EXCLUSIVE WITH: KARANI THOM MUTHARIKA | 19 JANUARY 2025

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 31 янв 2025

Комментарии • 93

  • @ernestmponda156
    @ernestmponda156 12 дней назад +2

    Koma njalayi kuvumbukuka amisala ambiri. 😂😂😂

  • @LytonMathanga
    @LytonMathanga 12 дней назад +1

    I admire SABC.Inu ma K1 anali okukwanirani

  • @BenaSamuel
    @BenaSamuel 11 дней назад

    Kodi mwati iyiii ndi exclusive interview or comedy chifukwa panalibe opangaza serious apa kuphatikiza ofunsayoso sanali serious

  • @edsonkamba3170
    @edsonkamba3170 11 дней назад +1

    Kudali Jumani kunja kuno amene amananso kuti adali mwana wa Kamuzu Zina ndi izi ati ndi mbale wake wa Mutharika. Aliponso wina amati ndi mwana wa Bakili koma amakanidwa.

  • @VKHOSILVERSILVER
    @VKHOSILVERSILVER 12 дней назад

    Cholinga APM akhare Oipa ...Mukhauraa APM my vote

  • @ArthurSuya
    @ArthurSuya 10 дней назад

    Aaah mchopenga ichii chadya zingat

  • @isaacntchentche2276
    @isaacntchentche2276 12 дней назад

    Munthuyutu ndiwaboza chifukwa zomwe akufotokoza sizikugwilizana ndizomwe akufusidwa😊

  • @PatukanVincent
    @PatukanVincent 11 дней назад

    Uyu ndigalu

  • @EdsonKamwendo
    @EdsonKamwendo 12 дней назад +2

    Ndikumuziwa amakonda kuwabera anthu kumawanamiza kuti ndi mbarewake wa Bingu anayamba Bingu asanamwalire inu a MCP mwalandira munthu wopenga

  • @AndersonBishop-i2t
    @AndersonBishop-i2t 12 дней назад

    Kaye kusemphana awa amachendewa ndizimene akuyakhulazo mmmmm inu tangopemphani musanamize amalawi Peter ndi bingu pamene amapita ku Tanzania history is best teacher waboza ameneyo wojiya wa mcp kmbe mukunama inuyo a mcp

  • @KelvinAnthony-f8x
    @KelvinAnthony-f8x 9 дней назад

    Kodi mbudzi imeneyi ikuti chani kapena mwina uyu ndi yes matiki😂

  • @LuckyKhonyongwa-pt7ck
    @LuckyKhonyongwa-pt7ck 11 дней назад

    Ifetu chomwe tikufuna ndi Black Box izizi sizitithandiza

  • @MisheckChinjala
    @MisheckChinjala 12 дней назад +1

    Fundo zimene akunena pamenepo,ndizokambirana kutundu wawo not in paburic

  • @YusufNdege-o2u
    @YusufNdege-o2u 11 дней назад

    Koma ine guys interview iyi ikundiwaza kwambiri ndaimvera ka 5 times mkuluyu aaaaaaaa

  • @MikeMteje
    @MikeMteje 12 дней назад +2

    Nkhope imeneyo siyakwa munthalika

  • @BarnetNsaka
    @BarnetNsaka 11 дней назад

    Chokuba si mchimwene wake wamutharika kuchikamwa😮

  • @edsonkamba3170
    @edsonkamba3170 11 дней назад

    He is a frustrated man. Umphawi ndiye vuto apa. Where was he when Bingu and APM were making their own future.

  • @PaulChaleka-lb4vx
    @PaulChaleka-lb4vx 12 дней назад +2

    Uyu ndi wakut? Uyu alibe nzeru

  • @AlickMalikebu
    @AlickMalikebu 11 дней назад

    Ken zikhale ng'oma akuziwa coz anamupasa 100k pin

    • @LuckyKhonyongwa-pt7ck
      @LuckyKhonyongwa-pt7ck 11 дней назад

      zikhare palibe chomwe angafotokozepo za izi nkhani ndiza ndale kufuna kuipisilana mbiri komanso kufuna kutenga mavoti mophweka koma nzolephereka izi

  • @HamuzahRoben
    @HamuzahRoben 11 дней назад

    Kusuta fodya ndi njala eee😂😂😂

  • @AustinSaidi
    @AustinSaidi 11 дней назад

    Komano zipindulanji izi kwa ife amalawi?

  • @AndersonBishop-i2t
    @AndersonBishop-i2t 12 дней назад

    Iwe tachoka apa zakuti akut zabozazo koditu inu mbczikuvutani iwe alinafe mulamba wojiyawo a mcp Peter ndi bingu ndi chemwali wake amenewo si akwamuthalika pa zaka 20 analikutiko
    Kodi iwe azinyemba alinafe azibale ake andaniyo ndi wojiya ameneyo akhawula ndiposo machende akeso ndi iweso ukufusa mafuso opepelaweso beans yako yofumbwayo

  • @BraveNyembere-h1n
    @BraveNyembere-h1n 12 дней назад

    Ndamvetsetsa sopan ndiuphawi umene wamutuma gogoyu

  • @MahuwadrillingGroup
    @MahuwadrillingGroup 11 дней назад

    Wadyela uyu

  • @PeterKainga-e3h
    @PeterKainga-e3h 10 дней назад

    Chakwera akhale wa nzeru dziko likanamukanika? Bambo ingopemphani muzipita

  • @IbrahimJackson-i8h
    @IbrahimJackson-i8h 12 дней назад

    Apite kwa uncle ake Apeter akafufuze zaubalezo osati pa television

  • @LukeMoyo-l9z
    @LukeMoyo-l9z 12 дней назад

    Okuba ameneyo

  • @AndyKhumbanyiwa
    @AndyKhumbanyiwa 12 дней назад

    Uyu ndi Onama. Angofuna kudyera anthu. Mmene wanna kuti Ambassador anauzidwa kuti azimpatsa galimoto ndi flag - wazigwilitsa. Mpaka akuti amalondera casket ya malemu Bingu - zonama zeni zeni....

  • @AustinSaidi
    @AustinSaidi 11 дней назад

    Tv yombwambwana dziko lonse lapansi

  • @SteveKhomani
    @SteveKhomani 12 дней назад

    Kodi zimemenezi nza ntchito yanji Ku dziko lino??? Fuel apezeka ? Fertilizer akhala 4,500 ? Passport ikhala 14,000 sugar 500 ?
    Zopanda ntchito izi

  • @StevenGopani
    @StevenGopani 12 дней назад

    Malume muyaluka nazo izi, iwe simulomwetu ukundimvekera kachiyawo yawo eeeee😂😂😂😂😂😂

  • @AmosRichieKumbanga-v8j
    @AmosRichieKumbanga-v8j 12 дней назад

    Wapatsidwa ndalama ndi MCP uyu ndipo ndiopoira

  • @YusufNdege-o2u
    @YusufNdege-o2u 11 дней назад

    Kkkk eshi kumalawi mkokoma kwabasi

  • @SamLee-j7p
    @SamLee-j7p 11 дней назад

    Koma kwinaku nditukwana

  • @Jimmy-e6r9x
    @Jimmy-e6r9x 11 дней назад

    MCP ili ndi ndalama zoseweletsa

  • @CathyMkwandala
    @CathyMkwandala 11 дней назад

    Koma anthu mumadziwa kunama 😂😂😂

  • @aubreymachelo8712
    @aubreymachelo8712 11 дней назад

    Sindikukhulupilra ndi mdoba mdoba wa mtawn😅😅😅😅

  • @thulambale2836
    @thulambale2836 12 дней назад

    Pa banja si onse mumaphunzila same class same university or same secondary same primary musamususe inu inu mbuzi chifukwa cha chipani cha DPP Nonse osusa mumasusa ndi manyi omwe. Chipani ndi china chibale ndi china

    • @kingwaltermdezo
      @kingwaltermdezo 12 дней назад

      Baba osapanga phuma, munthuyu naye wamikisa nkhani akuti walowa MCP kuchoka ku DPP.
      Zikanakhala kuti anangobwelera nkhani za chibale bwezi palibe nkhani za zipani

  • @GlucoMbewe
    @GlucoMbewe 12 дней назад

    Wangudwa

  • @IshmaelNesta-rb8dx
    @IshmaelNesta-rb8dx 12 дней назад

    Momwe anzake amaphunzira iyeyu anali busy ndi nyanga ....nkokhwima aka nkani abale ake amakathawa....kakuoneka so koipa mtima...fwetseki

  • @SandfourKatambo
    @SandfourKatambo 11 дней назад

    Kkkkkkkkkk km guyz mot ukaramba koseku km umuthu mulibe km ndalama ndisatanadi

  • @GiftMunyonga-ko9dz
    @GiftMunyonga-ko9dz 9 дней назад

    This just shows how much you fear APM 😂

  • @CharlesTambala
    @CharlesTambala 12 дней назад

    Uyu andilakwisa

  • @MustaphahTambuli
    @MustaphahTambuli 12 дней назад

    January yu njala yavuta abale sangachitire mwina koma kupeza njira yoti upezeke ufa nyumba, komanso umphawi wako USA blame munthu wina ndivuto lako limenelo ndi uchitsiru wako galu iwe

  • @EvanceWame-v7v
    @EvanceWame-v7v 12 дней назад

    Mulibe ma program ena ku MBC ko oti angathandize dziko?

  • @JosephyJonathan
    @JosephyJonathan 11 дней назад

    Mcp zawavuta mpaka kugura athu gogo wabodza uyuuu

  • @BlessingsRoss
    @BlessingsRoss 8 дней назад

    munthawi ya bingu anali kuti aaaa
    kutumidwa Kwinaku muziona ponamizila

  • @ChrissyBhima
    @ChrissyBhima 12 дней назад

    Koma abale umphawi sizinthu,ndipo ngati kuli munthu opya,ndiye ndimphawi,amalola kunena boza cholinga apeze thandizo

  • @Eric-gb9ms
    @Eric-gb9ms 11 дней назад

    Wakuba uyu watumidwa nd a mcp akamuthilile APM poison Koma game yawo yapheduka nanu a mbc yetsetsani ma program anu akhale womveka kwa amalawi chifukwa apa palibe chazelu.

  • @PatukanVincent
    @PatukanVincent 11 дней назад

    Mwabwera rit anganga inu zigawenga za mcp

  • @YassinAlli-u9n
    @YassinAlli-u9n 12 дней назад

    Musatengeke naye ameneyu simunthu wabmwino

  • @Kelvinbanda-c3x
    @Kelvinbanda-c3x 11 дней назад

    Wamisala uyu

  • @kenedychinyamula
    @kenedychinyamula 11 дней назад

    MBC 😂😂😂 izizi kwa ife amalawi zitithandiza chan

  • @JosephyJonathan
    @JosephyJonathan 11 дней назад

    Wabodza uyuuu

  • @JamesSaiti-h1l
    @JamesSaiti-h1l 12 дней назад

    Kodi kufanana mayina ndiye chibale 😂😂😂😂 zavuta ameneyu

  • @PetrosSamuel-rs9wk
    @PetrosSamuel-rs9wk 12 дней назад

    Awa mutu wawo sumagwila za udani wawo ndi muthalika zisatikhuze ife tikupanga zoti peter abwelele muboma athese njala akulu amenewa akuziwa ntengo wa thumba lachimanga pano ? Pasanapanu malume

  • @Spaw-BTheGogoBoy
    @Spaw-BTheGogoBoy 12 дней назад

    Nde mwat Dr Lazarus mc cathy kachero 😂😂😂😂😂

  • @Chitenje74
    @Chitenje74 12 дней назад

    Nkhani ndi ndalama 😅😅

  • @VictorMagona
    @VictorMagona 12 дней назад

    Nthawi yonseyi anali kutiko m'dalayu ndi mbava

  • @StanleyMakungwa-t6f
    @StanleyMakungwa-t6f 12 дней назад

    Nde mpaka kusapota khonglesi????

  • @FrancesPeter-xw3vb
    @FrancesPeter-xw3vb 12 дней назад

    Uyuyu ndiwaboza chifukwa dzina ndimoto chifukwa ngakhale mayina amafana unalikuti nthawi yonseyi ikufuna kumupha munthu uziwe kuti yemwe akukutumayo akupweteketsa kodi ngati ukumudziwa Peter munthalika uphale wake anakavinidwa kuti?

  • @VictorMateyu
    @VictorMateyu 12 дней назад

    AM NOT CONVINCED WITH THIS FOOL

  • @Ertyvhk
    @Ertyvhk 12 дней назад

    Ubale wake wotani komanso kuli abingu iwowa anali kuti ? Komanso ngati palidi chibale awawa ndi anthu oipa awoneswratu kuipa mtima ndipo sianthu owathandiza.

  • @jimmykatunga8100
    @jimmykatunga8100 9 дней назад

    Ndi Wabodza uyu

  • @ShareefKalima
    @ShareefKalima 12 дней назад

    Aaaaa palibe zimenezo Anthu akuziwa bwino lomwe za banja la Muthalika mugulen nfiti uyu Anthu ntchito za DPP akuziwa bwino lomwe

  • @francissumbulero2291
    @francissumbulero2291 12 дней назад

    Machende ako, kwa munthalika kulibeko mbuli galu iwe

  • @Piase-i8q
    @Piase-i8q 12 дней назад

    Wakuba Uyu sichibale

  • @MahuwadrillingGroup
    @MahuwadrillingGroup 11 дней назад

    Njala yavuta iyi

  • @GiftIssac-cw3fm
    @GiftIssac-cw3fm 12 дней назад

    Mene enawo amaphudzira iwe.
    Unali kut

  • @ShareefKalima
    @ShareefKalima 12 дней назад

    Kkkkkk nfundo za M.C.P zakupha Anthu ku chikangawa kkkkkk Mutaye si M'bale wa Bingu uyu kkkkkk uyuyu apanga chan uyu kkkkk vote A.P.M

  • @GlucoMbewe
    @GlucoMbewe 12 дней назад

    Kkkkkk kapolo uyu

  • @Godfreymkwachale
    @Godfreymkwachale 2 дня назад

    Useless interview ever😢

  • @JONAHMWALUGHALI
    @JONAHMWALUGHALI 11 дней назад

    Kkkk eeeh kwabvuta

  • @RAJABSTYLESTYLE-yi1el
    @RAJABSTYLESTYLE-yi1el 12 дней назад

    wabodza uyu watumidwa kongofanana mayina basi

  • @AubreyManganda-g7t
    @AubreyManganda-g7t 12 дней назад

    Wakuba

  • @harrymicah6140
    @harrymicah6140 12 дней назад

    Kape ameneo alibe chikondi

  • @SidreckRashid
    @SidreckRashid 11 дней назад

    Mbc zosabebatu.....

  • @RAJABSTYLESTYLE-yi1el
    @RAJABSTYLESTYLE-yi1el 12 дней назад

    wosangonena kut mukupempetsa

  • @FrancesPeter-xw3vb
    @FrancesPeter-xw3vb 12 дней назад

    Chakwera wamupasa ndalama madala opanda dzeru inu paliinupa mukufuna mukafa muzantchuke ndigulilidwa bokosi labwino mmmmmmm nthawi yatha iyi

  • @JamesChiphazi
    @JamesChiphazi 12 дней назад

    Uphawi sizithu

  • @GiftIssac-cw3fm
    @GiftIssac-cw3fm 12 дней назад

    Kulibe zimenezo

  • @Jafari-s3c
    @Jafari-s3c 12 дней назад

    Wabodza uyu wanamizidwa ndi nyau

  • @peterthawi
    @peterthawi 12 дней назад

    propaganda 😂😂😂😂😂😂😂

  • @andrewmvula-vh2ql
    @andrewmvula-vh2ql 11 дней назад

    Mbc

  • @peterthawi
    @peterthawi 12 дней назад

    sukulu simunalimbikile bwanji ???😂😂😂😂😂😂

  • @IshmaelNesta-rb8dx
    @IshmaelNesta-rb8dx 12 дней назад

    Wabodza uyu

  • @GeorgeZachariah-f3q
    @GeorgeZachariah-f3q 12 дней назад

    Mdala uyu ndiochenjela akufuna kudya nao waona kt zikudyeka zabooka ndpo aiphula kma asaname kt Pali ubale ndi akubaja kwaa Muthalika