KWAGWANJI / U KUSANKHIDWA KWA MICHAEL USI

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 3 окт 2024

Комментарии • 90

  • @blessiousphiri3109
    @blessiousphiri3109 3 месяца назад +5

    Kumakhala bwino ndi anthu muma office mu a Malawi chonde. Big up Banda, Chunga and Msiska

  • @KennedyChitunda
    @KennedyChitunda 3 месяца назад +6

    Dziko lalowa chibwana mpaka manganya kukhala vp,,,,ur not serious

  • @PaulChaleka-lb4vx
    @PaulChaleka-lb4vx 3 месяца назад +3

    Koma mcp mene yachitira treat chilima according to agreement manganya asamale mcp ndi yakupha and dishonest

  • @AlfredNazombe-me2ly
    @AlfredNazombe-me2ly 3 месяца назад +4

    Komtu azibambo inu musamakonde kumutchula Mulungu munkhani zandale bashop usatchule dzina la Yehova Mulungu lako pachapabe bashop bashop

    • @blessingsmunthali9202
      @blessingsmunthali9202 3 месяца назад

      Mwadziwa bwanj kut akumtchula pachabe??

    • @AlfredNazombe-me2ly
      @AlfredNazombe-me2ly 3 месяца назад +1

      Munthu amene akumuchemelelayo is good at dramer but ....... Something is wrong

  • @Geraldmkwewu
    @Geraldmkwewu 3 месяца назад +3

    Chisiru manganya yudasi atiphera chilima ndichakwera achina nkunkuyu zikhare ngoma osatchura mulungu zautsiru zimenezo manganya Mesa amafuna udindo kuyiwara kt ose ndichakwera kt awupeze udindowo ndichilima tikulira chilima wanthu lfe 😢

  • @clintonhodda9830
    @clintonhodda9830 3 месяца назад +3

    Zibwana zenizeni ndi dziko maliro sanathe koma asankha munthu

    • @wisdom20mkango49
      @wisdom20mkango49 3 месяца назад

      😂😂😂 Boy this is the country not family thing..... There is a constitution that runs not people feelings... Show maturity before you utter nonsense

  • @AminaPhiri-pp9tw
    @AminaPhiri-pp9tw 3 месяца назад +3

    Muzikagona azimayi a eni autsi muli ndi mbili yonyasa kwambili inu

  • @IssacMateyo
    @IssacMateyo 3 месяца назад +1

    Palibe ndipo ine ndiye ndakodwa kwambili ausi vice 🔥🔥

  • @SahijidNgwindima-qd3dk
    @SahijidNgwindima-qd3dk 3 месяца назад +3

    Koma mummuuze manganya akumbuke .mama sikono........chibwana. ......

  • @AAbiner
    @AAbiner 3 месяца назад

    Bwato sasisirana pakati panyanja🎉🎉🎉

  • @emmammatsa1284
    @emmammatsa1284 3 месяца назад

    Mr Ndevu zamwai timati, ❤Mdyanyemba amaiwala koma mtaya makoko saiwala chifukwa amazaloza pomwe anataya osati Mdyamakoko chitukwa makoko a nyemba sitidya ayi

  • @JosephNgona-f9v
    @JosephNgona-f9v 3 месяца назад +1

    Wakupha uyu chilima adali amfanaoganiza bho .akutha Mau sakudziwa ZA mawa a usi mau awawa adzakutembenukilani soon.ife tli ku ma stand

  • @IssacMateyo
    @IssacMateyo 3 месяца назад +2

    Koma palakwika pangono chifukwa thawi yachepa kwambili sikale lija aikidwa malilo lija ngati panafunika kudikila kaye

  • @AlfredNazombe-me2ly
    @AlfredNazombe-me2ly 3 месяца назад +3

    Kod awa atatu ndiamene ali oziwa kwambiri amangokhala pamenepa bwanji

  • @IssacMateyo
    @IssacMateyo 3 месяца назад

    Palibe ndipo ine ndiye ndakodwa kwambili ausi vice 🔥🔥

  • @josephhchimpepa8753
    @josephhchimpepa8753 3 месяца назад

    That's a good discussion! Those who have ears have heard something!

  • @FlynessWinga
    @FlynessWinga 3 месяца назад +1

    Ndipo mukhalisepo atumwi inu.....aaaa ma compassion aanthu mpaka zaka peletu ati sanasayinile.....

  • @clintonhodda9830
    @clintonhodda9830 3 месяца назад +1

    Kodi malamulo adziko amachokera kuti ndipo amapangidwa ndi anthu akuti?

  • @PatrickKandulu-i6g
    @PatrickKandulu-i6g 3 месяца назад

    Ausi adzakhara president.

  • @IssacMateyo
    @IssacMateyo 3 месяца назад

    Palibe ndipo ine ndiye ndakodwa kwambili ausi vice 🔥🔥

  • @JohnSoweso
    @JohnSoweso 3 месяца назад +1

    We are waiting incompetent inquiry
    Poor leadership
    Not following the democratic values
    Remember next year is just around the corner
    Things are not working on the ground
    Guys we need a servant leader

  • @ClementJacob-sd8lf
    @ClementJacob-sd8lf 3 месяца назад

    Malawians group of discussion without solutions doy you think you will change Malawi for the situations just wait and see

  • @DesireMphatsogama
    @DesireMphatsogama 3 месяца назад +1

    Tili nchisoni chanji,anagawana zovala zanga yesu anatero

  • @corretabanda7685
    @corretabanda7685 3 месяца назад +1

    Ine sanandipeze speech yawo nsaname

  • @ClementJacob-sd8lf
    @ClementJacob-sd8lf 3 месяца назад

    Wina president akachoka mtengo kumakwela liti zizasitha mpake tife tose zopusa

  • @HestingsZiba-d6k
    @HestingsZiba-d6k 3 месяца назад +1

    Manganya ndi ka yudasi kakafupi kwambili fiti kapha, zake chilima

  • @Dauson-j5i
    @Dauson-j5i 3 месяца назад +1

    Ndi andale ochepa amavomereza kuti chiweluzo chiliko ndi chifukwa chake samasamala za anthu Ena ngakhale akubvutika bora iwo zawo zikuyenda koma mulungu ndi oweluza olungama

  • @EsnartMartin
    @EsnartMartin 3 месяца назад +1

    Ma guy inuyo simuli serious ndale zakulowani

  • @AlfredNazombe-me2ly
    @AlfredNazombe-me2ly 3 месяца назад +2

    They think that this TTV it's belong to them kom kumakhala bwn ndi anzanu zatsogolo lamunth amaziwa ndi Mulungu

  • @yusufbakali
    @yusufbakali 3 месяца назад

    ❤ Manganya ndiyekhayo maso a malawi

  • @chitanibenito1109
    @chitanibenito1109 3 месяца назад

    Yaaa aghothiiii akhutukunve malo moti azitengera mphunziro pa zinzawo.

  • @ClementJacob-sd8lf
    @ClementJacob-sd8lf 3 месяца назад

    Sugar k200 Lifeboy soap k50 nthochi 20 t, zibwelele kwa d.r banda ngati sizitelo nde kutinamizako ife sitifuna ndale

  • @CalvinThabang
    @CalvinThabang 3 месяца назад

    Tikuferanji amaLawi pomwe Manganya ali m'bwaLo??!!

  • @blessiousphiri3109
    @blessiousphiri3109 3 месяца назад

    Suziwa zamawa yes. Fact to the point ❤

  • @Blessingsseleman-d4x
    @Blessingsseleman-d4x 3 месяца назад

    Mabwana chonde kuyamikila tiyamikile koma kod chikalidwe chathu monga amalawi chimati chani munthu akafa plz timakukulupililani

  • @ykzt
    @ykzt 3 месяца назад

    Walowa dziko litavunda kale palibe chingasithe apa😢😢

  • @blessingkamanga1781
    @blessingkamanga1781 3 месяца назад

    Very educative discussion

  • @80kiloputodaboacena9
    @80kiloputodaboacena9 3 месяца назад

    Mphaka Manganya kula vice president

  • @ChrissySasenga
    @ChrissySasenga 3 месяца назад

    Nice kma

  • @rabeccamasebo6261
    @rabeccamasebo6261 3 месяца назад

    Life is in stages

  • @AlfredNazombe-me2ly
    @AlfredNazombe-me2ly 3 месяца назад +1

    Zomwe lankhula sizingatheke muone azangoti pasakhale owasokoneza nduna zina zidangowelamila pansi muona when it comes to action let's wait

  • @MustafaAbdullah-pb5zv
    @MustafaAbdullah-pb5zv 3 месяца назад

    Powerful message

  • @LovemoreTaulo-yj3pj
    @LovemoreTaulo-yj3pj 3 месяца назад

    Times mcp tv mbuyomu inali times ya bwino km pano anawadyesa Baz awa

  • @PaulMvuma
    @PaulMvuma 3 месяца назад +1

    Wishing you the best , help chakwera he is the man of God

  • @AllanSanena
    @AllanSanena 3 месяца назад

    Zosakoma dzikoli😢😢

  • @PaulChaleka-lb4vx
    @PaulChaleka-lb4vx 3 месяца назад

    Koma mcp tikuchotsa 2025 yatililitsa koopsa

  • @Homeofpeace321
    @Homeofpeace321 3 месяца назад

    Akufuna Aphe Born Kalindo then APM, chenjerani nayoni boma ili zinali kokambilana dzulo

  • @MaggieCement
    @MaggieCement 3 месяца назад

    Kwathu kosauka ine olo wagalimoto kulibe

  • @MAYGOSPELALBUMSChawawa
    @MAYGOSPELALBUMSChawawa 3 месяца назад

    Don't take malawian as stupid because the president has got powers to make decisions like on this situation to change the decision because you can see when did we did the barial for Chilima and today you're busy enjoying with the post of vice president shamm on you mr. President and your vice president

  • @FortuneNkhoma-bc9hh
    @FortuneNkhoma-bc9hh 3 месяца назад

    Kharedwe ndichuma

  • @PaulChaleka-lb4vx
    @PaulChaleka-lb4vx 3 месяца назад

    Mulungu mutimenyele nkhondo taluza chilima munthu yemwe anthu adamukhulupilira

  • @AlfredNazombe-me2ly
    @AlfredNazombe-me2ly 3 месяца назад

    I hate nyana these guys bcoz even they isolate Jona Pankuku every program they put Jona at last sit why and they use to cat him word on the mouth when ever he is speaking just wash 5 kwagwanji and hot current u will agree with me

  • @dymonleven7571
    @dymonleven7571 3 месяца назад +1

    Abambo asikono kumeneko zalowa chibwana ndithu 😊

  • @adibwekumz3085
    @adibwekumz3085 3 месяца назад

    That's illegal. Kupusa

  • @blessiousphiri3109
    @blessiousphiri3109 3 месяца назад

    Mudya nyemba amayiwala, koma mudya makoko sayiwala

  • @PaulChaleka-lb4vx
    @PaulChaleka-lb4vx 3 месяца назад

    Chilima anali munthu osunga nthawi ndipo tidzamusowa

  • @AlexAlick-bx9by
    @AlexAlick-bx9by 3 месяца назад +2

    Times it's mcp TV

  • @maulanaallie6194
    @maulanaallie6194 3 месяца назад

    Umbuli

  • @wonganichakakanyirenda3299
    @wonganichakakanyirenda3299 3 месяца назад

    Inu inu abrayan musazafee

  • @PatrickMailos
    @PatrickMailos 3 месяца назад

    I disappointed MCP

  • @SamukLungu-zg7fl
    @SamukLungu-zg7fl 3 месяца назад

    Ausi kaya ndi usi wamutengo utiwo koma mumbari yopha chirima arimomo koma nawo apitabe basi

  • @wypatrickdakankhoma9655
    @wypatrickdakankhoma9655 3 месяца назад +3

    Mwakwera m c p😢

  • @IssaJohn-cb8vn
    @IssaJohn-cb8vn 3 месяца назад

    This stupid radio this days we must stop listening and trust

  • @ykzt
    @ykzt 3 месяца назад

    Kod pali chodyadira pamenepo anthu inu

  • @ZungeniBanet
    @ZungeniBanet 3 месяца назад +1

    Inu chupiti

  • @RobertNyaude
    @RobertNyaude 3 месяца назад

    Tizikhala bwino ndi anthu🤣🤣

  • @DavidPhiri-o6w
    @DavidPhiri-o6w 3 месяца назад

    Vote for USI ❤❤❤

  • @Yungjoe786
    @Yungjoe786 3 месяца назад

    Pachoka nzako palidi Malo...

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg 3 месяца назад

    Agalu atatuwaso atinyasa machende anu

  • @ChrissySasenga
    @ChrissySasenga 3 месяца назад

    Chilima anali dolo simukunama

  • @AubreyWiskes
    @AubreyWiskes 3 месяца назад +1

    Zopusa zeni- zeni,manganya mzomwe amafuna amamuyenda mmapazi chilima,mmmmmm ,dziko lamalawi larowa chibwana ,mpana Usi?mzimu wachilima komwe uliko ukunva chisoni

  • @polesanamakwenda6932
    @polesanamakwenda6932 3 месяца назад

    Kkkkkk

  • @RABSONSIKELO
    @RABSONSIKELO 3 месяца назад

    Moyodi ndi pelete

  • @RoseMkandawire-e2g
    @RoseMkandawire-e2g 3 месяца назад

    Iya mapazi anu

  • @0wenNkhambule
    @0wenNkhambule 3 месяца назад

    Dziko latha

  • @FrankKambwani
    @FrankKambwani 3 месяца назад +1

    MCP yamagazi yanuyo ngakhale itachita zabwino komabe mbiri yake ndiyamagazi basi

    • @SaidiMbawa-st6bj
      @SaidiMbawa-st6bj 3 месяца назад +1

      Dpp so ndi yamagazi ndiye musathe mawu boma ndi Boma

    • @tasmania527
      @tasmania527 3 месяца назад +2

      Ndipo DPP yinathiphela abale athu 20 ku Mzuzu mu 2011. Yinapha Chasowa, Njaunju, ndi ma membala a UTM ku Lilongwe; kodi amenewo si magazi a anthu? Kodi anthu onsewa ophedwa ndi DPP anali nkhumba? Nde musamalankhule kuti MCP yamagazi ngati muli ndi umboni- DPP umboni ulipo.

    • @MaryNyirenda-nq3mh
      @MaryNyirenda-nq3mh 3 месяца назад

      Kod anthu mulimbalibe ya MCP yomweyo uhuuuu bola zipani zina osat MCP yakupha

    • @tasmania527
      @tasmania527 3 месяца назад

      Za zii. I would rather support MCP than family parties of killers like DPP or UDF

    • @kingsleyhopematchaya5184
      @kingsleyhopematchaya5184 3 месяца назад

      Nanga popeza yakhala mcp yokha chipani cha phavu nanga muthu wa zaka 92 angaganize zulu zinatha tiyenazoni bola mukavote katatu aliyese koma kamodzi aaa mcp ikudutsa

  • @JafaliAkimu-ll1bf
    @JafaliAkimu-ll1bf 3 месяца назад +1

    boma lolamula ndi chigawenga