let's all take part in whatever is happening in our country that can develop our country and don't waste time and point fingers at the Government us as Malawians have the ability to develop or put Malawi on the map let's try to find a way to solve our daily problems together we can.
I stand with Ellen the hand over of government from one party to another has been ignored each every party one to implement there own programs throughout the old one how can we go ahead with this spirit
Ndagwilizana ndi fundo yakuti ndarama zimene zikuperekedwa zantukura pakhom ziziperekedwa kamba kakuwapasa athu tcito yakukoza misewu ndizinazotero cz zovuta ndizambili kom ngati mukuwapasa athu ndaram zaurero who is going to fixed our problem please let's think about it
Izizi zinandiphonya ..the first question was "what was wrong with this country kuti zinthu zisamayende bwino?" The answer is simple ...our economy is not stable ,why, the who panel of the cabinet and the president himself don't know nothing about economy azutsogoleri anthu alibe upangiri odziwa kayendetsedwe ka chuma Malawi muno akukanika kuika ndondomeko zoti kodi dzikoli katundu akhale stable asamangikwera every month titani nanga kuti anthu zakudya zipezeke titani
The lady in yellow killed it, very confident and straight
Fredokis this is great initiative, let the youths come together mobilize resources and have more of this conversations
Malawians youths and mum let's gather here ❤❤
Had time to watch eeeh this is What we all need Fredo you're a true leader Ntchana, let's change our Country 🔥🔥
As Malawian we need leader like him ❤❤❤
I wish zinthuzi zitapitilira ngati mademo aja ankati this week Lilongwe the other week Zomba. Nde kaya bwana Fredo mtitelo kaya.🎉🎉
I am beauty James from Dedza malawi but am watching this program in south Africa and l really like your program my brother fredokiss continues this
This is very greatly needed in all cites ndithu 🔥🔥🔥
Nice 👍 fredokiss keep it up of the good work
Thats good development mr Fredo keep it up biggy
Am with you fredo
Big Up Fredokiss
Good conversation
It has to rotate in whole country, so that many views can be heard and build one nation with strong pillar
PHYZIX HAS SAID A POWERFUL STATEMENT
This is beautiful, I like the way it has been given
Great brother fredo keep moving on that vision l hope you will build great Malawi 🇲🇼 am kenneth following in South african
Very good initiave
Honestly Fred has a big vision in Malawi wishing you a big best, keep it up
Good conversation, Fredo wandituma💥📷
let's all take part in whatever is happening in our country that can develop our country and don't waste time and point fingers at
the Government us as Malawians have the ability to develop or put Malawi on the map let's try to find a way to solve our daily problems together we can.
Congratulations pidokis i love this conversation ❤❤
Ambuye ana anu nde ali ndi ukali ndizochitika ku dziko la malawi kuno eeh🙌🏿
Your flowers 🎉🎉 Fredo
This is an important activity, yomwe tikufunika kupanga view as Malawian ,,
This is a good initiative. Nthaw inachepa koma kkkk
This discussion is very important as Malawian let's change our mindset Malawian
One time fizoo🎉🎉🎉
waiting for it in lilongwe
I like this program.... come to Lilongwe Fredo
Good move will be waiting for you in mzuzu bwana fredo❤
Bwana Fredo ulemu wanu. You're a great influence. Tchwe mwana thchwe Jr.
Step by step we get they united.big up🔥🔥🔥🔥
It's my wish kuti utapanga this program in every district kuti enafenso tithe kuika nzeru zanthu I really wish that Fredokiss
Interesting.. .keep it up
A step in the right direction. 🔥
Great conversation
This is great development.
🔥🔥🔥🔥🔥🔥
Ntchana fredo umayesesa big up you really love your country ntchana
Powerful 🔥
Change is here
What a way to go......
Malawi yimafunika asogoleri ngat Fredo umakwana
This should continue so that Malawians maso anthu atsegule.Tidziwona komwe tikupita
I stand with Ellen the hand over of government from one party to another has been ignored each every party one to implement there own programs throughout the old one how can we go ahead with this spirit
Bravo Sir Fredokis!
One time my man 💪
Ndagwilizana ndi fundo yakuti ndarama zimene zikuperekedwa zantukura pakhom ziziperekedwa kamba kakuwapasa athu tcito yakukoza misewu ndizinazotero cz zovuta ndizambili kom ngati mukuwapasa athu ndaram zaurero who is going to fixed our problem please let's think about it
Good conversation from fred
And l have questions what can I do to join this program cz am interested with it
Fredo my Vote 🔥
Thank you. Win or loose these discussions are important. Power to the people. ✊🏾
Ntchana 🔥
Vuto ndi Andale basi katangale wanyanya, Malawi alingati nyumba yopanda fandeshoni remember muluzi anagulitsa makapane aboma.omwe amathandiza kulimba ntchito anthu ambiri two madzi kuno amangoziyendala basi Malo mowagwiretsa ntchito zaulimi zimafunika kwambiri koma ndalama akungoba basi.malawi kuti zithu ziyende ndi zithu zitatu basi zaulemi misewo yabwino makhwala zipatala apezeke.
The conversation that matters
💥💥💥
Dangerous combination 😊
When next will I join you
I believe Fredoh will think about Mangochi, Dzatiyendelen nafe tidzamasuke
Good development❤
Izizi zinandiphonya ..the first question was "what was wrong with this country kuti zinthu zisamayende bwino?" The answer is simple ...our economy is not stable ,why, the who panel of the cabinet and the president himself don't know nothing about economy azutsogoleri anthu alibe upangiri odziwa kayendetsedwe ka chuma Malawi muno akukanika kuika ndondomeko zoti kodi dzikoli katundu akhale stable asamangikwera every month titani nanga kuti anthu zakudya zipezeke titani
Achina Mwayuta , power
Tchana🔥🔥🔥🔥
Kunali boiz yachamba 🎉🎉🎉
Kungopepherela kuti zipitilile ndizithu zabwino kwambili
Adha a jonzie aja osawatola 🔥
Fredokiss iweyo ndi shasha
Mwayiyambayi ndi more....
Mutibweretserenso pajoz pano
Kodi basi zithera Ku Blantyre?? Ma city enawa zifikeso
Fredokiss umakwana
That's my country kuwenge ku tk tok thena Pali ma comments especially ma video yakuvula
Phyzo🔥
Kugawana nzeru mwa nzeru
Zinthuzi zizichitika chitika mzabwino kwambiri
Ngini yabho
hahahahaha koma wandiwaza ndi mdala wamtukula pakhomo,masamu ake anaphunzila kuti?hahahahaha koma conversation inali nyatwa
Clement Kachisi 54:14
Kulilongwe mubwela liti??
Km a host eeeeee
Campeni
Initiative yabwino kwambiri Taphunzilapo zambiri
😂😂chibwe pipo
vuto lalikulu ku Malawi kuno ndi problem......
mayi a yellowa anakonzekatu
Following comments😂
zoonadi inenso ndinalipira mkw500000 koma passport ya ma page 35 komanso kuidikila zaka ziwiri
Malawi ananukha uyu
Time out tonse liar's🤣🤣🤣🤣 2025 mulila kt mfooooooooowooo!!!
kodi health bwanji palibe amakamba zachipatala
dziko lathu pasepezekeso muthu aliyese oyimilaso.2025 dzikoli yangoyenda m.manja mwamakhoba dziko liyenda bwino sindikuchiona chipani chinachilichose chimene chingasithe dziko lathu malawian😂?
Same things being talked over and over again.
Ntchana 🔥