PROPHETIC MESSAGE TO THE DPP ON SELECTION OF A RUNNING MATE | Prophet Emmanuel Zomba Malawi
HTML-код
- Опубликовано: 15 сен 2024
- Message to the DPP.
The DPP needs a man of God who is indeed sent by God to tell them what God is saying on this because in future there will be a problem.
#dpp
ARENA OF VICTORY MINISTRY OF ALL NATIONS - AVMOAN
We are in Naisi, Zomba.
RUclips: Prophet Emmanuel Zomba Malawi
Face Book: Prophet Emmanuel D. Peter
Twitter: emmanuelavmoan
Instagram: prophetemmanueldpeter
Email: emmanuelprophet0@gmail.com
WhatsApp: 0995 302 917
For booking:
+265 0880 451 134
Prayer Lines:
+265 0995 302 917 (Whatsapp ONLY)
+265 0992 579 390
+265 0997 174 773
+265 0991 480 448
+265 0885 317 997
+265 0880 895 441
+265 0883 647 049
Inetu ndikudabwa ma prophet akungokamba za ndale basi asiya ntchito yamulungu akufuna zosangalatsa anthu, ndi kuntchuka basi samalani pogwira ntchito yamulungu.
Ambuye akuchitireni chifundo pakuti simukudziwa chomwe mukuchita
One prophesied that chilima will govern the country km anatisya.... Abodza awa
Atsatu ndawi yophembela mulibe basi one day pa week ndaleso pomwepo kwanamisa anthu kuti mumalangulana ndimulungu koma kwiyo wamulungu ndimoto wosata samalani
Mukukamba zandale bwanji tapempelelani Malawi khozi zimene zikuchitika kuno
Mulungu yekha ndamene akudziwa zonse
Za ufumu wa kumwamba zilipo apa?
Aprophet akuona dpp ikupita kumasankho Opanda tsogoreri
It's your job to pray for them
Abusa mavesi ngsti atha yambani ndale mulungu wathu alibe chisokonezo
Kodi zimenezo ndi za Mulungu kapena zamutu
Koma ine kumalawi omwe anatembelera dziko lakumalawi iiiii aneneri
Kkkkkkk aprofit
Ndapangani za mulungu Nanu bwanji pomwe mwakhala basi za chipani kungofuna ndalama mzina la mulungu kkkkk