And we know kut zodiak, mbc and times media all zili pansi pa mcp does why you scared please try to tell people the Truth not just blaming dpp only what's about mcp
Pagulupa wa mcp ndi wonder enawa amangosatila but no wonder this is kandodos TV but zoona chakwera ndiolephera ndipo whether you like it or not mcp ikupita thank you
Ine mutanena bwanji za zoipa za DPP Koma ine ndikuwona Kuti DPP yinali bwino chifukwa fertilize wunali wosika , makhwara muzipatara analimo chimanga chinali palipose mapassport timawapeza kwina kulikose mosavuta Koma kubwera Kwa MCP moyo wolimba okhaokha angomba ndarama mopanda chisoni ndipo I like DPP
Kodi mumalimbana ndi dpp chifukwa chani,Kodi mwaiwala kuti mcp inapha anthu ambiri mu ulamuliro wao motsogozedwa ndi kamuzu Banda,timadziwatu kuti times ndi yakubanja kwa akamuzu,komaso timadziwa kuti ndinu anthu adyera komaso muli mkhwapa mwa mcp.
Yes Malawi izi sizingapitise chisogolo dzkoli chkufunika Inu maguys pakanemapa musamaope mukuona kwanga Inuyo madolo mukuopa mcp kut munene chilungamo mukubweza mau kwambiri and mcp ikusaka bakili muluzi tv chifukwa chachlungamo chimene iyeuja amalankhula Malawi yonse kuli Bakili muluzi tv and Bon kalindo saopa munthu and Inu zoona Malo mot boma likhale likuona mavto amalawi akulimbana ndkusaka bakili muluzi tv pali dzeru tonse yalepera pazonse bas we need new leadership chakwela ,chilima ,mutharika sakufunika boma and nankhumwa too we don't want them you should tell them please
Achakwera sogolo alibe, peter muthalika sogolo walibe ... Let find someone to lead us these two mubusa ndi professor tiwataye uko atinamiza chani Poti both of them akhala pa mpando wa upresident for 5yrs but nothing did for the nation Wonse Kuba, nepotism very excellent... Palibe wina wowapotsa
Guys mwalunkhula chilungamo, we must never say DPP but Peter muthalika munalipo pamupanfo zinthu zinakukanikani ,,, MCP yilibe vuto, problem ndi Chakwera walephera kukoza dziko. These two people please Malawian don't worst our time to vote for them at least they must handover to another person to represent their parties
Mcp my vote, during the time of DPP party,we have been killed by DPP party mainly the cost of dry maize,their cost was k60 per kg,but now we are going to admarc to sell dry maize at K650 per kg.But those they are not farming,they cry.Don't cry ,go to field and do farming you will not regret.
Peter is musogolele wapha ma albinos ambiri, kuba ndi chisale, nepotism racist Peter galu. DPP yilibe vuto, problem ndi Peter muthalika ndi mudala woipa mutima kwambiri
choti muziwe Chakwera sangazawine ampungu ndi amene azachuluke ngati sazapanga alliance
😂😂Chilungamo chimawa pepani pepani
And we know kut zodiak, mbc and times media all zili pansi pa mcp does why you scared please try to tell people the Truth not just blaming dpp only what's about mcp
Awanso ndi amantha asaname kuti samanyengerera mukuona ngati anzeru ndinu nokha
Olo mutayankhula bwanji, kulangiza bwanji, Chakwera sangasinthe ndi president wamwano ndioipa sinnaoneko eee. Ndinamukhulupilira koma ndinabetsa, bolanso tikanaika Chilima chifukwa amaoneka kuti zopusa safuna bwenzi zomamenyanazi anthu achipani cholamula kulibe 😢 ndezonse ndinthawi 2025 tiona chifukwa olo mulungu sakukondwa ndazo and l believe kuti malemu Sidik Mia bwenzi akusekelera izi
Pagulupa wa mcp ndi wonder enawa amangosatila but no wonder this is kandodos TV but zoona chakwera ndiolephera ndipo whether you like it or not mcp ikupita thank you
Mwadya banzitu iiiii koma ndalama anakonza
Kodi anthu akanena zosakukomelani ndekuti adya banzi? Do you think 20 million tonsefe tingakhale ndi maganizo amodzi?
@@ziyamporoma377 mwadya
Musavutike ndikuyankhula a Malawi akudziwa chabwino ndi choipa ndipo chomwe agwiracho ndi chomwecho DPP woyeeeeee
Koma inu simungathe kusiyanisa pa thawi ya dpp ndi ino tili ino?
Ine mutanena bwanji za zoipa za DPP Koma ine ndikuwona Kuti DPP yinali bwino chifukwa fertilize wunali wosika , makhwara muzipatara analimo chimanga chinali palipose mapassport timawapeza kwina kulikose mosavuta Koma kubwera Kwa MCP moyo wolimba okhaokha angomba ndarama mopanda chisoni ndipo I like DPP
Mufune musafune kaya ndinu a times kaya zodiac koma CHOTI muziwe ndichakuti nkhondo imeneyi Mulung aimenya ndiponso aimaliza yekha.kukanakhala kt peter anakakamila nthawi imene ija bwezi kuli nkhondo yoopsya .koma mulungu anamunong'oneza peter kt zisiye kaye lero anthu azindikila kt chakwela ndi chilima anatinamiza anthu ayambanso kumufuna peter Muthalika .Nkhondo iyi Mulungu aimaliza yekha
Mumaziona ngati anzeru ndinu nokha m'Malawi muno mukamati kut simmanyengerera popeza ndinu amanthanso
🎉
Mmmm awatu kubwera pa tv ndikusonyeza kulimba mtima
Inuyo azibambo atatunu mukudya ka 20 zidyan mudziwe kunjakuno kulimulungu komanso mulindiana muzaziona
Inu mwayamba kudya ndalama zachakwela iti
Anyamata a mcp ntchito mukuigwila
Kodi mumalimbana ndi dpp chifukwa chani,Kodi mwaiwala kuti mcp inapha anthu ambiri mu ulamuliro wao motsogozedwa ndi kamuzu Banda,timadziwatu kuti times ndi yakubanja kwa akamuzu,komaso timadziwa kuti ndinu anthu adyera komaso muli mkhwapa mwa mcp.
Umbuli uli ndiinunso 😂😂. You will hate MCP up to when? Mbuzi ya munthu,,
@@mosespemba8822 you have proven yourself of who you are,the nasty words always represent the real person.
Koma athu tiziganiza Chocho maka athu Ali aut Malawi
Vuto ndarama anapanga chakwela amaziwakuti uku ndikayikako chuma asatira ineyo wose amene akuyankhurapa nawoso anadwakare zake
Everyone knows that DPP has proven their worth, they are not perfect, yes..But they always deliver. You had been in Malawi, you have seen it yourself
Yes Malawi izi sizingapitise chisogolo dzkoli chkufunika Inu maguys pakanemapa musamaope mukuona kwanga Inuyo madolo mukuopa mcp kut munene chilungamo mukubweza mau kwambiri and mcp ikusaka bakili muluzi tv chifukwa chachlungamo chimene iyeuja amalankhula Malawi yonse kuli Bakili muluzi tv and Bon kalindo saopa munthu and Inu zoona Malo mot boma likhale likuona mavto amalawi akulimbana ndkusaka bakili muluzi tv pali dzeru tonse yalepera pazonse bas we need new leadership chakwela ,chilima ,mutharika sakufunika boma and nankhumwa too we don't want them you should tell them please
Dpp my vote olo mutanena bwanji
Mukamatero za dpp zimandinyasa kwambiri sindimafuna kumamva Zina limeneli Peter olo bingu amandinyasanso ndi zimbava zowononga dziko chonde musamatchule zinthu zimenezi
Mvuto la Malawi ndilimenelo saziwa chomwe akufuna ,DPP umakhala chete mukuti iyayi ikuyenera izuke MCP yatayirira chifukwa otsusa akhala chete ikati iyankhule mukuti inalikut isakhale angero lero
Dpp ndi moto
DPP 2025❤ from Cape Town South Africa Stellenbosch University
Dpp 2025 Boma
Achakwera sogolo alibe, peter muthalika sogolo walibe ... Let find someone to lead us these two mubusa ndi professor tiwataye uko atinamiza chani Poti both of them akhala pa mpando wa upresident for 5yrs but nothing did for the nation
Wonse Kuba, nepotism very excellent... Palibe wina wowapotsa
Dpp sizabwelanso tiwaleko amene aja amapha anthu achialubino anthu oipa kwabasi
Bwana ndevu zamwayi Diso laku right likuoneka lotupatu
Title yanu ikusephana ndizomwe akuluakuluwa amakambilana🤣🤣
Olo mudye baziii mulungu akuona mmene akuvutikila anthu ake ku malawi azaweluza
Munya muona bolan Dpp ili nd ma pictures abho ku mtundu wa amalawi
Sindikukaika kuti Nanunso mukudya nawo za chakwera
Aaa awasotu amakondela
Zipumi zanu mbuzi za anthu mukuzitenga ngati ndinu opambana
Guys mwalunkhula chilungamo, we must never say DPP but Peter muthalika munalipo pamupanfo zinthu zinakukanikani ,,, MCP yilibe vuto, problem ndi Chakwera walephera kukoza dziko.
These two people please Malawian don't worst our time to vote for them at least they must handover to another person to represent their parties
Mcp my vote, during the time of DPP party,we have been killed by DPP party mainly the cost of dry maize,their cost was k60 per kg,but now we are going to admarc to sell dry maize at K650 per kg.But those they are not farming,they cry.Don't cry ,go to field and do farming you will not regret.
You are selling that price bcoz of the devaluation your MCP brought but you can't see
Hot current 😂😂🔥🔥🔥❤❤❤
Hot current idatha ndi Brian banda
Mulungu akudalitseni nonse chifukwa chowaunikira amalawi I love guys inudi simutenga mbali mumangonena chilungamo chokha basi
Koma abale look at Wonder & Jona kumasoko ndi mmasayamo kodi anthuwa amenyedwa or I’m I just drunk?
Kodi andebvu zamwayi disolo akubulashani kapena Sakhalin bwanji?
Peter is musogolele wapha ma albinos ambiri, kuba ndi chisale, nepotism racist Peter galu. DPP yilibe vuto, problem ndi Peter muthalika ndi mudala woipa mutima kwambiri
Inu muli ndi umboni Kuti Peter amapha ma komanso Kuba???bwinotu musamatamike ndi kuyankhula nanga anthu akuphedwawa ndi munthalikanso
Andevu zamwayi mumaseka monyodora mumativetsa kukoma kwambiri kkkk
vuto ku mcp kwachuluka mbutuma za anthu anyawu ndi mbuzi zosapita ku xool
Ndipo ngati kuli chipani cha manyi nde ndi DPP anyamata inu
Bravo to you brilliant and breve gentlemen, you stand for us
chakwera ndi mbuzi ya munthu democras samaiwa kuti ndi chani vuto lili pamenepo or kungoti mcp ndi anthu ankhaza ndizitsiru
Izitu sizigwila ukamalemba utakwia umadumpha mau Ena 😂😂😂
Charge mpaka 45,000. Ngati ndi thini la chimanga kapena izicharger. Or magesi kulibe
Ndipo zoseketsa kwambiri
Pankuku wayakhula bwino
47:05
Zikulipana ndi dpp chifukwa mbuzi izi zikudya kwachakwela buli ndichakwela
Wel done ndevu zamwayi
Anthioipamcp
Zooona xzake
Keep up ❤❤❤guys
Achabe
mcp
Mau amphamvu
mmm kupusa bas,,, ngat mulinshunga makwanu