LIMPOPO FM 20 JUNE 2024NDI COMRADE NTANYIWA CHIGAWO CHAKU MADZULO

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 14 окт 2024

Комментарии • 296

  • @originalblack100
    @originalblack100 3 месяца назад

    Comrade you are the best. Investigative, informative and truth. Tikuyamika boss.

  • @BrandonThomas-le8eb
    @BrandonThomas-le8eb 2 месяца назад

    Ntanyiwa moto moto timakukondani❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤ Allah akupase moyo wautali ichala

  • @EmmanuelGasiten-fo5dr
    @EmmanuelGasiten-fo5dr 3 месяца назад +2

    Kalikonse tikaona. Following from BLK

  • @daviebrasil4480
    @daviebrasil4480 3 месяца назад +3

    Ntchito ilipo ku malawi ndipo yehovah ana muuza kain kuti ndamva kufuula mwazi pomwe pagwera mwazi wamunthu sipanama

  • @DavidJackson-ox4xm
    @DavidJackson-ox4xm 3 месяца назад +1

    The best Radio station in southern Africa.

  • @MebleNgulinga-hi6rg
    @MebleNgulinga-hi6rg 3 месяца назад +1

    Apatu Chilungamo chioneke basi çause its painful mene mwachotsera moyo wanzanu ujaaa so sad so painful 😭😭😭😭😭 Mulungu alowererepo

  • @MorrisMapiri
    @MorrisMapiri 3 месяца назад +1

    God is coming soon to judge this world, this is reminder to everyone who has hunger for power.

  • @EllinaBitto
    @EllinaBitto 3 месяца назад +2

    Everyday ndizikhala pa limpopo fm😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭

  • @CharlesmakveliNyirenda
    @CharlesmakveliNyirenda 3 месяца назад

    Comrade ntanyiwa yhe best always am washing limpompo fm

  • @IsaacMusa-py2jm
    @IsaacMusa-py2jm 3 месяца назад +1

    Loud n clear here Mpumalanga,, big up💪

  • @WinfordGondwe
    @WinfordGondwe 3 месяца назад

    Keep it up please 🙏 you are opening the eyes of the Malawians

  • @twavysibale4751
    @twavysibale4751 3 месяца назад +4

    Koma mtanyiwa becaréful,..dnt trust anyone...we value you bro, you're our eyes,..ena akhoza kumatumidwatu...just be careful,..

  • @BrandonThomas-le8eb
    @BrandonThomas-le8eb 2 месяца назад

    Thanyiwa umakwana mulungu azikusogolera

  • @spargomw
    @spargomw 3 месяца назад +5

    Ntanyiwa🎉🎉🎉🎉🎉 muzibwera kawiri patsiku mokupemphan😂😂😂😂😂

    • @EllinaBitto
      @EllinaBitto 3 месяца назад

      Kawiri patsiku kakuchepa mthanyiwa❣❣❣❣❣❣❣❣❣❣❣❣uzibwera after 2 hours

  • @EllinaBitto
    @EllinaBitto 3 месяца назад

    More fireeeeeeeeeeeeèeeee waiting comrade ❤❤❤❤❤❤❤

  • @Happ2y
    @Happ2y 3 месяца назад +4

    Kkkk kma guys limpopo fm and bakili muluzi TV and Mr born kalindo ndi MA akulu akulu apa malawi ndinu MA big 😂😂

  • @amoschataika7440
    @amoschataika7440 3 месяца назад

    May God protect you all the time Mr Ntanyiwa. Thanks for all your info, big up.

  • @HopesonMkomaula
    @HopesonMkomaula 3 месяца назад

    Limpompo fm you are the great radio master
    I salute you my people

  • @MuhajirAnusa
    @MuhajirAnusa 3 месяца назад

    Chilungamo chinenedwe basi Limpopo Radio station number one the whole Malawi more fire ❤❤❤

  • @Amgwagwa
    @Amgwagwa 3 месяца назад +3

    Kkkkk koma alimpopo umafufuza aiseee😮😮😮

  • @lazarusluciano6916
    @lazarusluciano6916 3 месяца назад +1

    We've been waiting for it❤️🌹

  • @SamukLungu-zg7fl
    @SamukLungu-zg7fl 3 месяца назад +6

    Ngati sinina vere program iyi sindimakhara mosangarara chifukwa nimava zenizeni

  • @UzeChongo
    @UzeChongo 3 месяца назад +2

    Welcome my brother ife chete kuno, ,from south africa De deur

  • @AnaLourencokan
    @AnaLourencokan 2 месяца назад

    Mulungu ..akudalitseni. Antanyiwa

  • @JohnsonMaulana
    @JohnsonMaulana 3 месяца назад +1

    Wathu wathu comrade more 🤜🤙😍💥

  • @BenissoneErnesto-eh6zs
    @BenissoneErnesto-eh6zs 3 месяца назад +2

    Welcome back Limpopo

  • @nellikkmwenda7087
    @nellikkmwenda7087 3 месяца назад +3

    Ulemowanu a limpopo

  • @MiddayDeleza
    @MiddayDeleza 3 месяца назад +2

    Ntanyiwa woyeeeeeeee usadzafe ntanyiwa Mulungu adzangokutengani mlenga mlenga. Ayaluka anthu amenewa. pa dziko lapansi palibe chinsisi Mulungu akukantheni ndithu anthu nonse munapanga chiwembu chimenechi ndipo mizimu ya anthu wonse munawaphawa idzakhala ikukusowetsani mtendere kulikonse mutadzapiteko idzakhala ikukusowetsani mtendere moyo wanu wonse

  • @SymonZemben-gd3ne
    @SymonZemben-gd3ne 3 месяца назад

    More ffffffffiiiiiiiirrrrrrrrreeeeeee🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥 I m behind you Limpopo FM akanganyawa aziwona sanati ana achepa😂😂😂😂😂🤸🤸🤸🤸🐐

  • @AgnessMatchado
    @AgnessMatchado 3 месяца назад +1

    Ntanyiwa usazafe ❤❤❤

  • @TwalikiWisiki
    @TwalikiWisiki 3 месяца назад

    Comrade nyimbo ija yatheka tribute ya a chilima the best tribute ever the most heart ❤️ breaking tribute ever please please send me a link to send this song to now

  • @MussahNamalomba-e3p
    @MussahNamalomba-e3p 3 месяца назад +3

    Likangolowa boma Lina likubwelali limpopo fm izakhale yaboma basi

  • @Fanzo-h2l
    @Fanzo-h2l 3 месяца назад +3

    Komansotu Antanyiwa musamalensotu mwina uyu amutumanso kutiakufufuzeni ngati akufuna kukupatsani imfomationa akufuna kuti akupezeni mosavuta plz brother ife tikudalira inu

    • @cynthiakananji1608
      @cynthiakananji1608 3 месяца назад

      Aaaa uyu sangamupeze akunama awawa amunamiza kanyimbo kakeko angokasunga yekha kapena akapititse Ku zodiac 😂

  • @MustafaAbdullah-pb5zv
    @MustafaAbdullah-pb5zv 3 месяца назад

    Mtanyiwa more fire LiLiLimpopo

  • @KelvinJpchimphepo-sh6nc
    @KelvinJpchimphepo-sh6nc 3 месяца назад

    More fire

  • @MPHATSOKALUWA-lm2uy
    @MPHATSOKALUWA-lm2uy 3 месяца назад

    Zina zmne amanena mind you zmakhla estimated zina Nd zoti zachtka km zina amanena kut tiyembekezere zmnezozo but to say the truth LIMPOPO FM si ya masewera🔥🔥🔥🔥

  • @YasinMusa-ym8lp
    @YasinMusa-ym8lp 3 месяца назад

    Umakwana bwan😊😊

  • @TonyOkoibedi
    @TonyOkoibedi 3 месяца назад +2

    Ndipo live Ntanyiwa tikungodikila kuulutsa mavot tinavota tsiku loikadi chilima M C P inakwililidwadi

  • @PatrickSamu-kp2xf
    @PatrickSamu-kp2xf 3 месяца назад

    Mumatha comrade Mthanyiwa, yomweyo galuiwe,

  • @GospelSoldiers-sr7np
    @GospelSoldiers-sr7np 3 месяца назад +1

    Kkkkk more fire palibe chobitsika pansi pa thambo,kuli Yehova kumwamba sagona kapena kuwodzera

  • @mariamahamadu8402
    @mariamahamadu8402 3 месяца назад +1

    😭😭😭😭😭 nkhani yo mvesa chisoni kwabasi dzowona kukamvotela chakwela nanga taonani Lero Achakwelatu koma Atha anthu kumalawi chigawenga chakumpa ndichilombo

  • @AslamCassim-b7n
    @AslamCassim-b7n 3 месяца назад

    Ipondeni fada inuyo mum antha Abro mtanyiwa more fire❤❤❤❤❤

  • @0wenNkhambule
    @0wenNkhambule 3 месяца назад +2

    Chakwela gwenembe you mast go

  • @BisonJackson
    @BisonJackson 3 месяца назад +2

    Mulungu akutetezeleni anthu Ngati inu mutakhalapo angapo mumalawi muja chakwela mukhoza kumuchotsa 2025 isanakwane mmmn galu aneneyi wawonjeza

  • @StechelectronicsRepair-qh5jl
    @StechelectronicsRepair-qh5jl 3 месяца назад

    ❤❤❤we just waiting for the truth

  • @ChimwemweKondowe-nj4lx
    @ChimwemweKondowe-nj4lx 3 месяца назад

    May God protect you Ntanyiwa together with all good and sound activists

  • @AaronLilexMphangwe
    @AaronLilexMphangwe 2 месяца назад

    A Mtanyiwa munabwera inuyo

  • @SangwaniThika
    @SangwaniThika 3 месяца назад

    Comrade wabwera

  • @DoreenEmmanuelj
    @DoreenEmmanuelj 3 месяца назад

    Ndikamavera waires iyi ndimakhala ndichiyembekezo Kuti Malawi asitha Zikomo ❤

  • @ThokoMakaika-o5u
    @ThokoMakaika-o5u 3 месяца назад +2

    Dzulo mwatiudza za Malunga...lero Manganya...

  • @LangfordMabaso-z7u
    @LangfordMabaso-z7u 3 месяца назад +1

    Padziko lapasi palibe chitsisi chilungamo chiwoneke ayaluka agaluwo

  • @augustinechibbalazi8897
    @augustinechibbalazi8897 3 месяца назад

    Where there is lack of philanthropy and patriotism, cupidity prevails.

  • @AminahMussah
    @AminahMussah 3 месяца назад

    ambuye kumwambako lolan mizimu ya ana anu osalakwa idzimenyele nkhondo patokha sitikwanitsa😭😭😭😭😭😭😭😭

  • @AchinaKellz
    @AchinaKellz 3 месяца назад +1

    Kkkkk yomweyo garu iwe, iponde fadah wina asathawe😂😂😂😂

  • @LeonardMhone-cg1tk
    @LeonardMhone-cg1tk 3 месяца назад +1

    May God guide you Ntanyiwa

  • @LiamTennessee
    @LiamTennessee 3 месяца назад +1

    Comrade inbox me I have a song ready, tribute to Late Chilima the hottest ever

  • @FrancisGama-qb7ze
    @FrancisGama-qb7ze 3 месяца назад +2

    MCP zoti nd chpani chokupha ife tikangonvatu pno takhulupilira ndthu

  • @LiamTennessee
    @LiamTennessee 3 месяца назад +1

    Comrade iam wating for the link to send my music video

    • @clubjunta
      @clubjunta  3 месяца назад

      Send in email now not emoji but video

  • @KhonzoBlose-wq7zm
    @KhonzoBlose-wq7zm 3 месяца назад

    Mumayitha brother Ntanyiwa timakunyadilani

  • @sheila5812
    @sheila5812 3 месяца назад +2

    Ntanyiwa usakhale wapereka number kwa Soldier yo,akumangitsa atha kukumanga mwina watumidwa ameneyo.

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 3 месяца назад +1

    Kafukufuku wamaliro achilima sitikufuna nyau kuti zigwire ntchito imeneyi, tufuna mabungwe oziyimira pawokha komanso mabungwe akunja agwire ntchitoyi, asatana nonse muwonekera ng'amba chaka chake ndichino cha 2024

  • @JafaliAkimu-ll1bf
    @JafaliAkimu-ll1bf 3 месяца назад +2

    chakwera ndichigawenga pamtumbo pa make ndithu

  • @MiddayDeleza
    @MiddayDeleza 3 месяца назад +2

    Koma anthu alibe chisoni munthu anawapangila kampeni kumuphanso, sadik miya anapangila kampeni kumuphanso
    Gwenembe ndithu anapha m, bale wake chisoni ndithu shame

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg 3 месяца назад

    Mr Ntanyiwa ineyo sinditukwana Koma ndi mkwiyo Mr chilima RIP😢😢😢 chakwera chakwera chakwera sikulina udzaona ngelo USANA 12:30😢😢

  • @dumisanihara
    @dumisanihara 3 месяца назад

    Mutanyiwa umakwana, more fire

  • @YasmeenYalabi-b2c
    @YasmeenYalabi-b2c 3 месяца назад

    Kuyenda ndi Limpopo simudzasowanso kumva bodza Lili lonse ikakhile kwa kuyaaaa Comrade Ntanyiwa

  • @MackdBanda
    @MackdBanda 3 месяца назад +1

    Comrade ing'aluliren afiti amenewa ayaluke akakhala chakwelawo diso ngat makilere afune asafune 2025 APM bomaaaa munyanafe agalu inu

  • @StellaCharles-dq8db
    @StellaCharles-dq8db 2 месяца назад

    Km abale inu chakwera mutu ukugwiran kd bwanj angofuna kuchosa miyoyo yanthu chonde bon kalindo samalan kmso mulungu akhale pasogolo panu 😭😭😭😭😭😭😭

  • @HalimaShafie
    @HalimaShafie 3 месяца назад +2

    Yomweyo galu iwe chakwera kukonda ndalama

  • @GiftManuel-er7yh
    @GiftManuel-er7yh 3 месяца назад

    Salute Limpopo fm

  • @AuspiciousKalambula-hp7gj
    @AuspiciousKalambula-hp7gj 3 месяца назад

    Best fm ever🔥🥳

  • @MichaelJannah-hn9qv
    @MichaelJannah-hn9qv 3 месяца назад +2

    Ndipo 2025 yo ikuchedwatu tiwachose anyani amenewa

  • @mustafailanga2585
    @mustafailanga2585 3 месяца назад

    Mkulu mmakwanila ndipo mmatimvesa kukoma kwambili ❤❤❤❤❤❤❤❤

  • @BrandonThomas-le8eb
    @BrandonThomas-le8eb 2 месяца назад

    Inu mumanena chilungamo

  • @dysonfysonchifundo2284
    @dysonfysonchifundo2284 3 месяца назад +1

    More 🔥🔥🔥🔥

  • @DonaldPonda-p2q
    @DonaldPonda-p2q 3 месяца назад +2

    Pansi pathambo palibe chobisika chakwera ndiumbuli wakowo kufuna kukakamira pomwe usakudziwa chilichonse

  • @AchinaKellz
    @AchinaKellz 3 месяца назад +1

    Abakili tidavapo zamilandu yawo koma apa wina azafera ndende ndithu plz akulu akulu ingoziphani kusiyana ndi ukaidi basi😂😂😂😂😅😅😅😅

  • @davidkadyakapita8836
    @davidkadyakapita8836 3 месяца назад

    Respect comrade Mtanyiwa .

  • @BacklinebwanaliBwanali
    @BacklinebwanaliBwanali 3 месяца назад +1

    Zooonad zokhazokha ndipo tikufuna chilungamo chidziwike

  • @DonaldPonda-p2q
    @DonaldPonda-p2q 3 месяца назад +2

    Ndipo mizimu ya anthu 9 amenewa ifinye chakwera

  • @LiamTennessee
    @LiamTennessee 3 месяца назад +2

    Comrade could you please hit my inbox your song is ready

    • @clubjunta
      @clubjunta  3 месяца назад

      +27822885847 tumiza pa WhatsApp

  • @marryphili5419
    @marryphili5419 3 месяца назад +3

    Sikisinja anapha mu bale wake chifukwa cha dyera ng' ona iwe

  • @mirriamwilliam-nq9wg
    @mirriamwilliam-nq9wg 3 месяца назад +2

    Bodza akupanga trace akupeza usapereke #

  • @wayafrank2405
    @wayafrank2405 3 месяца назад +1

    More than BBC ❤

  • @dontreybanda278
    @dontreybanda278 3 месяца назад +1

    More fire ntanyiwa 😂 ndipo ayalukatu

  • @AlgentChilanga
    @AlgentChilanga 3 месяца назад +1

    Chilungamo chiyende ngati madzi amalawi koma comrade ntanyiwa Inu ndi akatundu ndikamavera programuyi ndimasiya zonse kuchita kwanga kumakhala kumvesera .ndiye ndizoona magalimoto a army alowadi muziko lathu 9😞

  • @EllinaBitto
    @EllinaBitto 3 месяца назад

    Mthanyiwa keep it up😭😭😭😭😭😭😭😭😭

  • @ephraimphalawala4720
    @ephraimphalawala4720 3 месяца назад

    Limpopo FM more fire ahhh

  • @Carolynmzonde
    @Carolynmzonde 3 месяца назад +2

    😂😂 Afiti amenewa nawonso aphedwe basi opha mzake naye so aphedwe

  • @DollarChagamba
    @DollarChagamba 3 месяца назад

    ❤❤

  • @JerryNcube-gt3te
    @JerryNcube-gt3te 3 месяца назад

    Limpopo FM plz mwatani Kodi achewa tanyozeka koopswaa lelo shaaaa Koma mumatiimilila

  • @PeterSuwack
    @PeterSuwack 3 месяца назад

    Mumakwana Big man

  • @futurekanjanga1290
    @futurekanjanga1290 3 месяца назад

    Nyimboyi ndaifira hvy

  • @MosesSolomoni
    @MosesSolomoni 3 месяца назад +1

    Ine ndinagona palimpopo kunyumba kwa kalundo and muluzi TV bas

  • @inamrigala
    @inamrigala 3 месяца назад +1

    Ngati chakwela amaziwa kumanga anthu abwele ku Mangochi timugawe awone ifetu ndi ana oyipa kuzindikila kwambili

  • @AnimalproductionandVeterinarys
    @AnimalproductionandVeterinarys 3 месяца назад +2

    Aaaaa wabodza uyu akumatiphulitsa nalo bodza. Dzulo watipatsa dzina lina la vice president

    • @FarookHope
      @FarookHope 3 месяца назад

      iwe usamathe mau wava usamale

  • @sthoramexjrsa902
    @sthoramexjrsa902 3 месяца назад

    I like you mntanyiwa 👍👍👍

  • @yusufbakali
    @yusufbakali 3 месяца назад

    Timadalira inuyo limpopo fm

  • @ZungeniBanet
    @ZungeniBanet 3 месяца назад +3

    Yipase Moto ntanyiwa

  • @LeonardMhone-cg1tk
    @LeonardMhone-cg1tk 3 месяца назад +2

    Nkhanga lero zinasowa😂