Komatu think twice ali ndi mwai kuti samagwidwa , koma atantenga a police kuti akapelereke umboni pa zomwe amayankhula zija apeleke umboni weni weni okhoza kukhumudwa akukana kuti alibe umboni pa zina zimene amayankhula kwa ife zija koma vuto ndilakuti ali ndi mbali ndie zinazi angoyankhulapo mokwiya koma munthu oimilira osauka sakuenela ku khala ndi mbali any government ngati ikuchita bwino mbali zina ayamikile, mbali zina ngati si nachite bwino aneneso, koma kuti timfuse bon kalindo anena kuti boma ili chabwino ya chita ndi chani, akuyankhani kuti ndi zero kufusa alimpopo FM ayankhaso kuti ndi zero. So apa zongooneselatu kuti ali ndi mbali so if you see this guy's akunena chilungamo mbali zonse akugunda eyetu , but sorry umu ndimmeneso ine ndimazionela , koma ndalemekezaso maganizo ako basi.
Ma Tv station apamalawi amapembedza Boma basi ife kuno timamvera Limpopo FM osatizanuzo zomapembedza Bomalo ayi Brian Banda munanchotsa pa Hot current chifukwa samafuna zachinyengo ayi pajatu ndi m,busa weniweni osati ubusawake opha anthu ayi tikufuna Brian Banda abwelere pa hot current tidzayambanso kuikonda TTv
Tifunsireniko a wonder ndi apankuku expenditure ya maliro anthu 8 kuphatikizapo amene anali vice president Dr SKC, we are still waiting from Government
Pempho kwa ayini ake Chanel itchi zingatheke kuti ma program anu special videos kuti muziika full screen not other side pink then videos izikhala pakati I'm saying this because other people's the got small phone please we love your Chanel
I'll feel you guys keep it up osamakhala ndi mbali poyankhula, koma awa a MCP -wa zinawavuta zambili why achakwela luso la usogoleri waziko alibe mwina kumpingo analiko mwina coz enafe kunalibeko. Waonekelatu kuti ali ndi nzimu ongopempha basi waubusa-ubusa eeh okama yowonda kale in the name of Jesus ziko sili ngapite pasogolo
Ndalama Ali busy kumapeleka kuma fumu akapita ku state house komanso kumangolemelesana ku mipandoko yeti mzipala mankhwala akusowa ku emigration zinthu sizikuyendako machine sakupedzeka tinene kuti zeru zilipo pamenepo
Nkhani zimenezi ife timazinvesa bwino pa Limpopo FM bakili muludzi TV bon kalindo the DC inu tamalambalalani ndi timambanzi mukumadyato kung'alula kung'alula bas chilungamo chimamasula munthu iya.
The coming term they will be a world war 2, they will come with more excuses, let chakwera and his tonse alliance and his administration must go, we dont need chirichonse chokwera mdziko lathu
Today's hot current has not been realistic.a pankuku akuwoneka kuti ali bias. Coz analysis umanene the good and the bad But zonse zikuoneka ngati pallibiletu chomwe chachitika. Thats not fair l think Rayana chunga is more analytical than a pankuku.and l have missed him. Chonde timakukondani but you can do better than zomwe analysis yanu ya lero.
I support Limpopo FM with Comrade Mtanyiwa God bless you all the time.
Tangoyankhulai zoona mcp yagosaukisa dziko bisi pa 4 years
Tinasiya kuyikhulupilila Times pano ndi Limpopo fm comred m,'tanyiwa more fire m'tanyiwa
Komatu think twice ali ndi mwai kuti samagwidwa , koma atantenga a police kuti akapelereke umboni pa zomwe amayankhula zija apeleke umboni weni weni okhoza kukhumudwa akukana kuti alibe umboni pa zina zimene amayankhula kwa ife zija koma vuto ndilakuti ali ndi mbali ndie zinazi angoyankhulapo mokwiya koma munthu oimilira osauka sakuenela ku khala ndi mbali any government ngati ikuchita bwino mbali zina ayamikile, mbali zina ngati si nachite bwino aneneso, koma kuti timfuse bon kalindo anena kuti boma ili chabwino ya chita ndi chani, akuyankhani kuti ndi zero kufusa alimpopo FM ayankhaso kuti ndi zero. So apa zongooneselatu kuti ali ndi mbali so if you see this guy's akunena chilungamo mbali zonse akugunda eyetu , but sorry umu ndimmeneso ine ndimazionela , koma ndalemekezaso maganizo ako basi.
Exactly!!!!
MCP zaka 4 zomwe apangako ndikupha Chilima basi fiti zawathu💔💔💔💔💔
Azikhale ngati amakanika kuvala bwino okha .angakhale ndinthawi yowasamala apolice .ali bizy kumanga anthu .sakuziwa kuti nthawi yathera angoona ngati adakali chaka choyamba ....APM more fire🔥💪
Prgm lzikhara choncho better pangono lero osamabakira zopoyira bomari lachakwera osapanga zinthu ngt mwadyesedwa Bazi atimes yakhulani chilungamo ziko ndilanu plz
Ma Tv station apamalawi amapembedza Boma basi ife kuno timamvera Limpopo FM osatizanuzo zomapembedza Bomalo ayi Brian Banda munanchotsa pa Hot current chifukwa samafuna zachinyengo ayi pajatu ndi m,busa weniweni osati ubusawake opha anthu ayi tikufuna Brian Banda abwelere pa hot current tidzayambanso kuikonda TTv
Tifunsireniko a wonder ndi apankuku expenditure ya maliro anthu 8 kuphatikizapo amene anali vice president Dr SKC, we are still waiting from Government
Amalawife tinasiya kukumverani kalekale and zimenezo muziziwe from today onwards, inu ndamcp crocodile dance party
Pempho kwa ayini ake Chanel itchi zingatheke kuti ma program anu special videos kuti muziika full screen not other side pink then videos izikhala pakati I'm saying this because other people's the got small phone please we love your Chanel
Times ndiya mcp Anaigula, bakili muluzi tv is the best ❤ ever
Minimum wage is nothing with devaluation 80%😂😂😂😂
Musawanyengelele agalu amenewa palibe chapanga iwo olo chimodzi koma kupha chilima ndikuba ndalama zamisonkho yathu akagwere afiti amenewo
Sakuyankha mofanana ndimafusoo Ali ndimbali mcp palibe chachitika
I'll feel you guys keep it up osamakhala ndi mbali poyankhula, koma awa a MCP -wa zinawavuta zambili why achakwela luso la usogoleri waziko alibe mwina kumpingo analiko mwina coz enafe kunalibeko. Waonekelatu kuti ali ndi nzimu ongopempha basi waubusa-ubusa eeh okama yowonda kale in the name of Jesus ziko sili ngapite pasogolo
KUSWAKUSWA,kugagadakuhagada 👍
Kukhapa Kukhapa kkkkkkkkkk.
Atolakhani times mwakomedwa ndi ndalama
Limpopo FM omwe timamvera imatiuuza zoona!!! Inudi aaaa mwanyambititsidwaaaaa
Kodi masiku 21 wolira atha kale ku boma?
Mau oti ayambapo mumayenera kumayankhula two yrs ago now it's too late kuyamba xitukuko...nthawi Yao yatha kale....soon we are going them OUT
Musatithelepo bando yathu apaa, ife timamvela limpopo FM with mtanyiwa alongside bakili muluzi tv komanso Borne Kalindo
Ndalama Ali busy kumapeleka kuma fumu akapita ku state house komanso kumangolemelesana ku mipandoko yeti mzipala mankhwala akusowa ku emigration zinthu sizikuyendako machine sakupedzeka tinene kuti zeru zilipo pamenepo
Kupepesa kwa chani poti amaziwa chomwe akufuna ndi kupanga, kodi muli mbali iti????
Inu ndizisilu ngt muli nd zilu musiya kupanga ma program chakwela wapanga chani nyani ameney
jona ndi wa mcp uyuakulephera kuya kha
kkk hot hot lero ndemwalakhura zanzeru koma 4/10 mwanama amenewo or 2 sanafike ife a pre wo tinatopa nawo
Hot current wodree umafuna kumenyela a mcp compain
Nkhani zimenezi ife timazinvesa bwino pa Limpopo FM bakili muludzi TV bon kalindo the DC inu tamalambalalani ndi timambanzi mukumadyato kung'alula kung'alula bas chilungamo chimamasula munthu iya.
BMTV is the best
Mwadzya ndalama inu musatipusitse ndinu zitsiru za anthu mukubwera so ngati muyakhula za mzeru zili zopusa zokhazokha
Mcp palibe yapanga ky kwa athu odya banzi km kunena chilungamo mowopa mulungu awa zawakanika
Kkkkkk....a Zikhale ndi stretegist wa Tonse?? and the score is 4%😅😅😅😅... not 40%.
😂zikhale wake uti angaone zamavalidwe
Chakwera must go.
Koma ife tilila mpaka 2025 September. Osati 21 dys yanu iyo 😭😭😭😭
Talking guys 💪💪
Ndizimvela program ya Banda ? Wander dzakoyo ndi kape ameneyo wa MCP
Atolakhani times mwakomedwa ndi ndalama musatitayise nthawi 17:02
Palibe chabwino olo chimodzi hiyaaa osamangoti cyclone anasokonedza ngt anachitapo kanthu
Andevu zamwayi akupatsani ndalamainu a mcp
Kunena zoona chakwera chazelu chapanga iye muzaka 4 ndi kupha amalawi bas kugwesa kwacha kuwanamiza ndi kugulisa amalawi ku Israel bas
Imagine mene amavalira nachibuluku zikhale ng'oma muja you think angagamgulire wina nsapato
Mmmmm kodi nanu mwayamba utabwanji ??
A Brian alikuti tisrkeko apa
I repeat..the score is 4% end of story😅😅😅...I do not apologize to anyone..
Awuzeni kuti azipita asadikire masankho a malawi sitikufunanso kumamva za tonse a liance, palibenso chomwe ayamba nanu musamachite mantha poyankhula , chomwe achita ndi kupha chilima ndi ena komaso kumanga anthu, palibenso chanzeru mukuyankhula mukanangosiya tikufuna anthu osaikira boma kumbuyo iyaaaa
Palibe chomwe angapange awoo
Tamva Kale za inu mmalawi akutulukani ngati anzanu aja.
The coming term they will be a world war 2, they will come with more excuses, let chakwera and his tonse alliance and his administration must go, we dont need chirichonse chokwera mdziko lathu
Bakili Muluzi TV.
Palibe chimwe achita away mwina pakuopyseza anthu ndikomwe akwanilitsa kumamanga anthu mudzina lacyber crime
Inu ndi angalu kobas mokanene kuli ufulu wake uti
Andevu zamwai mkunena zoona kumakhala kunena kwaumphawi
Wali kuchitako Mzimba Bridge,
You're going to loose more customers if you will not caring.
Mbuli za dyera inu mukuyankhula za mcp kapena tonse muli Malawi momuno inu mbuli zeni zeni limpompo fm mofaya
Dziswe dzimenedzi😢
Apamkuku muli Ku rainbow mumaswa mosaopa NDA Aubrey kusakala koma Ku times mukumaopa chifukwa chani. Amsiska muitaneni kusakala azizaswa
Jona ndiwe wa mcp kupepetsa kwa chani
Cakwera canzeru comwe ampanga mudzaka four ndi kupha chilima imfa zosaneneka
Mwayamba kulephela kuyamkulatu mukuoneka kuti mwamezatu banzi
Lost hope
0. Pa 10😂😂😂😂 miliri ya chani
Lelotu Bola azimvere okha 😂😂
Munasiyilanji kwagwanji wakasabola uja lachinayi sanakuopsezani amcp
Nde mwati zikhale chani kkkkk
Bola lelo Times mwakambako zolongosoka.
Ulemu wanu
0
Iwe pankhuku zonse pa mmalawi wakumudzi zilibe ntchito anthu akufuna azidya katatu wosati zomwe ukunenazo
Tangonenani zowonga gyz 4 yrs MCP palibe chachitika makape a MCP azipita
Mumasiya pati kuzuzula zithu ngati zimenezi muli bho
I lespet blian bamba
Apankuku musakhale ngati chawezi Banda ayi Kodi kwatsalaku misewuyo aimalizakodi chakachimodzichi kapena mwadyanawo ndalama zamagazi zikungogawidwa chisawawazi musaipitse TTv ifetimaikonda mukapitiliza tikutumizani Ku mibawa muzikayamikira limodzi ndi chawezi Banda
Nkhani ndi limpopo fm not ziwanthu ixixi Zoti zidadya kale ndalamazi😡😡
Np
pankuku ndi wa Mcp chimwendo mene akumangozela amalawi angamve kupepesako sitingamva ayi musaipitse Tv yanu ayi lankhulani point yachilungamo kuti chakwela ndi Mcp yakeyo alephera basi ine ndikuwapatsa 1/10 osati 4/10 ayi watimzunza ife amalawi kwambiri
CHAKWERA MMUTUMO OKHA MAMINA 2026 NDIZAMUCHINDA MKAZIWAKO IWEYO UKUONA DIKILA UZAZIWA KUTI KHOBWE SI NYEMBA
P
P
kkkkk
Nanunso sixoti muziti ayamba, ayamba chani nawe chomwe akupanga ndichani? 😡😡
Faka moto. Ndanenandanena!
Today's hot current has not been realistic.a pankuku akuwoneka kuti ali bias.
Coz analysis umanene the good and the bad
But zonse zikuoneka ngati pallibiletu chomwe chachitika.
Thats not fair l think Rayana chunga is more analytical than a pankuku.and l have missed him.
Chonde timakukondani but you can do better than zomwe analysis yanu ya lero.
Very useless 😕 😒 😑 ufulu nawo palibe nanu muzinena ndikutha kumanenako chilungamo
Koma ndalama zogula anthu ndi zimene zilipo
Mcp siyinabwelele ku zakodza zinthu koma kwao ndi kuba kupha ndikuwononga. anthuwa amadana ndichilungamo ndanena ndanena
Komano izi amakhala ndi nthawi yomazimvera adindowo kapena tikumanvera ndi kuonera akafa tisiyanji tomwefe