Skeffa Chimoto -'' Ine Si wa sataniki'' kuchoka kogulisa zipewa Pano Ndi Billionare

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 19 окт 2024

Комментарии • 86

  • @AminaPhiri-pp9tw
    @AminaPhiri-pp9tw 7 месяцев назад +2

    Asikefa kodi kalata anasiya chinga sipanatuluke zina lanu kumbukilani kalata imeneyi mboni ndi grace chinga anasiya kalata dziko lonse likuziwa ndithu

  • @victorkazembe9631
    @victorkazembe9631 2 года назад +15

    Vuto la ife amalawi munthu akatukuka timayamba kupeka nkhani. Skeffa wavutika pamoyo wake. Pano mulungu wamuona anthu mwayamba kukamba zambili.

  • @ngomajohn1751
    @ngomajohn1751 2 года назад +2

    Watching live & direct from zambia , chipata , kasenegwa district - John Ngoma..skefa chimoto my blessing

  • @asmaljames9323
    @asmaljames9323 2 года назад +7

    Bambo ngati kalankhulidwe kanu mumaganiza kuti ndikachikoka aaaaaiiii ndithu sinthani kalankhulidweko thats my opinion

  • @harrymaganga5977
    @harrymaganga5977 2 года назад +2

    Muthuyu ndi luso lake Koma Muthu akatchuka kapena kulemela anthu amamukamba Koma skeffa usaoke ndithawi yako nyimbo zako Ife dzinatisitha

    • @macdonaldkorea2928
      @macdonaldkorea2928 2 года назад

      Amalawi tili ndi bvuto mchifukwa ambiri tili osauka mpaka panopo komano kusaukaku ndi kwammutu mwathu, tikadzalemera mmutu pamaganizidwe tidzayamba kutukulana tokha tokha like Indians......
      Ukatukuka akuti walowa satanic, ukasauka akuti anasemphanitsa chizimba, umphawi udzatipha kwabasi.....sinthani maganizidwe potero kuti Mulungu atisinthe nafe

    • @AishaChibwana-b8o
      @AishaChibwana-b8o 2 месяца назад

      Koma ife tikulondoloza kalata ya Grace Chinga

  • @RaffiqMahmoud
    @RaffiqMahmoud 3 месяца назад

    Akapusise azibale ako,ngati siiwe WA satanic why uli ndi page ya illuminat pa Facebook?? Wayiwala zomwe umapanga post pa FB zija,mavuto ogulisa zipewadzo ndizomwe zinakupangitsa kut ulowe ma cult opanda pake

  • @agnesssomaliland
    @agnesssomaliland Год назад

    Koma tone ya voice mukanasitha please news zanu sizikubeba zuoneka ngati kukakamiza zithu kumangolakhula voice yanu bwanji😂

  • @kinlosmachemba5046
    @kinlosmachemba5046 2 года назад +1

    Amalawi tidzitha kuyamika mzathu akachita bwino.Uyu ndi mmalawi akuyimba ku malawi akutukula malawi.Chonde tiphunzire kuyamika zimene wina wachita.

  • @rasheedmalunga9212
    @rasheedmalunga9212 Год назад +1

    Watching from UK

  • @sesfikileshop7344
    @sesfikileshop7344 Год назад

    Komatu zoti ndi Billionaire mukumulakwira inde ali ndi kanthu koma zoti ndi Billionaire mukuzitenga kuti? Mu list yama Billionaires m'Malawi muno iyeyo mulibemo

  • @mlezanyirenda2815
    @mlezanyirenda2815 2 года назад +3

    Oyimba ambiri akwathu ose awonongeka ndi usatanic vuto asogoleri nde akakuwuza kut ulowe
    Umarowa u satanic kwathuko sakubisa kharidwe lonyasa

    • @graciousrobertrobert6928
      @graciousrobertrobert6928 2 года назад

      Its true hé is thé satanic one

    • @ipyanamwanyongo4169
      @ipyanamwanyongo4169 2 года назад

      you're speaking the truth my brother all of them Malawian musician alowa usatanic, chifukwa anampha uyimba but we need to pray for Malawi that God most delivered this country from powers of darkness,

    • @christopherbadson699
      @christopherbadson699 2 года назад

      Inu mumati angavomere kuti iye ndi wa satanic?

    • @alexbanda4982
      @alexbanda4982 2 года назад

      Kaya abale Inu

    • @ishmaelchiponda7806
      @ishmaelchiponda7806 2 года назад

      Koma ndinu omvetsa chisoni, satanic kulibeko ku malawi...

  • @EdwardZuze-r7w
    @EdwardZuze-r7w 11 месяцев назад

    Nthawi yotsiliza ino Satana akugwira nthito kwambiri ndi anthu omwe mukuti ndi alusowo, Tamawelengani za kutha kwa nthawi ya pansi pano , komanso mudzisegula ma website ena mudzaseguka m'mitu mwanu, Inenso ndinkamukonda koma zomwe ndinapeza ku ma website ena zinandipangitssa kufuta nyimbo zake zonse komanso si yenkhayo ayi, alipo kagulu moti ena amati ndi a gospel koma akutumikila satana kuseli , inu simukuziwa komanso mwini wakeyo sangavomere ayi. Chomwe mukuona inu ndi nyimbo basi

  • @GraceTandani
    @GraceTandani 7 месяцев назад

    Watching live from United States

  • @cktutorials7998
    @cktutorials7998 2 года назад +1

    Skeffa is a blessing love from Zambia 🇿🇲🇿🇲🇿🇲

  • @RoseMkandawire-e2g
    @RoseMkandawire-e2g 3 месяца назад

    Oyimba ambiri nimasataniki uyuso sikefa nisataniki grace chinga anaurura kare

  • @PhatsoKapheta
    @PhatsoKapheta 9 месяцев назад

    Munipatseko nambar achimoto skef

  • @lastonnthenda2309
    @lastonnthenda2309 Год назад

    I lke that guy n he is so humble from thyolo

  • @dicksonphili3466
    @dicksonphili3466 2 года назад

    Sikefa kaya ndiwa sitac zilibe kanthu ine nyimbo zake zimandisintha

  • @clementbanda1137
    @clementbanda1137 2 года назад

    Watching from Port Elizabeth South Africa,,

  • @MarhaKamowa
    @MarhaKamowa 2 месяца назад

    ndiko lamalawi linachuluka kaduka kwambuli kaduka akuchedwetsani amalawi mulungu amadalitsa kwaolimbikila bwana skeffa ulemu wanu chanu sikanga chanu ndichanu bas

  • @mwayikayuza8164
    @mwayikayuza8164 Год назад

    I like chimoto so much

  • @AmosMalikebu
    @AmosMalikebu Месяц назад

    Amen

  • @blessingsmtambalika358
    @blessingsmtambalika358 2 года назад

    Sikefa chimoto
    Amadidalitsa ndi nyimbozake

  • @ajisonchimombo88
    @ajisonchimombo88 2 года назад +4

    Jealous people always loose

  • @TaitusNyamula-iv2mr
    @TaitusNyamula-iv2mr Год назад

    watching from kenya

  • @EliseuMoffatliver-vn1xg
    @EliseuMoffatliver-vn1xg 8 месяцев назад

    Musatinamizepo apa it's only God who knows everything

  • @miracleeneah5861
    @miracleeneah5861 Год назад

    Palibe chomwe mudziwa inu za skeffa aaaaaaaa dzina lake lenileni ndi joviara moti simuzidzuwaso

  • @miracleeneah5861
    @miracleeneah5861 Год назад

    Komaso alibe Galimoto registered number skeffa 1

  • @ruthtimothy9583
    @ruthtimothy9583 2 года назад

    Watching from Cape town

  • @FinishB
    @FinishB 3 месяца назад

    Zonse aziwa ndi mulungu siyeni muthu

  • @alfredbanda1732
    @alfredbanda1732 2 года назад +2

    Suziwa kumasulila nkhani ataaaa

    • @manuelmakonda2324
      @manuelmakonda2324 2 года назад

      I think better mukanapanga zanu tione, than kuti mukhale wazelu pazomwe wina wachita,

    • @ConcleyManeya
      @ConcleyManeya Год назад

      Osamadana ndi anthu olimbika pogwila ntchito .

  • @kelvinmwasinga1706
    @kelvinmwasinga1706 2 года назад

    Watching from Namibia

  • @Rabeccah-m2q
    @Rabeccah-m2q Год назад

    I like Driemo cfkwa sapanga nao

  • @dorafaartsigns6188
    @dorafaartsigns6188 2 года назад

    Vuto lakwathu kuno ku Malawi timadana ndi wolimbika ndipo wolimbikayo akalemera amampatsa nickname yotchedwa satanic.

  • @alexjeremanuel2541
    @alexjeremanuel2541 2 года назад

    Nthawi zambiri chifukwa cha kulephera kapena kufooka kwa munthu mapeto ake wina amayamba kuda anthu ena posafuna kuvomeredza kulephera kwake

  • @HestingsChapola
    @HestingsChapola 6 месяцев назад

    Ndichifukwa chake amatilimbikisa kwambiri munyimbo zake

  • @ntchindikondowe643
    @ntchindikondowe643 2 года назад

    Amalawi nzanu asachite bwino ndekuti ndi wa satanic inuyo mumayankhula chonchonu mumafuna kusauka mulinakoko ngati ndi wa satanic Inu mukulekelanji kukalowa kuti nanunso mulemele tamango kandani anthu opanda tsogolonu

  • @mwale1154
    @mwale1154 Год назад

    Wa was wa akulu akulu!

  • @benjaminjobo3525
    @benjaminjobo3525 Месяц назад

    Grace chingas letter dont forget you are included there so y are you saying you dont belong to the MARK OF THE BEAST 👹👹👹👹

  • @ericndizeye9490
    @ericndizeye9490 Год назад

    ooohhhh

  • @albertinamartins2593
    @albertinamartins2593 2 года назад +1

    Ndimakukondani achimuene

  • @AlfredbensonaogagmMunthali
    @AlfredbensonaogagmMunthali 7 месяцев назад

    Vuto a Malawi munthu akayiphula amati ndiwa satanic

  • @EliseuMoffatliver-vn1xg
    @EliseuMoffatliver-vn1xg 8 месяцев назад

    A Malawi ambiri mukutiopsa kwambiri mwasintha modabwitsa koma Bible imati mwini nyumba akadadziwa kuti mbala ldza boola nyumba si bwenzi ata gona koma akadadikirira kuti mbala lsa boole 'koma a Malawi mwataya chamoyo mwatola chakufa

  • @Littlefair7
    @Littlefair7 2 года назад +1

    Inu taziyankhulani bwino bwino apa.

  • @b.i.gndunab.i.gnduna7441
    @b.i.gndunab.i.gnduna7441 2 года назад

    Ai ndiwasataniki skefa yo guys

    • @rainfordisaacs6789
      @rainfordisaacs6789 2 года назад

      Muli ndi umboni inuyo?

    • @victormsika1538
      @victormsika1538 11 месяцев назад

      Wasatanic yo ndi iweyo ka. Ukhalilanji ndi nsanje ngt siiwe wa satana. Mfiti yachabechabe

  • @SymonNamalomba-sh3fu
    @SymonNamalomba-sh3fu Год назад

    Sangavomeredze olo ali wasatanik kma akudzuza ndi mulungu ekha basi

  • @masterevanschomora
    @masterevanschomora 2 года назад

    Vuto anthufe sitikufuna kuyesa zinthi kuti tiziwe mataleti athu mara muzati in ineso Wa Sataniki koma tikuyambila apa movutikira 👉aaronnemarere TV watch muone mmene timavutikila kuyamba zinthu

  • @hopekandle6707
    @hopekandle6707 2 года назад +1

    🤣🤣🤣🤣 koma adolo inu nde mmadziwa kulongosola nkhan eti

  • @willsonmzumala
    @willsonmzumala Год назад

    Akutameni

  • @henzomanzo9158
    @henzomanzo9158 2 года назад

    You are the best skeffa not this guys gwambizo fukolo man

  • @dondream5021
    @dondream5021 2 года назад

    🙉🙉🙉🙉

  • @stainmilanzi5293
    @stainmilanzi5293 2 года назад

    Palibe chilipo pamenepo guys

  • @vettasanga3876
    @vettasanga3876 2 года назад

    God bless you mr

  • @NespoliNanganga
    @NespoliNanganga Год назад

    Ndiwe dolo

  • @Adelaidebasera08
    @Adelaidebasera08 Год назад

    Ndi n'daliso wake basi

  • @yamie1
    @yamie1 2 года назад

    Munthu ndi olimbikira uyu

  • @modyanthuachino2074
    @modyanthuachino2074 2 года назад

    Ndi wa satanic uyu luso lake ija anakagulitsa kwa satana pano saimbanso bwino
    Mumuuze mmaso mwake skeffa yo

  • @snetawailiyasa3215
    @snetawailiyasa3215 2 года назад

    watching from jamaica