Keep it up my brother for standing and show the Nation that Tonse Alliance is usiless Government and let me warn Kumkuyu for playing with the Malawians.
Chitukuko chomwe abwelesa a chakwela kumpoto ndi kumanga kamulepo kaluwa basi osati zinazo bro palibe chomwe angapange let's wait will judge them better pa 2025. Osawopa, osafooka, osatopa.. Big up bro
Mabugwe kunja amapeleka ndalama koma zonse zimabedwa ndi chakwela ndi chifukwa chache anapha zake cholinga azibabe galu amenei zakoma ndalama mbava ndalama anavomeledzana Kale ku parliament zili kuti galu chakwela
Minister of transport Jacob hara akulephera kwawo kumzimba kulibetuu mseu, kumzimba kuliseu unayamba nthawi ya bingu mpaka pano amapangilapo kampeni bas alipheee. Mseu wa mzimba eswatini mzalangwe kudutsa kafukule kufika ekwendeni thakhala tikunamizidwa mpaka pano ma contractor anochoka kalekale. Komaso mavuto onsewa ndi mafumu athu sakutithandiza ai, Pepa mubale wanga zativuta bas miseu ikupangidwa komwe ku Lilongwe northern region zero pa 10
Koditu ngat kumangako akumanga ku Lilongwe kokhako kwawo amanama za msewu wa mangochi makanjira km ndi boza proper gander ikumaveka pa MBC ija kulibeko makanjira road sakumanga
Nduna ndi ma MP akumamupusisa president kumamunamiza kuti zimthu zimuyenda pomwe palibe chikuyenda nduna zones sizimamufunila zabwino president wawo akumunamiza
Kubwele a anyamata ndi atsikana'aku Kenya ngati muli ndi mantha kumeneko.apo,bi.kusa, anyamata ndi atsikana'kumangotibula, aliyese ngati uli pafupi ndi ma office.
Keep it up my brother for standing and show the Nation that Tonse Alliance is usiless Government and let me warn Kumkuyu for playing with the Malawians.
Chitukuko chomwe abwelesa a chakwela kumpoto ndi kumanga kamulepo kaluwa basi osati zinazo bro palibe chomwe angapange let's wait will judge them better pa 2025.
Osawopa, osafooka, osatopa..
Big up bro
Broz kulibe komwe zikuyenda ata! konse kuno mavuto man anthuwa ngakuba mukadzamva wina akuyamikira ameneyo ngo jiya
MCP ndi chakwera akuchoka kale osadandaula, no vote.
Mcp = kuba, kupha ndi kuononga amanga malawi yonse
Mulungu akwaona zonse zoyipa zonse akupanga ku mbuba ya Malawi, ku chokera ku mpoto, pakati ndi ku m'mwera tonse ndi a modzi .😊
Mabugwe kunja amapeleka ndalama koma zonse zimabedwa ndi chakwela ndi chifukwa chache anapha zake cholinga azibabe galu amenei zakoma ndalama mbava ndalama anavomeledzana Kale ku parliament zili kuti galu chakwela
Chakwera Na commit yako yose vimavi vinu Mose masende inu
Inu mukuganiza kuti zinyawu zingamange nsewu malo moti azikazola manyi kudambwe ndiye eeeee
Boma iri ndi manyaka kukanakhala ku Lilongwe bwezi atamanga kale
No voting for chakwela
Yes we don't need to vote for him
Beautiful Bg km utopa mcp ilibe organaisa oionela zachitukuko kulibeko athu azelu iweyo asiye thawiyatha kale ingodikila apm muthalika ndikatundu azakoza zimenezo mosamvuta mcp palibeso chimene amadziwa Akubwela ma drive adpp azaendetsa zonsezo
Shame Bagamoyo chikangawa💔💔💔🙌🙌🙌
Palibe chomwe akuziwa ngakhale reshafu cabinet sakuyiziwa mungobwerera Ku Church basi
Asiyeni amenewo Achakwera ndi Achisiru sangapange chitukuko kumpoto. Boma lawakanika basi
Kulibe komwe akuyamikila Boma la MCP ,ndipo pamenepo ndipang,ono madala Ife kuno ndiye kulibe chimanga
Minister of transport Jacob hara akulephera kwawo kumzimba kulibetuu mseu, kumzimba kuliseu unayamba nthawi ya bingu mpaka pano amapangilapo kampeni bas alipheee. Mseu wa mzimba eswatini mzalangwe kudutsa kafukule kufika ekwendeni thakhala tikunamizidwa mpaka pano ma contractor anochoka kalekale. Komaso mavuto onsewa ndi mafumu athu sakutithandiza ai, Pepa mubale wanga zativuta bas miseu ikupangidwa komwe ku Lilongwe northern region zero pa 10
Osawopa osatopa osafooka
Koditu ngat kumangako akumanga ku Lilongwe kokhako kwawo amanama za msewu wa mangochi makanjira km ndi boza proper gander ikumaveka pa MBC ija kulibeko makanjira road sakumanga
Chakwerayi Eeeeee Ndi nthakati
Nduna ndi ma MP akumamupusisa president kumamunamiza kuti zimthu zimuyenda pomwe palibe chikuyenda nduna zones sizimamufunila zabwino president wawo akumunamiza
Kubwele a anyamata ndi atsikana'aku Kenya ngati muli ndi mantha kumeneko.apo,bi.kusa, anyamata ndi atsikana'kumangotibula, aliyese ngati uli pafupi ndi ma office.
Chakwera no campain kupoto kulibe vote Yako
Amangileni msewu where is the money goes
Chakwera kwake kunatha kale kale yekhanso akudziwa
Ndalama anadya chakwela aboma awa AKUBA ndalama nanga zili kuti
Ndalama anagulira magalimoto
Koma vote nde yinapita mmatope basi kuvotela anthu akubawa
Ndipo ndipo brother mmm
munthu wa mulungu akugula ma Bible tiziwelenga
Chakwerayo ndi mbuzi yamunthu palibe chomwe akupanga
Koma Chakwera guys mmmmmm inu munthuyi amatamba ndithu eeeeeeeeeee ndi mfiti yotheratu Chakwera 😢😢😢
Akumanga kwawo ku lilongwe
Kuyankhula mu chizungu tomato vindele ivi Vili m'boma vambula mahara
Lucy tanditanthauzire pls
mawu abwino kwambili MCP boma lawuchitsiru
That's true
Mu campaign tikuzapha ndi mwala Chakwerayo sure
Keep it up brother good job
Chakwela satana wohipa
😂😂😂😂😂awuzeni inuyo
Mmmmmm mcp
Zoona wayitha
Iiii komatu so sad
Rumphi Rumphi work up
Okuba amenewa
Ndipo ku mpoto asazabwereso
Achakwera akuba ndalama
Chakwela uzikhala konko ku mpoto ndi ku mwela ilibe chako galu tizakuonesa pa kampeni Galu bwako ubele tu
Ndipo koopsa zedi azadziwanso
Namachende chakwera akudya ndalama zamisewu pamozi ndi nyau
Apo pofunika ku matcha basi atule udindo
Ndipo zoonad bro
Zazii
Useless boma
😂😂😂
Nywanamawo
Inuyo mumatamba akulu ndinu mfiti pali zotukwanira munthu apa kungobadwa mokuda mtima basi olo unditukwane sindikusamala km ndinu achitsilu mani.
I think ndalama anadya chatsika
Koma boma ili🤔
A chisilu inu
Chisilu Ndiwe
Mbuziii ya Mano kusi ndiweooohh
Useless government