Ndi chinyengo cha majajinso chinamuika chakwera pa mpando chifukwa popanda majaji chakwera sakanakhala pa mpando amalawi tikuvutika chifukwa cha chinyengo cha majaji
Prezident wathu Dr. Chakwera alibe maganizidwe a tsogolo LA dziko lino posaonetsa mphanvu zakuchita zinthu posatira malamulo oyendetsera dziko lino, komanso ndimunthu yemwe Ali ndi mtima osawerengeta kuti Malawi Ali pansi pa ulamuliro wa democracy, komanso Ali ndi moyo wodelera malamulo oyendetsera dziko lino
Chimwendo Banda kms Puppet wake Chakwera ndi omwe atiwonongera Dziko lanthu labwino bwinoli ( Mulungu akulangeni pansi pompano Mr Chimwendo band a kms iwe Chakwera afiti osekelera)
Nanga amalawi zikuvuta pati? Kunena chilungamo chakwera is a greedy president of all president's in Malawi. Amakomedwa ndi ndalama. That's why he is being used by many business tycoons to turn the country upside down.
Chitsiru china ku Zambia nkumayimba nyimbo kuyamikira Malawi shame 😢
Achakwera alibe mphavu zoposa Chimwendo Banda....Chakwera amawuzidwa zochita😢
Kodi ku Malawi kuno kuli President? Chakwera adakanika kutsogolera mpingo ndiye angakwanitse kutsogolera dziko? Chakwera akumayendera nzeru za Chimwendo Banda
Maiko osiyana mapresidentnso osiyana, wina ochangamuka wina opepela ogwa ndondoli
Zimene zikuchitika kumalawi Kuno kuziganizila zikuwawisa Mutu And chakwera zot ndi Muthu ndakaika
Simungafananize NDI Chakwera akuluwa uyu ngwa nzeru wathuyu alibe nzeru
Chakwera akuopa Chimwendo sangapangei chili Chonse Pano pule ndi Chimwendo 😊
Well done president Hichilema
🎉Mmesa anawasankha ndi Iyeyo alephera bwanji kuwachotsa, zowasankha ngati Alinazo zowacbotsanso Alinazo koma vuto a adyera mbale imodzi
Sangamakane..awa ndi ma real politician
Congratulations 🎊
He knows nothing about administration more especially inthe running of this country,but God is watching panda pusha
Umenewo ndiwo usogoleri kuganizira kuti anthu ambiri asabvutike chifukwa cha anthu ochepa well done apule akuzambia
Kuno acb inatha nthawi ija anagwila mayi chizuma MOTi anthu aku acb akulandila ndalama zaulele. Misonkho yathu kumangowonongeka zovuta kwambiri
Ndi chinyengo cha majajinso chinamuika chakwera pa mpando chifukwa popanda majaji chakwera sakanakhala pa mpando amalawi tikuvutika chifukwa cha chinyengo cha majaji
President Chilema Siwa Chinyengo, Ndichochifulwa wachotsa ma Judge a Chinyengo.
Wathuyu ndi ntchito yake. Sangachotse omwe akumubakira akaba.
Ndiyekuti majajiwo alimbali yaboma zachinyengozo zikukuza boma
Indedi tilibe nsogoleri ife oganiza bwino amaganiza mopelewela ndithu simukunama
Kuno kumalawi aliyese ndiwakuba ndiye amawopa kuyaluka
Good
Zovuta 😢 bolani aneba zawo zikuyenda
Chakwera sangapange zimenezo amamvera chimwendo
Chakwera ndi president opusa ogunata alibe luntha ndi nzeru za utsogoleri. Mulungu amulange galu ameneyi he doesn't deserve to rule this country.
Chakwera sangakwantse kuchosa munthu chifukwa pa anthu omwe akuba mubomamu iyeyo ali pa number 1
Chakwera ndiwachingo mwino ndiye achotsa bwanji ena iye zikunkhuza
Apulezident. Athu. Akuopa. Kuti. Adzawa ulula. Kuti. Nawonso. Ndi skatangale bola. Kungo. Khala. Chete.
Zochita mu dziko lathu utha kutopa ndiwe olankhurawe
Ngat mene ndatopela ine
@@WorriedNdhlovu watopa kodi
Prezident wathu Dr. Chakwera alibe maganizidwe a tsogolo LA dziko lino posaonetsa mphanvu zakuchita zinthu posatira malamulo oyendetsera dziko lino, komanso ndimunthu yemwe Ali ndi mtima osawerengeta kuti Malawi Ali pansi pa ulamuliro wa democracy, komanso Ali ndi moyo wodelera malamulo oyendetsera dziko lino
Ku Zambia achotsa ma Judge pamene ku Malawi akufuna atapha waulula chinyengowo
Chimwendo Banda kms Puppet wake Chakwera ndi omwe atiwonongera Dziko lanthu labwino bwinoli ( Mulungu akulangeni pansi pompano Mr Chimwendo band a kms iwe Chakwera afiti osekelera)
Ndi mbavatu osewo akaba winayo amadyera limodzi
Chakwera akuopa kuikapo mulomo chifukwa akudziwa naye zake ziululika
Chakwera sukuziwa kanthu pa kuyendetsa ziko,ubweleraso ku chipiku azikapakira Nima mu shelfu
Koditu dziko lanthu lamalawi likuyendesedwa ndi anthu amisala onkhaonkha
Hakainde wakhala ku opposition kwa zaka zambiri. Iyi ndi term yake yoyamba koma Ali ndimaganizo otukula dziko lawo. A pule athuwa sangachite manyazi?
Chakwela chomwe amadziwa ndi kuba ndi kupha
Malawi ndi dziko lovetsa chisoni
Always aMalawi mumayamikira zobwera shupit
That unpatriotic man, you sounds to be behind those schemes.
Achakwela ndi achitsiru palibe chimene akuchita chifukwa nayeso ndi wakuba akuopa kuti amuulula ndichifukwa akungokhala duu
Hakainde ali ndi maso mphenya uyuyu chakwera full of curruption its like mulibe president mudziko
Atsogoleri am'zeru okonda dziko lawo,,,,chakwela ndiwakubaso nde zikhoza kum'vuta
Chakwera osafanizila ndi H.H waku Zambia ai. Malawi ndi yopoila kwambiri. Zambia kuli utsogoleri osati ku Malawi.
Mwachakwela mulibe utsogoleli
Khoswe akakala pasuko sapheka
Kuno sizingatheke akuyambisa katangale ndi president yemweyo. Akakhala pakhate sapheka
Iwenso machende ako wasowa zochita kodi pitala wanuyonso nkhalamba ija analephela ma chende amako bussy kumangokhalila ndale basi nchifukwa chake mukudya ziteze agalunu
Kodi president ndi chakwera or chimwendo Malawi kuvusa chisoni neba wathu uyu kuchita chiganizo mwasanga osati disotuzu osachitapo kathu zochita kuoneka kuti uyu ndewaba koma kusakha kukhala chete
Nanga kuno zikhala bwanji?
Pa jatu Ali pamenopo chifukwa chachinyengo
Nanga amalawi zikuvuta pati? Kunena chilungamo chakwera is a greedy president of all president's in Malawi. Amakomedwa ndi ndalama. That's why he is being used by many business tycoons to turn the country upside down.
Iwe unasowatu timawu tachifuwa eee, usanamize amalawi pano ndili konkuno ku zambia. Ma judge omwe awachotsa kuno akuyikila kumbuyo former president ecl kuti ayimenso, osamanamiza a malawi kuno mazambian akuwona kuchedwa 2026 kuti a kulamulayu amuchotse
Watuyu ndichisilu opanda mzelu ndiwa kumidima
Chakwera ndiye mwini Yake wakatangale
Wachinyengo wankulu ndi chakwela
Chikawa aligulumo kubamo
1USD =26000MK
Kuno abaliti
Yes😢😢