Weather they give u money or not but the massage is good to every Malawian, we struggle to get chitukuko in the communities, nde tidziphwanyeso chifukwa cha anthu andale🙄🙄🙄🙄
Nkasa your the best owina anawinadi kale kwinaku anthu angozivutitsa basi, kodi ngati anthu akuononga choncho kuwapasa mpando sazagulitsayi Malawi yense? Nkasa your the best kuononga zinthu sikungapangiseyi kuti awine chisankho Ndipo ulamuliro sumafunayi mphamvu koma nzeru basi. Owina anawina kale
Inu panopa Ndie how do you feel? Munthu Wina wawina Ndie mukukayamba kuphwanya Zinthu Kumeneko ndikukoza or kuononga? You need to think twice before you vommit that nonsense okay
This is really educative and master class keep it up our on Minister wa amphawi umatha zedi koopsa ❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
Nkasa he's Legend ❤❤❤❤❤❤
Nkasa alibe size pa Malawi kumbali ya nyimbo kapena Luso
Tikananvera zamunyimbo iyi ntbawi imeneija panopa Malawi Ali pabwino zinthu zikutchipa Chilima ndi anthu Ena ajaaa alipo komanso Malawi atatukuka koopsa Zedi Komanso njala kulibeko
Song of the month. Very true big up mkasa
Weather they give u money or not but the massage is good to every Malawian, we struggle to get chitukuko in the communities, nde tidziphwanyeso chifukwa cha anthu andale🙄🙄🙄🙄
Owina wawina kale basi 😆😆😆😆 we proud with u mkasa, away from Japan
Nkasa your the best owina anawinadi kale kwinaku anthu angozivutitsa basi, kodi ngati anthu akuononga choncho kuwapasa mpando sazagulitsayi Malawi yense? Nkasa your the best kuononga zinthu sikungapangiseyi kuti awine chisankho Ndipo ulamuliro sumafunayi mphamvu koma nzeru basi. Owina anawina kale
Ndi awa akuononga dzikoli brother Sinanga anachita kulowa mwaupo momgolanda Boma brother
Ndiwebwanabasi lusoulinalo
Very nice song i like it
from cape town ngati tikuphwanyadi misewu ndiye phindu ndichiyani anthu ndiwolemera kale
Ndipo brother wanga Mmmmmm, watching from Capetown too
Zopusa, Nkasa dyera basi. Akawina Chakwera adzaimba yina, angofuna kudya nawo. I know this guy. Am following from Stuttgart, Germany..
Uli kwa Adolf how can you follow what Malawi is going thru... Via Facebook?
Ndiopepera uyu mutayeni yekha akuti Ali Ku Germany simisala imeneyi aaaa
ngati uli pachibwezi akukuomba makofi kodi ungapitirize kumanga naye banja?
Vuto ankasa mulibe mbali mumangoti uku chakoma uko chakoma
Very true mkasa
Mwaonongeranji zitukuko ZANU zomwe?????owina anawina kale bas ndipo yehova kumwamba anasainila kalekale
Amudyesa bazi ameneyo mkasa
From America akunena zoona kuononga dziko lanu lomwe
Malawi ndichoncho
Akunena Chilungamo kaaah Makani anu odana ndi Chilungamowo ndiizi Malawi wathapo Chilima kuphedwa
Mkasa amudyetsa CHIOBAMA UYU, alira pompano awa
Inu panopa Ndie how do you feel? Munthu Wina wawina Ndie mukukayamba kuphwanya Zinthu Kumeneko ndikukoza or kuononga? You need to think twice before you vommit that nonsense okay
Owina awoneka pa 19 osati za tippex
Can you sing this now Mkasa????? Umphawi siwabwino ayi
Zoonadi Phungu wa Osauka
Dada mumantha
Ankasa mwafa nayo 🤣🤣🤣🤣
Mkasa ndi mambala
😂😂😂😂 auze ase
Manzy Magreta 😝😝😝👍
No 1
True
Mphungu Joseph nkhasa Striked again
Kkkkkk
Kkkkkkkkkk nkasa sadzatha basi kkkkkkk
Kkkkk aaaaa
I mean really?
Ine ndikanakhala mkasa nkana deleter video iyi🤣🤣🤣
Galu
Amudyesa mkasa
Owina wawina kale 😅😅😅 Dpp boma basi
Iwe ndichitsiru choopsa ndithu mbuzi ya munthu, suukuonayi m'mene amalawi tikuvutikiramu? Mbuzi
I like the beat but I don't like the message who else agree with me
You don't like to be told the truth even when you are wrong then you got a problem