BON KALINDO 27 JULY 2024 KUSALAZA KWA PA SATURDAY

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 17 окт 2024

Комментарии • 124

  • @AmosJere-ir4zr
    @AmosJere-ir4zr 2 месяца назад +1

    Awa a MCP ndimakape kwabasi ndipo ndi mbuzi za anthu, ife tili pa mbuyo panu a DC

  • @giftkayome3568
    @giftkayome3568 2 месяца назад +2

    Mwayankhula zoona akulu, The DC.

  • @chrisschikozera7271
    @chrisschikozera7271 2 месяца назад +1

    Big up Mr president we love u ❤

  • @MikeArthur-jd2ij
    @MikeArthur-jd2ij 2 месяца назад

    Ng'alurization😄😄😄
    The DC 🔥

  • @DalitsoMatope
    @DalitsoMatope 2 месяца назад +5

    My president just imagine fertilizer cost 89,000 kwacha is this a way of life or a way of death

  • @scoltenroma6240
    @scoltenroma6240 2 месяца назад

    Koma DC adaaaaa😂😂✊

  • @GiftSoko-w4h
    @GiftSoko-w4h 2 месяца назад

    Koma iwe Bon kalindo usazafe uzangosowa wava ndipo iwe unforeseeable kuima uprezidenti uzawona Malawi 🇲🇼 kukuvotela umaganiza osati zisiru iziiiii

  • @lyiemax
    @lyiemax 2 месяца назад +1

    That's our beloved president ❤❤❤

  • @sarahmphande6108
    @sarahmphande6108 2 месяца назад +1

    Our angel from above

  • @KunyengaMoyo
    @KunyengaMoyo 2 месяца назад

    Chilungamo ichi cha nyooo, angogawa ndalama mopanda dongotsolo moti apange zoti zinthu zitsike mmmmm mukamva ndafa wandipha😂😂😂😂

  • @razackibrahim5880
    @razackibrahim5880 2 месяца назад

    Bon Kalindo ❤❤❤❤❤❤❤ I love you so much

  • @HopeLuwangakaunda
    @HopeLuwangakaunda 2 месяца назад +1

    Our president BON KALINDO ❤❤❤

  • @hamiltonsolomon3756
    @hamiltonsolomon3756 2 месяца назад +1

    More Fire 🔥 🤧......Bon Kalindo....Auze amenewo amvetsese...Chakwera wationongera Mother Malawi...
    People are suffering tindikwera kwa zithu zofunika kwambiri.

  • @LaikaSaidi
    @LaikaSaidi 2 месяца назад +1

    Athilen mau anthu osaopa Mulungu amenewo

  • @Kabwilachikangawa
    @Kabwilachikangawa 2 месяца назад +1

    Just meet the DC outside my home. What an honor to meet him...🤝

  • @BruceChirambo-ly8jm
    @BruceChirambo-ly8jm 2 месяца назад

    BOOOOOON KALINDO🔥🔥🔥🔥🔥💯💯💯

  • @Homeofpeace321
    @Homeofpeace321 2 месяца назад +1

    Ayi dzikoli ndilaiweyo kalindo, osamakhala ndi nsanje

  • @CalvinThomson-ys5zf
    @CalvinThomson-ys5zf 2 месяца назад +1

    Uniform mpaka muisoka zikizaki 😂😂😂😂😂😂

    • @YassinAmbali
      @YassinAmbali 2 месяца назад

      😂😂😂😂😂😂

  • @arthurkayuza
    @arthurkayuza 2 месяца назад

    Ndiye mwati chani "ng'alulazation"😂

  • @OwamiSimeon
    @OwamiSimeon 2 месяца назад

    West of west president in the world 🌎

  • @ghamagift4591
    @ghamagift4591 2 месяца назад +1

    Lets go.....umati tsegula mutu

  • @GeraldChikalema
    @GeraldChikalema 2 месяца назад

    😂😂😂 Ng'alulazation yomweyo kuti wawawaaaaa

  • @JonaZimpita
    @JonaZimpita 2 месяца назад +1

    Mbu🥵li iwe tang,aluluko chizungu

  • @MoeshahIbrahim
    @MoeshahIbrahim 2 месяца назад +2

    Alot is not going well amalawi tiziombela mmanja sitima 😂 ifeyo kodi aliyense amateurs galimoto aaah njala ndalama izipezeka

  • @GRACIOUSKENAN
    @GRACIOUSKENAN 2 месяца назад +2

    Hello our president bbboooonnnn kalindoooooo

  • @loneymagwera915
    @loneymagwera915 2 месяца назад

    Ng'alulasation🎉🎉🎉🎉🎉🎉

  • @Mervic-vm8eo
    @Mervic-vm8eo 2 месяца назад +1

    Tilimu zimu wa chikangawa pano 🙌🙌🙌🤣🤣🤣🤣🤣

  • @AlinafeLinje
    @AlinafeLinje 2 месяца назад

    Mr DC mumakwana

  • @RitaKainga
    @RitaKainga 2 месяца назад +2

    Ng'alulaaaa!!!!!!! THE DC CCCCCV!!!!

  • @DavidJackson-ox4xm
    @DavidJackson-ox4xm 2 месяца назад +1

    A Malawi tili pa mavuto oopsa kwambiri MULUNGU atithandize kwambiri

  • @SamuelKulimah
    @SamuelKulimah 2 месяца назад

    Shallomo Malawi shallomo 😂😂

  • @EmmaculateChadambuka
    @EmmaculateChadambuka 2 месяца назад +2

    ❤❤❤❤❤❤I love you Mr. DC

  • @inessmsiyambiri8517
    @inessmsiyambiri8517 2 месяца назад

    Koma DC ndimakhala ndi chidwi ndi apolicewa iiiiiii unifom eti mpaka kuisokasoka eti

  • @GeraldChisokeza-er5cf
    @GeraldChisokeza-er5cf 2 месяца назад

    Nthawi yaathera bas

  • @MoosaSame
    @MoosaSame 2 месяца назад +1

    The DC ❤❤❤❤❤❤❤❤

  • @JohnAsendi
    @JohnAsendi 2 месяца назад +2

    Ukumba manda Achakwera adzakaitena Ukumba zisime kuti chizakhale chakuya tidzachite kunponya ngati galu😂😂😂😂😂

  • @EmmanuelNgambi-y6h
    @EmmanuelNgambi-y6h 2 месяца назад

    Tiyeni tipange ngati zaku kenya

  • @inamrigala
    @inamrigala 2 месяца назад +4

    Malawi idyan ndalama Za makape omuvotela tamuziwa kale ife

  • @MphatsoGamah-v3v
    @MphatsoGamah-v3v 2 месяца назад +2

    Big up Mr president!!

  • @watsonmhango8794
    @watsonmhango8794 2 месяца назад

    DC ukulasa mfundo zoveka bwino, ukulasa mfundo

  • @DavidJackson-ox4xm
    @DavidJackson-ox4xm 2 месяца назад +1

    The DC'S mwana woooopsa kwambiri akhalise Malawi chilungamo chiyende ngat madzi

  • @ThandiMbewe
    @ThandiMbewe 2 месяца назад +1

    Zikizaki indeed koma ndalama nde zikusakazidwa eish

  • @inessmsiyambiri8517
    @inessmsiyambiri8517 2 месяца назад

    Mzimu wa chilima

  • @DeenesNurudMeke
    @DeenesNurudMeke 2 месяца назад +2

    Boma iri likulangadi eeesh mbola ndithu mmm

  • @temwarachaelkhonje3733
    @temwarachaelkhonje3733 2 месяца назад

    Mwanza mwanza adaaa😂

  • @TapiwaKhwisula
    @TapiwaKhwisula 2 месяца назад +1

    The dc tiyeni paseu basi bomali latitola kwambili sizoona akuchitazi dzikoli silabuyao mmmm

  • @KingsleySitima
    @KingsleySitima 2 месяца назад +1

    Kkkkk welcome the DC Inu nd one tili pa mbuyo panu bwana

  • @Thewarrior7093
    @Thewarrior7093 2 месяца назад

    Akuti samalani oipa watsikira komweko

  • @ArchangelMdzinga
    @ArchangelMdzinga 2 месяца назад

    Osabayo ndi ndani? Olo iweyo sungathandize amalawi

  • @petrooverton6643
    @petrooverton6643 2 месяца назад

    Mzimu WA CHILIMA

  • @ViserKabango-jt1hs
    @ViserKabango-jt1hs 2 месяца назад +2

    Musamayiwale kuyikapo mau akuti achimwene aku nthochiiiiiii,the DC !!!! mukatsanzika

  • @DalitsoMichongwe
    @DalitsoMichongwe 2 месяца назад

    Kulankhula zoona zokhazokha....chilungamo chimawawa

  • @SaudhaKatete
    @SaudhaKatete 2 месяца назад +1

    Kumun'galula kumene Mr chikangawa more fire the dc

  • @PatrickNkumba
    @PatrickNkumba 2 месяца назад

    Bon kalindo amanena chilugamo

  • @Robertmkango
    @Robertmkango 2 месяца назад +2

    Mademowo akhàre omuchosa mpopano bas

  • @BeckhamDavid-v6c
    @BeckhamDavid-v6c 2 месяца назад +2

    Born kalindo ndi wa one auze chilungamo avetse boma lonyasa iri

  • @Emmanuelisraelsimbi
    @Emmanuelisraelsimbi 2 месяца назад

    Koma iwe DC ma demo aliko liti Kodi 10 days ija sinathe?

  • @DeenesNurudMeke
    @DeenesNurudMeke 2 месяца назад

    Mnyamata uja waiphula kwabas

  • @PatrickViyache
    @PatrickViyache 2 месяца назад +3

    DC inuyo mumatiimilila ife amalawi?

  • @BenNgreziman
    @BenNgreziman 2 месяца назад +2

    And Malawi ambiri anali ndizoyankhula kma timaopa kukadyela mgaiwa pawindo big inuyo mumatiimilira ulemu wanu

  • @FunnyKatchenga
    @FunnyKatchenga 2 месяца назад

    Our president ❤❤❤

  • @G00dwillPhiri
    @G00dwillPhiri 2 месяца назад

    Mmakwana mbwiye

  • @billymhoni9527
    @billymhoni9527 2 месяца назад

    Utm moto

  • @FrancisMazamba
    @FrancisMazamba 2 месяца назад

    Ulemu wanu bwana

  • @Dentera215Music
    @Dentera215Music 2 месяца назад

    😂😂😂😂chimwana choopsa kwambiri

  • @AustinBornface
    @AustinBornface 2 месяца назад

    The DC!

  • @ajudyaustine984
    @ajudyaustine984 2 месяца назад

    The DC 🔥🔥🔥

  • @GanieAlidih-gu7no
    @GanieAlidih-gu7no 2 месяца назад

    Zimu wagadama

  • @JosephLemani-qq1is
    @JosephLemani-qq1is 2 месяца назад +5

    Mbambande bon kalindo ndipo ife tili nanu nanupaka zinthu zizasunthe 💥💥💥💥💪

  • @KennedyKanyama-ce8lb
    @KennedyKanyama-ce8lb 2 месяца назад +1

    Mbambande bon kalindo auze

  • @prettytambala5687
    @prettytambala5687 2 месяца назад

    Koma the DC 😅😅😅😅😅😅

  • @ALEXKAUYE-it9os
    @ALEXKAUYE-it9os 2 месяца назад

    Kodi, DC wamanidwa dollar to, ndiye mwayamba kuululakkkkkmm

    • @RemitterFlik1130
      @RemitterFlik1130 2 месяца назад +1

      Ndiwe opusa iwe eti ukuona ngati The DC ndioshota ngati iwe pita uzikakanda uko mbuzi

  • @DONNEXKhama-bk1gy
    @DONNEXKhama-bk1gy 2 месяца назад

    Chakwera zomwe akuchita Atha kukuchimwisa ndithu kod ulamuliro wanji umeneu

  • @GospelSoldiers-sr7np
    @GospelSoldiers-sr7np 2 месяца назад +1

    Ndipo zomvetsa chisoni kwambili komatu kuli Mulungu ichi ndiye asamaiwale ay

  • @DalitsoMbalanje-n2p
    @DalitsoMbalanje-n2p 2 месяца назад +2

    Mmakwana apule

  • @JoelMwenegamba
    @JoelMwenegamba 2 месяца назад

    DC chilungamo ngati madzi amu lake Malawi.

  • @SprianoJeke
    @SprianoJeke 2 месяца назад +2

    Azanyamula makala Kwa kalulu ku Dedza

  • @Robertmkango
    @Robertmkango 2 месяца назад

    Ndipo live umakwana DC

  • @geraldgomati9624
    @geraldgomati9624 2 месяца назад +3

    Mzimu wa Chilima

  • @YoramChimtakabanda
    @YoramChimtakabanda 2 месяца назад

    Inu mulibe zelu Ife tupindula nazo

  • @ZioneMkwanda-y6i
    @ZioneMkwanda-y6i 2 месяца назад

    Winawe olo manyazi ulibe, ukulimbana ndi Bon Kalindo apa , CHOTI udziwe Bon Kalindo ndi president waife osauka ndipo izi akuuza ife, iweyo abale ako nda a Chikangawa Party takudziwa shame on you! Our president please more 🔥🔥🔥 Tell them the truth, winawe uziluma pa mchombo, wekha- wekha- kunyoza Bon Kalindo yaaa , Useless boy

  • @dytonmoyo4629
    @dytonmoyo4629 2 месяца назад

    🔥🔥🔥🔥

  • @DixonChimanya
    @DixonChimanya 2 месяца назад

    Kubwera kumeneko tawauza bwino

  • @SimonBanda-b1f
    @SimonBanda-b1f 2 месяца назад

    Ayiwala kuti ndalama zo agule fertilizer NDI mbewu za subsidy kuti mwina anthu alandile mwachangu komanso anthu ambiri
    Koma azapeleka mbewuzo February chaka chamawa

  • @DixonChimanya
    @DixonChimanya 2 месяца назад

    Dyson @tasona mbolo yako sukukuoa kuti ku Malawi pano kwafika nyasi
    Pantumbo pako
    Ngati ukamadya za kape wakoyo chikangawa udzingodya

  • @Geraldmkwewu
    @Geraldmkwewu 2 месяца назад

    Mumakwana madara chakwera chikangawa watikwana kd ndalamazo muzipatara mulibe makhwala katundu wadura nde atagure zake ndani bznesiyo chakwera akanafa km amanganya nanuso mungoyenga ngt wamisara muzayaruka nxt year

  • @JamesKhengemussa-t1d
    @JamesKhengemussa-t1d 2 месяца назад

    Big man,asyene kunga'alula

  • @RemitterFlik1130
    @RemitterFlik1130 2 месяца назад

    Ndipo mutipase number yanu bwana tizikuuzani zambiri zomwe nguluwezi zikuchita

  • @MaryPanje
    @MaryPanje 2 месяца назад

    ❤keep it up

  • @GeraldMustafa
    @GeraldMustafa 2 месяца назад

    The DC ❤❤❤

  • @EMILYKAWALANGA
    @EMILYKAWALANGA 2 месяца назад

    Ndipo kukasiyako akuchita kulandila ma 1 milion koma chikhalikenicho kwinaku analemba kut anthu azilandila 150 paka pano ndalama anthu sanalandilebe koma kwao anthu akuva kukoma munthu woipa uyu akungoona kwao konkha

  • @valenceemmanuel74
    @valenceemmanuel74 2 месяца назад

    Ng'alulization 😂

  • @gracemkandawire8769
    @gracemkandawire8769 2 месяца назад

    Zoona ndi Mizimu ,,a Joyce Banda Nyumba anamanga

  • @Aisha-db6ds
    @Aisha-db6ds 2 месяца назад +1

    😂😂 mzimu wa mgadama

  • @capitalaction4107
    @capitalaction4107 2 месяца назад

    Ng’aluration😂

  • @MarthaMbewe-uk5nn
    @MarthaMbewe-uk5nn 2 месяца назад

    Ambuye Kodi chakwela afa liti tipume?

  • @EMILYKAWALANGA
    @EMILYKAWALANGA 2 месяца назад

    The DC fire mabomba

  • @SamuelAntone-mz6nq
    @SamuelAntone-mz6nq 2 месяца назад +4

    Yakhulani bwana timakunyadirani bigy

  • @priscillamangata4023
    @priscillamangata4023 2 месяца назад

    Ine ophika zakudya zakumademo

  • @williamalvis6028
    @williamalvis6028 2 месяца назад

    Munthu wankulu mumatitsegula mitu