Big up Mr bon kalindo we president 🎉🎉🎉❤❤❤❤zikuntha pa 10 zimenezo za maminazo apampa tipanga za ku kenya 🇰🇪 pa 10 si patali ai so soon ife amalawi ndife wokwiya ndi boma la chakwera never go back
Ndipo apolisi amanyi nonse mukonzeke pa ten pano tikaphane basi oyamba kufa sindikhala ine ndatopa nazo mungosekelala zopsa basi kandalama kake kati komwe mukugulisila anthu osalakwa
Very true The great Bon Kalindo. Opposition need to go and challenge this new rule of no 🆔 no voting. Otherwise, we don't need NRB in our country because they're working for MCP and not Malawians
Muziko mwanthu muno mukuchitika zinthu zonyasa kwambili koma ife anthu timawopa kuphedwa kapena kumangidwa!!! Ili ndi ziko la democracy not one matparty system
Dc muchita bwino nkhani ma ID muitengere ku court ndikutheka a opposition anaphwisiridwa ndi agule mulumusan malawi. Ponda anthu angati unu ziko lathu likafera ku banga moyo
The DC koma otsusa akudziwa chilichotse chimene aboma koma ndele ndidzimenedzo akufuna aboma adziwona ngati zawo dziyenda chifukwa chachinyengo chomwe NRP ikupanga pa kalembela wa ma ID muthalika chihana atupele mayi patelo ndi akaluwa ndianthu oti angalole DZOPUTSA ZA ID ALEMBANA CHIGAWO CHAPAKATI CHOKHA AAAA AKADZALENGEDZA KUTI ALEMBETSA VOTE NDI AMENE ALI NDI MA ID WOKHA NDIPAMENE AMALAWI OTSE KUMWELA KUPOTO DZIWONETSELO PAKA PAKA TIZAVOTE NGATI MBUYOMU ADZATSINTHE NDIPAMENE TIDZASIYE KUMANTCHA KUPANDA APO CHITSANGO KUDZAKHALA KULIBE KOMA CHAKWELA NDI MCP YAKEYO ADZACHOKA PAPANDO ASATITENGA NGATI AMALAWI DZISILU CHAKWELA NDI MCP AYAKOYO NDINU AGALU KWABASI
Pa ten wa police wamakani tikaonetsana ,apolice mumakhala ngati inuyo kut mukugula sugar 5hundred pomwe tonse tikuvutika limodzi ndiye mukachuluka nzeru pa ten muluza miyoyo ovutika akhala abale anu , and mufera zaini chuma akudya mabwana anu inu okathira tear gas pansewu ,muzuzutsa abale anu ndi ana .
Akulu inu pamutu panu sipakuyenda bwino!! The D.C is only man come on public and tell the president true!! Ifetu tili kumbuyo kwa kalindo ndipo inu a MCP musanyengeke kuti mukalowa ku 2025 otherwise third-wool ija izayambika!!
Big up Mr bon kalindo we president 🎉🎉🎉❤❤❤❤zikuntha pa 10 zimenezo za maminazo apampa tipanga za ku kenya 🇰🇪 pa 10 si patali ai so soon ife amalawi ndife wokwiya ndi boma la chakwera never go back
Ndipo apolisi amanyi nonse mukonzeke pa ten pano tikaphane basi oyamba kufa sindikhala ine ndatopa nazo mungosekelala zopsa basi kandalama kake kati komwe mukugulisila anthu osalakwa
Very true The great Bon Kalindo. Opposition need to go and challenge this new rule of no 🆔 no voting.
Otherwise, we don't need NRB in our country because they're working for MCP and not Malawians
munthu amene amadana ndikalindo ndifiti kwambiri Kalindo amatiimirila ife amalawi
The DC mwana oopsaaa kwambiri gwilan ntchito boss
💔💔💔
❤❤❤❤ The DC nthawi zonse kuima pa chilungamo. Ndipo chilungamotu sichimawopsa stand with u all the time
Kuyakhula mwatchutchu bon ❤
Kuyankhura molikonda zdiko mowakonda a Malawi mulungu apitilize kupatani mphavu Komaso madalitso ochuluka
Mr pangolin tatulutsireni ndodo ija achinagwenembewa
Muziko mwanthu muno mukuchitika zinthu zonyasa kwambili koma ife anthu timawopa kuphedwa kapena kumangidwa!!! Ili ndi ziko la democracy not one matparty system
The DC 🔥🔥🔥🔥🔥🔥
Munthu uyu amenyela nkhondo Malawi it's up to you Malawians kukhala mene mulili olo kutengapo step
Nkhaniyo ndiyowona
I support The DCs mwana woooopsa kwambiri akhalise Malawi.
Powerful massenge fadah ❤❤
The dc ..mwana owopsa kwambiri 🤣🤣
Anabwelatu pa shop yanga ndi nfuti akuti kuzatolela ndalamaya nsongo kkkk mpaka mfuti tiziwopa zomwezi?
Ndipo message ya apolice ndi iyi mukazagopezeka mukutenga bali ya chakwera uzazima sitikuchedza pa 10 ok we need change our Malawi 🇲🇼
❤❤❤❤❤ DC
Nanga munthu oti anachita kukatengedwa ku Church angaziwe kulamulira dziko? Ndinkona amangolembana mbutuma zokha zokha
Panopa ine ndikupanga biziness koma profit ndiyaying'ono kwambiri. Mutu wanga wayima.
Ulemu wanu Malume ❤
Za ma hca zo ndee eeeeh zavuta zedi
That's true Mr. D.C
Mashing opangila mashin anzake D. C NUFF RESPECT TO YOU MUMATIIMILIRA 💯💯💯
Oletsa zoyankhula zanu munthu wamkulu,ameneyo ndiye kuti ndi mfiti.mulungu akudalitseni bwana
Good Messnge my Bon Kalindo
Olo uyankhule mbwelera, timamukondabe The DC.
Boma lokuba kwambri
Mmakwana boss mn
Kalindo...The Great Man....winawe osangochoka bwanji
Dc muchita bwino nkhani ma ID muitengere ku court ndikutheka a opposition anaphwisiridwa ndi agule mulumusan malawi. Ponda anthu angati unu ziko lathu likafera ku banga moyo
Good massage boss
Munthu wamkulu zedi, the DC
The DC!!!!
Chakwela ndi mbutuma yamunthu ndi gulu lake
Vuto lovotela mulimi ndi kupanga president ndi limenelo munthu wakukakasiya ndikukukhala president manthongo Ali tho azasukusula liti
The Dc 👹👹👹👹
The DC chimwana cholimba mtima kwa osauka more 🔥🔥 Mr Kalindo Tell them😅😅
The DC koma otsusa akudziwa chilichotse chimene aboma koma ndele ndidzimenedzo akufuna aboma adziwona ngati zawo dziyenda chifukwa chachinyengo chomwe NRP ikupanga pa kalembela wa ma ID muthalika chihana atupele mayi patelo ndi akaluwa ndianthu oti angalole DZOPUTSA ZA ID ALEMBANA CHIGAWO CHAPAKATI CHOKHA AAAA AKADZALENGEDZA KUTI ALEMBETSA VOTE NDI AMENE ALI NDI MA ID WOKHA NDIPAMENE AMALAWI OTSE KUMWELA KUPOTO DZIWONETSELO PAKA PAKA TIZAVOTE NGATI MBUYOMU ADZATSINTHE NDIPAMENE TIDZASIYE KUMANTCHA KUPANDA APO CHITSANGO KUDZAKHALA KULIBE KOMA CHAKWELA NDI MCP YAKEYO ADZACHOKA PAPANDO ASATITENGA NGATI AMALAWI DZISILU CHAKWELA NDI MCP AYAKOYO NDINU AGALU KWABASI
Pa ten wa police wamakani tikaonetsana ,apolice mumakhala ngati inuyo kut mukugula sugar 5hundred pomwe tonse tikuvutika limodzi ndiye mukachuluka nzeru pa ten muluza miyoyo ovutika akhala abale anu , and mufera zaini chuma akudya mabwana anu inu okathira tear gas pansewu ,muzuzutsa abale anu ndi ana .
Nde nkhani zake
Boma la anthu opusa ma savage
Akuluwa akufuna kusochelesa anthu iwowa akudana ndikusakhara pa udindotu
Akulu inu pamutu panu sipakuyenda bwino!! The D.C is only man come on public and tell the president true!! Ifetu tili kumbuyo kwa kalindo ndipo inu a MCP musanyengeke kuti mukalowa ku 2025 otherwise third-wool ija izayambika!!
Umakwana
Ndipo inu a China pharaoh amenewa Sali bwino mulungu wa Israel awayendele
Chakwela wamupha chilima zasala zosatila Zach
Audio iyi yandikhudza kwambiri.
A opposition afasa ngati Chilima
Kod ma track ndi zida zoopya zomwe zinalowa m'muziko mwanthu zija zikuzatani! Kapena boma linagula zida zankhondo za M.D.F? Tatifufuzileni mr kalindo please! Otherwise chakwela atha kutigulisapo apa!!
The DC mwana woooopsa kwambiri
The DC. Chimwana choopsa kwambiri ..ine buzines wanga anaduka kale kale.
The DC
Nde mwati Yosefe anali wa number chani? Nanga Benjamin? Pilizi chonde!
Joseph wa 11 Benjamin 12 walakwitsa pati munthu
Dangerous child ❤
Indeed it's bullshit a MRA the DC ayankhula
D c ❤️❤️❤️❤️❤️
Proud of DC
The DC mwana olimba mtima
❤❤❤❤❤ great full story poor DC
Munthu ukuzitama wekha iwe ndiwe chitsiru chenchen
Iwetu akupasazo ukabweza
Chitsiru ndi wagule akulephela kuyendesa dzikoli, kwacha kumangogwa siku ndi siku
Morning the DC
Assani,keti
Wi love you ❤❤ bon kalindo
Amalawi tiyeni tikhale maso osalola zimenezo zoonadi ndikuba poyera
❤❤❤ The Dc
Mwana owopsa kwambili
💪💪💪💪💪 Bon K
Powerful 👊
Timam'konda Dc,,,iwanawe ušamalimbane ndi Dc
Wenawe ngati wadya ndalama za eni tuluka usamanvele apa ife ndi bon ❤ wagwana nayo pita ukabweze ndalamazo cos apa walephela 😂😂😂😂😂😂
Amutuma kuti azasunzumile kuno Ha😅😅😅😅😅😂😂😂😂wanya nayo wadya ndalama zaulele
Powerful!!!!
Akudziwana onsewatu
Mumakwana kunena dzoona the dc
Ndipo Ine andikhomela pa shop akut ndisokhele 80
D.C ukhalise umatiimilila kwambil
❤❤❤❤karido
Timakunyadiran bg
Ndili pambuyo pako bon kalindo the D.C
🔥🔥🔥
❤❤❤❤❤
Mcp boma lakuba kwambiri.
Auzeni chilungamu
❤❤
The DC 😂
Rest in peace Redson Munlo 😢😢😢😢😢.
We love you the DC
Anganga
The DC
A DPP ADYA BANZI NDIIIIITHu!!?
The DC umakwans
Tingopita ku cort basi
Timakunyadiran bg
📌
Dc
Boni kalindo watha basi
Iwe usamalimakimbane ndi DC ukutaya thawi
I stopped listening to this nonsense frm coz I don't see any profit
Who told you to listen get out
Iwe ndiwe chitsulu osangatuka bwanji ndani akukukamiza kuti uzimvela zomwe akunena bon kalindo musiyeni akutokota za nzelu zothandiza ife iwe unalandila ndalama kuti uzifowola anthu choka galu