Akapusise azibale ako,ngati siiwe WA satanic why uli ndi page ya illuminat pa Facebook?? Wayiwala zomwe umapanga post pa FB zija,mavuto ogulisa zipewadzo ndizomwe zinakupangitsa kut ulowe ma cult opanda pake
Komatu zoti ndi Billionaire mukumulakwira inde ali ndi kanthu koma zoti ndi Billionaire mukuzitenga kuti? Mu list yama Billionaires m'Malawi muno iyeyo mulibemo
you're speaking the truth my brother all of them Malawian musician alowa usatanic, chifukwa anampha uyimba but we need to pray for Malawi that God most delivered this country from powers of darkness,
Nthawi yotsiliza ino Satana akugwira nthito kwambiri ndi anthu omwe mukuti ndi alusowo, Tamawelengani za kutha kwa nthawi ya pansi pano , komanso mudzisegula ma website ena mudzaseguka m'mitu mwanu, Inenso ndinkamukonda koma zomwe ndinapeza ku ma website ena zinandipangitssa kufuta nyimbo zake zonse komanso si yenkhayo ayi, alipo kagulu moti ena amati ndi a gospel koma akutumikila satana kuseli , inu simukuziwa komanso mwini wakeyo sangavomere ayi. Chomwe mukuona inu ndi nyimbo basi
A Malawi ambiri mukutiopsa kwambiri mwasintha modabwitsa koma Bible imati mwini nyumba akadadziwa kuti mbala ldza boola nyumba si bwenzi ata gona koma akadadikirira kuti mbala lsa boole 'koma a Malawi mwataya chamoyo mwatola chakufa
Vuto anthufe sitikufuna kuyesa zinthi kuti tiziwe mataleti athu mara muzati in ineso Wa Sataniki koma tikuyambila apa movutikira 👉aaronnemarere TV watch muone mmene timavutikila kuyamba zinthu
Asikefa kodi kalata anasiya chinga sipanatuluke zina lanu kumbukilani kalata imeneyi mboni ndi grace chinga anasiya kalata dziko lonse likuziwa ndithu
Vuto la ife amalawi munthu akatukuka timayamba kupeka nkhani. Skeffa wavutika pamoyo wake. Pano mulungu wamuona anthu mwayamba kukamba zambili.
Inu amalawi sazatheka samafuna kuti. Azawo alemele
Watching live & direct from zambia , chipata , kasenegwa district - John Ngoma..skefa chimoto my blessing
Bambo ngati kalankhulidwe kanu mumaganiza kuti ndikachikoka aaaaaiiii ndithu sinthani kalankhulidweko thats my opinion
Mbuzi ya munthu iyi kkkkk
zowonadi man
Muthuyu ndi luso lake Koma Muthu akatchuka kapena kulemela anthu amamukamba Koma skeffa usaoke ndithawi yako nyimbo zako Ife dzinatisitha
Amalawi tili ndi bvuto mchifukwa ambiri tili osauka mpaka panopo komano kusaukaku ndi kwammutu mwathu, tikadzalemera mmutu pamaganizidwe tidzayamba kutukulana tokha tokha like Indians......
Ukatukuka akuti walowa satanic, ukasauka akuti anasemphanitsa chizimba, umphawi udzatipha kwabasi.....sinthani maganizidwe potero kuti Mulungu atisinthe nafe
Koma ife tikulondoloza kalata ya Grace Chinga
Akapusise azibale ako,ngati siiwe WA satanic why uli ndi page ya illuminat pa Facebook?? Wayiwala zomwe umapanga post pa FB zija,mavuto ogulisa zipewadzo ndizomwe zinakupangitsa kut ulowe ma cult opanda pake
Koma tone ya voice mukanasitha please news zanu sizikubeba zuoneka ngati kukakamiza zithu kumangolakhula voice yanu bwanji😂
Amalawi tidzitha kuyamika mzathu akachita bwino.Uyu ndi mmalawi akuyimba ku malawi akutukula malawi.Chonde tiphunzire kuyamika zimene wina wachita.
Watching from UK
Komatu zoti ndi Billionaire mukumulakwira inde ali ndi kanthu koma zoti ndi Billionaire mukuzitenga kuti? Mu list yama Billionaires m'Malawi muno iyeyo mulibemo
Oyimba ambiri akwathu ose awonongeka ndi usatanic vuto asogoleri nde akakuwuza kut ulowe
Umarowa u satanic kwathuko sakubisa kharidwe lonyasa
Its true hé is thé satanic one
you're speaking the truth my brother all of them Malawian musician alowa usatanic, chifukwa anampha uyimba but we need to pray for Malawi that God most delivered this country from powers of darkness,
Inu mumati angavomere kuti iye ndi wa satanic?
Kaya abale Inu
Koma ndinu omvetsa chisoni, satanic kulibeko ku malawi...
Nthawi yotsiliza ino Satana akugwira nthito kwambiri ndi anthu omwe mukuti ndi alusowo, Tamawelengani za kutha kwa nthawi ya pansi pano , komanso mudzisegula ma website ena mudzaseguka m'mitu mwanu, Inenso ndinkamukonda koma zomwe ndinapeza ku ma website ena zinandipangitssa kufuta nyimbo zake zonse komanso si yenkhayo ayi, alipo kagulu moti ena amati ndi a gospel koma akutumikila satana kuseli , inu simukuziwa komanso mwini wakeyo sangavomere ayi. Chomwe mukuona inu ndi nyimbo basi
Watching live from United States
Skeffa is a blessing love from Zambia 🇿🇲🇿🇲🇿🇲
Oyimba ambiri nimasataniki uyuso sikefa nisataniki grace chinga anaurura kare
Munipatseko nambar achimoto skef
I lke that guy n he is so humble from thyolo
Sikefa kaya ndiwa sitac zilibe kanthu ine nyimbo zake zimandisintha
Watching from Port Elizabeth South Africa,,
ndiko lamalawi linachuluka kaduka kwambuli kaduka akuchedwetsani amalawi mulungu amadalitsa kwaolimbikila bwana skeffa ulemu wanu chanu sikanga chanu ndichanu bas
I like chimoto so much
Amen
Sikefa chimoto
Amadidalitsa ndi nyimbozake
Jealous people always loose
watching from kenya
Musatinamizepo apa it's only God who knows everything
Palibe chomwe mudziwa inu za skeffa aaaaaaaa dzina lake lenileni ndi joviara moti simuzidzuwaso
Komaso alibe Galimoto registered number skeffa 1
Watching from Cape town
Zonse aziwa ndi mulungu siyeni muthu
Suziwa kumasulila nkhani ataaaa
I think better mukanapanga zanu tione, than kuti mukhale wazelu pazomwe wina wachita,
Osamadana ndi anthu olimbika pogwila ntchito .
Watching from Namibia
I like Driemo cfkwa sapanga nao
Vuto lakwathu kuno ku Malawi timadana ndi wolimbika ndipo wolimbikayo akalemera amampatsa nickname yotchedwa satanic.
Nthawi zambiri chifukwa cha kulephera kapena kufooka kwa munthu mapeto ake wina amayamba kuda anthu ena posafuna kuvomeredza kulephera kwake
Ndichifukwa chake amatilimbikisa kwambiri munyimbo zake
Amalawi nzanu asachite bwino ndekuti ndi wa satanic inuyo mumayankhula chonchonu mumafuna kusauka mulinakoko ngati ndi wa satanic Inu mukulekelanji kukalowa kuti nanunso mulemele tamango kandani anthu opanda tsogolonu
Wa was wa akulu akulu!
Grace chingas letter dont forget you are included there so y are you saying you dont belong to the MARK OF THE BEAST 👹👹👹👹
ooohhhh
Ndimakukondani achimuene
Vuto a Malawi munthu akayiphula amati ndiwa satanic
A Malawi ambiri mukutiopsa kwambiri mwasintha modabwitsa koma Bible imati mwini nyumba akadadziwa kuti mbala ldza boola nyumba si bwenzi ata gona koma akadadikirira kuti mbala lsa boole 'koma a Malawi mwataya chamoyo mwatola chakufa
Inu taziyankhulani bwino bwino apa.
Ai ndiwasataniki skefa yo guys
Muli ndi umboni inuyo?
Wasatanic yo ndi iweyo ka. Ukhalilanji ndi nsanje ngt siiwe wa satana. Mfiti yachabechabe
Sangavomeredze olo ali wasatanik kma akudzuza ndi mulungu ekha basi
Vuto anthufe sitikufuna kuyesa zinthi kuti tiziwe mataleti athu mara muzati in ineso Wa Sataniki koma tikuyambila apa movutikira 👉aaronnemarere TV watch muone mmene timavutikila kuyamba zinthu
🤣🤣🤣🤣 koma adolo inu nde mmadziwa kulongosola nkhan eti
Tenho uma ttt
Hie
Akutameni
You are the best skeffa not this guys gwambizo fukolo man
🙉🙉🙉🙉
Palibe chilipo pamenepo guys
God bless you mr
Ndiwe dolo
Ndi n'daliso wake basi
Munthu ndi olimbikira uyu
Ndi wa satanic uyu luso lake ija anakagulitsa kwa satana pano saimbanso bwino
Mumuuze mmaso mwake skeffa yo
Prove it sir
Bring relevant information big,,it seems you know each other
Aliyese ophula pa Malawi paja ndi wa Satanic
Kkkkkkk km nkhan zakeso
Don't judge anyone please musiyileni mulungu yekha
watching from jamaica
Sk
Kodi iwe Hanifa sungamayakhule bwino bwino ine amanditopetsa kwabasi