Rev Alexander Kambiri preaching at Malawi Immigration Head Office -Lilongwe Malawi

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 28 окт 2024

Комментарии • 82

  • @sichaliwilson
    @sichaliwilson 9 месяцев назад +3

    Please continue organizing this program frequently as very helpful to such.God bless you Rev.Kambiri

  • @ceciliasibande7936
    @ceciliasibande7936 9 месяцев назад +4

    Kupezeka ku immigration ndi chisomo cha Mulungu zoonadi
    Mulungu adasankhadi inu kuti mupezeke pa maudindo muli nawowo. A big Amen

  • @blessingkamanga1781
    @blessingkamanga1781 9 месяцев назад +8

    Maybe they can stop corruption. The one who organized this program may God bless him or her abundantly.

  • @MaggieKapalamula
    @MaggieKapalamula 7 месяцев назад

    This is beautiful may God bless immigration office for honoring God words

  • @catherinechisale9567
    @catherinechisale9567 7 месяцев назад

    Good initiative by Immigration Department. May good Lord bless you. Zikungofunika kulapa basi, mgt Pampanga mbali yake.

  • @VictoriaWilliam-ms2ft
    @VictoriaWilliam-ms2ft 7 месяцев назад

    Amvekere Amen ngati za nzeru mbava zachabechabe izo ndipo alape anthu amenewo

  • @Blessed-w2e
    @Blessed-w2e 6 месяцев назад

    May God bless you pastor powerful message wakhutu wamva

  • @enipherphiri207
    @enipherphiri207 9 месяцев назад

    Wow! This is the divine definition of grace to individual staff at immigration. Review yourself and stop maladministration. The spirit has spoken. Thank you pastor Kambwiri

  • @KammangaEp22
    @KammangaEp22 8 месяцев назад

    God continue talking to us through the ones you have chosen
    So that we can know why we are in our positions
    Amen

  • @marypatriciamakuru226
    @marypatriciamakuru226 8 месяцев назад +1

    Amen Amen Amen.
    Mwina asinthe mchitidwe wa corruption. Abusa mudziwayendera kawiri kawiri.

    • @UmiwuWasiya004
      @UmiwuWasiya004 8 месяцев назад

      Sipangakhale kusintha because pamwambapo pali mbava yeni-yeni Shakwera ndi afalisi azinzake

  • @suzyomanda4359
    @suzyomanda4359 9 месяцев назад

    Amen, thank you for the word of encouragement Abusa. God bless you

  • @abdulrafiquekalembo469
    @abdulrafiquekalembo469 8 месяцев назад

    I always agree with this man.He knows how put sense into people mind.

  • @mchipengule
    @mchipengule 9 месяцев назад +1

    Mau a Mulungu sasankha Malo. God is everywhere!!

  • @FloneyKawina
    @FloneyKawina 8 месяцев назад

    Mbava za kuba MULUNGU awakanthe onse awa fire 🔥🔥🔥🔥 pano tilibe mtendere ndipo zoonadi akayamkhadi

  • @DysonChangantuwa
    @DysonChangantuwa 8 месяцев назад

    To God be glory, ndadalitsika nawo uthengau ndipo wandikhudza

  • @AminaPhiri-pp9tw
    @AminaPhiri-pp9tw 9 месяцев назад

    Amen Abusa awuzeni kwambili ave masozi ya anthu ili pamutu wawo

  • @GiftHlungwane-q5o
    @GiftHlungwane-q5o 7 месяцев назад

    Tadalitsika kwambiri Pastor

  • @YanjananiZybion
    @YanjananiZybion 9 месяцев назад

    More blessings to you pastor

  • @robertrichman9376
    @robertrichman9376 9 месяцев назад +2

    Best place to preach, next time to our Parliament

  • @bensonnkhatatonje6007
    @bensonnkhatatonje6007 8 месяцев назад +1

    Amen

  • @GraciouschfrohLestongama
    @GraciouschfrohLestongama 8 месяцев назад

    Amen man of God 🙏🙏🙏🙏🙏

  • @LimbanChasasaThawi
    @LimbanChasasaThawi 7 месяцев назад

    Amen man of God

  • @e.r.mchanel1460
    @e.r.mchanel1460 8 месяцев назад

    Munasowatu a Rev

  • @PaulMungoma-rs2st
    @PaulMungoma-rs2st 8 месяцев назад

    Amen tadalitsika nawo

  • @JoseevaristoDiriamo
    @JoseevaristoDiriamo 8 месяцев назад

    Ndizoonadi abusa amthu anenewa amati zuza ndi tauzika kudedza mulungu atithandize awakhululukike ambili akulila😢😢

  • @mphatsojosephynyamatawakun3965
    @mphatsojosephynyamatawakun3965 7 месяцев назад +1

    lapan anyamata Inu aku immigration mukuba kwambiri tikamapangitsa ma passport

  • @LinesiKanzota-fw7sj
    @LinesiKanzota-fw7sj 4 месяца назад

    Amen 🙏

  • @abdulrafiquekalembo469
    @abdulrafiquekalembo469 8 месяцев назад +1

    Anthu amenewa uthenga aumve ndithu.Ma past port athu ali mmanja mwa ma Burundi,Ma Nigeria ndi Amwenye pomwe ife anuwake timavutika kuti tipeze passport.

  • @quespeykatame2595
    @quespeykatame2595 9 месяцев назад +1

    Ma uthenga akumveka ndithu 😊

  • @AlliUsuman-mj1mr
    @AlliUsuman-mj1mr 8 месяцев назад +1

    Km musiye kuba anthu inuuu aku immigration

  • @adsonphiri6497
    @adsonphiri6497 8 месяцев назад

    Awa akufunikadi mapemphero,mbava zotheratu

  • @ChikondiLameckPhiri
    @ChikondiLameckPhiri 8 месяцев назад

    Thus Great

  • @WatsonGutah-d1p
    @WatsonGutah-d1p 9 месяцев назад +2

    Zinyengo ameneo zili mitu bibi

  • @ruthnangwale
    @ruthnangwale 8 месяцев назад

    Powerful 🤝

  • @UchiziNyirenda
    @UchiziNyirenda 9 месяцев назад

    Preach on man of God

  • @IdrissaEnock
    @IdrissaEnock 9 месяцев назад +2

    Anthu akatangale opondeleza ngati awa until they change that God has nothing to do with them

  • @amabhohlela.3492
    @amabhohlela.3492 8 месяцев назад

    Abusa next week pitani ku STATE HOUSE,,kwaphulika zimimba kumeneko...

  • @andrewchirwa2193
    @andrewchirwa2193 8 месяцев назад

    mwina angasiyeko chinyengo

  • @PirtekDriver
    @PirtekDriver 9 месяцев назад +1

    Will the corruption stop????

  • @Dan-Buleya
    @Dan-Buleya 9 месяцев назад +1

    Anthu awa eeeeeeh ambuye awayendere

  • @khumbomkorongo4108
    @khumbomkorongo4108 8 месяцев назад

    Powerful

  • @funnychinsalu6198
    @funnychinsalu6198 9 месяцев назад +1

    Kukonda ndalama a immigration

  • @sweeneykamwendo6251
    @sweeneykamwendo6251 9 месяцев назад +1

    Ada awo anadya 100pin yanga...maofesara achinyengo😅

  • @Binamsiska
    @Binamsiska 8 месяцев назад

    Mulungu alemekezeke

  • @mwale1154
    @mwale1154 9 месяцев назад

    Amen 🇿🇲🇿🇲🇿🇲

  • @HarryMakwale
    @HarryMakwale 9 месяцев назад +1

    Mrs luhanga ndakuonani number yanu bwanji

  • @funnychinsalu6198
    @funnychinsalu6198 9 месяцев назад

    Mukayankha pa maso ps mulungu ndalama mutazisiya pansi pano

  • @geoffreykalinda2672
    @geoffreykalinda2672 8 месяцев назад +1

    Apitekoso ku police (road traffic)

  • @MosesMaulana-y5r
    @MosesMaulana-y5r 8 месяцев назад

    Abusa musataye thawi ndi athu amenewo muchedwa nazo, zonsezo ndi mbamva zotheratu,funso nkumati mwasakha bwanji kulalikira office ya athu akubayo Bola munakapita kumamizi kulalikira km naizi Mmmmmm mbamva

  • @masterkachingwe7448
    @masterkachingwe7448 9 месяцев назад +1

    Ma officers chinyengo awa alibzyoli anyenga okha okha mwina kumaalalikira Daily

  • @KarimSydney-d6p
    @KarimSydney-d6p 8 месяцев назад +1

    Abusa zilingati mukulalika palibe coz muli pakati pa nkhosa zosochela😂😂😂

  • @AminaPhiri-pp9tw
    @AminaPhiri-pp9tw 9 месяцев назад +1

    Abusa nthuwa Alape kaye katangale amanyanyila kwambili alape ndithu

  • @amabhohlela.3492
    @amabhohlela.3492 8 месяцев назад

    Mukafikeso ku Ma Court...kuli mamafia kumeneko.

  • @dumisanimoyo3152
    @dumisanimoyo3152 9 месяцев назад +1

    That is a very corrupt ministry in Malawi government plz from there kambiri go to traffic department

  • @josiahgarley3824
    @josiahgarley3824 9 месяцев назад

    Mpaka mmaoffesi?

  • @NgomaRaheem
    @NgomaRaheem 9 месяцев назад

    Athokeni ngamo agalu amenewa akutilangadi passport ya 90pin kudisha 300,pin mulungu awaonedi

  • @numelimtenje5846
    @numelimtenje5846 9 месяцев назад +1

    Mwina angalapeko anthu ozunza awa

  • @amabhohlela.3492
    @amabhohlela.3492 8 месяцев назад +1

    Ingakhale mukuwalakhula choncho,sakumva kanthu ai ndithu"moti enawo angokutukwanani,angoti Galu iwe mumtimamo. tikakudyera kuti.

  • @gesinasutherland9241
    @gesinasutherland9241 9 месяцев назад +1

    komatu simukuwoneka abusa kapena Maliro achepa dera lanu..ulaliki wanu umatitsitsimutsa ndipo umatisintha..kapena 2024 Mwabwera ndi zina..😂😂

    • @rev.alexanderkambiri892
      @rev.alexanderkambiri892  9 месяцев назад +3

      uthenga si waku maliro okha, tili nawo ma videos ambiri koma sitimatha kutumiza kamba ka kuwonongeka kwa zipangizo zathu zogwiritsa ntchito. pang'ono ndi pang'ono tayambapo kuzitolera ndipo Ambuye atithandiza.

  • @victormunthali-l6n
    @victormunthali-l6n 9 месяцев назад +1

    Kumapetoko munakawapemphelela

  • @GraceZgambo-x9j
    @GraceZgambo-x9j 9 месяцев назад +1

    Madalayo wosapanga retire bwanji akapume

  • @amabhohlela.3492
    @amabhohlela.3492 8 месяцев назад

    Pomaliza chopereka abusa,,,

  • @EricBotha-g4t
    @EricBotha-g4t 9 месяцев назад

    Please stop corruption

  • @fahadmilanzi
    @fahadmilanzi 8 месяцев назад

    Ulaliki wabwino aRev gulu lozuza limenelo

  • @YasiduPemba
    @YasiduPemba 8 месяцев назад

    Immigration ya malawi ntchito ya NRB mumaidziwa koma chipangisireni chitupa changa sitinafunsidwepo mpaka pano from 2018 ndimafunsidwa ndikapita Zambia Mozambique Tanzania 😂😢😅😅

  • @EvanceWame-v7v
    @EvanceWame-v7v 9 месяцев назад

    Anthu awa amakhalangati anachoka direct kumwamba kuti azagwire ntchito ku immigration

  • @damianokachingwe3531
    @damianokachingwe3531 8 месяцев назад

    Anthu opanda chisoni amenewa kuteroko lero lomwe lino amubera wina ndalama kulephera kugwira ntchito mwachilungamo too much corruption

  • @clintonhodda9830
    @clintonhodda9830 9 месяцев назад

    Anthu a corruption awa

  • @juliusnjerengo2610
    @juliusnjerengo2610 8 месяцев назад

    Pastor you are preaching to evil people. Ndinakanika ulendo wanga opita ku UK chifukwa cha asatana ameneo.

  • @AlexMwalec
    @AlexMwalec 8 месяцев назад

    Amen

  • @JohnChibanda-h6b
    @JohnChibanda-h6b 9 месяцев назад

    Amen man of GOD

  • @HarryMakwale
    @HarryMakwale 9 месяцев назад

    Amen 🙏 🙏

  • @alexbanda8463
    @alexbanda8463 9 месяцев назад

    Amen ❤

  • @MikeHlongo
    @MikeHlongo 8 месяцев назад

    Amen

  • @mphatsojosephynyamatawakun3965
    @mphatsojosephynyamatawakun3965 7 месяцев назад

    amen

  • @chisomonyerere7197
    @chisomonyerere7197 9 месяцев назад

    Amen

  • @HappyBanda-v6c
    @HappyBanda-v6c 9 месяцев назад

    Amen Amen

  • @gesinasutherland9241
    @gesinasutherland9241 9 месяцев назад

    Amen