A UDF M'Dani Wathu Number One Ndi Chipani Cha DPP - Mr Adbull
HTML-код
- Опубликовано: 12 сен 2024
- As the DPP prepares for its elective convention, it has sent out invitations to other political parties, including the UDF. Mr. Abdull, a supporter of the UDF, believes the UDF should decline the invitation because the DPP has never had the UDF's interests at heart.
Pamene chipani cha DPP chikukonzekera msonkhano wawo wachisankho, chatumiza zoitanira zipani zina za ndale, kuphatikizapo chipani cha UDF. Bambo Abdull, omwe amatsatira chipani cha UDF, akukhulupirira kuti chipani cha UDF chiyenera kukana kuitanidwako chifukwa DPP sichinakhalepo ndi zofuna za chipani cha UDF.
#malawi
Momwe zafikira dzikoli stikuyenera kuyang'ana zambuyo ai.ngati mbuyomu panali zolakwika ndibwino kuziunikirana than kufukulana,fukwa zimenezo sizithandiza
Good point my brother awawa achipongwe kwabasi bakili kumupanga theki ndiposo kumumanga muluzi zaziii mupakana mulando watha panopa kamba ka chakwera
Inuyotu mwachidziwikire ndinu wa mcp mwangobisalira ku udf
Koma Awa mwalandira ndarama chani pitani wuko
UDF DPP Palibe udani sakale simeso❤❤❤❤❤❤❤❤
Munthuyu akunena zoona kwamunthu ozindikira chifukwa ambiri akunena zonyoza mkuluyu ndi a DPP. Panopa UDF poti inatha ilibe zimene ingachite ilibe mphamvu paja azungu anati `IF YOU CANNOT FIGHT THEM JUST JOIN THEM` UDF ikuyendera zimenezo.
M'dani wanu kunyumba kwanu nde mudziti M'dani wanu not wathu 😢😢😢
DPP it's best aise❤❤❤ and iwina 2025
Kkkkkk iiii baba pepani ndinthu tatiyeni tigokoza pemwe tikufookapo ku UDF ko ndiposo musapiteko sanayitane inu tatiyeni tizigodya nawo ndalama tikulandirazi palibe zeru apa
Wamisala iwe sumatha Chichewa
Mmmmmmm koma kodi kumangochi kuli anthu azelu chotchi et chilungamo chimawawa
Chipani cha mcp ndichipani cha anthu oyipa kuteleko akufuna zioani zidane komatu izi sizitheka
....amalawi chilungamo achiziwa
Iwe Abdull,mbolo yako,mawere akawilirana amayanjananso .Quaran & Bible zonsezo zimatiphunzitsa kukhululukirana.
Ngati ubale awubwezeletsa a MCP ndi mozambique 🇲🇿 pali chani DPP and UDF
Awa lero ayankhula zaziii sakundiwaza
😅😅😅😅 Amagonanso kukamwa kuli yasa kodi sadzamiza ntchetche may chakwela 😂😂😂😂
Chipani cha UDF chithe kumene, sitikuchifuna. Ine ndine m'chawa koma UDF sindikuyifuna chifukwa Bakili Muluzi ndiamene adapha chipanichi chifukwa cha nsanje. Ndipo uyuyu akunena zowonadi koma chifukwa choti a Chawa ndi mbuzi, zonsezi sakuwona. Dzitsiru a Chawa.
Zowona fada alomwe ndi a manyi.....
Zoona zake ndizimenezo sunaname ase
Kuteleko watumidwa wapasidwa ndalama
Koma kukuvala kokhako mwalakwisa ngati inuyo mumavaka zothina siouti winaso azatenga zovala zanu ayi ndiye kumeneko ndikulakwa smile yimene inuyo mulinayo ziyonse alinayo tangonenani zazipnizo koma ukuku mwalowa kwina chilungamo.chiwoneke ngati mazi
Komadi ndizoona udf udatha chifukwa cha bingu kuyambila nthawi imenyo udf kulibe mpaka lero chulungamo koma Abdul maganizo abwino kwatu kwachuluka anthu obwela ozigulila malo kd kumulanje kulibe malo ife akumangochi timapita kumulanje ai bwanji zimalo abwino choke kumangochi abwelere kwawo kumulanje basi chewa abwele kulelongwe akumatitela ntchito kumangochi apolisi onse achigawo chapakati azipita kwawo akumatitela ntchito kumangochi mupite ku immigration kumangochi achewa okawoka ai abwelele kwawo ntchitoyo ndiyatu atisiyile ife anuwake kusukulu tidapitako ife
Kkkkkk kkkkk ooh koma azibambo anatopa 😂😂😂😂😂😂😂
UDF inatha chifukwa cha dpp
Pita uno iwe
Tayaambapotu kutukwanana tokhatokha Mmmm apa ndiye MCP kuyipatsa mpata kuti idzadutse mosavuta central region ikakunganaa tidzalimba? Tayiganizirani mmene imavotera lilongwe, dowa, dedza, kasungu and etc tilimba? Ulendo uno lilongwe Ndithuditu ifika 1 million plus idzabweza mavoti onse amaboma 11 akumwera enawo kudzangokwaniritsa 50%+1 voter DPP out
Kodi uli ndi udindi wanji kuchipani sukudziwaso kulankhula
Abudul za mbuyozo zisiyeni chomwe tikufuna ife ndi umodzi pano pa Malawi ndi mtendele UDF ipiteko bs
Good voice for ever
😂😂😂pa UDF ndi DPP apo ndye wanama ndipo wanamilatu DPP ndi UDF ndi amodzi ndipo amagwirizanaso kwambiri, iweyo wekha ndyemwe uli ndi mvuto ndi zipani ziwirizi
Koma awa nzeru 2014 kunalibe zili panozi
Usadane ndi dpp udf inatha mkale mkale nena za zeru apa what we need is coalition to boot out mcp osamasungila mangawa u can't achieve anything mvuto umbuli siwabwino
Chakwelawamupha chilima zasala zosatila Zach
Komatu uyu sakuziwa chomwe akufuna akatero MCP yamudyesa sikono udani ulinawo ndiwe osati onse a UDF ayi
Otumidwa awa
Zaziii zangokuvutan
Athu sangakuvele iwe mwana wa hule
😂😂😂😂 koma ndiye wabandulatu MONICA!
Kuvala nde chaninso abakha inu
Mukatelo mwaninkhidwa yolankhulila
Mayi ameneyi kaya anakatengedwa kuti kayi .....amakhala ngati mbuli .....kuyang,ana masowo nkhwezule weniweni
Abdullah mukulakhula zoonadi komano ziko mmene lafikiramu tisayang'aneso m'mbuyo khanindikuchosa manyaka amcp awa basi
Amwene, ndizowonadi DPP ndimene idachotsa ife a UDF m'boma koma lero ife a Chawa, mijomba, tayiwala zimenezo. Achawa ndife atsankho kupambana aTumbuka. Chomwe a Chawa tikufuna nkuti tiwone kuti Atupele Muluzi ali pa mpando wa u president, koma tayiwala kuti president amachita kuvoteledwa ndi Wanthu. Ngati tilibe ma vote okwanila sitingalowe m'boma.
So what's going on? what are you trying to say?
Abdullah zinazo takumvani koma zonena zakuphazo mukunama palibo boma limene silinawonongo miyoyo ya anthu mu malawi kodi kuti tikufunseni matafale anafela muwulamuliro wanji achina billy kaunda kuwawasaka mupakana kuthawa mumalawi ndiye mukunena zimenezo musanamizepo anthu apa muzinena chabe za wubwino wachipani chanu osati zakuphazi panopa mcp tikukhala mwaufulu sitinamve kuti munthu wagwida ndiziwaro uko kuti muwone amene kale anali kupanga nkhaza mu mcp ndi amenewoso anapanga zipani zawo kuwukira mcp ndiye nenani zina osati zimene mukunenazo tikususani
Open Openga iwe
Nkhaza anthu inu eeeeee km amalawi 😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂
Galu
Ndie udf ingawine payokha? Kunganiza kwabwanji uku
Zakale zapita kaloweni ku mcp
😂😂😂😂 sukunama aise monica iiishii
Bwinotu
Munthuyu akunena chilungamo ,mavuto onsewa ndi dpp kugawanisa mutundu no one zambiri zawonongeka mene dpp inafikila Malawi munomm
Adati onongela chipani chathu cha UDF opusa ameneyi
DPP is nasrt, you are very right