Palibe Chamuyaya Pa Dziko La Pansi - Hon Kamlepo Kalua

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 10 июл 2024
  • On Nyasa VoiceBox, Hon Kamlepo Kalua says nothing is forever. Especially Political Power and Politicians.
    Pa Nyasa VoiceBox, Olemekezeka a Kamlepo Kalua akuti pa Dziko La Pansi Palibe Chamuyaya. Makamaka Mphamvu za Ndale Komanso anthu andale.
    #malawi

Комментарии • 37

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y 22 дня назад +6

    Good Messnge Mr Kamulepo kaluwa, Chakwela you mast go

  • @user-be5fc3ed1i
    @user-be5fc3ed1i 22 дня назад +3

    Amene kamulepo kalua ndimamziwa ndi ameneyo nthawi yamakezanayo ankayimba nyimbo zamatikitikii tiki tiki zamatikitiki so samalani amcp ndi chakwera wanuyo

  • @CHARLESMASINA-xx5kt
    @CHARLESMASINA-xx5kt 21 день назад +1

    A great speech sir ...so wise and mature

  • @SteveAngaMuwellah
    @SteveAngaMuwellah 21 день назад +1

    Mwaputa olakwika....

  • @user-qq3ip1od6i
    @user-qq3ip1od6i 22 дня назад

    We are wit you sir, all the way.... God be wit u n the whole family

  • @user-mh7cc8up4i
    @user-mh7cc8up4i 21 день назад

    Ulemu wanu Mr kamulepo ambuye akutetezeni Ku khwandwe za MCP we love you ❤

  • @PrincepreciousMwasangwale
    @PrincepreciousMwasangwale 21 день назад

    Wise man 😊

  • @MadalitsoTamayenda-ez5pj
    @MadalitsoTamayenda-ez5pj 22 дня назад +1

    Yex thus fact becareful ma fon amene anaranda apolice akufune ayikemo ma poison at the end aperekeno what kind of this government am be shame😢😢😢

  • @user-eh1mg3ww6d
    @user-eh1mg3ww6d 21 день назад +1

    Ndipo ndizoonadi apolice akumalawi ziwani kuti mawa limafika ine ndikupepha kuti ualamulilo wakuphau ukazangochoka apolice ose azawachotse tchito mmm ayi

  • @beakab2378
    @beakab2378 22 дня назад

    Viva KK, great message 👍

  • @user-fi7ko7bl6f
    @user-fi7ko7bl6f 22 дня назад

    I salute you Mr K K

  • @frankiechasokoneza5802
    @frankiechasokoneza5802 21 день назад

    Bravo Mr kamlepi kaluwa

  • @AdoptedNaijaBoy
    @AdoptedNaijaBoy 21 день назад

    Patiently waiting for the day to see cctv footage of the fools mumu police

  • @princedetbozsmallboy1749
    @princedetbozsmallboy1749 22 дня назад

    Listen is better than beautiful sacrifice, palibe chamuyaya

  • @Raph-kayRaph-kay-g5v
    @Raph-kayRaph-kay-g5v 22 дня назад

    Respect to you Mr kamulepo

  • @user-fi7ko7bl6f
    @user-fi7ko7bl6f 22 дня назад +1

    Tell them the liyaliya😅😅😅

  • @lovenesskampira
    @lovenesskampira 22 дня назад

    Ku Malawi si kulilongwe kapena kukasungu hiyaaaa!!!!

  • @aubrygrasten1441
    @aubrygrasten1441 21 день назад

    Great voice sir

  • @frankjolijo
    @frankjolijo 22 дня назад

    Kamulepo Kaluwa🙏🔥👊🔥

  • @juliusnjerengo2610
    @juliusnjerengo2610 21 день назад +1

    We worn you guys about Chakwera and MCP you didn't listen. Chakwera ndi munthu oipa mtima and he has never been a pastor.

  • @LumbaniNeba-d9n
    @LumbaniNeba-d9n 22 дня назад

    Mawu amphavu Mr Kalua

  • @user-db3mh9wr9v
    @user-db3mh9wr9v 21 день назад

    This Chakwera must go they take people like fools

  • @user-fi7ko7bl6f
    @user-fi7ko7bl6f 22 дня назад

    Hiyaa! Mwanyanya a MCP kwatola amalawi lero mwakumana nazo,muyesa Malawi yu ndi wamanu agalu okupha

  • @cacksygustarf6260
    @cacksygustarf6260 22 дня назад

    Tell dem sir agalu amenewa hiyaaa

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda8711 21 день назад

    Aaaa MCP anadzolowela kupha ndi kudzuza anthu mistake tinapanga poyibwedzelatso boma iiii

  • @MadalitsoTamayenda-ez5pj
    @MadalitsoTamayenda-ez5pj 22 дня назад

    Respect

  • @Cathy-oc7vd
    @Cathy-oc7vd 21 день назад

    You always chase money... thumba mukauma (dry) you make noise.. it has been ur tricks.. you have been always following the party that is ruling kusaka ndalama... ine simungandipusise nawo Mr Kalua...

  • @StevenGoodson-kn7ug
    @StevenGoodson-kn7ug 22 дня назад

    😂😂😂😂 kwachema

  • @IsabelMvula-xn8po
    @IsabelMvula-xn8po 21 день назад

    Kukula kumeneko kkkkkk

  • @phillipstamaley7901
    @phillipstamaley7901 21 день назад

    🤣🤣🤣🤣🤣

  • @finchiadriano
    @finchiadriano 21 день назад

    Bwanawa alindi umboni kapena akungolumbwalubwa

  • @user-hm9nc7lz6e
    @user-hm9nc7lz6e 21 день назад

    Ambuye mutetedzereni penjani kalua mmanja mwa satanic awa chakwera ndi mcp akufuna aononge moyo wace but ladzalo cakwera why moyo wako umakondwa ukamapha anthu popanda kukhetsa mwazi thupi lako kukapwanya tulo silibwera mmaso mwako bwanji osamupha nick chakwera bwanji

  • @inessmsiyambiri8517
    @inessmsiyambiri8517 21 день назад

    Zoona munthu uyu anathana kale ndi kamuzu ku one party system panonso aszuzinke mmmmmm koma chakwera bwenzi utakhala ndi umuthu pena

  • @iamandypandy
    @iamandypandy 22 дня назад

    Mwalasa honourable Kaluwa you should stand for presidency you will get support from Malawians

  • @crosbyphiri1745
    @crosbyphiri1745 22 дня назад

    Please do not abandon the Lord Jesus Christ for the sake of politics. Please be a true Christian. It's surprising that the former man of God has gone satanic.

  • @user-kk4uj8ko8k
    @user-kk4uj8ko8k 22 дня назад

    Awuzeni dppppppppppp

  • @johnarushamasese108
    @johnarushamasese108 22 дня назад

    ❤awudzeni chilungamo 🔥