BON KALINDO THE D.C 4 JULY 2024

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 3 окт 2024

Комментарии • 105

  • @joyahmedjoma4615
    @joyahmedjoma4615 3 месяца назад +1

    Big up Mr bon kalindo we president 🎉🎉🎉❤❤❤❤zikuntha pa 10 zimenezo za maminazo apampa tipanga za ku kenya 🇰🇪 pa 10 si patali ai so soon ife amalawi ndife wokwiya ndi boma la chakwera never go back

  • @RadsonTimoteo
    @RadsonTimoteo 3 месяца назад +4

    Ndipo apolisi amanyi nonse mukonzeke pa ten pano tikaphane basi oyamba kufa sindikhala ine ndatopa nazo mungosekelala zopsa basi kandalama kake kati komwe mukugulisila anthu osalakwa

  • @ChimwemweKondowe-nj4lx
    @ChimwemweKondowe-nj4lx 3 месяца назад +2

    Very true The great Bon Kalindo. Opposition need to go and challenge this new rule of no 🆔 no voting.
    Otherwise, we don't need NRB in our country because they're working for MCP and not Malawians

  • @jamusnamwino-br2iz
    @jamusnamwino-br2iz 3 месяца назад +3

    munthu amene amadana ndikalindo ndifiti kwambiri Kalindo amatiimirila ife amalawi

  • @ChristopherMadulira
    @ChristopherMadulira 3 месяца назад +3

    The DC mwana oopsaaa kwambiri gwilan ntchito boss

  • @omanm2919
    @omanm2919 3 месяца назад +1

    ❤❤❤❤ The DC nthawi zonse kuima pa chilungamo. Ndipo chilungamotu sichimawopsa stand with u all the time

  • @EllenPhiri-xt8pt
    @EllenPhiri-xt8pt 3 месяца назад +3

    Kuyakhula mwatchutchu bon ❤

  • @ElasonAimon
    @ElasonAimon 3 месяца назад +3

    Kuyankhura molikonda zdiko mowakonda a Malawi mulungu apitilize kupatani mphavu Komaso madalitso ochuluka

  • @MiddayDeleza
    @MiddayDeleza 3 месяца назад +2

    Mr pangolin tatulutsireni ndodo ija achinagwenembewa

  • @lameckmajiga5426
    @lameckmajiga5426 3 месяца назад +2

    Muziko mwanthu muno mukuchitika zinthu zonyasa kwambili koma ife anthu timawopa kuphedwa kapena kumangidwa!!! Ili ndi ziko la democracy not one matparty system

  • @Maxcarcare-g1d
    @Maxcarcare-g1d 3 месяца назад +2

    The DC 🔥🔥🔥🔥🔥🔥

  • @chirpykachingwe6802
    @chirpykachingwe6802 3 месяца назад +2

    Munthu uyu amenyela nkhondo Malawi it's up to you Malawians kukhala mene mulili olo kutengapo step

  • @DavidJackson-ox4xm
    @DavidJackson-ox4xm 3 месяца назад +1

    I support The DCs mwana woooopsa kwambiri akhalise Malawi.

  • @Robbie-w4w
    @Robbie-w4w 3 месяца назад +1

    Powerful massenge fadah ❤❤

  • @twavysibale4751
    @twavysibale4751 3 месяца назад +1

    The dc ..mwana owopsa kwambiri 🤣🤣

  • @MosesShaibu-ee8hn
    @MosesShaibu-ee8hn 3 месяца назад +2

    Anabwelatu pa shop yanga ndi nfuti akuti kuzatolela ndalamaya nsongo kkkk mpaka mfuti tiziwopa zomwezi?

  • @joyahmedjoma4615
    @joyahmedjoma4615 3 месяца назад +2

    Ndipo message ya apolice ndi iyi mukazagopezeka mukutenga bali ya chakwera uzazima sitikuchedza pa 10 ok we need change our Malawi 🇲🇼

  • @AliciaMaphanga
    @AliciaMaphanga 3 месяца назад +2

    ❤❤❤❤❤ DC

  • @MiddayDeleza
    @MiddayDeleza 3 месяца назад +2

    Nanga munthu oti anachita kukatengedwa ku Church angaziwe kulamulira dziko? Ndinkona amangolembana mbutuma zokha zokha

  • @actuarialscience2283
    @actuarialscience2283 3 месяца назад +1

    Panopa ine ndikupanga biziness koma profit ndiyaying'ono kwambiri. Mutu wanga wayima.

  • @DoricaGoweka
    @DoricaGoweka 3 месяца назад +2

    Ulemu wanu Malume ❤

  • @DONOR265
    @DONOR265 3 месяца назад +2

    Za ma hca zo ndee eeeeh zavuta zedi

  • @johnnyeliah4302
    @johnnyeliah4302 3 месяца назад +1

    That's true Mr. D.C

  • @McshonWilliam
    @McshonWilliam 3 месяца назад

    Mashing opangila mashin anzake D. C NUFF RESPECT TO YOU MUMATIIMILIRA 💯💯💯

  • @TecksonKaima-dr6er
    @TecksonKaima-dr6er 3 месяца назад +1

    Oletsa zoyankhula zanu munthu wamkulu,ameneyo ndiye kuti ndi mfiti.mulungu akudalitseni bwana

  • @0wenNkhambule
    @0wenNkhambule 3 месяца назад +1

    Good Messnge my Bon Kalindo

  • @FunnyKatchenga
    @FunnyKatchenga 3 месяца назад +1

    Olo uyankhule mbwelera, timamukondabe The DC.

  • @FrancisGama-qb7ze
    @FrancisGama-qb7ze 3 месяца назад +2

    Boma lokuba kwambri

  • @MisheckSenga-q4i
    @MisheckSenga-q4i 3 месяца назад +1

    Mmakwana boss mn

  • @miraclekayira9613
    @miraclekayira9613 3 месяца назад

    Kalindo...The Great Man....winawe osangochoka bwanji

  • @LuciusPatrick-f2c
    @LuciusPatrick-f2c 3 месяца назад +1

    Dc muchita bwino nkhani ma ID muitengere ku court ndikutheka a opposition anaphwisiridwa ndi agule mulumusan malawi. Ponda anthu angati unu ziko lathu likafera ku banga moyo

  • @dontreybanda278
    @dontreybanda278 3 месяца назад +1

    Good massage boss

  • @VictoriaWilly
    @VictoriaWilly 3 месяца назад +2

    Munthu wamkulu zedi, the DC

  • @DanNzima
    @DanNzima 3 месяца назад +1

    The DC!!!!

  • @LawrenceMalinda
    @LawrenceMalinda 3 месяца назад +1

    Chakwela ndi mbutuma yamunthu ndi gulu lake

  • @MarthaJafali
    @MarthaJafali 3 месяца назад +1

    Vuto lovotela mulimi ndi kupanga president ndi limenelo munthu wakukakasiya ndikukukhala president manthongo Ali tho azasukusula liti

  • @Leo-fj6gz
    @Leo-fj6gz 3 месяца назад

    The Dc 👹👹👹👹

  • @ZioneMkwanda-y6i
    @ZioneMkwanda-y6i 3 месяца назад

    The DC chimwana cholimba mtima kwa osauka more 🔥🔥 Mr Kalindo Tell them😅😅

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda8711 3 месяца назад +1

    The DC koma otsusa akudziwa chilichotse chimene aboma koma ndele ndidzimenedzo akufuna aboma adziwona ngati zawo dziyenda chifukwa chachinyengo chomwe NRP ikupanga pa kalembela wa ma ID muthalika chihana atupele mayi patelo ndi akaluwa ndianthu oti angalole DZOPUTSA ZA ID ALEMBANA CHIGAWO CHAPAKATI CHOKHA AAAA AKADZALENGEDZA KUTI ALEMBETSA VOTE NDI AMENE ALI NDI MA ID WOKHA NDIPAMENE AMALAWI OTSE KUMWELA KUPOTO DZIWONETSELO PAKA PAKA TIZAVOTE NGATI MBUYOMU ADZATSINTHE NDIPAMENE TIDZASIYE KUMANTCHA KUPANDA APO CHITSANGO KUDZAKHALA KULIBE KOMA CHAKWELA NDI MCP YAKEYO ADZACHOKA PAPANDO ASATITENGA NGATI AMALAWI DZISILU CHAKWELA NDI MCP AYAKOYO NDINU AGALU KWABASI

  • @GiftPhiri-tt7nn
    @GiftPhiri-tt7nn 3 месяца назад +1

    Pa ten wa police wamakani tikaonetsana ,apolice mumakhala ngati inuyo kut mukugula sugar 5hundred pomwe tonse tikuvutika limodzi ndiye mukachuluka nzeru pa ten muluza miyoyo ovutika akhala abale anu , and mufera zaini chuma akudya mabwana anu inu okathira tear gas pansewu ,muzuzutsa abale anu ndi ana .

  • @thomasbodo4099
    @thomasbodo4099 3 месяца назад +2

    Boma la anthu opusa ma savage

  • @ChrifordBiziel
    @ChrifordBiziel 3 месяца назад +1

    Akuluwa akufuna kusochelesa anthu iwowa akudana ndikusakhara pa udindotu

    • @lameckmajiga5426
      @lameckmajiga5426 3 месяца назад

      Akulu inu pamutu panu sipakuyenda bwino!! The D.C is only man come on public and tell the president true!! Ifetu tili kumbuyo kwa kalindo ndipo inu a MCP musanyengeke kuti mukalowa ku 2025 otherwise third-wool ija izayambika!!

  • @PatrickSamson-po7uy
    @PatrickSamson-po7uy 3 месяца назад +1

    Umakwana

  • @MarthaJafali
    @MarthaJafali 3 месяца назад +1

    Ndipo inu a China pharaoh amenewa Sali bwino mulungu wa Israel awayendele

  • @BENSONRANGWANI
    @BENSONRANGWANI 3 месяца назад +1

    Chakwela wamupha chilima zasala zosatila Zach

  • @SolomonNjolomole
    @SolomonNjolomole 3 месяца назад +1

    Audio iyi yandikhudza kwambiri.

  • @Enock-c9l
    @Enock-c9l 3 месяца назад +1

    A opposition afasa ngati Chilima

  • @lameckmajiga5426
    @lameckmajiga5426 3 месяца назад

    Kod ma track ndi zida zoopya zomwe zinalowa m'muziko mwanthu zija zikuzatani! Kapena boma linagula zida zankhondo za M.D.F? Tatifufuzileni mr kalindo please! Otherwise chakwela atha kutigulisapo apa!!

  • @PreciousChlima
    @PreciousChlima 3 месяца назад

    The DC mwana woooopsa kwambiri

  • @PeterChimbayo
    @PeterChimbayo 3 месяца назад

    The DC. Chimwana choopsa kwambiri ..ine buzines wanga anaduka kale kale.

  • @Pangolinimw
    @Pangolinimw 3 месяца назад +1

    The DC

  • @AnnoyedFallingLeaves-zp8dy
    @AnnoyedFallingLeaves-zp8dy 3 месяца назад +1

    Nde mwati Yosefe anali wa number chani? Nanga Benjamin? Pilizi chonde!

    • @FrankMsiska-i9j
      @FrankMsiska-i9j 3 месяца назад

      Joseph wa 11 Benjamin 12 walakwitsa pati munthu

  • @oscarchafulumira3127
    @oscarchafulumira3127 3 месяца назад

    Dangerous child ❤

  • @AskMeDalitso
    @AskMeDalitso 3 месяца назад

    Indeed it's bullshit a MRA the DC ayankhula

  • @PempheroMoleni
    @PempheroMoleni 3 месяца назад

    D c ❤️❤️❤️❤️❤️

  • @Ennlesssodoma
    @Ennlesssodoma 3 месяца назад

    Proud of DC

  • @clintonhodda9830
    @clintonhodda9830 3 месяца назад

    The DC mwana olimba mtima

  • @YusufuKaifa-fr4wt
    @YusufuKaifa-fr4wt 3 месяца назад

    ❤❤❤❤❤ great full story poor DC

  • @GeshoMwakitwile
    @GeshoMwakitwile 3 месяца назад +1

    Munthu ukuzitama wekha iwe ndiwe chitsiru chenchen

    • @ZionekaMember
      @ZionekaMember 3 месяца назад

      Iwetu akupasazo ukabweza

    • @dalitson3558
      @dalitson3558 3 месяца назад

      Chitsiru ndi wagule akulephela kuyendesa dzikoli, kwacha kumangogwa siku ndi siku

  • @ZioneMkwanda-y6i
    @ZioneMkwanda-y6i 3 месяца назад

    Morning the DC

  • @rachidecaundealy8335
    @rachidecaundealy8335 3 месяца назад

    Assani,keti

  • @YasinMusa-ym8lp
    @YasinMusa-ym8lp 3 месяца назад

    Wi love you ❤❤ bon kalindo

  • @LimbikaniKadzongwe
    @LimbikaniKadzongwe 3 месяца назад

    Amalawi tiyeni tikhale maso osalola zimenezo zoonadi ndikuba poyera

  • @Aubreysekeyah
    @Aubreysekeyah 3 месяца назад

    ❤❤❤ The Dc

  • @MartseMichael
    @MartseMichael 3 месяца назад

    Mwana owopsa kwambili

  • @macDonaldKuwani-zo3nv
    @macDonaldKuwani-zo3nv 3 месяца назад

    💪💪💪💪💪 Bon K

  • @IsaacMusa-py2jm
    @IsaacMusa-py2jm 3 месяца назад

    Powerful 👊

  • @TopoTopo-bm4vw
    @TopoTopo-bm4vw 3 месяца назад

    Timam'konda Dc,,,iwanawe ušamalimbane ndi Dc

  • @EllenPhiri-xt8pt
    @EllenPhiri-xt8pt 3 месяца назад

    Wenawe ngati wadya ndalama za eni tuluka usamanvele apa ife ndi bon ❤ wagwana nayo pita ukabweze ndalamazo cos apa walephela 😂😂😂😂😂😂

    • @zimmekapachika6784
      @zimmekapachika6784 3 месяца назад

      Amutuma kuti azasunzumile kuno Ha😅😅😅😅😅😂😂😂😂wanya nayo wadya ndalama zaulele

  • @lyiemax
    @lyiemax 3 месяца назад

    Powerful!!!!

  • @KennedyBaton
    @KennedyBaton 3 месяца назад

    Akudziwana onsewatu

  • @AdamYas-ec9oc
    @AdamYas-ec9oc 3 месяца назад +1

    Mumakwana kunena dzoona the dc

  • @IssahTchakato
    @IssahTchakato 3 месяца назад

    Ndipo Ine andikhomela pa shop akut ndisokhele 80

  • @LazarusEvasonchafachaola
    @LazarusEvasonchafachaola 3 месяца назад

    D.C ukhalise umatiimilila kwambil

  • @JunaKananji
    @JunaKananji 3 месяца назад

    ❤❤❤❤karido

  • @GiftKananji
    @GiftKananji 3 месяца назад +1

    Timakunyadiran bg

  • @LazarusStanford
    @LazarusStanford 3 месяца назад +2

    Ndili pambuyo pako bon kalindo the D.C

  • @DoreenMuhota
    @DoreenMuhota 3 месяца назад

    🔥🔥🔥

  • @ElickMalindima-s3t
    @ElickMalindima-s3t 3 месяца назад

    ❤❤❤❤❤

  • @DavidJackson-ox4xm
    @DavidJackson-ox4xm 3 месяца назад

    Mcp boma lakuba kwambiri.

  • @kondwaniwhite2871
    @kondwaniwhite2871 3 месяца назад

    Auzeni chilungamu

  • @Wellingtonphiri-op8pp
    @Wellingtonphiri-op8pp 3 месяца назад

    ❤❤

  • @PoxisNation-fe1kr
    @PoxisNation-fe1kr 2 месяца назад

    The DC 😂

  • @Homeofpeace321
    @Homeofpeace321 3 месяца назад

    Rest in peace Redson Munlo 😢😢😢😢😢.
    We love you the DC

  • @HarryMakwale
    @HarryMakwale 3 месяца назад

    Anganga

  • @IsmailRahim-yy3yr
    @IsmailRahim-yy3yr 3 месяца назад

    The DC

  • @MarthaMbewe-uk5nn
    @MarthaMbewe-uk5nn 3 месяца назад

    A DPP ADYA BANZI NDIIIIITHu!!?

  • @MussahSmart-wn5ue
    @MussahSmart-wn5ue 3 месяца назад

    The DC umakwans

  • @Drmuhammadchiwona
    @Drmuhammadchiwona 3 месяца назад

    Tingopita ku cort basi

  • @GiftKananji
    @GiftKananji 3 месяца назад

    Timakunyadiran bg

  • @MasterHeadson
    @MasterHeadson 3 месяца назад

    📌

  • @paulpaseli6310
    @paulpaseli6310 3 месяца назад

    Dc

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of 3 месяца назад

    Boni kalindo watha basi

    • @TopoTopo-bm4vw
      @TopoTopo-bm4vw 3 месяца назад

      Iwe usamalimakimbane ndi DC ukutaya thawi

  • @GeshoMwakitwile
    @GeshoMwakitwile 3 месяца назад

    I stopped listening to this nonsense frm coz I don't see any profit

    • @MarthaJafali
      @MarthaJafali 3 месяца назад

      Who told you to listen get out

    • @EllenPhiri-xt8pt
      @EllenPhiri-xt8pt 3 месяца назад

      Iwe ndiwe chitsulu osangatuka bwanji ndani akukukamiza kuti uzimvela zomwe akunena bon kalindo musiyeni akutokota za nzelu zothandiza ife iwe unalandila ndalama kuti uzifowola anthu choka galu