More Fire 🔥 🤧......Bon Kalindo....Auze amenewo amvetsese...Chakwera wationongera Mother Malawi... People are suffering tindikwera kwa zithu zofunika kwambiri.
Winawe olo manyazi ulibe, ukulimbana ndi Bon Kalindo apa , CHOTI udziwe Bon Kalindo ndi president waife osauka ndipo izi akuuza ife, iweyo abale ako nda a Chikangawa Party takudziwa shame on you! Our president please more 🔥🔥🔥 Tell them the truth, winawe uziluma pa mchombo, wekha- wekha- kunyoza Bon Kalindo yaaa , Useless boy
Ayiwala kuti ndalama zo agule fertilizer NDI mbewu za subsidy kuti mwina anthu alandile mwachangu komanso anthu ambiri Koma azapeleka mbewuzo February chaka chamawa
Awa a MCP ndimakape kwabasi ndipo ndi mbuzi za anthu, ife tili pa mbuyo panu a DC
Mwayankhula zoona akulu, The DC.
Big up Mr president we love u ❤
Ng'alurization😄😄😄
The DC 🔥
My president just imagine fertilizer cost 89,000 kwacha is this a way of life or a way of death
Kufa basi za moyo palibepo apa
Mmmm ndiponso
Koma DC adaaaaa😂😂✊
Koma iwe Bon kalindo usazafe uzangosowa wava ndipo iwe unforeseeable kuima uprezidenti uzawona Malawi 🇲🇼 kukuvotela umaganiza osati zisiru iziiiii
That's our beloved president ❤❤❤
Our angel from above
Chilungamo ichi cha nyooo, angogawa ndalama mopanda dongotsolo moti apange zoti zinthu zitsike mmmmm mukamva ndafa wandipha😂😂😂😂
Bon Kalindo ❤❤❤❤❤❤❤ I love you so much
Our president BON KALINDO ❤❤❤
More Fire 🔥 🤧......Bon Kalindo....Auze amenewo amvetsese...Chakwera wationongera Mother Malawi...
People are suffering tindikwera kwa zithu zofunika kwambiri.
Athilen mau anthu osaopa Mulungu amenewo
Just meet the DC outside my home. What an honor to meet him...🤝
BOOOOOON KALINDO🔥🔥🔥🔥🔥💯💯💯
Ayi dzikoli ndilaiweyo kalindo, osamakhala ndi nsanje
Uniform mpaka muisoka zikizaki 😂😂😂😂😂😂
😂😂😂😂😂😂
Ndiye mwati chani "ng'alulazation"😂
West of west president in the world 🌎
Lets go.....umati tsegula mutu
😂😂😂 Ng'alulazation yomweyo kuti wawawaaaaa
Mbu🥵li iwe tang,aluluko chizungu
Alot is not going well amalawi tiziombela mmanja sitima 😂 ifeyo kodi aliyense amateurs galimoto aaah njala ndalama izipezeka
Hello our president bbboooonnnn kalindoooooo
Ng'alulasation🎉🎉🎉🎉🎉🎉
Tilimu zimu wa chikangawa pano 🙌🙌🙌🤣🤣🤣🤣🤣
Mr DC mumakwana
Ng'alulaaaa!!!!!!! THE DC CCCCCV!!!!
A Malawi tili pa mavuto oopsa kwambiri MULUNGU atithandize kwambiri
Shallomo Malawi shallomo 😂😂
❤❤❤❤❤❤I love you Mr. DC
Koma DC ndimakhala ndi chidwi ndi apolicewa iiiiiii unifom eti mpaka kuisokasoka eti
Nthawi yaathera bas
The DC ❤❤❤❤❤❤❤❤
Ukumba manda Achakwera adzakaitena Ukumba zisime kuti chizakhale chakuya tidzachite kunponya ngati galu😂😂😂😂😂
Tiyeni tipange ngati zaku kenya
Malawi idyan ndalama Za makape omuvotela tamuziwa kale ife
Big up Mr president!!
DC ukulasa mfundo zoveka bwino, ukulasa mfundo
The DC'S mwana woooopsa kwambiri akhalise Malawi chilungamo chiyende ngat madzi
Zikizaki indeed koma ndalama nde zikusakazidwa eish
Mzimu wa chilima
Boma iri likulangadi eeesh mbola ndithu mmm
Mwanza mwanza adaaa😂
The dc tiyeni paseu basi bomali latitola kwambili sizoona akuchitazi dzikoli silabuyao mmmm
Kkkkk welcome the DC Inu nd one tili pa mbuyo panu bwana
Akuti samalani oipa watsikira komweko
Osabayo ndi ndani? Olo iweyo sungathandize amalawi
Mzimu WA CHILIMA
Musamayiwale kuyikapo mau akuti achimwene aku nthochiiiiiii,the DC !!!! mukatsanzika
Kulankhula zoona zokhazokha....chilungamo chimawawa
Kumun'galula kumene Mr chikangawa more fire the dc
Bon kalindo amanena chilugamo
Mademowo akhàre omuchosa mpopano bas
Born kalindo ndi wa one auze chilungamo avetse boma lonyasa iri
Koma iwe DC ma demo aliko liti Kodi 10 days ija sinathe?
Mnyamata uja waiphula kwabas
DC inuyo mumatiimilila ife amalawi?
And Malawi ambiri anali ndizoyankhula kma timaopa kukadyela mgaiwa pawindo big inuyo mumatiimilira ulemu wanu
Our president ❤❤❤
Mmakwana mbwiye
Utm moto
Ulemu wanu bwana
😂😂😂😂chimwana choopsa kwambiri
The DC!
The DC 🔥🔥🔥
Zimu wagadama
Mbambande bon kalindo ndipo ife tili nanu nanupaka zinthu zizasunthe 💥💥💥💥💪
Mbambande bon kalindo auze
Koma the DC 😅😅😅😅😅😅
Kodi, DC wamanidwa dollar to, ndiye mwayamba kuululakkkkkmm
Ndiwe opusa iwe eti ukuona ngati The DC ndioshota ngati iwe pita uzikakanda uko mbuzi
Chakwera zomwe akuchita Atha kukuchimwisa ndithu kod ulamuliro wanji umeneu
Ndipo zomvetsa chisoni kwambili komatu kuli Mulungu ichi ndiye asamaiwale ay
Mmakwana apule
DC chilungamo ngati madzi amu lake Malawi.
Azanyamula makala Kwa kalulu ku Dedza
Ndipo live umakwana DC
Mzimu wa Chilima
Inu mulibe zelu Ife tupindula nazo
Winawe olo manyazi ulibe, ukulimbana ndi Bon Kalindo apa , CHOTI udziwe Bon Kalindo ndi president waife osauka ndipo izi akuuza ife, iweyo abale ako nda a Chikangawa Party takudziwa shame on you! Our president please more 🔥🔥🔥 Tell them the truth, winawe uziluma pa mchombo, wekha- wekha- kunyoza Bon Kalindo yaaa , Useless boy
🔥🔥🔥🔥
Kubwera kumeneko tawauza bwino
Ayiwala kuti ndalama zo agule fertilizer NDI mbewu za subsidy kuti mwina anthu alandile mwachangu komanso anthu ambiri
Koma azapeleka mbewuzo February chaka chamawa
Dyson @tasona mbolo yako sukukuoa kuti ku Malawi pano kwafika nyasi
Pantumbo pako
Ngati ukamadya za kape wakoyo chikangawa udzingodya
Mumakwana madara chakwera chikangawa watikwana kd ndalamazo muzipatara mulibe makhwala katundu wadura nde atagure zake ndani bznesiyo chakwera akanafa km amanganya nanuso mungoyenga ngt wamisara muzayaruka nxt year
😂😂😂😂😂😂
Big man,asyene kunga'alula
Ndipo mutipase number yanu bwana tizikuuzani zambiri zomwe nguluwezi zikuchita
❤keep it up
The DC ❤❤❤
Ndipo kukasiyako akuchita kulandila ma 1 milion koma chikhalikenicho kwinaku analemba kut anthu azilandila 150 paka pano ndalama anthu sanalandilebe koma kwao anthu akuva kukoma munthu woipa uyu akungoona kwao konkha
Munthu oipa uyu ing'alure basi the DC ulemu wako
Ng'alulization 😂
Zoona ndi Mizimu ,,a Joyce Banda Nyumba anamanga
😂😂 mzimu wa mgadama
Ng’aluration😂
Ambuye Kodi chakwela afa liti tipume?
The DC fire mabomba
Yakhulani bwana timakunyadirani bigy
Ine ophika zakudya zakumademo
Kkkkk iwe zakudya ine madzi othira mutu
Munthu wankulu mumatitsegula mitu