Palibe Chamuyaya Pa Dziko La Pansi - Hon Kamlepo Kalua
HTML-код
- Опубликовано: 10 июл 2024
- On Nyasa VoiceBox, Hon Kamlepo Kalua says nothing is forever. Especially Political Power and Politicians.
Pa Nyasa VoiceBox, Olemekezeka a Kamlepo Kalua akuti pa Dziko La Pansi Palibe Chamuyaya. Makamaka Mphamvu za Ndale Komanso anthu andale.
#malawi
Good Messnge Mr Kamulepo kaluwa, Chakwela you mast go
Amene kamulepo kalua ndimamziwa ndi ameneyo nthawi yamakezanayo ankayimba nyimbo zamatikitikii tiki tiki zamatikitiki so samalani amcp ndi chakwera wanuyo
A great speech sir ...so wise and mature
Mwaputa olakwika....
We are wit you sir, all the way.... God be wit u n the whole family
Ulemu wanu Mr kamulepo ambuye akutetezeni Ku khwandwe za MCP we love you ❤
Wise man 😊
Yex thus fact becareful ma fon amene anaranda apolice akufune ayikemo ma poison at the end aperekeno what kind of this government am be shame😢😢😢
Ndipo ndizoonadi apolice akumalawi ziwani kuti mawa limafika ine ndikupepha kuti ualamulilo wakuphau ukazangochoka apolice ose azawachotse tchito mmm ayi
Viva KK, great message 👍
I salute you Mr K K
Bravo Mr kamlepi kaluwa
Patiently waiting for the day to see cctv footage of the fools mumu police
Listen is better than beautiful sacrifice, palibe chamuyaya
Respect to you Mr kamulepo
Tell them the liyaliya😅😅😅
Ku Malawi si kulilongwe kapena kukasungu hiyaaaa!!!!
Great voice sir
Kamulepo Kaluwa🙏🔥👊🔥
We worn you guys about Chakwera and MCP you didn't listen. Chakwera ndi munthu oipa mtima and he has never been a pastor.
Mawu amphavu Mr Kalua
This Chakwera must go they take people like fools
Hiyaa! Mwanyanya a MCP kwatola amalawi lero mwakumana nazo,muyesa Malawi yu ndi wamanu agalu okupha
Tell dem sir agalu amenewa hiyaaa
Aaaa MCP anadzolowela kupha ndi kudzuza anthu mistake tinapanga poyibwedzelatso boma iiii
Respect
You always chase money... thumba mukauma (dry) you make noise.. it has been ur tricks.. you have been always following the party that is ruling kusaka ndalama... ine simungandipusise nawo Mr Kalua...
😂😂😂😂 kwachema
Kukula kumeneko kkkkkk
🤣🤣🤣🤣🤣
Bwanawa alindi umboni kapena akungolumbwalubwa
Ambuye mutetedzereni penjani kalua mmanja mwa satanic awa chakwera ndi mcp akufuna aononge moyo wace but ladzalo cakwera why moyo wako umakondwa ukamapha anthu popanda kukhetsa mwazi thupi lako kukapwanya tulo silibwera mmaso mwako bwanji osamupha nick chakwera bwanji
Zoona munthu uyu anathana kale ndi kamuzu ku one party system panonso aszuzinke mmmmmm koma chakwera bwenzi utakhala ndi umuthu pena
Mwalasa honourable Kaluwa you should stand for presidency you will get support from Malawians
Please do not abandon the Lord Jesus Christ for the sake of politics. Please be a true Christian. It's surprising that the former man of God has gone satanic.
Awuzeni dppppppppppp
❤awudzeni chilungamo 🔥