbava za mcp zilamulire dziko lathuli AMen!!

  • @BernadettaTengula
    @BernadettaTengula Месяц назад

    Koma ine uyu ndimasowa pomuyika ,,ati chifukwa cha udindo😂😂😂

  • @user-dm6xq6cp1m
    @user-dm6xq6cp1m Месяц назад

    Ai zikomo 🥱

  • @user-be5fc3ed1i
    @user-be5fc3ed1i Месяц назад

    Awa ndi machine poyankhula the DC mwana wowopsya kwambiri 😂😂😂

  • @user-lg6ym4hz3w
    @user-lg6ym4hz3w Месяц назад +1

    Kkkkkkkkkk ana ofewa odya mipungu nthawi ya mayeso apolice akungosilira

  • @PrinceBlessings-bv5bs
    @PrinceBlessings-bv5bs Месяц назад

    😂😂😂😂😂 lero wayaka moto kalindo❤❤❤❤❤ a opposition please chitanipo kanthu awawa aikanika dziko olo manyazi alibe

  • @JoyceChitsulo-mw7wg
    @JoyceChitsulo-mw7wg Месяц назад +1

    Makosana apa nde mwapita

  • @VincentMalika-w7x
    @VincentMalika-w7x Месяц назад +1

    Ndipo eeeeee tikudziwona kuno tikulemba mayeso apolici ache akupemphaso dzokudza zakudya zath

  • @D.RJALLI-qo6yd
    @D.RJALLI-qo6yd Месяц назад

    Ine ndikudana ndi ma opposition akumalawi ndi agalu kobasi makamaka dpp ikungoyang'anila wosalangula khatu kumbonà lamasuso ngati ili ndiye boma adzalipesa bwanji dpp tadzukani ife tampudzilapo ndipo talapa mamisiteki athu bwelani nditu mutiwombole kwa agalu awa

  • @BlessingsKalonga
    @BlessingsKalonga Месяц назад

    Aliyese ndi wakuba koma kusagwidwa Judgement day tidikire oweruza

  • @ChisomoamitoniSauzandeamiton
    @ChisomoamitoniSauzandeamiton Месяц назад

    bwana ng'alurani ndithu tili nanu nanu

  • @BlessingsKalonga
    @BlessingsKalonga Месяц назад

    Ubwino wake ukuzimenyera wekha khondo uzalemera wekha

  • @EllinaBitto
    @EllinaBitto Месяц назад

    Bulaza wathu❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤

  • @SmartMoles
    @SmartMoles Месяц назад

    Zofunikila kulangura mwayangure kumene

  • @UthmanKapungu
    @UthmanKapungu Месяц назад

    Fire!!!!!!!!!! Bon kalindo nazoni tatopa ife

  • @FrankMilias-og3js
    @FrankMilias-og3js Месяц назад

    Kulankhula mosaopa nyooo sss winiko

  • @FwasanMwenefumbo-zq7sg
    @FwasanMwenefumbo-zq7sg Месяц назад

    The DC 🔥

  • @Shelifibraheem
    @Shelifibraheem Месяц назад

    Big up bro

  • @benjulius6070
    @benjulius6070 Месяц назад +2

    😂😂😂😂😂😂

  • @NdawaPhillipfortunePhakatie
    @NdawaPhillipfortunePhakatie Месяц назад

    Motor 💥 kalindoooo

  • @user-yl3lg5fk8f
    @user-yl3lg5fk8f Месяц назад

    Koma amalawi tinalakwanji kt tizunzike,,,galu uyu wazunza miyoyo ya anthu osalakwa,,chitsiru cha m'busa munthu opanda conscious

  • @ChrispinEdward
    @ChrispinEdward Месяц назад

    Bwanawe pafika boma umuthu walimbe akungo funa kumupanikiza Muthu osawuka kut azikhala ndima strees bas komano azidikile kut Pali mwambi waphala lakaka ukaza fika pomva kukoma limakhakut lathamo mupoto

  • @user-tw5iw7gf2v
    @user-tw5iw7gf2v Месяц назад

    😂😂😂😂 mpaka muchenga license

  • @DaudiAbdullah-o5l
    @DaudiAbdullah-o5l Месяц назад

    Mumatiyimilila

  • @directorkfuture118
    @directorkfuture118 Месяц назад

    Ameneyo asamwe mowa 😂😂😂

  • @gerrardgladstone2473
    @gerrardgladstone2473 Месяц назад

    Akuti kufuna kumangidwaaaaa 🤣🤣🤣

  • @user-kx4cj7iu9q
    @user-kx4cj7iu9q Месяц назад

    Dc

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 Месяц назад

    Mpakana tizigulisana mchenga wamudziko lathu zoona?, kusavukatu uku sopano aati!?, chaza ndiyan choti tizikhala ndi linces yovuwulila mchenga ?, ndepoti amalawi mumkafuna kusintha zinthu , zimene mumkafuna kwa abusa zija mzimenezi😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂❤❤ , mo 🔥🔥🔥🔥🔥🔥 mcp kkkkkk

  • @PeterGrant-ih1sr
    @PeterGrant-ih1sr Месяц назад

    Athuawa atakhala alipo okwana 4 ziko muno athuwa atasitha ndithu😂😂😂😂

  • @TshepoModise-xs4qu
    @TshepoModise-xs4qu Месяц назад

    Koma nkhaza zake mpaka licence ya mnchenga Mmmm zovuta bwanji eeee

  • @EdwardMukholi
    @EdwardMukholi Месяц назад

    Kkkkkkkkkk koma chakwera ndiye ndiye zikuchoka kuti zimenezi

  • @pempheroraynnoxmpesi8713
    @pempheroraynnoxmpesi8713 Месяц назад

    😂😂😂😂msusi olo nthuli amatayapotu a dpp

  • @HelenamoisésLisboaMoisésLisboa
    @HelenamoisésLisboaMoisésLisboa Месяц назад

    Ambuye akudalitsen

  • @user-wm4rs4kd7d
    @user-wm4rs4kd7d Месяц назад

  • @RamseyWasi
    @RamseyWasi Месяц назад

    Blasa,
    Malawi saadzatheka mpaka kale kale. This is my second SMS to you mr Dangerous Child (DC)
    My opinion:
    Kungosiiya utsogoleri wa anthu osawukawu.chfkwa or titatan,kusawukaako sikudzaatha.

  • @CaptainNyenga
    @CaptainNyenga Месяц назад

    😂😂😂😂😂 koma DC

  • @ericlarks8165
    @ericlarks8165 Месяц назад

    ,🔥🔥🔥🔥

  • @MathpeterLemon-ls1ns
    @MathpeterLemon-ls1ns Месяц назад

    Ati kutitola kapena chani

  • @nicholasmutano6017
    @nicholasmutano6017 Месяц назад

    Uyuyu ndi mandrax sichamba, akufuna titani tilowele kuti si misala iyi?

  • @HendersonDziwa
    @HendersonDziwa Месяц назад

    Dzelu zachepa kkkk

  • @maxwellcaptain3937
    @maxwellcaptain3937 Месяц назад

    Kalindo samaopa😂😂

  • @lytonmaseko4534
    @lytonmaseko4534 Месяц назад

    😂😂 kung'alulatu

  • @user-ls5zj8qn6k
    @user-ls5zj8qn6k Месяц назад

    Koma uyu inu kkkk ati apolice osilila mpunga wa nyama 😂😂😂😂 ayi zikomo

  • @AnthoniohMazengera
    @AnthoniohMazengera Месяц назад

    Hahahahahahahahahaha😂😂😂

  • @YonaMartin-kb3do
    @YonaMartin-kb3do Месяц назад

    😂😂😂😂 akavoterana ndi amawo yemweyo kupuma palibe

  • @ikmusic-s9f
    @ikmusic-s9f Месяц назад

    koma nde eeee mpaka licence mchenga

  • @GiftKulture
    @GiftKulture Месяц назад

    🤣🤣🤣🤣 mipunga

  • @sir-wanton-2001
    @sir-wanton-2001 Месяц назад

    Kkkkk Kkkkk uyu akazankhala president azamujaje nda uyu ndi dolo

  • @AaronLitete
    @AaronLitete Месяц назад

    Kkkkk boma lopusa

  • @wangachindeya8577
    @wangachindeya8577 Месяц назад

    Bigiliman naweni

  • @JuliusMunthali-z7j
    @JuliusMunthali-z7j Месяц назад

    Awuzeni

  • @Aluwenkareem-ev3ro
    @Aluwenkareem-ev3ro Месяц назад

    😂🤣😂🤣

  • @BenjaminKayembe-j7j
    @BenjaminKayembe-j7j Месяц назад +1

    km eeee awawa ndsbwsna gayz mmmmmm amakwana km

  • @user-vn1wq6wg6i
    @user-vn1wq6wg6i Месяц назад

    K.K😂

  • @PhillipMtonga-g7o
    @PhillipMtonga-g7o Месяц назад

    🤣🤣🤣🤣🤣🤣 zamanyazi kuntonse alliance

  • @YohaneMbewe-u4k
    @YohaneMbewe-u4k Месяц назад

    😂😂😂😂

  • @user-ky8us1ff5b
    @user-ky8us1ff5b Месяц назад

    😅😅😅😅

  • @Kachelephiri
    @Kachelephiri Месяц назад

    Awa.akulila.ayesetse.2025.azawinekwawo.ump.kwawo.kma.ngatiakukanakwawo.ndiakanene.jilose.tingamuvele.galu.wachabechabe.

    • @ChristopherKawilam
      @ChristopherKawilam Месяц назад

      Uku nyoza bon kalindo,, zeru ulibe iwe uku Kanika kulemba kumene galu iwe

    • @ChristopherKawilam
      @ChristopherKawilam Месяц назад

      Yamba wapita Kaye Ku school ya mkaka uziwe kulemba...... galu iwe

  • @user-wz6jy3re8n
    @user-wz6jy3re8n Месяц назад +1

    😂😂😂😂😂😂

  • @myheartforkids2876
    @myheartforkids2876 Месяц назад

    😂😂😂😂😂