We are waiting incompetent inquiry Poor leadership Not following the democratic values Remember next year is just around the corner Things are not working on the ground Guys we need a servant leader
Ndi andale ochepa amavomereza kuti chiweluzo chiliko ndi chifukwa chake samasamala za anthu Ena ngakhale akubvutika bora iwo zawo zikuyenda koma mulungu ndi oweluza olungama
Don't take malawian as stupid because the president has got powers to make decisions like on this situation to change the decision because you can see when did we did the barial for Chilima and today you're busy enjoying with the post of vice president shamm on you mr. President and your vice president
I hate nyana these guys bcoz even they isolate Jona Pankuku every program they put Jona at last sit why and they use to cat him word on the mouth when ever he is speaking just wash 5 kwagwanji and hot current u will agree with me
Ndipo DPP yinathiphela abale athu 20 ku Mzuzu mu 2011. Yinapha Chasowa, Njaunju, ndi ma membala a UTM ku Lilongwe; kodi amenewo si magazi a anthu? Kodi anthu onsewa ophedwa ndi DPP anali nkhumba? Nde musamalankhule kuti MCP yamagazi ngati muli ndi umboni- DPP umboni ulipo.
Kumakhala bwino ndi anthu muma office mu a Malawi chonde. Big up Banda, Chunga and Msiska
Dziko lalowa chibwana mpaka manganya kukhala vp,,,,ur not serious
Koma mcp mene yachitira treat chilima according to agreement manganya asamale mcp ndi yakupha and dishonest
Komtu azibambo inu musamakonde kumutchula Mulungu munkhani zandale bashop usatchule dzina la Yehova Mulungu lako pachapabe bashop bashop
Mwadziwa bwanj kut akumtchula pachabe??
Munthu amene akumuchemelelayo is good at dramer but ....... Something is wrong
Chisiru manganya yudasi atiphera chilima ndichakwera achina nkunkuyu zikhare ngoma osatchura mulungu zautsiru zimenezo manganya Mesa amafuna udindo kuyiwara kt ose ndichakwera kt awupeze udindowo ndichilima tikulira chilima wanthu lfe 😢
Zibwana zenizeni ndi dziko maliro sanathe koma asankha munthu
😂😂😂 Boy this is the country not family thing..... There is a constitution that runs not people feelings... Show maturity before you utter nonsense
Muzikagona azimayi a eni autsi muli ndi mbili yonyasa kwambili inu
Palibe ndipo ine ndiye ndakodwa kwambili ausi vice 🔥🔥
Koma mummuuze manganya akumbuke .mama sikono........chibwana. ......
Bwato sasisirana pakati panyanja🎉🎉🎉
Mr Ndevu zamwai timati, ❤Mdyanyemba amaiwala koma mtaya makoko saiwala chifukwa amazaloza pomwe anataya osati Mdyamakoko chitukwa makoko a nyemba sitidya ayi
Wakupha uyu chilima adali amfanaoganiza bho .akutha Mau sakudziwa ZA mawa a usi mau awawa adzakutembenukilani soon.ife tli ku ma stand
Koma palakwika pangono chifukwa thawi yachepa kwambili sikale lija aikidwa malilo lija ngati panafunika kudikila kaye
Malamulo amati asankhe kwa 7 day's
Kod awa atatu ndiamene ali oziwa kwambiri amangokhala pamenepa bwanji
Palibe ndipo ine ndiye ndakodwa kwambili ausi vice 🔥🔥
That's a good discussion! Those who have ears have heard something!
Ndipo mukhalisepo atumwi inu.....aaaa ma compassion aanthu mpaka zaka peletu ati sanasayinile.....
Kodi malamulo adziko amachokera kuti ndipo amapangidwa ndi anthu akuti?
Ausi adzakhara president.
Palibe ndipo ine ndiye ndakodwa kwambili ausi vice 🔥🔥
We are waiting incompetent inquiry
Poor leadership
Not following the democratic values
Remember next year is just around the corner
Things are not working on the ground
Guys we need a servant leader
Malawians group of discussion without solutions doy you think you will change Malawi for the situations just wait and see
Tili nchisoni chanji,anagawana zovala zanga yesu anatero
Ine sanandipeze speech yawo nsaname
Wina president akachoka mtengo kumakwela liti zizasitha mpake tife tose zopusa
Manganya ndi ka yudasi kakafupi kwambili fiti kapha, zake chilima
Ndi andale ochepa amavomereza kuti chiweluzo chiliko ndi chifukwa chake samasamala za anthu Ena ngakhale akubvutika bora iwo zawo zikuyenda koma mulungu ndi oweluza olungama
Ma guy inuyo simuli serious ndale zakulowani
They think that this TTV it's belong to them kom kumakhala bwn ndi anzanu zatsogolo lamunth amaziwa ndi Mulungu
❤ Manganya ndiyekhayo maso a malawi
Yaaa aghothiiii akhutukunve malo moti azitengera mphunziro pa zinzawo.
Sugar k200 Lifeboy soap k50 nthochi 20 t, zibwelele kwa d.r banda ngati sizitelo nde kutinamizako ife sitifuna ndale
Tikuferanji amaLawi pomwe Manganya ali m'bwaLo??!!
Suziwa zamawa yes. Fact to the point ❤
Mabwana chonde kuyamikila tiyamikile koma kod chikalidwe chathu monga amalawi chimati chani munthu akafa plz timakukulupililani
Walowa dziko litavunda kale palibe chingasithe apa😢😢
Very educative discussion
Mphaka Manganya kula vice president
Nice kma
Life is in stages
Zomwe lankhula sizingatheke muone azangoti pasakhale owasokoneza nduna zina zidangowelamila pansi muona when it comes to action let's wait
Unawomaso eti!!?
Powerful message
Times mcp tv mbuyomu inali times ya bwino km pano anawadyesa Baz awa
Wishing you the best , help chakwera he is the man of God
😅 killing man
Zosakoma dzikoli😢😢
Koma mcp tikuchotsa 2025 yatililitsa koopsa
Akufuna Aphe Born Kalindo then APM, chenjerani nayoni boma ili zinali kokambilana dzulo
Kwathu kosauka ine olo wagalimoto kulibe
Don't take malawian as stupid because the president has got powers to make decisions like on this situation to change the decision because you can see when did we did the barial for Chilima and today you're busy enjoying with the post of vice president shamm on you mr. President and your vice president
Kharedwe ndichuma
Mulungu mutimenyele nkhondo taluza chilima munthu yemwe anthu adamukhulupilira
I hate nyana these guys bcoz even they isolate Jona Pankuku every program they put Jona at last sit why and they use to cat him word on the mouth when ever he is speaking just wash 5 kwagwanji and hot current u will agree with me
Abambo asikono kumeneko zalowa chibwana ndithu 😊
That's illegal. Kupusa
Mudya nyemba amayiwala, koma mudya makoko sayiwala
Chilima anali munthu osunga nthawi ndipo tidzamusowa
Times it's mcp TV
Umbuli
Inu inu abrayan musazafee
I disappointed MCP
Ausi kaya ndi usi wamutengo utiwo koma mumbari yopha chirima arimomo koma nawo apitabe basi
Mwakwera m c p😢
This stupid radio this days we must stop listening and trust
Kod pali chodyadira pamenepo anthu inu
Inu chupiti
Tizikhala bwino ndi anthu🤣🤣
Vote for USI ❤❤❤
Pachoka nzako palidi Malo...
Agalu atatuwaso atinyasa machende anu
Chilima anali dolo simukunama
Zopusa zeni- zeni,manganya mzomwe amafuna amamuyenda mmapazi chilima,mmmmmm ,dziko lamalawi larowa chibwana ,mpana Usi?mzimu wachilima komwe uliko ukunva chisoni
Kkkkkk
Moyodi ndi pelete
Iya mapazi anu
Dziko latha
MCP yamagazi yanuyo ngakhale itachita zabwino komabe mbiri yake ndiyamagazi basi
Dpp so ndi yamagazi ndiye musathe mawu boma ndi Boma
Ndipo DPP yinathiphela abale athu 20 ku Mzuzu mu 2011. Yinapha Chasowa, Njaunju, ndi ma membala a UTM ku Lilongwe; kodi amenewo si magazi a anthu? Kodi anthu onsewa ophedwa ndi DPP anali nkhumba? Nde musamalankhule kuti MCP yamagazi ngati muli ndi umboni- DPP umboni ulipo.
Kod anthu mulimbalibe ya MCP yomweyo uhuuuu bola zipani zina osat MCP yakupha
Za zii. I would rather support MCP than family parties of killers like DPP or UDF
Nanga popeza yakhala mcp yokha chipani cha phavu nanga muthu wa zaka 92 angaganize zulu zinatha tiyenazoni bola mukavote katatu aliyese koma kamodzi aaa mcp ikudutsa
boma lolamula ndi chigawenga