Комментарии •

  • @DavidJackson-ox4xm
    @DavidJackson-ox4xm 6 дней назад +7

    I support Limpopo FM with Comrade Mtanyiwa God bless you all the time.

  • @simonpaul6567
    @simonpaul6567 6 дней назад +13

    Tangoyankhulai zoona mcp yagosaukisa dziko bisi pa 4 years

  • @TopoTopo-bm4vw
    @TopoTopo-bm4vw 6 дней назад +14

    Tinasiya kuyikhulupilila Times pano ndi Limpopo fm comred m,'tanyiwa more fire m'tanyiwa

    • @user-jk8sh7fh2d
      @user-jk8sh7fh2d 6 дней назад

      Komatu think twice ali ndi mwai kuti samagwidwa , koma atantenga a police kuti akapelereke umboni pa zomwe amayankhula zija apeleke umboni weni weni okhoza kukhumudwa akukana kuti alibe umboni pa zina zimene amayankhula kwa ife zija koma vuto ndilakuti ali ndi mbali ndie zinazi angoyankhulapo mokwiya koma munthu oimilira osauka sakuenela ku khala ndi mbali any government ngati ikuchita bwino mbali zina ayamikile, mbali zina ngati si nachite bwino aneneso, koma kuti timfuse bon kalindo anena kuti boma ili chabwino ya chita ndi chani, akuyankhani kuti ndi zero kufusa alimpopo FM ayankhaso kuti ndi zero. So apa zongooneselatu kuti ali ndi mbali so if you see this guy's akunena chilungamo mbali zonse akugunda eyetu , but sorry umu ndimmeneso ine ndimazionela , koma ndalemekezaso maganizo ako basi.

    • @JohnmarkNazombe-hi9xd
      @JohnmarkNazombe-hi9xd 5 дней назад

      Exactly!!!!

  • @Musa1828-l5d
    @Musa1828-l5d 6 дней назад +11

    MCP zaka 4 zomwe apangako ndikupha Chilima basi fiti zawathu💔💔💔💔💔

  • @TheresaNtodwa
    @TheresaNtodwa 6 дней назад +3

    Azikhale ngati amakanika kuvala bwino okha .angakhale ndinthawi yowasamala apolice .ali bizy kumanga anthu .sakuziwa kuti nthawi yathera angoona ngati adakali chaka choyamba ....APM more fire🔥💪

  • @Geraldmkwewu
    @Geraldmkwewu 6 дней назад +6

    Prgm lzikhara choncho better pangono lero osamabakira zopoyira bomari lachakwera osapanga zinthu ngt mwadyesedwa Bazi atimes yakhulani chilungamo ziko ndilanu plz

  • @mathewsmakina7845
    @mathewsmakina7845 6 дней назад +3

    Ma Tv station apamalawi amapembedza Boma basi ife kuno timamvera Limpopo FM osatizanuzo zomapembedza Bomalo ayi Brian Banda munanchotsa pa Hot current chifukwa samafuna zachinyengo ayi pajatu ndi m,busa weniweni osati ubusawake opha anthu ayi tikufuna Brian Banda abwelere pa hot current tidzayambanso kuikonda TTv

  • @JosephNsona
    @JosephNsona 6 дней назад +3

    Tifunsireniko a wonder ndi apankuku expenditure ya maliro anthu 8 kuphatikizapo amene anali vice president Dr SKC, we are still waiting from Government

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 6 дней назад +1

    Amalawife tinasiya kukumverani kalekale and zimenezo muziziwe from today onwards, inu ndamcp crocodile dance party

  • @ibrahimalfred6539
    @ibrahimalfred6539 6 дней назад +2

    Pempho kwa ayini ake Chanel itchi zingatheke kuti ma program anu special videos kuti muziika full screen not other side pink then videos izikhala pakati I'm saying this because other people's the got small phone please we love your Chanel

  • @SharifMajiga
    @SharifMajiga 5 дней назад

    Times ndiya mcp Anaigula, bakili muluzi tv is the best ❤ ever

  • @InnocentMlowoka-ew4lo
    @InnocentMlowoka-ew4lo 6 дней назад +2

    Minimum wage is nothing with devaluation 80%😂😂😂😂

  • @GraceMaida
    @GraceMaida 6 дней назад +2

    Musawanyengelele agalu amenewa palibe chapanga iwo olo chimodzi koma kupha chilima ndikuba ndalama zamisonkho yathu akagwere afiti amenewo

  • @PetroMatias
    @PetroMatias 6 дней назад +2

    Sakuyankha mofanana ndimafusoo Ali ndimbali mcp palibe chachitika

  • @user-jk8sh7fh2d
    @user-jk8sh7fh2d 6 дней назад

    I'll feel you guys keep it up osamakhala ndi mbali poyankhula, koma awa a MCP -wa zinawavuta zambili why achakwela luso la usogoleri waziko alibe mwina kumpingo analiko mwina coz enafe kunalibeko. Waonekelatu kuti ali ndi nzimu ongopempha basi waubusa-ubusa eeh okama yowonda kale in the name of Jesus ziko sili ngapite pasogolo

  • @alexsumani6823
    @alexsumani6823 6 дней назад +1

    KUSWAKUSWA,kugagadakuhagada 👍

  • @AllunaBenjamin
    @AllunaBenjamin 6 дней назад +1

    Atolakhani times mwakomedwa ndi ndalama

  • @liz9425
    @liz9425 6 дней назад

    Limpopo FM omwe timamvera imatiuuza zoona!!! Inudi aaaa mwanyambititsidwaaaaa

  • @martinsailesi1731
    @martinsailesi1731 6 дней назад

    Kodi masiku 21 wolira atha kale ku boma?

  • @IshmaelNesta-rb8dx
    @IshmaelNesta-rb8dx 6 дней назад +1

    Mau oti ayambapo mumayenera kumayankhula two yrs ago now it's too late kuyamba xitukuko...nthawi Yao yatha kale....soon we are going them OUT

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 6 дней назад

    Musatithelepo bando yathu apaa, ife timamvela limpopo FM with mtanyiwa alongside bakili muluzi tv komanso Borne Kalindo

  • @DalitsoPhiri-sq5nl
    @DalitsoPhiri-sq5nl 6 дней назад +1

    Ndalama Ali busy kumapeleka kuma fumu akapita ku state house komanso kumangolemelesana ku mipandoko yeti mzipala mankhwala akusowa ku emigration zinthu sizikuyendako machine sakupedzeka tinene kuti zeru zilipo pamenepo

  • @ThandiMbewe
    @ThandiMbewe 6 дней назад +1

    Kupepesa kwa chani poti amaziwa chomwe akufuna ndi kupanga, kodi muli mbali iti????

  • @AnaffSayamika-uh6vg
    @AnaffSayamika-uh6vg 6 дней назад +1

    Inu ndizisilu ngt muli nd zilu musiya kupanga ma program chakwela wapanga chani nyani ameney

  • @AmusedDimSum-hd5yp
    @AmusedDimSum-hd5yp 6 дней назад +1

    jona ndi wa mcp uyuakulephera kuya kha

  • @user-qg4it7my9n
    @user-qg4it7my9n 5 дней назад

    kkk hot hot lero ndemwalakhura zanzeru koma 4/10 mwanama amenewo or 2 sanafike ife a pre wo tinatopa nawo

  • @JIMMYWATHONJE
    @JIMMYWATHONJE 6 дней назад

    Hot current wodree umafuna kumenyela a mcp compain

  • @DominicNantowa-t4d
    @DominicNantowa-t4d 6 дней назад

    Nkhani zimenezi ife timazinvesa bwino pa Limpopo FM bakili muludzi TV bon kalindo the DC inu tamalambalalani ndi timambanzi mukumadyato kung'alula kung'alula bas chilungamo chimamasula munthu iya.

  • @sweeneykamwendo6251
    @sweeneykamwendo6251 5 дней назад

    BMTV is the best

  • @Musa1828-l5d
    @Musa1828-l5d 5 дней назад

    Mwadzya ndalama inu musatipusitse ndinu zitsiru za anthu mukubwera so ngati muyakhula za mzeru zili zopusa zokhazokha

  • @paulpaseli6310
    @paulpaseli6310 6 дней назад +1

    Mcp palibe yapanga ky kwa athu odya banzi km kunena chilungamo mowopa mulungu awa zawakanika

  • @user-qn2nu4xs9i
    @user-qn2nu4xs9i 6 дней назад +1

    Kkkkkk....a Zikhale ndi stretegist wa Tonse?? and the score is 4%😅😅😅😅... not 40%.

  • @JuuuKomba
    @JuuuKomba 5 дней назад

    😂zikhale wake uti angaone zamavalidwe

  • @DavidJackson-ox4xm
    @DavidJackson-ox4xm 6 дней назад

    Chakwera must go.

  • @LuciusLungu
    @LuciusLungu 5 дней назад

    Koma ife tilila mpaka 2025 September. Osati 21 dys yanu iyo 😭😭😭😭

  • @user-wl4nd7ic1s
    @user-wl4nd7ic1s 6 дней назад

    Talking guys 💪💪

  • @AronAlfazema
    @AronAlfazema 5 дней назад

    Ndizimvela program ya Banda ? Wander dzakoyo ndi kape ameneyo wa MCP

  • @AllunaBenjamin
    @AllunaBenjamin 6 дней назад +1

    Atolakhani times mwakomedwa ndi ndalama musatitayise nthawi 17:02

  • @KunyengaMoyo
    @KunyengaMoyo 4 дня назад

    Palibe chabwino olo chimodzi hiyaaa osamangoti cyclone anasokonedza ngt anachitapo kanthu

  • @MosesShaibu-ee8hn
    @MosesShaibu-ee8hn 6 дней назад +1

    Andevu zamwayi akupatsani ndalamainu a mcp

  • @ArexBright
    @ArexBright 5 дней назад

    Kunena zoona chakwera chazelu chapanga iye muzaka 4 ndi kupha amalawi bas kugwesa kwacha kuwanamiza ndi kugulisa amalawi ku Israel bas

  • @awardjafar2928
    @awardjafar2928 6 дней назад

    Imagine mene amavalira nachibuluku zikhale ng'oma muja you think angagamgulire wina nsapato

  • @Enock-c9l
    @Enock-c9l 5 дней назад

    Mmmmm kodi nanu mwayamba utabwanji ??

  • @gracemkandawire8769
    @gracemkandawire8769 6 дней назад

    A Brian alikuti tisrkeko apa

  • @user-qn2nu4xs9i
    @user-qn2nu4xs9i 6 дней назад +1

    I repeat..the score is 4% end of story😅😅😅...I do not apologize to anyone..

  • @HalisonSolomon
    @HalisonSolomon 6 дней назад

    Awuzeni kuti azipita asadikire masankho a malawi sitikufunanso kumamva za tonse a liance, palibenso chomwe ayamba nanu musamachite mantha poyankhula , chomwe achita ndi kupha chilima ndi ena komaso kumanga anthu, palibenso chanzeru mukuyankhula mukanangosiya tikufuna anthu osaikira boma kumbuyo iyaaaa

  • @ChikondiAbdul-hk9cd
    @ChikondiAbdul-hk9cd 6 дней назад +1

    Palibe chomwe angapange awoo

  • @SamuelYakobe
    @SamuelYakobe 6 дней назад

    Tamva Kale za inu mmalawi akutulukani ngati anzanu aja.

  • @prophetjacksonmakonda63
    @prophetjacksonmakonda63 6 дней назад

    The coming term they will be a world war 2, they will come with more excuses, let chakwera and his tonse alliance and his administration must go, we dont need chirichonse chokwera mdziko lathu

  • @actuarialscience2283
    @actuarialscience2283 6 дней назад

    Bakili Muluzi TV.

  • @CharlesChipwere
    @CharlesChipwere 5 дней назад

    Palibe chimwe achita away mwina pakuopyseza anthu ndikomwe akwanilitsa kumamanga anthu mudzina lacyber crime

  • @paulpaseli6310
    @paulpaseli6310 6 дней назад +1

    Inu ndi angalu kobas mokanene kuli ufulu wake uti

  • @user-un6qv6sj3h
    @user-un6qv6sj3h 6 дней назад

    Andevu zamwai mkunena zoona kumakhala kunena kwaumphawi

  • @MsondaBanda
    @MsondaBanda 6 дней назад

    Wali kuchitako Mzimba Bridge,

  • @SamuelYakobe
    @SamuelYakobe 6 дней назад

    You're going to loose more customers if you will not caring.

  • @NgongireMwakasungula
    @NgongireMwakasungula 6 дней назад

    Mbuli za dyera inu mukuyankhula za mcp kapena tonse muli Malawi momuno inu mbuli zeni zeni limpompo fm mofaya

  • @vegon357
    @vegon357 6 дней назад

    Dziswe dzimenedzi😢

  • @user-ne7rn4ki3c
    @user-ne7rn4ki3c 5 дней назад

    Apamkuku muli Ku rainbow mumaswa mosaopa NDA Aubrey kusakala koma Ku times mukumaopa chifukwa chani. Amsiska muitaneni kusakala azizaswa

  • @simonpaul6567
    @simonpaul6567 6 дней назад

    Jona ndiwe wa mcp kupepetsa kwa chani

  • @user-hm9nc7lz6e
    @user-hm9nc7lz6e 6 дней назад

    Cakwera canzeru comwe ampanga mudzaka four ndi kupha chilima imfa zosaneneka

  • @Enock-c9l
    @Enock-c9l 5 дней назад

    Mwayamba kulephela kuyamkulatu mukuoneka kuti mwamezatu banzi

  • @DKMWALE-ew3lp
    @DKMWALE-ew3lp 6 дней назад +1

    Lost hope

  • @user-un6qv6sj3h
    @user-un6qv6sj3h 6 дней назад

    0. Pa 10😂😂😂😂 miliri ya chani

  • @user-rl8xs2kf1o
    @user-rl8xs2kf1o 6 дней назад

    Lelotu Bola azimvere okha 😂😂

  • @JonathanChinomba
    @JonathanChinomba 6 дней назад

    Munasiyilanji kwagwanji wakasabola uja lachinayi sanakuopsezani amcp

  • @FelixBoss-yn9pe
    @FelixBoss-yn9pe 6 дней назад

    Nde mwati zikhale chani kkkkk

  • @user-vr5jn8sz5r
    @user-vr5jn8sz5r 6 дней назад

    Bola lelo Times mwakambako zolongosoka.

  • @NelsonMhango-j1d
    @NelsonMhango-j1d 6 дней назад

    Ulemu wanu

  • @user-to5of3ks3g
    @user-to5of3ks3g 6 дней назад +1

    0

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl 6 дней назад

    Iwe pankhuku zonse pa mmalawi wakumudzi zilibe ntchito anthu akufuna azidya katatu wosati zomwe ukunenazo

  • @sparkdymon3429
    @sparkdymon3429 2 дня назад

    Tangonenani zowonga gyz 4 yrs MCP palibe chachitika makape a MCP azipita

  • @AwaliBlack
    @AwaliBlack 6 дней назад

    Mumasiya pati kuzuzula zithu ngati zimenezi muli bho

  • @GodiflyNazombe
    @GodiflyNazombe 6 дней назад

    I lespet blian bamba

  • @mathewsmakina7845
    @mathewsmakina7845 6 дней назад

    Apankuku musakhale ngati chawezi Banda ayi Kodi kwatsalaku misewuyo aimalizakodi chakachimodzichi kapena mwadyanawo ndalama zamagazi zikungogawidwa chisawawazi musaipitse TTv ifetimaikonda mukapitiliza tikutumizani Ku mibawa muzikayamikira limodzi ndi chawezi Banda

  • @ThokohPrescotKalonga
    @ThokohPrescotKalonga 6 дней назад

    Nkhani ndi limpopo fm not ziwanthu ixixi Zoti zidadya kale ndalamazi😡😡

  • @user-to5of3ks3g
    @user-to5of3ks3g 6 дней назад

    Np

  • @mathewsmakina7845
    @mathewsmakina7845 6 дней назад

    pankuku ndi wa Mcp chimwendo mene akumangozela amalawi angamve kupepesako sitingamva ayi musaipitse Tv yanu ayi lankhulani point yachilungamo kuti chakwela ndi Mcp yakeyo alephera basi ine ndikuwapatsa 1/10 osati 4/10 ayi watimzunza ife amalawi kwambiri

  • @HaliJana
    @HaliJana 4 дня назад

    CHAKWERA MMUTUMO OKHA MAMINA 2026 NDIZAMUCHINDA MKAZIWAKO IWEYO UKUONA DIKILA UZAZIWA KUTI KHOBWE SI NYEMBA

  • @user-to5of3ks3g
    @user-to5of3ks3g 6 дней назад

    P
    P

  • @mayomayo-uf9hu
    @mayomayo-uf9hu 6 дней назад

    kkkkk

  • @ThokohPrescotKalonga
    @ThokohPrescotKalonga 6 дней назад

    Nanunso sixoti muziti ayamba, ayamba chani nawe chomwe akupanga ndichani? 😡😡

  • @chimwemwechiundira6002
    @chimwemwechiundira6002 5 дней назад

    Faka moto. Ndanenandanena!

  • @miltonkanyamula9486
    @miltonkanyamula9486 6 дней назад

    Today's hot current has not been realistic.a pankuku akuwoneka kuti ali bias.
    Coz analysis umanene the good and the bad
    But zonse zikuoneka ngati pallibiletu chomwe chachitika.
    Thats not fair l think Rayana chunga is more analytical than a pankuku.and l have missed him.
    Chonde timakukondani but you can do better than zomwe analysis yanu ya lero.

  • @JUMAHSabiti
    @JUMAHSabiti 6 дней назад

    Very useless 😕 😒 😑 ufulu nawo palibe nanu muzinena ndikutha kumanenako chilungamo

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b 6 дней назад

    Koma ndalama zogula anthu ndi zimene zilipo

  • @user-sh5wq4uf6r
    @user-sh5wq4uf6r 6 дней назад

    Mcp siyinabwelele ku zakodza zinthu koma kwao ndi kuba kupha ndikuwononga. anthuwa amadana ndichilungamo ndanena ndanena

  • @GogomphatsoSinosi
    @GogomphatsoSinosi 5 дней назад

    Komano izi amakhala ndi nthawi yomazimvera adindowo kapena tikumanvera ndi kuonera akafa tisiyanji tomwefe