Размер видео: 1280 X 720853 X 480640 X 360
Показать панель управления
Автовоспроизведение
Автоповтор
Zomwe mwachita ndi a mec anuwo taziziwa mai uyu sitikufunaso
Congratulations to the MCP Counselor. We'll meet again in 2025.
Zaziiic see you 2025
Opposition yonse ndiyatulo MCP sitikuyifuna ikutizunza lero mukulola MCP kumawina kudera kwanuko
I wonder why? ngat kuli kubera ma vote, Shem on them wokubawo. ngat zachitika mu chilungamo, Mmmmm dziko Lili mmavuto. ndipo dziko lilipamoto
Anthu akumangochi ndiatulo mmene MCP ikuzunzira anthumu inunso zoona kumavotera MCP? Fertilizer lero alipantengo wanji thumbs la Chimanga liri pantengo wanji zoona kumavotera MCP anthu simuchedwadi kuyiwala
Opposition kungona kwambili,ndipo zikuoneseratu kuti ngakale zisankho za president mcp ikumenyani m'mimba masoanu😮 ali zwiiiii......
Awuzeni asiye zotukwana zija koma ngati ndare zawo ndizomwe zija ayi azaluzaso ndithu chifukwa kutukwana kuja sikukopa anthu koma kuchosa anthu muchipani
Ndale sapangila pa social media...
Mayi awa masiku awo asala pang'ono
Aaa apostion ake zisiru zokhazokha zongo songana bola Yomwe idali 2019 idali yochenjela 😭😭😭😭😭
Ndipo kwambiri chitsilu za anthu
Muzimayi uyu achisedwe ku mec abera chisakho MCP singawine
@@marryphili5419 pitani ku police mukasume kkkkk
Zausilu kumangochi angawine wa mcp
Mangochi yinali kale
Nooo MCP siingawine M'mangochi zosatheka zimenezo
Komatu ya wina ..what is the explanation?
Mpira ndi pa ground osamaka pa social media
Mwabera amcp simungawine kumangochi agaru inu
Kkkkk basi inu kawelengeni achilungamo
Kodi iweyo unakavota naooo
Mukhalira yomweyo yoti tionayo paja tidakuuzani kuti pa u tube sipopangira ndale mukadaluzabe mcp woyeeeèe
Woyeeee❤❤
Dr Chikangawa woyeeee😂😂😂😂😂
Auzeni akuona ngati tonse tingakhale osutsa boma
@@MCAnthonyNdauanthu akupha inu mubera mpaka liti
Zitsiru ndi otsutsa afuna anthu oti si achipani chawo awamenyere nkhondo paokha ayi musamale 2025
Ndipo inu
I like the last part of the interview, that's the truth.Ndiye iweyo WA MCP usapuse nkumaona ngati Mangochi ndiya MCP udzakhumudwa kudzisankho za president and MP
Koma nonse mukuyamikila mcp mutumbo mwanu ndithu mulibe chisoni ziko likiyendelamu
Malawi gradually is getting finished via MCP into dictatorship and zisankho izi opposition phunzilanipo kanthu and wake up Dpp anthu akuvutika.
Chakwela palibe amene akumufuna or madela onse awina bwanji zaugalu
Bread alipakhosi pa anthu amec
All the best cu there
Ukhatsala siwu president guy's
Muzilamulila mpaka kutha kwadziko zaugalu
Nanga poti za unzikazo sizikutulika amene alibe muwataniii?
Tamva alankhula a mec iweso ukuwongezera
Zisiru za anthu mpaka kubera zomwez
Zokomela nawe ukulengezawe amaiako osati amalawi
Zopusa dikirani tione a must 2025
Mai uyu tamuonani bwino ???
Mayi opanda nzeru uyu Mulungu amuone mwapadera
mwabela ndiye mukuthokoza ndani
Atupele ,apm chihana ndi utm onsewu ndi atulo ndipo MCP yabayadi mmimba
Malawians cannot be fooled by mere political rhetoric muzingochedwa nkumatukwana mcp pa social media malawians know what is right
Nde you’ll know what is right ikazangowinansotu 😂. Ngt uli wanzeru you shouldn’t take it lightly
Why ku mec mostly top officials are women?....fishy
Easily used materials
@@montfordkaulesi223exactly. It’s rare to see women who are not moved by anything else but stand for the truth. God bless them
Sitikuyembekezera khansala ife koma president, akhoza kuwina khansala wa mcp koma apm ndikuzatenga boma.
Agalu amnewa afuna atiphese ife lelo mcp yawina chisakho Cha makhasala xmwe ife amalawi sitikugwilixana naxo
Ukati amalawi ineyo undichosemo chifukwa ine ndugwilizana nazo 😂
Kmaso agalu inu a MCP Sizitheka zmeneso mwanya
@@Freedomchennl47 zikuwani ngati agalu achiwewe mukhalila yomweyo tuuu kkk
15:33 15:33 15:33
Iwe ndiwe galu pamodzi ndi makolo ako
Ndi nzimayi so sindikukayika mpang’ono pomwe kuti ngwamabodza
Mwabera agaru inu
Zikuwawani ndipang.ono apa tikumenyani 20205
Mmmmmm malume Poland moto munkhumudawatu paja mumapenhatu wakukhoti
Inutu mzingotukana pa social media azanu akugaya mcp mpaka 2030
Srs atitukwana zawozo azawo akupita chisogolo
@@NancyNyirenda-v9owhatever you saying one day you will be amazing mcp out of the country
Zachitika zimenezo oro mungakwiye motani MCP yawina basi😅😅
Asanyadire makhansala kuti awina adikire next year
Mcp ndiyakuba komaso achakwera anabela kaleso agalu awa
Kupwambwana utsusa boma timing kulephera kukuchenjezani osamva chihana peter atupile nonse agalu zisilu asagolili iwalani zozawinaso
Size makape a opposition ali pheeee
muli kungowawata pasocial media wosavhota ma stuctures paground zipani zanu zilibe muwina bwanji
Zizingatheke kwathu
Mcp moto kutibuuuuu... kkkkkk
Chitsogozo chabwino chikuoneka
Ifetimanziwa kutiawina a m cp basi
😮😮😮😮😮😮😮😮
Awadi ndi anthu opusa kwachenjeza ayi azanong'onedza bondo 2025 mcp izawinanso a chihana apeter atupele mukugona kwambili muchenjele
Ndipo inu A Chilima inuuuuuuuuuuuu😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭
😂😂😂😂😂 zopusa
What i know that Malawian is the people's you won't understand them i know and i believe that the votes mcp and you will see crying what the votes for
Abela inu
Za ziiii
Abale mungovutika mcp singaluze or galu atayamba kugona mnyumba sizingatheke
Mukuzuza amalawi inu a mcp
Abela
Apo àmaba inu munali kuti pitani ku police umbuli bas
Mcp is not on social media kkkkk muzingoziwa zotukwana pa social media azanu akujiya
Chienjelani amalawi mcp mbava zohipa
Mbamva yayikulu ndiweyo paja musogoleli wawo😅😅😅
Kkkkkkklll😂😂😂😂😂
,unatani kukaberako nawe.
Mcp hoyeeeeeee!!!!!!!!
Chakwera oyeeeee
Ku Bela ma vote
Zokonyelela za mcp zopusa
Opusa kwambiri ndi DPP
Khansala si president
vhuto muli kungoyangula pa social media pitani mukavhote
@@lazaruschitsamba8394 eti inu mvutoso amawapopa kwambili ndi anthu oti sali kumalawi 😅
Mcp boma;!!!
Anthu adazindikira kuti pa RUclips ndipa anthu aganyu pomwe ife a mcp ndipa ground ndi zitukuko zomwe anthu akufuna. Tamuonani uyoyo wa ndale pa u tube Masaya ngati changa wagwa nayo ndipo mabwana ake amukwiyira. Zama yazi abwatusa. Mcp moto kuti buuuuu
???????
Futsek
Mcp moto
Dzisankho dzake dzamanyakadzo mcp dzimene yapanga pa Chilima ndindani angayifunenso,mwapatsidwa chibanzi a Mec inu.
Amalawi zoona mukuvoteraso mcp shame mkuyiona njara anthu akufa ni njara zinthu zikudura kwambiri bwanji tivotereko chipani china tioneko kuti zinthu mwina zingasitheko
Congrats to casual wa mcp
MCP moto
Abela Mcp singawine ku mangochi
Ife Tikudikila bakili muluzi 📺 atiuze zenzen
Kkkkk😂😂😂
MCP woooyee
Woyeèeeee❤❤❤
Mbava inu mwadya bazi agalu inu
Zoputsa
??????
Zomwe mwachita ndi a mec anuwo taziziwa mai uyu sitikufunaso
Congratulations to the MCP Counselor. We'll meet again in 2025.
Zaziiic see you 2025
Opposition yonse ndiyatulo MCP sitikuyifuna ikutizunza lero mukulola MCP kumawina kudera kwanuko
I wonder why? ngat kuli kubera ma vote, Shem on them wokubawo. ngat zachitika mu chilungamo, Mmmmm dziko Lili mmavuto. ndipo dziko lilipamoto
Anthu akumangochi ndiatulo mmene MCP ikuzunzira anthumu inunso zoona kumavotera MCP? Fertilizer lero alipantengo wanji thumbs la Chimanga liri pantengo wanji zoona kumavotera MCP anthu simuchedwadi kuyiwala
Opposition kungona kwambili,ndipo zikuoneseratu kuti ngakale zisankho za president mcp ikumenyani m'mimba masoanu😮 ali zwiiiii......
Awuzeni asiye zotukwana zija koma ngati ndare zawo ndizomwe zija ayi azaluzaso ndithu chifukwa kutukwana kuja sikukopa anthu koma kuchosa anthu muchipani
Ndale sapangila pa social media...
Mayi awa masiku awo asala pang'ono
Aaa apostion ake zisiru zokhazokha zongo songana bola Yomwe idali 2019 idali yochenjela 😭😭😭😭😭
Ndipo kwambiri chitsilu za anthu
Muzimayi uyu achisedwe ku mec abera chisakho MCP singawine
@@marryphili5419 pitani ku police mukasume kkkkk
Zausilu kumangochi angawine wa mcp
Mangochi yinali kale
Nooo MCP siingawine M'mangochi zosatheka zimenezo
Komatu ya wina ..what is the explanation?
Mpira ndi pa ground osamaka pa social media
Mwabera amcp simungawine kumangochi agaru inu
Kkkkk basi inu kawelengeni achilungamo
Kodi iweyo unakavota naooo
Mukhalira yomweyo yoti tionayo paja tidakuuzani kuti pa u tube sipopangira ndale mukadaluzabe mcp woyeeeèe
Woyeeee❤❤
Dr Chikangawa woyeeee😂😂😂😂😂
Auzeni akuona ngati tonse tingakhale osutsa boma
@@MCAnthonyNdauanthu akupha inu mubera mpaka liti
Zitsiru ndi otsutsa afuna anthu oti si achipani chawo awamenyere nkhondo paokha ayi musamale 2025
Ndipo inu
I like the last part of the interview, that's the truth.
Ndiye iweyo WA MCP usapuse nkumaona ngati Mangochi ndiya MCP udzakhumudwa kudzisankho za president and MP
Koma nonse mukuyamikila mcp mutumbo mwanu ndithu mulibe chisoni ziko likiyendelamu
Malawi gradually is getting finished via MCP into dictatorship and zisankho izi opposition phunzilanipo kanthu and wake up Dpp anthu akuvutika.
Chakwela palibe amene akumufuna or madela onse awina bwanji zaugalu
Bread alipakhosi pa anthu amec
All the best cu there
Ukhatsala siwu president guy's
Muzilamulila mpaka kutha kwadziko zaugalu
Nanga poti za unzikazo sizikutulika amene alibe muwataniii?
Tamva alankhula a mec iweso ukuwongezera
Zisiru za anthu mpaka kubera zomwez
Zokomela nawe ukulengezawe amaiako osati amalawi
Zopusa dikirani tione a must 2025
Mai uyu tamuonani bwino ???
Mayi opanda nzeru uyu Mulungu amuone mwapadera
mwabela ndiye mukuthokoza ndani
Atupele ,apm chihana ndi utm onsewu ndi atulo ndipo MCP yabayadi mmimba
Malawians cannot be fooled by mere political rhetoric muzingochedwa nkumatukwana mcp pa social media malawians know what is right
Nde you’ll know what is right ikazangowinansotu 😂. Ngt uli wanzeru you shouldn’t take it lightly
Why ku mec mostly top officials are women?....fishy
Easily used materials
@@montfordkaulesi223exactly. It’s rare to see women who are not moved by anything else but stand for the truth. God bless them
Sitikuyembekezera khansala ife koma president, akhoza kuwina khansala wa mcp koma apm ndikuzatenga boma.
Agalu amnewa afuna atiphese ife lelo mcp yawina chisakho Cha makhasala xmwe ife amalawi sitikugwilixana naxo
Ukati amalawi ineyo undichosemo chifukwa ine ndugwilizana nazo 😂
Kmaso agalu inu a MCP Sizitheka zmeneso mwanya
@@Freedomchennl47 zikuwani ngati agalu achiwewe mukhalila yomweyo tuuu kkk
15:33 15:33 15:33
Iwe ndiwe galu pamodzi ndi makolo ako
Ndi nzimayi so sindikukayika mpang’ono pomwe kuti ngwamabodza
Mwabera agaru inu
Zikuwawani ndipang.ono apa tikumenyani 20205
Mmmmmm malume Poland moto munkhumudawatu paja mumapenhatu wakukhoti
Inutu mzingotukana pa social media azanu akugaya mcp mpaka 2030
Srs atitukwana zawozo azawo akupita chisogolo
@@NancyNyirenda-v9owhatever you saying one day you will be amazing mcp out of the country
Zachitika zimenezo oro mungakwiye motani MCP yawina basi😅😅
Asanyadire makhansala kuti awina adikire next year
Mcp ndiyakuba komaso achakwera anabela kaleso agalu awa
Kupwambwana utsusa boma timing kulephera kukuchenjezani osamva chihana peter atupile nonse agalu zisilu asagolili iwalani zozawinaso
Size makape a opposition ali pheeee
muli kungowawata pasocial media wosavhota ma stuctures paground zipani zanu zilibe muwina bwanji
Zizingatheke kwathu
Mcp moto kutibuuuuu... kkkkkk
Chitsogozo chabwino chikuoneka
Ifetimanziwa kutiawina a m cp basi
😮😮😮😮😮😮😮😮
Awadi ndi anthu opusa kwachenjeza ayi azanong'onedza bondo 2025 mcp izawinanso a chihana apeter atupele mukugona kwambili muchenjele
Ndipo inu A Chilima inuuuuuuuuuuuu😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭
😂😂😂😂😂 zopusa
What i know that Malawian is the people's you won't understand them i know and i believe that the votes mcp and you will see crying what the votes for
Abela inu
Za ziiii
Abale mungovutika mcp singaluze or galu atayamba kugona mnyumba sizingatheke
Mukuzuza amalawi inu a mcp
Abela
Apo àmaba inu munali kuti pitani ku police umbuli bas
Mcp is not on social media kkkkk muzingoziwa zotukwana pa social media azanu akujiya
Chienjelani amalawi mcp mbava zohipa
Mbamva yayikulu ndiweyo paja musogoleli wawo😅😅😅
Kkkkkkklll😂😂😂😂😂
,unatani kukaberako nawe.
Mcp hoyeeeeeee!!!!!!!!
Chakwera oyeeeee
Ku Bela ma vote
Zokonyelela za mcp zopusa
Opusa kwambiri ndi DPP
Khansala si president
vhuto muli kungoyangula pa social media pitani mukavhote
@@lazaruschitsamba8394 eti inu mvutoso amawapopa kwambili ndi anthu oti sali kumalawi 😅
Mcp boma;!!!
Anthu adazindikira kuti pa RUclips ndipa anthu aganyu pomwe ife a mcp ndipa ground ndi zitukuko zomwe anthu akufuna. Tamuonani uyoyo wa ndale pa u tube Masaya ngati changa wagwa nayo ndipo mabwana ake amukwiyira. Zama yazi abwatusa. Mcp moto kuti buuuuu
???????
Futsek
Mcp moto
Dzisankho dzake dzamanyakadzo mcp dzimene yapanga pa Chilima ndindani angayifunenso,mwapatsidwa chibanzi a Mec inu.
Amalawi zoona mukuvoteraso mcp shame mkuyiona njara anthu akufa ni njara zinthu zikudura kwambiri bwanji tivotereko chipani china tioneko kuti zinthu mwina zingasitheko
Congrats to casual wa mcp
MCP moto
Abela Mcp singawine ku mangochi
Ife Tikudikila bakili muluzi 📺 atiuze zenzen
Kkkkk😂😂😂
MCP woooyee
Woyeèeeee❤❤❤
Dr Chikangawa woyeeee😂😂😂😂😂
Mbava inu mwadya bazi agalu inu
Zoputsa
Opposition yonse ndiyatulo MCP sitikuyifuna ikutizunza lero mukulola MCP kumawina kudera kwanuko
15:33 15:33 15:33
??????
Opposition yonse ndiyatulo MCP sitikuyifuna ikutizunza lero mukulola MCP kumawina kudera kwanuko