Dat's true bro, we're in a democratic society and noone lemme repeat noone can come and intimidate us in our own country!, Bakili Muluzi tv is a genuine freedom fighter and He's a Hero and watever is saying or talking is the truth!, mukuleka kusakana ndikumangana nokhanokha am'boma inu amene mukutionongela misonkho yathu, pano mwagundika kupanga hire kapena kuti hayala mbava ndizigawenga zimzanu zaku Zimbabwe ndi Ruanda kuti zithane ndi anthu olankhula chilungamo, for wat!, shame on you zikhale ng'oma and mozesi kumukuyu, shame on you!, . Bakili muluzi tv will Never ever be arrested and if u'll try to do dat, we'll fight each other!,
Kodi..uwu wa mutu ngati nkhonkhwe mmati ndani... ? Kunkuyu ..akunama kwambiri.... My brother, you are opening the minds of vulnerable Malawians. Keep it up...afa ndi mtima
Kunyasa ngati manyi ulibe manyazi ukamayankhula zimezo malo moti muzipanga solted out za kwacha devaluetion mboli zanu muyelekeze mu gwile wa bakili muluzi tv muziwona nosenu tithana nanu
Boma lolephera ngati ili have never see it before.... instead of getting busy fixing major problems that many Malawians are facing today they are busy hunting BAKILI MULUZI TV, shame on you useless leaders
Bakili muluzi TV RUclips channel Never arrested I'm telling you this is home land we are democracy now🇲🇼🇲🇼🇲🇼
Dat's true bro, we're in a democratic society and noone lemme repeat noone can come and intimidate us in our own country!, Bakili Muluzi tv is a genuine freedom fighter and He's a Hero and watever is saying or talking is the truth!, mukuleka kusakana ndikumangana nokhanokha am'boma inu amene mukutionongela misonkho yathu, pano mwagundika kupanga hire kapena kuti hayala mbava ndizigawenga zimzanu zaku Zimbabwe ndi Ruanda kuti zithane ndi anthu olankhula chilungamo, for wat!, shame on you zikhale ng'oma and mozesi kumukuyu, shame on you!, .
Bakili muluzi tv will Never ever be arrested and if u'll try to do dat, we'll fight each other!,
Kodi kukukumbutsani bodza lomwe munkatisambitsa nalo 2020 lija kukhaleso mulandu?? Mukuba ndipo aliyense akuona komaso Akudziwa kukuwululani ukhale mulandu??? Viva Bakili muluzi Tv ❤❤❤❤
Ndipo inu ati tidzisangalala ngt zukomela tose kma Mulungu alipo ndipo ndimwini chitetezo ameen
We love bakili muluzi tv than chakwera
Amaphoyisa bophani yonke uyathuka Mulungameli , bayadelela laba banthu
Keep it up bakili muluzi TV ziyaluke mbamva zimenezi
Nkukuyu phwala lako ndithu osakungwira iwe unapha alani witika bwanji bolo yako kuphatikiza zinkhale ng'oma ndi chakwera nose bolo zosadulindwazo zozaza madeya muuzane ❤❤ bakili muludzi channel tsimupata munyera manyi onukha
Akumangatu iwe 😂😂😂😂😂
Palibe, we love bakili muluzi tv....osati tv ya muluzi..😂😂😂😂😂
We love Bakili muludzi tv best TV ever
Kodi..uwu wa mutu ngati nkhonkhwe mmati ndani... ? Kunkuyu ..akunama kwambiri....
My brother, you are opening the minds of vulnerable Malawians. Keep it up...afa ndi mtima
😂😂😂😂😂😂😂 koma ndaseka
😂😂😂😂😂, wamutu ngati chikwele cha nkhunda kkkkkkk
😂😂😂😂😂😂
Machende achakwela ndi agalu azake osavinidwa am here Durban lamontville ngati akufuna andipeze viva bakili muluzi 📺 we are behind you
God protect bakili muluzi channels tv
Aaaa koma ana inu mwasowa zochita et wa bakili muluzi tv Mulungu amutezera
God BLESS You
Appreciate TE You
AND RESPECT You
DEFINI TELY For You
Long Live bakili muluzi tv 🎉🎉
The angles of God will be always around you protecting you where ever you are sir Mr bakili TV 🙏❤❤❤❤
Ndakayika ngat angazikwanise akuziyambazi, people loves you boss and I'm one of them ❤
Akuyiyambayi ndi ndewu ya nkhondo
Koma Mwapanga ko note kuti WA Bakili Muluzi TV kuti ziiiiii?
We stand with bakili muluz
Koma guys nduna ziwiri kukanika kugwira ntchito za Boma nkhani koma Bakili muluzi tv zoona?😂😂😂
Muuzeni galu was kaunjikayo kuti its not TV ya muluzi Bakili, it's TV on its own
Malawi police kukanika kugwila munthu wamba ndiye angagwile zikale ng'oima homeland security wakubayo 🤣🤣🤣
Stay safe my brother!!! We love you and we wish you a long life
Kuliufulu Mani tsitsani suger soap ndi Xina musiyeni muthu
No worries we are together atigwira tonse
Mcp kupumila ku nkhwapa chifukwa cha bakili muluzi tv munya agalu inu ndi corruption yanuyo bakili muluzi inabwera kuzakhala pano ndipo sizasitha
Mitu siukugwila kulimbana ndianthu Malo moto akonze ziko
Boma lopusa kwambiri satana amadana ndichilungamo ziwanda izi
Zimapanga hate akubanu, pomwe ife osawukafe timanjoya ndi bakili muluzi TV kuposa chilichose
Agalu anenewa asagwila mbava zikuba ndalama boma
Komadi inuu eish
Bakili muluzi tv osafooka ndip osaopa Pali chilungamo sipakhala mantha kip it up love you more
Kkkkk koma azikhale mwangokula mutu koma ulibe nzelu bakili muluzi tv simungamukwanise ameneuja ndipatali ife tithane ndinu sopapano agwape inu
Akutaya nthawi Yao zangamupeze ameneyo Chakwera must go
Mphwanga iweyo ndi akatundu police ya ku malawi yakukanika 😂😂😂😂😂 kenako akunena zosemphana brother keep it the fire burning one year left
Yesani kumumanga muwone ngati mukuganiza kuti timakuopani.
Mukuona ngati ndinu amuyaya inuyo eti.
Nafensotu mifuti tilinayo
Best tv ever in Malawi ❤❤❤
Tchito kulimbana ndi anthu azanu si kukweza kwacha we love this guy bakuli TV mo 🔥
Mmmmmhu mpaka asilikali akuja akuchedwa brother Bakili Muluzi TV 🔥 iwowatu ai Mulungu ai ndbwino kuti azingopanga zoti adyeretu chifukwa nthawi yawathera 2025 ulamuliro wao ukutha monga momwe MULUNGU anawatulusa Aisrae ku Egypt ifenso ku Bagga moyo tikutulukako ndithu Mulungu wamphamvuzonse apitiliza tchito imene anayamba mwa Inu Ndipo azikutetezani 🙏
Paja kalindo amawuza kuti ndilipano mundimange amamuopa asamakuopsyezeni ameneo thawi Yao yatha akupita ameneo
Bomba sakhalisa chifukwa likaphulika silibisika
Keep up bakili muludzi best TV in Malawi 🇲🇼💯
Uyu2 amanena chilungamo mugwile mbava zili m,boma nanga mpaka kulimbana ndi mwana ngat ameneyo. Pangani zina
You will never get Bakili muluzi TV he's always with God and I am praying for him to be safe bakili muluzi TV is there to tell us truth
Akamupeza chakwela azankhala wamuyaya bolezamawo muonaso Kodi bakili muluzi ndiye ikugwesa kwacha iiiya zausilu basi
Ndine mosi kwa andu amene amasapota Bakili muluzi TV sikomo amalawi asanga
Kodi aboma mulibe zina zochita kuma offece anuwa mwatikwanatu pano bakili muluzi simavuto athu ife tikufuna ma passport agaru inu kodi mukufuna anthu atani
😂😂😂😂😂, amenewa siagalu ayi koma imbwa za dogs
Mmalo mosaka zakudya anthu akufa ndinjala ndiye kumaononga ndalama kusaka wa tv mbuzi zanthu
Sitikuopa ,mukudana ndi chilungamo inu.mukufuna kumaba opanda okudzudzulani.Brother usanyumwe nawo makapewa.
That will not happen
Bakili tv God bless you ❤❤
Mukapanga masewela tiyambisa gulu lazigawenga tithana namwe sitingakuopeni ayi
Number one tv❤❤❤🎉🎉
Zisilu izizi Bakili Muluzi TV. Musakhotese nkhan pamenepo akuti TV ya abakili mapazi ao anthu okuba inu
Komanso nkulu ameniyi akuti nduna yanji sichidakwa chimenechi
Zitsiru za anthu izi
Mwavomereza kuti akunena zowona
Mulungu amutetezere B muluzi ❤❤❤
Mulungu atithandize ameneyi asamupeze ndithu, mwaiyeyi tikudziwako zinsisi zambiri🙏
Mitu yanu simagwira. Malo mokoza mavuto amene akukumananawo a Malawi
anthu akuba awa ndipo mayazi zitsilu izi zichoke boma zikuba kwambiri
Muchoka chaka chamawa inuyo ndipo simumukwanitsa wa bakili muluzi
😂😂😂😂😂😂😂 chimimba ngati finye
Ifeyo we Love ❤️ Bakiri muluzi TV
Koma kusowa zochita boma ili aaaaa koma kuputsa kwenikweni uku
Boma lazaza ndi zisilu mwava
Asa azibambonakulu akulu ngati inu mpaka kusaka bakili muluzi TV ASA kuwopa chilungamo koma azathu mwalemelatu ma tissue ndindalama
Komatu God is watching what u are doing guyz nd mcp yanuyo
Koma zoona bomali ndalama azionongela zachibwanaziii
Imeneyi ndiye nkhondo, mukuona ngati chipani chanuchi ndi chamuyaya eti
Bakili muluzi TV ❤❤
Remember security is rule number one maintain your situation awareness coz ili ndi boma but all in all keep it up
Zikhale ng'ona musamadana ndi chizuzulo zikalakwika zalakwika
Awuzen agulewa
I love bakili muluzi tv,, Mcp nthawi yanu koma chaka cha mawa tionana
Best tv
Ana achepa
Bakili muluzi tv is our bold Best whole Malawi
Mbuzi ya munthu president ameneyo kuchita kuwopa bakili muluzi Mesa kubako achina mapwalanu
Mungoonanga ndalama zaboma a zikhale ng'oma Pangani za minster of finance ija ndinu agalu kwabasi
Ayelekeze kukumanga Ku Malawi kuvuta ndithu
Viva bakili muluzi tv 📺 ♥️ viva, bakili muluzi tv woyeeee ku nkuli kwereko kuchitekete.
Iyi ndi tv #1 kumalawi
Zisilu iizi zosowa zochita mmalo mokodza ziko ndiye munakula bwanji
Chakwela ndi cabinet yake zisilu
Imagine the whole government now it's against bakili muluz tv chilungamo baba munya
osaopa ndi agaluu amenewo chilungamo chikuwawawa
We are in democracy
Kd za mikangano ya Malawi ndi Mozambique chinachitika ndichani ?
A achipani cholamula odana ndi chulungamo, ndee mwati Bakili tv ikulakwitsa pati?
Pepe kale kod uuzitenga ngat ndiiwe wamuyaya et ediot Nkukuyu mbuz
Useless politicians
Keep fire burning
Bro is on the run
Boma la ambuli but do you know social media 😂😂
The power truth, God protect your Angel, he is unlocking most of received civilians
Kunyasa ngati manyi ulibe manyazi ukamayankhula zimezo malo moti muzipanga solted out za kwacha devaluetion mboli zanu muyelekeze mu gwile wa bakili muluzi tv muziwona nosenu tithana nanu
Sizoopsesa anthu mdziko muno ali mu democracy
Ungamugwire ndani iwe
Tandifunsileni please
Zaziiiii nduna zina zomwe zilizopandq zeru zimenezi
Kukula mutu koma zeru zero basi tamaendani mmidzimu koma muende opanda ma guard ok
Akulu ife tidzalowelera serious tidzapanga mademo coz palibe zimene mukhoza kumagwidwila mudziko la democracy
Mbuzi za wanthu mmalo mothana ndi mavuto awanthu ndalama muzionongela kumanga munthu
Anthu sakugona tulo eti 🙌🙌
Ife ndye bakili muluz tv yo😂😂😂😂 paja amat chilungamo nd mwano😅
Koma nayo nduna busy kufuna munthu wapq yutube abare instead of focusing on PASSPORT PROBLEM
Kutengera nd video iyi ikiperekera umboni oti anthuwa si anthu
Pa mtumbo pake Chakwera ndi anzake
Kusiya kusaka akumba ndlama mboma koma tv yathu eeti
Musiye kumba tisiya kunena za inu
Boma lolephera ngati ili have never see it before.... instead of getting busy fixing major problems that many Malawians are facing today they are busy hunting BAKILI MULUZI TV, shame on you useless leaders