Это видео недоступно.
Сожалеем об этом.

Kachikenaso Born Kalindo 😂🙌😂😂🙌 pa Chi Sunday 14 July 2024

Поделиться
HTML-код
  • Опубликовано: 13 июл 2024

Комментарии • 85

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b Месяц назад +9

    Ndalama zingowonongedwa anthu angofa mdzipatalamu mankhwala kulibe anthu angofa sisawawa Mulungu akuwoneni mwapaderadera

  • @user-nz7bd7lm4i
    @user-nz7bd7lm4i Месяц назад +8

    Born mulungu azikudalitsa kwambiliiiiiiiiiiii ndipo azikuteteza🙏🙏🙏

  • @MustaphaCassim
    @MustaphaCassim Месяц назад +6

    Chakwera akuwalipira azungu pa ntchito yomwe adagwila pakupha chilima

  • @ExcitedBreakingWaves-oh3zb
    @ExcitedBreakingWaves-oh3zb Месяц назад +5

    Achakwera akuwononga dziko lathu kwambiri.

  • @user-wd9yd1bg9n
    @user-wd9yd1bg9n Месяц назад +4

    Dziko lochitisa manyanzi, nkumati achakwera akugwira ntchito ngati president.

  • @user-fh7sd6gp3f
    @user-fh7sd6gp3f Месяц назад +3

    Tiyamike kubwera kwa tonse Alliance anthu mukung'alula kuti anthu tiziwe zenizeni more 🔥 🔥

  • @officemoyenda-rj2hz
    @officemoyenda-rj2hz Месяц назад +5

    Koma this very very shameful 😢😢😢😢😢

  • @cjaymw496
    @cjaymw496 Месяц назад +1

    Ya balance I think so too😂😂😂

  • @fredsemu7136
    @fredsemu7136 Месяц назад +2

    KOMA CHIKANGAWA ATIPWETEKA NDITHU

  • @MisheckAselo
    @MisheckAselo Месяц назад +3

    Chakwera mchifukwa chake anakapemphera ku CCAP kamutu kataya mission yapheduka, umkaona ngati wapha chilima zako ziziyenda, chilima sanafe akanalipo muona zakuda inu😂

  • @ThokozaniMunkhondia
    @ThokozaniMunkhondia Месяц назад

    A born kalindo,inu ndi mbambande😢😢

  • @edsonnyasulu5394
    @edsonnyasulu5394 Месяц назад

    Koma bon mulungu akuteteze

  • @ClearKondowe-m3j
    @ClearKondowe-m3j 28 дней назад

    Very sorry a Malawi kaya dziko lathu likonzedwa. Yoooo

  • @HappyAbyssinianCat-xt2bm
    @HappyAbyssinianCat-xt2bm Месяц назад

    Mulungu wakiya nawe chakwera waona mulungu wakwiya ndpo mulungu achita nawe iweyo

  • @user-qn2nu4xs9i
    @user-qn2nu4xs9i Месяц назад

    Ati akukonza zinthu!....😅😅😅😅😅😅😅...koma kukonza kunasintha..

  • @ZettaImuranYunusu
    @ZettaImuranYunusu Месяц назад

    Osati Ifeyo Amalawi ai.... But all opposition party's we are with you Trap

  • @user-ik5sz8hc6f
    @user-ik5sz8hc6f Месяц назад

    Ima poyela ndipo aliyense azimva ndithu.Tinasankha satana

  • @crosbeygondwe5403
    @crosbeygondwe5403 Месяц назад +2

    Kung'alulaaaa😂😂😂😂

  • @robertkamtimaleka4394
    @robertkamtimaleka4394 Месяц назад

    a Born Kalindo 42 million yommweyi basi

  • @wonganichakakanyirenda3299
    @wonganichakakanyirenda3299 Месяц назад

    Chakwera iweyooo

  • @user-hh4wn4vf9e
    @user-hh4wn4vf9e Месяц назад

    Auze DC ❤ agaru amenewo

  • @SumanJames
    @SumanJames Месяц назад

    Akalindo sakunama

  • @stevenbanda6665
    @stevenbanda6665 Месяц назад

    Tiuzeni zambiri bwana .kma dziko lathu lomwe kuzunzika

  • @DineoKotjomela
    @DineoKotjomela Месяц назад

    Ma mafia ati😂😂😂

  • @user-oy6dl1pv9e
    @user-oy6dl1pv9e Месяц назад

    The DiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiiCiiiiiiiiiiiiiiiiiiiii

  • @JamesTeacher-b3o
    @JamesTeacher-b3o Месяц назад +1

    Bwana inuyo mmatha kuyankhula ulemu wanu

  • @AufiThera
    @AufiThera Месяц назад

    Wathu wathu born kalindo ✌️🔥 Kung,alula💯💪

  • @HalisonSolomon
    @HalisonSolomon Месяц назад

    KKKKKKKKKK BALANCE KUWAMALIZIRA PANTCHITO YOMWE ANAGWIRA PAKUPHA CHIRIMA NDI ANZAKE SHAME CHAKWERA

  • @user-ck7eb7tb7v
    @user-ck7eb7tb7v Месяц назад

    Munyengo yakung'alula

  • @Mikekajawo-pq9nr
    @Mikekajawo-pq9nr Месяц назад +1

    At we are building Malawi yet ndalama zikutuluka

  • @Musa1828-l5d
    @Musa1828-l5d Месяц назад

    Ndalamq zathu misokho yutha ukupeleka kwazigawenga azipha azibale anthu osalakwa Chakwera sukuwina ase ndakuuza

  • @peternashyo9850
    @peternashyo9850 Месяц назад

    Malawi akulowera kuti abale? Long live the DC

  • @SolomonNjolomole
    @SolomonNjolomole Месяц назад

    The DC ❤❤❤

  • @DineoKotjomela
    @DineoKotjomela Месяц назад

    Ma mafia 😂

  • @Pangolinimw
    @Pangolinimw Месяц назад

    The DC 😅😅😅

  • @user-xx4mt8ox8e
    @user-xx4mt8ox8e Месяц назад

    Mwati ndi Balance?

  • @RitaKainga
    @RitaKainga Месяц назад

    Ulemu wanu the DC

  • @GeoffreyMaulana-rh5rx
    @GeoffreyMaulana-rh5rx Месяц назад +1

    Ng'ona zalusa kufuna kusaulisa Malawi

  • @patrickmacheso5062
    @patrickmacheso5062 Месяц назад

    Mr Bon Kalindo ndinu oyankhuliradi a Malawi tonse, keep it up the DC.

  • @WilliamKawaza
    @WilliamKawaza Месяц назад

    Tell them DC

  • @jamesgama5489
    @jamesgama5489 Месяц назад

    Ayi zikomo

  • @BlessingsMikeyasi
    @BlessingsMikeyasi Месяц назад

    Nazoooo

  • @adzonzicomedy
    @adzonzicomedy Месяц назад +1

    😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b Месяц назад

    Chili chonse chingowululika kumwamba kulandire ulemu

  • @AnnastasiaChakwiya
    @AnnastasiaChakwiya Месяц назад

    Ai zikomo achakwera

  • @Leo-fj6gz
    @Leo-fj6gz Месяц назад

    😢😢😢😢😢

  • @user-rs7vx6hc1k
    @user-rs7vx6hc1k Месяц назад

    Koma what is the use of our currency in Zambia? I don't understand this.

  • @BornfiyesignalSignalmtema
    @BornfiyesignalSignalmtema Месяц назад

    The dc

  • @pempheroraynnoxmpesi8713
    @pempheroraynnoxmpesi8713 Месяц назад

    Ya balance 😢
    RIP SKC

  • @user-bd5kw8oq1r
    @user-bd5kw8oq1r Месяц назад

    Choka iwe mbuli zokhazokha zomwe ziimakunvera iwe gawanani ndlmazo paja ndiyo ntchito yanu 😂😂😂mwayi ndi MCP ukudya bwino kamba ka mabodza akowo azipani akumakulipila 😅😅😅uziyamklika wamva

    • @tingamasi106
      @tingamasi106 Месяц назад +1

      Mbuli ndiwe mavuzi okhwimawo

    • @Dysonkhofi
      @Dysonkhofi Месяц назад +1

      Iwenso ndiwe galu,chitsiru

    • @user-bd5kw8oq1r
      @user-bd5kw8oq1r Месяц назад +1

      @@Dysonkhofi fisi,chule,mbuzi,,bulu munayiwala zimenezo zikomo God bless you 😊😊❤️❤️❤️ work up time is almost finished Jesus Christ is coming soon get ready before we die

    • @ednakaluwa5414
      @ednakaluwa5414 Месяц назад

      ​@@user-bd5kw8oq1rutukwana anzako..opanda chifukwa ena akubwexera utchula dzina la Mulungu shame on you.

    • @ednakaluwa5414
      @ednakaluwa5414 Месяц назад

      Vuto u need attention

  • @JamesAlinafe
    @JamesAlinafe Месяц назад

    Tha DDDDD ccccccccc

  • @katalamajames4947
    @katalamajames4947 Месяц назад

    Koma keni nsonda amadya mutu nkhope the same sekeleton ma R. V.sakugwira nchito

    • @zimmekapachika6784
      @zimmekapachika6784 Месяц назад

      😅😅😅😅😂😂😂mankwala anapima sakugwila 😅😅😅😅😅😂😂😂yomweyo galu iwe

  • @GanieAlidih-gu7no
    @GanieAlidih-gu7no Месяц назад

    Kukuyu nyamayake

  • @user-wd9yd1bg9n
    @user-wd9yd1bg9n Месяц назад

    Komanso chibadwireni ine ntchito ya asilikali athu muno mu malawi sindikuiziwa, chifukwa ngati nkuteteza dziko .bwezi atalipanga boma ili held responsible pa nkhani iyi infact predent akadamuchosa.

  • @user-lc3sw8iz2g
    @user-lc3sw8iz2g Месяц назад

    Balance

  • @AndersonChimwala-hz4so
    @AndersonChimwala-hz4so Месяц назад

    koma amalawi

  • @LiamTennessee
    @LiamTennessee Месяц назад +1

    Amazalandila malipilo a ntchito yomwe adagwila

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl Месяц назад

    Born kalindo 🙏🙏🙏🙏🙏

  • @user-jn7bt1uy5s
    @user-jn7bt1uy5s Месяц назад

    Zovetsa chisoni 😢

  • @JohnConar-kq4hi
    @JohnConar-kq4hi Месяц назад

    The DDDDDDDDDCCCCCCCCCCCC 🤔

  • @kelvinsibande8779
    @kelvinsibande8779 Месяц назад

    The DDDDDCCCCCCC

  • @WilliamBandaWili
    @WilliamBandaWili Месяц назад

    Mmmmm haa?

  • @CharityChikomo-hl1gz
    @CharityChikomo-hl1gz Месяц назад +1

    Ma 20kwachawooo??

  • @chadreckchibwithala1493
    @chadreckchibwithala1493 Месяц назад

    ANTHU PANO MMANGO PANGA MA COMMENT KOPANDA KUSATILA ZINTHU . NDALAMA ZOMWE ZAPEZEKA KU ZAMBIA NDI ZAMAYIKO ANGAPO KUPHATIKIZA MALAWI ANTHU OMWE APEZEKA NAZO NDIZINKA ZA KU RUSSIA OMWE AKUPANGA MA BUSSINES A MA DRUGS OSATI ZOTI BOMA AYI MMM KALINDO ECHI BOZA LENILENI ZINAMIZA ACHILOMWE AKOWO

    • @TysonMwenye
      @TysonMwenye Месяц назад

      Ndiye anthu aku Russia wo angapeze ndi ndalama zathu chifukwa choti akugulitsa ma Drugs? Ifeyo tikamapita ku mayiko akunja timasintha ndalama zadziko lomwe tikupitako.Ndipo tikamaliza business yathuyo tisanatuluke mudzikolo timasinthilatu zamalawi.Ndiye awowo apezeka bwanji ndi ndalama zathu (Mwk) koma kudziko lina chinawakanikitsa kusintha kumalawi konko ndichani ngati ndizachilungamo ndalamazo

    • @tingamasi106
      @tingamasi106 Месяц назад

      Ndalama zama drug mpaka sealed? Iwe ndichimbutumwa wamva

    • @munashemoyo4190
      @munashemoyo4190 Месяц назад

      Kusonyeza kt zomwe zikuchitika dziko muno iwe zikukusangalasa et i uzaziwona ukazakwatila ukasiya kudyesedwako mbudzi yamunthu iwe kape

    • @AmosScott-z9x
      @AmosScott-z9x Месяц назад

      Kape iwe

    • @chadreckchibwithala1493
      @chadreckchibwithala1493 Месяц назад

      mbutuma ndinu osaziwa zinthu alomwe matama basi tiyeni uko .
      mleke kutivuska mngalamuliraso yai chalo ichi jiiiiiiiii peter wanuyo no

  • @user-si8vm5vj8s
    @user-si8vm5vj8s Месяц назад

    Shame on you chakwera

  • @warrenmwambazi8342
    @warrenmwambazi8342 Месяц назад

    Very bad 😊😊😊

  • @FrancoKaunga-rq2ki
    @FrancoKaunga-rq2ki Месяц назад

    Kalindo ndi nyatwa auze zitsiru izi.

  • @DineoKotjomela
    @DineoKotjomela Месяц назад

    Ma mafia 😂