- Видео 123
- Просмотров 633 416
MALAWI WATHU
Великобритания
Добавлен 27 фев 2023
This a channel that we talk about anything to do with Malawi.Things that affect Malawi either positively or negatively.This ranges from politics, entertainment,economy to religion.So join us as we discuss these things.
Masintha Yalira Imfa ya Chilima!!
UTM memorial rally at Masintha ground Lilongwe..in memory of Dr Saulosi K Chilima,,Rest in Eternal Peace General!!
Просмотров: 10 472
Видео
AKWENI ALAVULA PANO...?
Просмотров 2622 месяца назад
UTM,a Tonse Alliance partner with MCP has just announced that they are out of the alliance..watch the Press Announcement as it happens...
UTM YATULUKA MU TONSE ALLIANCE...Zitha bwanji ndi a Michael Usi?
Просмотров 2633 месяца назад
UTM,a Tonse Alliance partner with MCP has just announced that they are out of the alliance..watch the Press Announcement as it happens...
Osayiwara Kuti Zinayamba Bwanji?
Просмотров 3,6 тыс.3 месяца назад
We talk about the benefits of mines in Malawi and who are the beneficiaries?Does Malawi really benefit from them?
A PETER MUTHALIKA ASIMIKIZA KUTI AYIMASO || ZINTHU zakwera MITENGO chifukwa cha a CHAKWERA akutero?
Просмотров 5775 месяцев назад
Following the Peter Muthalika Rally in Blantyre at Njamba Park
Mabungwe Omwe Siaboma AKWIYA Ndikuthesedwa kwa Mlandu wa Dr Saulosi Chilima...Mverani Nokha!!
Просмотров 1,3 тыс.5 месяцев назад
CSO Press Briefing..
Dr Saulosi Chilima Milandu YATHA||TSOPANO 2025 ULENDO UYAMBIKE!!
Просмотров 3,1 тыс.5 месяцев назад
Malawi Government has just discharged all corruption charges against the vice President Dr Saulosi Chlima...We say this when battle for the 2025 General Elections starts!!!
A Chakwera Akuti Mabvuto tili Nao Ku Malawi ndi atempolare....Njala,Katangale,Zinthu kudura?
Просмотров 1,1 тыс.5 месяцев назад
We talk about the benefits of mines in Malawi and who are the beneficiaries?Does Malawi really benefit from them?
KODI A VAISI PULESIDENTI AYAMBA KUTUMIDWA NDI A PULESIDENTI CHAKWERA PANO?
Просмотров 11 тыс.5 месяцев назад
We talk about the benefits of mines in Malawi and who are the beneficiaries?Does Malawi really benefit from them?
KODI AKUPINDULA NDI MIGODI KU MALAWI KUNO NDI NDANI?
Просмотров 3945 месяцев назад
We talk about the benefits of mines in Malawi and who are the beneficiaries?Does Malawi really benefit from them?
Ambuye Mntengeni| Mowa Wachilendo Wagwedeza Mnzinda wa Blantyre|Anthu 8 Afa Kale...
Просмотров 1,2 тыс.6 месяцев назад
We are discussing the mysterious alcoholic drink which has caused 8 fatalities in Blantyre Malawi
Aphungu a DPP kukunthana mu Paliyamenti|Age Bill Yavuta!!!
Просмотров 2,7 тыс.6 месяцев назад
We are reacting and commenting on what the former MCP publicity secretary is saying about Tonse Alliance Government failure to fulfill campaign promises.. Malawi is Worse off than it was 5 years ago...he admits!!
Mwina Tinayiwala Mmene Zinaliri 2019 Kuti Enafe Tilowe M'Boma?Kotsutsa Kutatiphweteka !!
Просмотров 3,8 тыс.6 месяцев назад
Chilima press briefing 20219..
A John Kapito Akuti Katangale Wanyanya ndi Boma la Tonse Alliance?
Просмотров 7 тыс.7 месяцев назад
We are reacting and commenting on what the former MCP publicity secretary is saying about Tonse Alliance Government failure to fulfill campaign promises.. Malawi is Worse off than it was 5 years ago...he admits!!
Kamuzu Chibambo Kutsimikiza Kuti Tonse Alliance Sakudziwa chimene Akuchita|Amamangidwa Mmasamba
Просмотров 3,9 тыс.7 месяцев назад
We are reacting and commenting on what the former MCP publicity secretary is saying about Tonse Alliance Government failure to fulfill campaign promises.. Malawi is Worse off than it was 5 years ago...he admits!!
Mmene a Tonse Alliance Akuthawira Kulephera Kwao Posintha Malawi| Kuloza Chala Ogwira Ntchito m'boma
Просмотров 2,8 тыс.7 месяцев назад
Mmene a Tonse Alliance Akuthawira Kulephera Kwao Posintha Malawi| Kuloza Chala Ogwira Ntchito m'boma
AKUSINTHA MALAMULO KU MCP CHIFUKWA CHAKULOWA KWA ULADI MUSSA M'CHIPANIMO?
Просмотров 2,6 тыс.7 месяцев назад
AKUSINTHA MALAMULO KU MCP CHIFUKWA CHAKULOWA KWA ULADI MUSSA M'CHIPANIMO?
Peter Muthalika KUZUZURA President Chakwera kuti Wasokoneza Malawi...Amuchosa Chakwera 2025!!
Просмотров 3,2 тыс.7 месяцев назад
Peter Muthalika KUZUZURA President Chakwera kuti Wasokoneza Malawi...Amuchosa Chakwera 2025!!
Kalanga Ife,Tithawira kuti?Akuti Namondwe Filipo Akuphikidwa pa Nyanja ya Indian Ocean Kubwera ku MW
Просмотров 2,3 тыс.7 месяцев назад
Kalanga Ife,Tithawira kuti?Akuti Namondwe Filipo Akuphikidwa pa Nyanja ya Indian Ocean Kubwera ku MW
Zayamba KUULULIKA ZAMALIFOMU ANAPELEKA CHILIMA kwa a PULESIDENTI
Просмотров 33 тыс.7 месяцев назад
Zayamba KUULULIKA ZAMALIFOMU ANAPELEKA CHILIMA kwa a PULESIDENTI
Mneneri Wakale wa MCP Wazomeleza kuti A CHAKWERA AKANIKA KUKWANILITSA ZIMENE ANAWAUZA A MALAWI?
Просмотров 9 тыс.7 месяцев назад
Mneneri Wakale wa MCP Wazomeleza kuti A CHAKWERA AKANIKA KUKWANILITSA ZIMENE ANAWAUZA A MALAWI?
MaBishop Akuti Utsogoleri Wa Masomphenya Kulibe ku Malawi|Akufuna Kutsintha 50%+1 Zikumveka Ngati?
Просмотров 14 тыс.7 месяцев назад
MaBishop Akuti Utsogoleri Wa Masomphenya Kulibe ku Malawi|Akufuna Kutsintha 50% 1 Zikumveka Ngati?
Kodi Aphungu Athu Amatiyimiladi Ife a Malawi kapena Zipani Zao?
Просмотров 1,3 тыс.7 месяцев назад
Kodi Aphungu Athu Amatiyimiladi Ife a Malawi kapena Zipani Zao?
Mmene Anthu awa Otchedwa 'OMENYERA UFULU' Amatipusisira a Malawi?
Просмотров 7 тыс.7 месяцев назад
Mmene Anthu awa Otchedwa 'OMENYERA UFULU' Amatipusisira a Malawi?
Mmene ANASAUKIRA a MIKE CHILEWE chifukwa cha Anthu Asanje ndi Andale!!
Просмотров 4,7 тыс.8 месяцев назад
Mmene ANASAUKIRA a MIKE CHILEWE chifukwa cha Anthu Asanje ndi Andale!!
Mmene John Tembo Anaphera Tsogolo La Kinnah Phiri Losewela Mpira Kunja !!!
Просмотров 5 тыс.8 месяцев назад
Mmene John Tembo Anaphera Tsogolo La Kinnah Phiri Losewela Mpira Kunja !!!
Mary Navitcha a DPP Kuyanka Zimene Anayankhula a Pulesidenti mu Parliament...Kusambwaza SONA !!
Просмотров 1,1 тыс.8 месяцев назад
Mary Navitcha a DPP Kuyanka Zimene Anayankhula a Pulesidenti mu Parliament...Kusambwaza SONA !!
A Malawi Ambiri Akuti a Chakwera Amangodziwa Kuyankhula Osati Kugwira Nchitoyo...Mvelani Nokha!!
Просмотров 4,2 тыс.8 месяцев назад
A Malawi Ambiri Akuti a Chakwera Amangodziwa Kuyankhula Osati Kugwira Nchitoyo...Mvelani Nokha!!
BREAKING NEWS!!! a ACB SANAUDZIDWE KUTI NDALAMA ZAPELEKEDWA KWA SATTAR?
Просмотров 2,4 тыс.8 месяцев назад
BREAKING NEWS!!! a ACB SANAUDZIDWE KUTI NDALAMA ZAPELEKEDWA KWA SATTAR?
Kodi a Nyuzipepala Apepesa Zokhuzana ndi Sattar ndi Boma kuti Contract Palibepo Yanyuwani?
Просмотров 8868 месяцев назад
Kodi a Nyuzipepala Apepesa Zokhuzana ndi Sattar ndi Boma kuti Contract Palibepo Yanyuwani?
Malumewa amakwanira ine pastor chilimba chiladzulu
Big Gwaladi zabhobho
Mabotolo abwino kwambili he need government support
0 pa 10 aaaa kukanika kifusa mafuso azeru ndithu shaaa
Kodi jogwaladi ndiwosauka?
Onanizimodzi inu kumanga nyumba ndi kodula koma kugula mowa ndikochipa
Kkkkk
Mbambande gwaladi
Zili bo
This is awesome, it's very good to check on pple whilst alive osat munthu wafa ndiye bas ma camera lendelende sizipereka nzeru
Washing from midland south Africa,nice program 😊
Amalawi mukavotera chekwela muthako kumneko.
Ndipo osafowoka
Inuyo ya prensident mwakana kuti ndiyaboza ndiye sankhani inuyo ndakubanja ndimu zikufunikira
Ngati lipoti mukuyikana ndiye bwanji mupeze anu wofufuza tizamve lipoti lenireni
Kodi ku Malawi kuli anthu othani osekelera zoipa ngati chikangawa misozi iyi talira iphindura no matter what! God created man & watching
Moto unandi guys tilipo ife🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥
😢😢
Ticking
Gwarad unayamba Kare kuyimba Koma Roko nyuma eeeeeeee .umagura chiyani ndarama nzimene umapanga choooooo😢😢😢😢
Kkkkkkkkkkkkk
Amunyanyiwa ntchito simuiziwa ayi mukulephera kumfusa mafuso mwaonongatu ndalama ulele
Komaso dzilikooooo
nice one
Chithandizo cho iye ndalama amapeza koma mowa aaaa..... Tazikhalani serious kuzolowera kupempha eti? 🤔
Kuyembekezera kuti ndimva funso loti joe ali ndi Ana angati? Ationetsa madam a joe ayi ndithu za ziiiii..... 🤭
Mfundo zikuwoneka zikuwoneka mulibe next time. Zafuseni zazeru . Komaso gwaladi mwatichitisa Mandyazi asa asa hiya
Akomaamakana ndipotimawanyadila
Akamunaamenewo amativesakukoma jo
Is this comedy 😅😅😅😅
Gwaradi sakufunika kumupasa ndarama ayi kuthandiza kwake kuimirire ndi munthu wina azimupangira kaya ndi nyumba iyeyo akapeze yomanga kare ndikumuikamo mmmm zokhudza bwanji kuntchuka koseku 🤔
Jumping Jack !
Zopanda ntchito izi, anthu akuvutika kwambiri kumudzi, okalamba, aumphawi, olumala, amasiye, odwala, osamalankhula mwachibwana kut Mulungu Ali mbari yanu yet zinthu sizili bwino, kulankhula ngati anthu opanda mzeru, palibe chanzeru chomwe mukuchita chopindulira Malawi kuposa kumangomanga wanthu ndi kusintha maina azipatala zoti simudamange ndinu, 4 years just for nothing, shame on you guys, mzipatala mankhwala mulibe, chitetezo taaa, ma school Nde mwakweza ma fees, anthu akumudzi omwe alibiletu chiyembekezo ndipo alibe chilichose akwanitsa bwanji kulipilira Ana awo ma school, chakudya Nde kulibiletu, chomwe mukuganiza mkuti tidzadzitsa bwanji matumba wathu kuti tidzabele zisankho, AGALATIYA opusa, oyamba ndi zabwino kutsiliza ndi zoipa, When I said amalawi akuvutika I mean it, mukamadya bwino kumitundako musamati aliyese a kudya, go to the villages and see how life is, you will cry, anthu a kugona ndi njala and you are expecting those people to go and vote for you this coming 2025 nonsense, MAY The Soul of SKC continue to Rest well and hope he is watching you all,
Ufiti
amapanga sewero
Kuyankhula koputsa kwambili,Kodi moyo ndi wanu??? Inu anthu omvetsa chisoni kwambili
It is supposed to happen.. MCP is a big party sangalore kuberekedwa
Chakwera ndi mbudzi yamunthu
Koma malawi kodi mukhalabwamji? monga azomba ndi azisuzo mumamwalila apanda kanthu kalikose.
Mwagwanayo UTM yakutulukani forever Chakwela kwamai ako
chisankho chabwino koma osanyoza adzanu ayi
Chakwera ndi munthu olephela ....mkazi olanda amavuta
Anamangindwa chifukwa chani
Ayi ndth anthu matha kuvina eeeee😄
Osayiwala chipande ndipowomola
Tso pali chimene wapanga chakwera success! Agalu achabe chabe.
Za ziiiiiiii! Chakwera ndi MCP yake akagwere uko
Zakuvutani bas
2025 president wanu chakwela? Is so sad for Chilima 😢 rest well
Ubwino simuvota nokha