Chikangawa boys on a Mission, Koma ziliko liko. Tchimo limazunza. Ngati akudziwa Kuti ndiabwino mchifukwa chani matukutuku akuchiluka . Macathy Chikangawa muyaluka . There is God out there who created heaven and Earth
Ankolo mtanyiwa vumbutso la late grace chinga lundipezano , Chipani Cha Thukuta ndi mwadzi chija ichitu,, ankolo Bushiri ndi Mai Banda aja amati sazaonekera koma azakhala Ali momo SI izi kodi😢 Ambuye chitani nawo agaluwa
Koma zotsenzi amene ndi chifukwa cha Ife anthu ndi amene thikuphangitsa zotsenzi ndi Ife anthu osauka chifukwa MCP ayikha ndalama phatsogolo kwanyengelera
Thank you ntanyiwa may Tha almighty God be with you always God is watching what is happening in Malawi, Mulungu kumwambako tetezerani wina aliyense wakonzekeredwa chiwembu chofuna kuti aphedwe afungatireni ndi mapiko anu yehova mchtitseni manyazi mdyerekezi musalore kuti apambane, tipulumutseni mu chimzimu cha imfa pakati pathu Mulungu
IFETU TIMANENA KUTI USI NDI GALU NYANI OPUSA KUYENDA AKUYENDERA ZIPATALA NDI MISIKA SIKUTI NDI NTENDERE ALINDI CHOLINGA , SIZIMENEZI KOMA SIZITHEKA MUKUNGU AKUONA
Oh Zosakhala bwinotu mmmmmmm MCP WHY? Komatu chaona nzako chapita m'mawa chili kwaiweeee This is your time you can do what you want MCP and everything it is well now.....but wait your day for God's revenge for his People and usana mudzauwona ngati usiku kuli kuwawa ndi ululu wachilango
I support Limpopo FM with Comrade Mtanyiwa.
Kumvera mwachidwi limpopo with comrade nta
God will protect our country in Jesus name, Limpopo love ife
Inuyo Mr ntanyiwa mumatimilira ndipo enafe tikudziwa direction chifukwa cha inu ndipo popanda inu sibwenzi tikudziwa mene zinthu zikuyendera mdziko muno inuyo ndi nyali ndipo musadzafe mudzangosowa ngati elliya❤❤
Mwalakhula dzoona without Limpopo bwezi enafe tili chabe azasowedi Ngati Elijah wakumwamba🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥
I love you My brother Ntanyiwa mumakwana Mulungu ankhale Nanu nthawi zonse
Powerful massage ❤❤
Live from south Africa Durban Pietermaritzburg
Live from Durban South Africa ❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
Sizingatheke Coomrade,kummwela Kuno kudzera pa Limpopo FM anthu achenjera,palibe angamvere zamamina zaozo, Salute Limpopo Staff
Umatha upitilidze ife dzikuti wawabe ndipo tsitiza iwara imfa
In Jesus name, Bon Kalindo will be protected.
We always pray for you comrade ntanyiwa❤❤❤
Mulungu akukute ndi chitetezo Chake mtanyiwa
This is Comred ntanyiwa on Lipompo FM kuzangoturikira ndi khanga zaona more 🔥🔥🔥
Ulemu wanu big mumakwana
ndilimphee kuvela limpompo tv and ikungong'alula
Chikangawa boys on a Mission, Koma ziliko liko.
Tchimo limazunza. Ngati akudziwa Kuti ndiabwino mchifukwa chani matukutuku akuchiluka .
Macathy Chikangawa muyaluka . There is God out there who created heaven and Earth
Live from Canada
Ankolo mtanyiwa vumbutso la late grace chinga lundipezano , Chipani Cha Thukuta ndi mwadzi chija ichitu,, ankolo Bushiri ndi Mai Banda aja amati sazaonekera koma azakhala Ali momo SI izi kodi😢 Ambuye chitani nawo agaluwa
Wishing you more life our Malawian voice Comrade Mtanyiwa
Zikomo poti ziwitsa km mulungu akutimva anthufe kulira kwanthu kwa tsiku ndi tsiku atimenyere nkhondo iyi patekha sitintha 👏👏 ulem wanu fm ladio
Posowa masomphenya dziko limaonongeka.
Ndipo ndikuona dziko lino likulowa nkhondodi tisamare AMALAWI ndithutu
Here in mfuwe zambia we are happy with you mntanyiwa, keep it up with your good job
Ndipo amene samvera Limpopo FM ndi awa akumatamanda zigawengazi Lazarus Chakwera ndi zigawenga zimzake
Ntayiwa ndi boni karondo mumatiimilira murungu akudaliseni timakupephererani kwambir
Limpopo ifetu tili ndi inu.akangoyelekeza kuphaso wina ,dziko lathu ndinkhondo basi
Kodi napatumbo ameneyu akufuna athe tundu wathu wa Malawi mulungu akuwone zonsezo
Ndiyetu aombera Malawi yensetu.chifukwa amene atatsale mbiri ilipobe.
Umakwana iwe wa rimpopo
Ndiwe wekha Mtanyuwa 😅😅😅
Ntanyiwa umakwana
Aaaaaa apolice amenewo ndi opusa ine sangandipange zamanyizo ndipo sindingaimbe, aphwanyeni agaluwo
Ulemu wanu Big
Koma zotsenzi amene ndi chifukwa cha Ife anthu ndi amene thikuphangitsa zotsenzi ndi Ife anthu osauka chifukwa MCP ayikha ndalama phatsogolo kwanyengelera
Tikuona chilichose chomwe chikuchitika tili mmaso
Ndichocho manganya ndi wakudzimbabwe apotende mwabaya mr tanyiwa
Basi chikangawa chakwera akhalira yomweyo kupha iiii
May God intervene
Powerful message
Mutamuuza umatha big up
Zikupeleka sense ndithu,sikuveka zoona,chifukwa manganya akudabwitsa,wagundikilanji ndikumwela
Comrade nta your the best with Limpopo fm❤❤❤❤
Anthu amasegula mimba kamba ka tanyuwa Muona moto tanyuwa osaopa ana mwachepa inu Mcp atanyuwa kachakumwa bwaaaa
Ife pa 31 july tikukayatsa moto ma Demo anyooo
Chakwera this time sitikusiya try kupha modzi kwa amenewa
Agwiridzanedi kuti achotse nyansizo
Mulungu wathu sakhala chete
Tiuzeni Bwana, musatope nafe iyayi
Thank you ntanyiwa may Tha almighty God be with you always God is watching what is happening in Malawi, Mulungu kumwambako tetezerani wina aliyense wakonzekeredwa chiwembu chofuna kuti aphedwe afungatireni ndi mapiko anu yehova mchtitseni manyazi mdyerekezi musalore kuti apambane, tipulumutseni mu chimzimu cha imfa pakati pathu Mulungu
Mulungu apitilize kukutetezela kt oipawo agwe mumatope
Kungofa munthu wina panopa ndinkhondo
Komatu akangoyelekeza kupha wakumwela aziwe kuti tsiku lomwelo iyeyo azachoka pamoando siku lomwelo
Olo atalanda ma galimoto,,, ife vote yathu palibe angayisokoneze
UTM yamakandulo Boma!!!!
🔥🔥🔥
Zoona zake zitsiru zokha-zokha
Lero nde wayamba ndi mototu kkkkk😂
❤❤❤
Lililililililimpopo fm, nd Comrade ntanyiwa u make me feel gud
IFETU TIMANENA KUTI USI NDI GALU NYANI OPUSA KUYENDA AKUYENDERA ZIPATALA NDI MISIKA SIKUTI NDI NTENDERE ALINDI CHOLINGA , SIZIMENEZI KOMA SIZITHEKA MUKUNGU AKUONA
Akomred ntanyiwa ndinu nyale yathu mulungu azikutetezani kwa adani amenewa kuti mupitilize kutiuniila🔥🔥🔥
Mya God bless you brother for what your doing to Malawian's 🙏🙏
Ntanyiwa is talking true, anthu a MCP akudziwa kut kumwela kuzakhala kovuta kut apeze mavot ndichifukwa chake akulimbana kukopa anthu akumwela koma ife manso ali kuchikangawa munya muona
❤ Bravo Limpopo 🔥🔥🔥 Malawi waopsa 🤔Kodi chilango chosemphana maganizo ndi kupha????💔💔😭😭😭👹👹👹
Koma kungoti timve kuti mulomwe aliyense waphedwa Malawi a zavuta kwambiri ifenso tizapha ochewa ✊✊✊✊✊✊✊ sitikuoopa
Manganya sangamupeze munthu kumwera kuno ife zausilu kuno ayi
Live from Welkom Free state
Our truth station radio more fire
MCP ilinso ndi magalimoto a chipani tipemphe ACB afufuzenso ku Congress ngati alidi pa chilungamo
Timamukond zedi Mr ntanyiwa ambuye azikupatsa chitetedzo chokwana ndi moyo wautali nose ku kustudio kwanu❤❤❤❤❤
Oh Zosakhala bwinotu mmmmmmm MCP WHY?
Komatu chaona nzako chapita m'mawa chili kwaiweeee
This is your time you can do what you want MCP and everything it is well now.....but wait your day for God's revenge for his People and usana mudzauwona ngati usiku kuli kuwawa ndi ululu wachilango
Ntanyiwa mumatiyimilila ndipo timakunyadilani kwambili
Mwela madzi, Ntanyiwa umatha umatiimilira.
Akawombela mwa ena amaina antchulidwawa nafe tiyamba po uchifwamba nafe olimbana ndi atsogole a MCP kumawaphanso
I love limpompo ❤.......more lv keep doing lv
Oh Dziko lathu Abale
Mr Ntanyiwa mulungu azikudalitsani opanda inu ife tiri chabe
Akunamidzana ife kumwera sitidzavotera MCP
Anthu nonse mukukonzekera zopha anzanu nde ngt inuyo ndi amuyaya mutakafe ndi inuyo
Atanyiwa munthu wofuna kupanga zimenezo sangalalikire angopanga zimenezo kuti payere payere basi wosati kulalikira angothana nawo ngati mankhwalawo alipodi
Jane Asah knew this 😭😭😭
Ndikutitu anthu amenewa apenge misala ngati Nebuchadnezzar.
Akufuna anthu ayankhule kuti awaphe. Ndege muli nazo zingati zophera anthu
Akulephere kuulutsa uthenga wa kuchikangawa anthu qkutulutsa ndalama mboma momo koma kungopha anthu what type of government is this may God help us
Ndipo ndi chimfiti chimangonama kuti ndi M'busa Ali chigawenga cha chabe-chabe
Comrade Ntanyiwa limpopo 🎉❤
Big up Limpopo FM
Koma tili pa mavuto oopsya, ambuye titetezeleni ife ana anu tili chabe pa tokha sitithasititha😢😢😢
Antanyiwa..inuyo....zikomo..mulungu..akudalitseni ..inuyo ...aaa
Lelo nditapita ku limbe ndapeza azimai amabelo akumvela limpopo
My favorite ntanyiwa
Apaseni umboni akalindo akasume ku khoti or mtambo yo asanaphedwe abale 😢
Akuona ngat tikavota chifukwa cha mantha?
Moto kuti buuu pa 31 atitola amenewa
Kodi Limpopo FM ili pa frequency yanji?
Ntanyiwa pasavute apa ndiyekuti mulungu akutipatsira zigawenga zinja manja mwanthu wina atelekeze kuwomba mfuti ndikudziwa kuti kwawobedwa mfuti uku haaaa auzana chikangawa yose chifukwa nde tipha mokanyanga ndimanja anthu atipata mokwanira zingawenga za chikangawazi aaa ayelekeze ankhubira mulungu kubwera kudzawalanditsa ayese awone zachibwana eti
Ife tili ku overseas tikukuvelanso ndipo iweyo umakamba zoona.
God protect malawians.
Mtanyiwa❤
Mulungu akufungatileni Atanyiwa
Udzingot ntiko osat wa utm
Ndiye aombele anthu onsewa ndiye dzikoli likhalapo koma mmmmmmmmmm
ulemu wanu
Wabwera iweyo❤
Ife athu akumwela ngakhale atimane kuti atikope ife sitikukopeka misozi sinathe maso mwathu