Guys palibe chimene chingalepheretse kuti Namadingo asakhale president wa dziko ....iyeso ndi munthu atha kukhala mtsogoleri, remember aliyese Ali ndi humble begining (anabadwa Ali maliseche ) don't underrate human... the future remains in hand of God....
Ngati analephera kukhulupirika pa sin ija yofuna ku thandiza odwala koma kuhasula what about anthu oti sakudwala timankonda ngati oyimba osati mtsogoleli
Wayamba kuonetsa mbali. This may be starting of your downfall. Ena sakonda Namadingo like team Gwamba n team Onesmus. These fans will blindly hate you including some of their fans. Za mkutu zakozo ukooo
Thanks for watching... Remember to like the video and share.... 🎉
Namadingo is are good person me from Lusaka Zambia am coming to vote for namadingo 👍👍👍
😂😂😂 you
Guys palibe chimene chingalepheretse kuti Namadingo asakhale president wa dziko ....iyeso ndi munthu atha kukhala mtsogoleri, remember aliyese Ali ndi humble begining (anabadwa Ali maliseche ) don't underrate human... the future remains in hand of God....
The voice and story line is promising for the great future
Tinkati abusa ndamene akhoza kutitsogolera bwino pano aliyense akulira .nde or Namadingo atakhala president kucheza naye kwathela pomwepo ,pompo kusintha anzake ocheza naye
We will vote for Namadingo
Ameneyo ngat watopa nd kuimba akayambe kuphunzitsa ku primary
Keep up the good work
Adzaimila ku Zambia kapena Malawi I understand that he is a Zambian citizen
"Dziko linapita patsogolo ndi ma jokes"... Inu kazikakumbani manda palibe chanzeru mukukamba
❤sure
Alise athakukhala president chifukwa bili imatuuza sukulu sotsongoleli kunali president ambili Ku African osapita kusulu
Much as i love Namadingo but he is not fit to be a president.Mwayamba zachibwana
Nanunso mumasowa zokamba nthaw zina bwanji
Tauze
I think Namandingo atakhala president azathula dziko la Malawi .
Why not Lucius Banda
va ziii iwe chimanga no music kagoneni che
Kodi Namadingo simunthu woyimba, iyeyo ndi wa mash up not singer
Achinyamata Bola mwina zitukuko zingapitile kutsogolo nanga achikulire awa amapanga zatsogolo lawo ndi Banja lawo zayeseni namadingo zizaoneka 2025
Kudwala sikugona pa phasa pokhayi, ena amayenda akudwa ngati iweyo zooona ungamaganize mbwelerazo😅😅😅
🤣
James aise ndakomoka ndi kuseka,ndikugwirizana naye anthu ena saganiza bwino
Sam apa ndiye mwapala tu sikhani youza amalawi iyi
Pa woyimba onse mwaganiza za Namadingo why?
Doc
Ayesere ife tizamuvotera
Kodi iwe ukudwala mutu waukulu eti, ukuona ngata uprestent ndiopweka
Tili naye kaye fredo ntchana
Mwakhuta eti,,mungokamba Za Muzik bs, mxieew iweso eti
Zaziiiiiiii!!!!tu zenizeni!!!kungowononga Data langa
Aaaaa uyu wasuta uyu iyaaaaa😂😂😂😂😂😂😂😂😂
Namadingo happey
Ife tikudikila ufumu umene uthetse maufumu osewa posachedwapa zochitika dikilani ndipo anthu amene angazalamulidwe ndi ufumu umenewo sazakhumudwa nawo osati izi mukunenazi ayi mwalephela nose apa
Mboni za Yehova kod?
Uhule ku state house
Anzanuwa Ali ndi Chibwana eti??
Inu musamakambe bwerera zanuzo,,,aaaaah zandinyasa bwanj
Ngati analephera kukhulupirika pa sin ija yofuna ku thandiza odwala koma kuhasula what about anthu oti sakudwala timankonda ngati oyimba osati mtsogoleli
Kd zimene mukunena apazi wakuwuzan ndani?
Ndalama pena paliponse
Abusa ajaso munawakokomeza motele
Tizidzangoimba basi, sitingatachite chilichonse
Dziko likhoza kuwonongeka namadingo atakhala President chifukwa ndi mbuli
Or Ataima mu 2025 akhodza kuwina🎉
wabwalesa nkhani yi pamyana pambuye ako ukut mavusa kaya kutt ndani ngati ukufuna ndama pamsana pako
Mwasowa choyankhula iwe
Tiuzen kaye za peter ndi razalo
Kwabwera kale Gaddafi 2025 mwana
Iwe pala wakhuta nsima gonanga wapulika vazii ukuyooya vambula natchito so vivichi ivi ntheee , asaa
The Dc😂😂😂
Zilibwino kwambili
Mbudzi iweyo
Wakhuta utaka eti ukusowa khani, wamatama ameneyo
Nkhani zake😅😅😅😅
Chibwana ife ai waimva iwe👎👎👎👎👎👎👎👎
Wayamba kuonetsa mbali. This may be starting of your downfall. Ena sakonda Namadingo like team Gwamba n team Onesmus. These fans will blindly hate you including some of their fans.
Za mkutu zakozo ukooo
Bushiri can be ,,,
😂😂😂 Mwapopa2 Doc iiiish 😅😅😅
Aaaaah kkkkkkk,,,nde kulilowetsa zibwana dzikolitu mpakana Namadingo???
Zooonad
Aaah inunso mpaka Namadingo...ndie azizangotimbatu
Tizavota
Mumalotanso eti
mmmmmmm
Kodi iwe ndiwakuti aaaa hahaha 😂😂😂😂😂😂😂 ukutinso economis instead of economics kikkkkk ku Malawi tikapuma kumwamba shuwaaa
Ndiwe galu kobasi
Insha-Allah Namadingo
Aaaa zachambabasi
Aaaa maloto ako amenewo lweyo
Zazii
Ndeye kut ziko latha
Kkkkkkkkk
Aaaaaaaa 😂😂😂😂😂
Haaa kufuna kusokoneza dziko munthu ozikonda ngati Namadingo,iyeyo ali ngati Kamwana kenakake kamatchedwa,Kelly K, what nonsense of this name 😅
Iwe waboza