Это видео недоступно.
Сожалеем об этом.

BLACK BOX YA NDEGE IJA AKUTI ILI KU STATE HOUSE TAMVANI ZOMWE AKUNENA

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 13 июл 2024

Комментарии • 93

  • @geraldtuwaga-iz6ll
    @geraldtuwaga-iz6ll Месяц назад +10

    😅 Lucifer chakwera , 2025 uzikalamulira ku Maula prison

  • @Mamahashim-xw2bg
    @Mamahashim-xw2bg Месяц назад +7

    Ambuye mulungu wowona zapaziko lapasi ndi kumwamba anthu amenewo awonekere poyera ndithu ayaluke wallah😭😭😭💔

    • @BrownMulipaa
      @BrownMulipaa Месяц назад

      Kkkkkkkk( mbuzi zawanthu amaona ngat abisala

  • @user-pv9uk6sc3w
    @user-pv9uk6sc3w Месяц назад +4

    Fufuzani zonse zibwele poyela, , sakugona Chakwera ndi mizimu , nchifukwa chake wayamba kupemhela lero, wanya.

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y Месяц назад +1

    Chakwela you mast go ❤

  • @shayrafernandeslatif9556
    @shayrafernandeslatif9556 Месяц назад +2

    May the souls rest in peace,tisasiye imfa yawo ulele,Malawi tuyeni timenyele nkhondo ufulu wathu,ngati anzathu AK kenya

  • @AchinaKellz
    @AchinaKellz Месяц назад +6

    chikangawa party kumwamba kuli mulungu ndithu prison woyeeeeeee😂

  • @AnthonyMhango-e9q
    @AnthonyMhango-e9q Месяц назад +1

    Thanks for let us known watching in Cape town Athlon

  • @FloraRonard
    @FloraRonard Месяц назад +2

    Ayi zikomo.Mizimu yawo iwuse ndi mtendere

  • @mariamahamadu8402
    @mariamahamadu8402 Месяц назад +1

    Mulungu malungu mulungu wanga chonde chonde chonde titandidzeni ife

  • @Prekkaq
    @Prekkaq Месяц назад

    God keep on blessing chakwera

  • @SymonNamalomba-sh3fu
    @SymonNamalomba-sh3fu Месяц назад +1

    Chakwera he is very wicked man under the sun

  • @GospelSoldiers-sr7np
    @GospelSoldiers-sr7np Месяц назад +3

    Kumwamba kuli Yehova palibe chobitsika pansi pathambo

  • @user-zh9kb2sj2i
    @user-zh9kb2sj2i Месяц назад +1

    Ambuye mwatisiyila mikango

  • @AnnieKwisanja
    @AnnieKwisanja Месяц назад +3

    Zobisika zonse zizabwela poyera

  • @user-bd5kw8oq1r
    @user-bd5kw8oq1r 29 дней назад

    Zilibwino kuti ili ku state house Ndi kumalo otetezeka kwambili musade nkhawa 😅😅😅😅😂😂

  • @user-px9jd9co3v
    @user-px9jd9co3v 23 дня назад

    By and by, the truth is being uncovered

  • @DevisonHala
    @DevisonHala 25 дней назад

    Manyazi bwaaaa

  • @CharityMkandawire-t8u
    @CharityMkandawire-t8u Месяц назад +1

    Pa dziko lapansi palibe chinsinsi, nd tikulira ndi amalawi ambiri mulungu akumva ma dandaulo athu

  • @AtupeleChitenje
    @AtupeleChitenje Месяц назад +2

    Ambuye ndiwabwino tiyenazoni

  • @KattieKamangirah
    @KattieKamangirah Месяц назад +1

    Ndipo chilungamo chiyende ngati madzi onse amene anatenga gawo pa imfa za anthu amenenewa ambuye awakathe pansi pompano.

  • @user-fd2su4ig1f
    @user-fd2su4ig1f Месяц назад +2

    Saima nawo

  • @MebleNgulinga-hi6rg
    @MebleNgulinga-hi6rg Месяц назад

    Oh my God
    Ambuye achite nanu inu nonse mudampha anthu awaaaa palibe chinsinsi padziko la pansi

  • @Jasper-xk9iv
    @Jasper-xk9iv Месяц назад +3

    Mitima itsika pokhapoka chakeraxo afe basi

  • @DavidJoel-l5q
    @DavidJoel-l5q Месяц назад +2

    Mulungu wabwino masiku omaliza za chinsinsi zizaululika

  • @YasinMusa-ym8lp
    @YasinMusa-ym8lp Месяц назад +2

    Chakwera akafera kundende 2025 aafune asafune simeneso sitekanditu musawonaso zicomo

  • @ChristopherChimbalanga-ez5he
    @ChristopherChimbalanga-ez5he Месяц назад +2

    Ayaluka bas

  • @HoseKatsekera
    @HoseKatsekera Месяц назад

    mulungu ndiwachifundo, ziwululika

  • @elias.m.chunga
    @elias.m.chunga Месяц назад +1

    Koma mbuli zinazi... GPS? Imatanthauza chani mwati?? 😅😂😅😂

  • @user-je8jm5uy1q
    @user-je8jm5uy1q Месяц назад

    Mulungu yekha ndi amene akudziwa koma chilungamo chidziwika

  • @cassimyusuf6683
    @cassimyusuf6683 Месяц назад +1

    Obviously boma la chakwera ndilomwe linapha chilima

  • @IssahAluba
    @IssahAluba Месяц назад

    Uyuyu chakwerayu murandu ukadziwika bwinobwino akuyenera kukhara Ku perisson

  • @Henry-vw2cz
    @Henry-vw2cz Месяц назад

    Wanya basi galu ameneyi chakwela

  • @Prekkaq
    @Prekkaq Месяц назад

    MCP boma tikayivotelabe

  • @user-pv9uk6sc3w
    @user-pv9uk6sc3w Месяц назад +1

    Chakwera sapuma ndi maliro amenewa, adzazimangilila ameneyu.

  • @edsonnyasulu5394
    @edsonnyasulu5394 Месяц назад +1

    Alibe manyazi ayima

  • @lyiemanganjira9708
    @lyiemanganjira9708 Месяц назад

    Kkkkkk sayimanso ndithu

  • @cynthiakananji1608
    @cynthiakananji1608 Месяц назад +4

    Mundege munali zigawenga Ambuye tiyankhulen

    • @eunicesaiti
      @eunicesaiti Месяц назад +1

      😢😢😢😢😢😢😢

    • @philemontitusnkhoma7740
      @philemontitusnkhoma7740 Месяц назад

      Iyeyu adakwera nawo ndegeyo ndi zigawengazo?

    • @philemontitusnkhoma7740
      @philemontitusnkhoma7740 Месяц назад +1

      Inenso ndikuti, Uyu agwidwa posachedwa, pakuti Mulungu adzaulula chilichonse kuphatikiza uyu akudzitcha mboni yu.

    • @cynthiakananji1608
      @cynthiakananji1608 Месяц назад

      @@philemontitusnkhoma7740 angakwere nawo akudziwa kut ndege yo waitchera? Mtsogoleri wathu ndi chigawenga chachikuru. Koma mulungu simunthu. Mzimu wa chilima suzagona mpaka chilombochi chitalangika.. He will never know peace in this world

  • @user-je8jm5uy1q
    @user-je8jm5uy1q Месяц назад

    Apodi ndekt anthu amenewa anali mudege mommo

  • @JasonMailos
    @JasonMailos Месяц назад +1

    Chakwela ndiwakupha

  • @michaelamon9691
    @michaelamon9691 Месяц назад +2

    Koma yaaa, papa muli NDI bodza

    • @petertaulo8014
      @petertaulo8014 Месяц назад +1

      Iwe ndiye kape kwambili, nkhani yoti ilipalipose.

    • @MercyChimaliro-fi6mv
      @MercyChimaliro-fi6mv Месяц назад +1

      Ngati ndi bodza ndiye iweyo tiwuze chilungamo chako.

    • @Jasper-xk9iv
      @Jasper-xk9iv Месяц назад +1

      @@michaelamon9691 iwe macende ako ife zikutiwawatu timufuna chilima

    • @user-eh1mg3ww6d
      @user-eh1mg3ww6d Месяц назад +2

      Muthu uyu amakonda kuikila kumbuyo chakwela thawi zose mungutu adzakulangani kwambili chifukwa ifa zimenezija aliyese m,pakana panopa samavetsetse muyaluka mwasala pang,ono

    • @Musa1828-l5d
      @Musa1828-l5d Месяц назад

      @@petertaulo8014pamtumbo pamako galu iwe, iweyo panga wekha GPS uikepo number ya ndege ija ikupatsa option ya black box nde ufufuze uwone Komwe kuli black box galu iwe

  • @SandreckBezai
    @SandreckBezai Месяц назад

    Iwe ndiopusa udzazindkil okay

  • @FrankSimfukwe-w1s
    @FrankSimfukwe-w1s Месяц назад +2

    Pangani mulimose ife tikufuna zenizeni zibwele poyela

  • @patrickscott9086
    @patrickscott9086 Месяц назад

    Km ndye kuli kuyesesa kut chilungamo chisawoneke km Only God knows

  • @Prekkaq
    @Prekkaq Месяц назад

    😂😂😂 mcp ikukuvetsani kuwawa

    • @user-nv3rf7bl7r
      @user-nv3rf7bl7r Месяц назад

      Ndipo akusehula nayo mumimba 😅😅😅

  • @ChristopherKabanga
    @ChristopherKabanga Месяц назад

    mbuli zazikulu ndinuyo kulongolora kwanuko mukuwapasa mapulani kuti akataye blac box mmadzi kupusa basi kamene mwva kukamwa mbwembwembwe kharani chete afufuze chomwe cili mkati mwa black box

  • @MariamJaffali
    @MariamJaffali Месяц назад

    Ayaluka basi chakwera

    • @user-nv3rf7bl7r
      @user-nv3rf7bl7r Месяц назад

      Kkkk munayamba liti nanu apa nthawi yamalilo mumati poyika chilima chakwera nayeso agone apa kuti mukuwona ngati moyo wachakwera uli mumanja mwanu timvomeleze imfa iliko aliyese adzafa ndindani angamulese mulungu zofuna zake

  • @solomonlapson
    @solomonlapson Месяц назад

    Kodi ndindani ameneyu akulankhulayi,, and channel yake ndi yanji

    • @user-lp8wj3vq4x
      @user-lp8wj3vq4x Месяц назад

      Ukufuna mukamupheso anthu amcp inu. Manyazi bwa

  • @lillynhlema9656
    @lillynhlema9656 Месяц назад

    Ku statehouse yikutqniko

  • @user-mw3kj4qz7b
    @user-mw3kj4qz7b Месяц назад

    Chakwela you're evil evil

  • @BenedictChikaoneka
    @BenedictChikaoneka Месяц назад

    Mudzakhumudwatu report litatchula zosiyana ndimaganizo anu.Chakwera ine Ndikuona kut Ali innocent sure.

    • @user-nv3rf7bl7r
      @user-nv3rf7bl7r Месяц назад

      Ndipo srs akungotekeseka nwini wake aliphee akudziwa choonadi

  • @FrankBaison
    @FrankBaison Месяц назад

    Chakwera amangidwe

  • @LimbikaniChirwa
    @LimbikaniChirwa Месяц назад

    Inu mkususanu kuti ndizonama tatiuzeni black box yilikuti mitumbo yamanu

    • @user-nv3rf7bl7r
      @user-nv3rf7bl7r Месяц назад

      Ubwino wake amako alibe sorry for that 😂

  • @Jerry-vm6mo
    @Jerry-vm6mo Месяц назад

    Guys olo munene zotani mzanu chilima anapita inuyo muli Moyo nde bola mugosiya nkhani Yii coz palibe chomwe chingatike nde musatinyase so chilima anapita basi zikomo

    • @user-nv3rf7bl7r
      @user-nv3rf7bl7r Месяц назад

      Srs ndipo or ayankhule motani kunatha uja basi lasala ndi tsiku lachiukitso ndinthawi yokoza mitima yathu osati mabozawa atichimwisa ulele ndithu anthuwa mumutu mwawo kaya muyenda chani

  • @philemontitusnkhoma7740
    @philemontitusnkhoma7740 Месяц назад

    Galu iwe usaoutsitse a Malawi. Kodi enanu mukungoti ndondondo kwa atolankhani abodza awa moti simudadzukebe kuti uyu angifuna kuononga Malawi? Iweyo umati Achakwera asiye blackbox kuthengo komweko mpaka lero? Amalawi dzukani. Sukusulani. Uyu apezeka posachedwa. Mwana wa mfiti

    • @user-qn9vc8em6z
      @user-qn9vc8em6z Месяц назад

      Kagwere uko akutma et? Tisiye ife ndipo tidakamverabe untill 2025 woooooo ku chonguuuuu

  • @ChrifordBiziel
    @ChrifordBiziel Месяц назад

    Komano minthu akadziwa chilungamo samakhara ndimantha gyz

  • @EdnaChiumia-h4d
    @EdnaChiumia-h4d Месяц назад +2

    Trading Lie's.... Nawe kumwamba sukalowa....let the truth revealed first b4 judging any one

  • @ChrifordBiziel
    @ChrifordBiziel Месяц назад

    Kut gyz social media simunayizolowelembe stt house yakut?

    • @Musa1828-l5d
      @Musa1828-l5d Месяц назад

      Panyopa pako iwe ndi Chakwera wakoyo munyera muona simunati

    • @user-nv3rf7bl7r
      @user-nv3rf7bl7r Месяц назад

      ​@@Musa1828-l5dkkkkk koma ndiye muli srs tuuu nganti amako alibe

  • @user-mh7cc8up4i
    @user-mh7cc8up4i 29 дней назад

    Mulungu alipo ndipo ifa ya chilima ndiathu ena 8 ziziwika kuti anafa bwanji